BRIAN BANDA KUFUNSA MAFUNSO PAMAPERO PA CONVENTION

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 26 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 135

  • @IvyMkhura
    @IvyMkhura 2 หลายเดือนก่อน +3

    Peter Mutharika is so genius, amene anamuchalira kuti abweranso ku convention kachiwiri wauponda.

    • @isaihmagani5697
      @isaihmagani5697 2 หลายเดือนก่อน

      Adatopa ndi achikulire

  • @PetroKachingwe-jf7dh
    @PetroKachingwe-jf7dh 2 หลายเดือนก่อน +3

    Nkhalamba zokhazokha osasiyila achinyamata bwanji
    Mbava izi
    Uyu George Chaponda anaba chimanga chonse ndalama za Admark
    Mbava iyi asakudziwa ndani
    Admark inatha chifukwa cha Anthu awa

    • @Victoriabwaira
      @Victoriabwaira 2 หลายเดือนก่อน

      Mpakana Osayila kkkk

  • @ishmaelsiffah9900
    @ishmaelsiffah9900 2 หลายเดือนก่อน +1

    Peter muthalika ndiochenjera guys,kuteroku ndiye kuti oyedzeka anzao aja anamuchalilira lero auponda iye sanabwere 😂😂😂

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo 2 หลายเดือนก่อน +12

    Muthu waluza musamukwezi tima ayi musiyeni wafotokoza bwino kwambiri

    • @JustinLipipa
      @JustinLipipa 2 หลายเดือนก่อน

      Kkkkkkkkk ndizakuchipani izi.

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 2 หลายเดือนก่อน +6

    Ndiwayankhile ine a Chaponda kukula komwe akula sizikutanthauza kut akhale pansi ai..azakhala pansi ntchito yao ikazatha pa Dziko lino..this is why we have a Old testament qnd new testament..

  • @MauriceMukona
    @MauriceMukona 2 หลายเดือนก่อน +1

    Nonse amene mukunena zokalambazo mbolo zanu ndi nyini zanu mxiiiii.manamvapo kuti ukalamba ndimatenda?

  • @FatimaUmali-pc8sy
    @FatimaUmali-pc8sy 2 หลายเดือนก่อน

    Zoona zake ndi ZImenezo kuti a nawona adani ake alipafupi ndi munthu wankulu Peter akaona patali genius Peter ❤❤❤ mphechempheche mea njovu Salita awiri

  • @mayachikadewa7551
    @mayachikadewa7551 2 หลายเดือนก่อน +2

    Zitheka bwanji Kuti president asapezeke potseka convention?

    • @JohnsonMaulana
      @JohnsonMaulana 2 หลายเดือนก่อน +1

      Adani achuluka amaionela patali mkuluyu wachita bwin😊

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 2 หลายเดือนก่อน +7

    Koma Briane ukufuna kukweza BP munthu wachikulileyo Kodi komanso zakhala bwino akula azigwila ndi anyamata ntchito

  • @LewisJumbe
    @LewisJumbe 2 หลายเดือนก่อน

    Conversation yayenda bullet,mafunso Anu,sapindula kanthu.lets look forward.

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju 2 หลายเดือนก่อน

    Age is just a number indeed...DPP my vote

  • @MadalitsoBokosi-j3u
    @MadalitsoBokosi-j3u 2 หลายเดือนก่อน +3

    Akulu ndi dambo mozimira moto ... Anyamata azikathamanga pa ground akolo azilangizi

  • @Chikwina
    @Chikwina 2 หลายเดือนก่อน +2

    Chaponda waledzera ndipo mutharika akupuma after ukalamba azigonagona

  • @stalickkafera3454
    @stalickkafera3454 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mutalika wantha mukumukakamza kugwirabe ntchito😂😂
    Osamusiya apume bwanji
    Adzaferatu pa msokhano😂

    • @thomaswyson-e2q
      @thomaswyson-e2q 2 หลายเดือนก่อน

      Iwe namachende asanafe peter ayambe kufa ndiabambo ako

  • @AlickChima
    @AlickChima 2 หลายเดือนก่อน

    Maharaja nde mwawapanikizatu onyamata inu 😅😅😅 mpaka chibwibwi kudzitamandira ati Leader of opposition ndi power 😅😅😅😅

