Oyimba Akugulidwa Ndi MCP

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 3 ก.พ. 2025

ความคิดเห็น • 116

  • @user-gp10.10
    @user-gp10.10 4 หลายเดือนก่อน +12

    Grace Chinga bwera udzawone kuno zijazi😢

    • @LomezyWhite-vq9bv
      @LomezyWhite-vq9bv 4 หลายเดือนก่อน

      Ndipotu adaulula zija ndi zimenez

  • @GiftKananji
    @GiftKananji 4 หลายเดือนก่อน +12

    Inetu ndigwirizana ndi zomwe dj munyanane wanena anthu sakungo lowa mwa kufuna kwawo koma mphavu za akumidima ndalama yomwe ikugawidwa ku mcp ili ndi chikoka chakumidima

    • @MCAnthonyNdau
      @MCAnthonyNdau 3 หลายเดือนก่อน

      Ndiwe opusa kwambili ndichi fukwa chani zipani zimakhala ndi director of recruitment kapena simumadziwa tanthauzo lake

  • @HappyMunthari
    @HappyMunthari 4 หลายเดือนก่อน +5

    Or onse oyimbawa atapita ku mcp ife ku mpoto sitikuopa chifukwa tikudziwa kuti chakwera sakudziwa kuyendesa dziko

  • @Alexchikweza
    @Alexchikweza 4 หลายเดือนก่อน

    Big up boys

  • @AaronMsewezi
    @AaronMsewezi 4 หลายเดือนก่อน +3

    Boma ndi lomweli, zoona, a Malawi chimene tikufuna si president wina koma chitukuko basi , let us work with Chakwera, wonani pa ground

    • @EsChinombo
      @EsChinombo 4 หลายเดือนก่อน

      Boma ndi lomweli

    • @jafarirajabu2719
      @jafarirajabu2719 4 หลายเดือนก่อน

      Galu iwe kagwileni uko mboloyako ndi MCP yakoyo

    • @LinlyMathewe
      @LinlyMathewe หลายเดือนก่อน

      Zaziii president panda mnzeru ngati uyu ine chibdwire changa sindinamuonepo

  • @JohnGreen-v8f
    @JohnGreen-v8f 4 หลายเดือนก่อน +3

    Ngati kwalembedwa kuti pita awine azawina

  • @PedroTomas-y9h
    @PedroTomas-y9h 4 หลายเดือนก่อน +2

    Tamutulukabeeeeeeeeeee

  • @Madalitsoy6o
    @Madalitsoy6o 4 หลายเดือนก่อน

    ❤ umakwana iweyo

  • @MosesDicostar
    @MosesDicostar 4 หลายเดือนก่อน +3

    Athu akusatako ndalama koma ife MCP ayi taikana

  • @VeronicaSekobi-is6dk
    @VeronicaSekobi-is6dk 4 หลายเดือนก่อน

    🎉❤

  • @FidesChandama
    @FidesChandama 4 หลายเดือนก่อน +1

    Ndi okha okha a illuminate awa pitani ku masamba awo antchezo mupeza kuti ndi apasi panyanja pompo

  • @Dayanschirwa
    @Dayanschirwa หลายเดือนก่อน

    Grace mulungu akudariseni mnaunikira amalawi kom kusava kwa2 zizindikiro zaoneks mot mavuto ndiambili

  • @Manlymw
    @Manlymw 4 หลายเดือนก่อน +1

    Zonsedzi dza temporary

  • @SammyChakwana
    @SammyChakwana 4 หลายเดือนก่อน

    Ukunama aise legacy yavaya.azikufira ndi a mcp akowo aise watha basi in music industry in malawi believe you me.

  • @Chitani100
    @Chitani100 4 หลายเดือนก่อน +1

    Ine ndili pano kuvetsela mwa tchelu 😊

  • @JamesKamwendo-s9f
    @JamesKamwendo-s9f 3 หลายเดือนก่อน

    😅😅😅

  • @PeterChimbayo
    @PeterChimbayo 4 หลายเดือนก่อน

    Just take this note.....OIMBA SANGAWINITSE CHIPANI.......🎉🎉

  • @VincentMatola-s8g
    @VincentMatola-s8g 4 หลายเดือนก่อน

    Kkkkk MCP kulibe anthu ambiri oti akhoza kuwavotela mpaka kuwawinisa

  • @NikolasNanawe
    @NikolasNanawe 4 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤

  • @AndrewChasweka
    @AndrewChasweka 4 หลายเดือนก่อน

    Oimba alingati opanga sewerotu achina manganya umaona ngat muli limodzi kumapeto umazangomva odya zake alibe mulandu🤣🤣🤣🤣🤣

  • @CathreenKadwala
    @CathreenKadwala 4 หลายเดือนก่อน

    Rip Grace Chinga😢

  • @AaronMsewezi
    @AaronMsewezi 4 หลายเดือนก่อน

    Ndi bodza ilo kuti oyimba anagulidwa, nthawi ija Dan Lu anali ku DPP tinganene kuti dpp inamugula? , munthu ali ndi ufulu wolowa ndi kutuluka, ndikudabwa kuti anthu mumangoti a Malawi adabwa zoti mwakuti, aaaaa.

