Mr Abdul,don't tell us to vote for Atupele chifukwa ndi wa ntundu wanu ayi,ndale zovotela munthu chifukwa ndi wakwathu ndi zomwe zikutibwezera m'mbuyo ife a Malawi.Tizivotela munthu mosayang'anila dela lomwe akuchokela koma yemwe ali ndi mtima ofuna kusintha zinthu mokomera dziko lonse osati mtundu umodzi kapena kwao kokha ayi Therefore,Mr Abdul,do not bring divide and rule,with your tribalistic sentiments
Mwalankhula bho man Koma enafe ndi a DPP☑️
Powerful!!!! UDF ibweleredi m'boma
Mulungu akudaliseni Abdulu
Koma Chakwera ndi boma lake la MCP akuti boma likuyenda bwino kwambiri , ndipo akuti lipilila mpaka 2030 😂😂😂😂😂😂
Mr Abdul,don't tell us to vote for Atupele chifukwa ndi wa ntundu wanu ayi,ndale zovotela munthu chifukwa ndi wakwathu ndi zomwe zikutibwezera m'mbuyo ife a Malawi.Tizivotela munthu mosayang'anila dela lomwe akuchokela koma yemwe ali ndi mtima ofuna kusintha zinthu mokomera dziko lonse osati mtundu umodzi kapena kwao kokha ayi
Therefore,Mr Abdul,do not bring divide and rule,with your tribalistic sentiments
Bomali aziyendetsa Asilikali basi ,zovoter zo ayi.
Achakwera Maine agaluwa akuba kwambili
Atupele muluzi ndiye ayi mwanama man😂
Komaso u d f singawine atupere nayeso azaononga osati masewera
Nkhani ya mayi Mia
Dziko lonse lapansi likudziwa za katangale
UDF ndi DPP Bola UDF atupele sanga fanane ndienawa