  • @MisheckKamwendo-w9n
    @MisheckKamwendo-w9n 2 หลายเดือนก่อน +4

    Koma Brian ndi azako muthu waluza koma mafuso ameneo muthu atha kukomoka

  • @charleskazembe5728
    @charleskazembe5728 2 หลายเดือนก่อน

    Brayan thanks you always make program sacessfull 😅😅😅

  • @christopherkamphinga
    @christopherkamphinga 2 หลายเดือนก่อน +2

    Zayambika uku. Azizathawanso mu office ndi ukalamba.

    • @giftsululu4274
      @giftsululu4274 2 หลายเดือนก่อน

      Malawi muno tupusitsana kobas

  • @UchizieFMtemela
    @UchizieFMtemela 2 หลายเดือนก่อน

    A chair mwayankha bwino 😂😂alekeni chabe😂😂

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 2 หลายเดือนก่อน

    Profe sikape guys ... , munthu uja amayiwelenga

  • @VenançioZocueza
    @VenançioZocueza 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe Brian peter amaopa kuphedwa ndi dzigawenga dza mcp

  • @AlihIbrahim-s7v
    @AlihIbrahim-s7v 2 หลายเดือนก่อน +2

    Koma inusotu Chanel chanuchi ndiye gaga weniwenotu Madera bwanji ingoduka basi chimphwetelele

    • @samsonmtumbati4855
      @samsonmtumbati4855 2 หลายเดือนก่อน +1

      Iwe chikangawa choka ap tulutsani report basi

  • @tasmania527
    @tasmania527 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe Namalomba, njala inabwera chifukwa ma leaders anu ammbuyo sanapange za irrigation kuphatikiza ndi ng'amba ya Southern Africa. Mwakhala mukunena kuti achina Mutharika ndipatali, nanga anayika madziko anji mu nthawi ya ulamuliro wawo kuti ku Malawi kusakhale njala ? Mulibe fundo koma kunama ndi kupusitsa anthu.

  • @PreciousPhiri-l8w
    @PreciousPhiri-l8w 2 หลายเดือนก่อน

    Koma chi peter chija osazachiphwekes chochenjera ❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @Apostolic.faith7044
    @Apostolic.faith7044 2 หลายเดือนก่อน

    These are elders supposed to rest for sure. Old to a point where they can't function to bring change in Malawi. People must accept they are old and tired, not even able to close a convention. They can't even see the difference of frail health on P. Mutarika. He did his best part in the past but must retire all these who are not able to see that they a madalas

  • @Blessings-b7h
    @Blessings-b7h 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi Brian bwanji ukuwavutitsa anthu dpp?
    Munthu wamkulu akuphunzitsa ana ntchito.

  • @AnnastanziaMhango
    @AnnastanziaMhango หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂 Kusakhalapo pa musokha umenewo zikuoneka kulemphera kuti sazalowaso mu boma

  • @BrianMaganga
    @BrianMaganga 2 หลายเดือนก่อน

    Adad akuyendani pansi, muona kuti mutani 😂😂

  • @MaxwellChiwaya-i8q
    @MaxwellChiwaya-i8q 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkkkk koma anamalomba ndi achina Brian kkkkk

  • @BrianAmos-s2k
    @BrianAmos-s2k 2 หลายเดือนก่อน

    Zomwe akuyankhulazo ndidziwona chomwe chinachititsa kuti msonkhano uwonjezeledwe matsiku Malo motha tsiku le ileni ndichani?which means adani amakonz a chiwembu.President adachita bwino kungolemba note yotsekela msonkhano wawo basi

  • @FanizoKawindula
    @FanizoKawindula 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi Hon Mchacha alipo?

  • @CleverlyKanthyos-ds5sg
    @CleverlyKanthyos-ds5sg 2 หลายเดือนก่อน +1

    DPP khalamba zokhazokha
    Zoyha mano

  • @GreyMwanyimbo
    @GreyMwanyimbo 2 หลายเดือนก่อน

    Koma zitithandiza??????