  • @BlessingsmadalitsoShumba
    @BlessingsmadalitsoShumba 4 หลายเดือนก่อน

    😂😂😅😅 oimba abalilalika ,
    Mdyeleni chakwera 😂😂 azalila munthuyu kwabasi,
    Zachamba izi ma artist wose alowa mcp athela pompa .

  • @CASSIMDinala-z7e
    @CASSIMDinala-z7e 4 หลายเดือนก่อน +2

    komano boma ili kuli ndalama osati zochedZ

  • @AkoneyThomas
    @AkoneyThomas 4 หลายเดือนก่อน

    Koma nanga amavota ndioimba kod 😂

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 4 หลายเดือนก่อน

    Akuti unali mgwilizanotu ndi oimbawa ndiye ndi ndani safuna moyo kkkk

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 4 หลายเดือนก่อน

    Onsewo akugulidwa ndi Mcp, zambia, Nigeria, south Africa and Malawi

  • @AKAVIHENGOATHOSI
    @AKAVIHENGOATHOSI 4 หลายเดือนก่อน

    Kkkkk koma ndalama ziphesa anthu

  • @MCAnthonyNdau
    @MCAnthonyNdau 4 หลายเดือนก่อน

    Akalowa ku dpp ndekuti sana gulidwe koma mcp agulidwa eti nanunso mukhoza kumagula palibe akukulesani

  • @JaneHunga
    @JaneHunga 4 หลายเดือนก่อน

    Or chakwera azawine or ayiii koma yemwe wawinayo azakhalabe Apure anthu basi mlungu tiyendereni😊

  • @daviechikopa-r6w
    @daviechikopa-r6w 4 หลายเดือนก่อน

    falling down of bab lone

  • @DanWawo
    @DanWawo 4 หลายเดือนก่อน

    Adaga ndalama daniyo

  • @KentWilliam-r2v
    @KentWilliam-r2v 4 หลายเดือนก่อน

    Mr chikangawa wagwa bsi or atagula oyimba sangawinise zisankho

  • @SceloManqele-y9o
    @SceloManqele-y9o 4 หลายเดือนก่อน

    Hi what language are you speaking

  • @RexonKamwana-c2r
    @RexonKamwana-c2r 4 หลายเดือนก่อน

    Azigula oyimbawo aziwe kt akuluza ma followadzi oyimba ofuna ndalama osati kuganizila amalawi akukhutitsa mimba zawo.anthu akudya chiteze mamizimu ena mango athira juwisi.

  • @EduardocadamanjatomasCadamanja
    @EduardocadamanjatomasCadamanja 4 หลายเดือนก่อน +1

    Iweso orengenzawe bhori yako watumidwa

  • @DaguDere
    @DaguDere 4 หลายเดือนก่อน

    Iweso ndiwa mcp eeet

  • @Victoriabwaira
    @Victoriabwaira 4 หลายเดือนก่อน

    azamuvotela garu oyimba omwewo

  • @WesleyKalimwayi
    @WesleyKalimwayi 4 หลายเดือนก่อน

    Bwino lake ndi oyimba lokoni atatenga ose oyimba Malawi munu sangawine

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 4 หลายเดือนก่อน

    Peter sangasiye kuwina chifukwa cha woyimba onse awagule ife tili pambuyo pa dpp

  • @GiftMatiki-cb1tq
    @GiftMatiki-cb1tq 4 หลายเดือนก่อน

    🤕🤕🤕

  • @mikeelmsukwa
    @mikeelmsukwa 4 หลายเดือนก่อน

    Tamutukabe ameneyo

  • @IslamMapepa
    @IslamMapepa 3 หลายเดือนก่อน

    Sazabwelelaso tiziwona bola osapepesa

  • @EsChinombo
    @EsChinombo 4 หลายเดือนก่อน

    Iwetu ukufuna kuti anthu akutame😊 boma ndilomweli man

  • @AtupeleChitenje
    @AtupeleChitenje 4 หลายเดือนก่อน

    Grace uja munaphela zoonadi

  • @LameckBanda-gk6ri
    @LameckBanda-gk6ri 4 หลายเดือนก่อน

    Kodi oyimbawa mukufuna azilowa DPP poti ndichipani chakubanja kwanu,akalowa MCP aguridwa Mesa DPP yalamulirako dziko lino 14 years kusinthana pachibare ngati ufumu oyimba makuyimbirani aja mumagura nde mulibe ndalama zogurira ngati mumachikonda chipani chakubanja kwa muntharika athandizeni muwagurire oyimba akunja

  • @WysonSadiki
    @WysonSadiki 4 หลายเดือนก่อน

    Zikuthanthawuza kut Giboh adawuza Nkasa kuti ku Mcp ndalama yapweka ayi zikomo... basi ife tizidya chitezechi achuke iwowo😭

  • @RaffiqMahmoud
    @RaffiqMahmoud 4 หลายเดือนก่อน

    Nanu a sam muyaluka ndi channel chanu chomangopanga za wanthu

  • @BilaliJafali-b9x
    @BilaliJafali-b9x 4 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi iwe zandale siziyeni uzingopanga za oyimba

  • @MatthewsBanda-e6o
    @MatthewsBanda-e6o 4 หลายเดือนก่อน

    Mwina wakula ndi umphawi koma oimba sayenera kuonetsa mbali choncho,,zimatsitsa carrier yawo ngat oimba

  • @enerstapologize
    @enerstapologize 3 หลายเดือนก่อน

    Oimba sangawinise

  • @GREGORYBERNARDMATAMBO
    @GREGORYBERNARDMATAMBO 3 หลายเดือนก่อน

    ndiye vuto mchani

  • @ShaneiJames-n1v
    @ShaneiJames-n1v 4 หลายเดือนก่อน

    Kugulidwa sikhani ndiokavotayo😅

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 4 หลายเดือนก่อน

    Ku MCP kuli ndalamah zochuluka kadyeni km never MCP sikuwina,,, inukadyeni zabooka

  • @SimonBanda-b1f
    @SimonBanda-b1f 4 หลายเดือนก่อน

    Oyimba ambiri pano alibe ndalama ndiye akufuna ndalama.
    Anthu ngati mukufuna kupitiriza kudya chitedze zanu zimenezo

  • @LacksonLombwa-b6x
    @LacksonLombwa-b6x 4 หลายเดือนก่อน

    Basi people are after money, leave them

  • @ChrissWtness-e1z
    @ChrissWtness-e1z 4 หลายเดือนก่อน

    Giboh nyimbo xako timazisatila koma walowako ayi

  • @SammyChakwana
    @SammyChakwana 4 หลายเดือนก่อน

    Asikefa nde tataya kare muona mukatulusa nyimbozo ine pheeee kumastand

  • @paulmanyamba5437
    @paulmanyamba5437 4 หลายเดือนก่อน

    Atenge oyimba onse tilibe nazo ntchito ife

  • @JBMIKEBUNNAYAH
    @JBMIKEBUNNAYAH 4 หลายเดือนก่อน

    O imba omwe Ali bize kuimba zo yamikila chakwera ameneyo ndi kalu obanda uzimu ma udasi nonse ukuyamikira chakwera chikangawa busa unyenga sikaliyoti okuba anthu osalakwa nonse afiti

  • @ChristinaStambuli-q3e
    @ChristinaStambuli-q3e 4 หลายเดือนก่อน

    Ulendo uno zisinthe come 2025 adzakhale komweko ku mcp koz definitely ikuzakhala pa bench mcp yo ena achilendo atakhala pa driver's seat.

  • @WilliamChopika-u5b
    @WilliamChopika-u5b 4 หลายเดือนก่อน

    Eeee zilikotu

  • @AminaAfink
    @AminaAfink 4 หลายเดือนก่อน

    Koma abare aziagura athuwo koma vot sazayiwona 2025

  • @RodaLabana
    @RodaLabana 4 หลายเดือนก่อน

    Ndiye nanga giboh akupezekamo bwanji

  • @GeorgeMoyo-w9m
    @GeorgeMoyo-w9m 4 หลายเดือนก่อน

    Dziko la malawi ndi la democracy, chovuta ndi chiyani oimba kugwira ntchito ndi boma lolamula? Zaipa lero chifukwa anthuwa akutumikira boma, koma mmbuyo monsemu analipo oimba amene amayamikira DPP, PP, UTM vuto lanu ndi chiyani?

  • @NgalizeBanda
    @NgalizeBanda 4 หลายเดือนก่อน

    Agulidwa poti ndi MCP ndi DPP adangolowa ndale zaku Malawi zimenezo mtima wajerasi okhaokha basi

  • @GiftMaolera-l1g
    @GiftMaolera-l1g 4 หลายเดือนก่อน

    Ziko lapasa

  • @KalongaWhy
    @KalongaWhy 4 หลายเดือนก่อน

    Koma ghibo ufuse anthu akutulukidwatu oooo wakura watha

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xd 4 หลายเดือนก่อน

    PETER MUNTHULIKA AKAWINA NEXT YEAR PLEASE STAY AT MCP ....

  • @IbrahimPhiri-ky5jk
    @IbrahimPhiri-ky5jk 4 หลายเดือนก่อน

    Paja osewatu anachulidwapo ndi mayi gres chinga ndiye ndi zosadabwisa anthuwa ndi satanic ndintu mosakaika chifukwa zonse zaonekela poyela

  • @SteveniKhoMbanoBadoboyi-z8c
    @SteveniKhoMbanoBadoboyi-z8c 3 หลายเดือนก่อน

    kupusa ma muscian akumalawi

  • @MCAnthonyNdau
    @MCAnthonyNdau 3 หลายเดือนก่อน

    Mwina zipani sizimadziwa ntchito ya director of recruitment.... Ndikukopa anthu kuti aloee chipani timagwiritsa ntchito xipangizo zonse zomwe tilinaxo kukopa anthu ngati inuyo mulibe shauli yako

  • @SalomeManda-c1i
    @SalomeManda-c1i 4 หลายเดือนก่อน

    Ma chendeyake Dan lu ndi gibo matumbi nose pa ntumbo panu

  • @ErnestMkambwe-l2g
    @ErnestMkambwe-l2g 4 หลายเดือนก่อน

    MMAWA

  • @NyangwaKoma
    @NyangwaKoma 4 หลายเดือนก่อน

    Asiyeni oyimba akalowe ife sitikupitako popano tiwagwesela limozi

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 4 หลายเดือนก่อน

    Ntaba yakoyija. Uwabaye chijakeseni anawa akuziwe

  • @ElifalaThole
    @ElifalaThole 4 หลายเดือนก่อน

    Nanuso zigulani anu oyimbawo

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 4 หลายเดือนก่อน

    Iweso wadziwabwanji kit wasataniki kod aliposo atsogoleri abwino aaaa iwe samala wava

  • @AlicksonMakata
    @AlicksonMakata 4 หลายเดือนก่อน

    Mcp ikundigirigisha anthu akuthawa dpp chifukwa cha kalindo

  • @MaxonKambazithe
    @MaxonKambazithe 4 หลายเดือนก่อน

    Koma agalu oyiimba shaaaa satikonda ifeee amalawi tooonse ambiri oimba aiiiiiiiii niaagule zitsiru apite pamenepo oimba ambiri ukuopa kufa ni satanic money from galu bushiri

  • @ElishaMkandawire-j7o
    @ElishaMkandawire-j7o 4 หลายเดือนก่อน

    Boma ndilomweli koma pd tkusitha

  • @chiletsobisweck5007
    @chiletsobisweck5007 4 หลายเดือนก่อน

    Ubwino wake sitimadya nyimbo

  • @VitumbikoKaunga
    @VitumbikoKaunga 4 หลายเดือนก่อน

    guys music industry Nd ya. Bushiri mkuziwa nose. Nde bushiriyo Ndi chikangawa alilimodzi msadabwe. Oyimba , amene salowa MCP Ndi ulendo

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj 4 หลายเดือนก่อน

    Shinkangawaw satanic yinkuphangsa simeneso serious

  • @InnocentMsokera-h1t
    @InnocentMsokera-h1t 4 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂😂😂

  • @austinallie302
    @austinallie302 2 หลายเดือนก่อน

    Bodza si dziko lonse mwanama

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 4 หลายเดือนก่อน

    Ineyo wakupoto usamat Ifé kupoto ngat unatifusa ai iweyo ndiye wadpp.osat.kupoto ngat tonse ai pangazako

  • @VitumbikoKaunga
    @VitumbikoKaunga 4 หลายเดือนก่อน

    Ndizaurura ananena

  • @chikamandala7436
    @chikamandala7436 4 หลายเดือนก่อน

    Ndie Pali vuto kod??, opposition ikulephera kuwagula bwanji

    • @RuthBeyala
      @RuthBeyala 4 หลายเดือนก่อน

      𝐀𝐤𝐚𝐧𝐚𝐤𝐡𝐚𝐥𝐚 𝐤𝐮𝐭𝐢 𝐚𝐥𝐢 𝐩𝐚 𝐦𝐭𝐞𝐧𝐝𝐞𝐫𝐞 𝐬𝐢𝐛𝐰𝐞𝐳𝐢 𝐚𝐤𝐮𝐩𝐚𝐧𝐠𝐚 𝐢𝐳𝐢 𝐦𝐚𝐯𝐮𝐭𝐨 𝐤𝐨𝐦𝐚𝐬𝐨 𝐳𝐢𝐤𝐮𝐤𝐰𝐚𝐧𝐢𝐥𝐢𝐬𝐢𝐝𝐰𝐚 𝐧𝐝𝐢𝐳𝐨𝐦𝐰𝐞 𝐚𝐤𝐮𝐜𝐡𝐢𝐭𝐚𝐳𝐢 𝐜𝐡𝐨𝐦𝐰𝐞 𝐮𝐝𝐳𝐢𝐰𝐞 𝐦𝐜𝐡𝐚𝐤𝐮𝐭𝐢 𝐦𝐮𝐭𝐡𝐚𝐰𝐢 𝐲𝐚 𝐁𝐢𝐧𝐠𝐮 𝐤𝐨𝐦𝐚𝐬𝐨 𝐉𝐨𝐢𝐜𝐞 𝐁𝐚𝐧𝐝𝐚 𝐦𝐮𝐭𝐡𝐚𝐰𝐢𝐬𝐨 𝐲𝐚 𝐏𝐞𝐭𝐞𝐫 𝐢𝐳𝐢 𝐤𝐮𝐧𝐚𝐥𝐢𝐛𝐞 𝐤𝐨𝐦𝐚 𝐜𝐡𝐢𝐟𝐮𝐤𝐰𝐚 𝐜𝐡𝐚𝐤𝐮𝐤𝐰𝐚𝐧𝐢𝐥𝐢𝐬𝐢𝐝𝐰𝐚 𝐤𝐰𝐚 𝐦𝐚𝐥𝐞𝐦𝐛𝐚 𝐭𝐢𝐲𝐞𝐧𝐢 𝐭𝐢𝐳𝐢𝐩𝐞𝐩𝐡𝐞𝐫𝐚 𝐦𝐨𝐨𝐧𝐚 𝐦𝐭𝐢𝐦𝐚 𝐦𝐮𝐥𝐮𝐧𝐠𝐮 𝐚𝐭𝐢𝐜𝐡𝐢𝐭𝐢𝐥𝐞 𝐜𝐡𝐢𝐟𝐮𝐧𝐝𝐨 𝐜𝐡𝐢𝐟𝐮𝐤𝐰𝐚 𝐢𝐳𝐢𝐳𝐢 𝐬𝐢𝐳𝐨𝐨𝐧𝐚 𝐦𝐮𝐥𝐮𝐧𝐠𝐮 𝐚𝐭𝐢𝐤𝐡𝐮𝐥𝐮𝐥𝐮𝐤𝐢𝐥𝐞 𝐛𝐚𝐬𝐢

  • @PatricePhiri
    @PatricePhiri 4 หลายเดือนก่อน

    Akagwele UKo amenewo akufuna angodya ndalama zaphweka ku mcp km zikatha abwelela

  • @DaisonPiston
    @DaisonPiston 4 หลายเดือนก่อน

    Zowona

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 4 หลายเดือนก่อน

    Komaye mau kukhalangat ugalamule iweyo adzawineyo ndameneadzlamuletu bas

  • @BandahLemos
    @BandahLemos 4 หลายเดือนก่อน

    Ndilamulo laku satanic onse oyimba akulambila chakwera ili ndi lamulo la bushiri

  • @GreyMwanyimbo
    @GreyMwanyimbo 4 หลายเดือนก่อน

    Ali ndiufulu olowa chipani chilichonse

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 4 หลายเดือนก่อน

    Ndipo satanic yafikapo ku Malawi kkkkkkkkkkk

  • @KondwaniNgoma-o5u
    @KondwaniNgoma-o5u 4 หลายเดือนก่อน

    Asiyeni 2025 boma Dpp

  • @ChisomoMakanda
    @ChisomoMakanda 4 หลายเดือนก่อน

    This is a bad development of the music industry our own artists should differenciate between arts and science

  • @thulambale2836
    @thulambale2836 4 หลายเดือนก่อน

    Dpp iiiiiii yilibe nkhalidwe

  • @KalongaWhy
    @KalongaWhy 4 หลายเดือนก่อน

    Koma dan lu iwe ndimuyawo ineso ndimuyawo petoga ryenu bwanawe wamvatu

  • @starlonJames-qr4xl
    @starlonJames-qr4xl 4 หลายเดือนก่อน

    zilibe ntchito zimenezi