  • @husseinjabu8866
    @husseinjabu8866 2 หลายเดือนก่อน

    Poor quality of coverage improve guys

  • @KenAipa-r3r
    @KenAipa-r3r 2 หลายเดือนก่อน +2

    Kkkkkkkk Kuchita kubwereza kuti Kodi aluza ????

  • @thomphalavi5027
    @thomphalavi5027 2 หลายเดือนก่อน +2

    Dpp yatsakha bwino mipando komaso mukutipasilanu mukulemphera

  • @beinhardkausiwa7107
    @beinhardkausiwa7107 2 หลายเดือนก่อน +1

    The question is unprofessional

  • @AnnastanziaMhango
    @AnnastanziaMhango หลายเดือนก่อน

    Chaponda tinamutopela ife anthu a Malawi sitikufuna olo ngati sakuziwa umunthu alibe

  • @JohnBanda-ux9fy
    @JohnBanda-ux9fy 2 หลายเดือนก่อน +2

    Munthu wamkulu APM anachoka lero mmawa chifukwa anadziwa Kuti Ku dpp kulibe kukhapana ngati achita chikangawa party..anachezera convenshon .. Koma kurephera kukayang,ana ndege Ku chikangawa 😂😂

  • @EmmanuelChirwa-z3n
    @EmmanuelChirwa-z3n 2 หลายเดือนก่อน

    Chokani mwakalamba oba chimanga inu🤣🤣🤣

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli 2 หลายเดือนก่อน

    Munthalika ndi dolo Mesa anthu amachachila kuti amupange zina ndi zina ndiye iyeyo wabanduka ndi dolo

  • @GladsonBanda-m3e
    @GladsonBanda-m3e 2 หลายเดือนก่อน

    Nkumati tiyendetsa Boma pumani mwakula kukanika kukatseka msonkhano ngakhare campaign idzawavuta

  • @AnnastanziaMhango
    @AnnastanziaMhango หลายเดือนก่อน

    Wakalele waka adzukulu nakuonera mbuzi muchiwaya kumudzi fundo mulije ndipo akalamba basi

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 2 หลายเดือนก่อน

    Muthalika ndiwochenjela wayenda kwambili uja ndiwozindikila

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 2 หลายเดือนก่อน

    Sakumwa akutero ma ujeniwa 😂😂

  • @KingsleyKunneno
    @KingsleyKunneno 2 หลายเดือนก่อน

    Koma nkhalamba izi nazo 😂

  • @83kwak
    @83kwak 2 หลายเดือนก่อน +3

    I love Malawi,let's keep praying to Lord,Jesus Christ ...........

    • @LightonKamwana
      @LightonKamwana 2 หลายเดือนก่อน +1

      Ukakamira nkhalamba.

  • @leonardmalirana7423
    @leonardmalirana7423 2 หลายเดือนก่อน

    Brian osatero, osamuyankhulitsa chibwibwi munthu, Muthalika watopa akapumule

  • @hassammaulana4529
    @hassammaulana4529 2 หลายเดือนก่อน +1

    Koma guys akuti alipomwepana ali kubuyoko

  • @EnerstBanda-m4s
    @EnerstBanda-m4s 2 หลายเดือนก่อน

    Please abale athu a Dpp tamumverani chisoni Gogo wakula munthu sangakwanitse kulamulira dzikoli ndi munthu okalamba kwambiri his a good President sibodza but tasakhani munthu weniweni wamoyo osati izizi Please mukulimbana ndi chipani choti chili m'boma kale woke up Malawians we can't continue ruled by old person 85yrs or muli serious

  • @johnchicoti
    @johnchicoti 2 หลายเดือนก่อน

    Peter wadwalika ndichifukwa chake sanabweleso

  • @JusticeKawilira
    @JusticeKawilira 2 หลายเดือนก่อน +3

    Munthu wankulu posakhalapopo sanafune zopalana pakamwazo

    • @FainessMwanza
      @FainessMwanza 2 หลายเดือนก่อน

      ❤you Peter

  • @EmmieChikuseKoreya
    @EmmieChikuseKoreya 2 หลายเดือนก่อน

    Zokalamvazo ndiye usanene iweso osakalamba iwe unkhoza kufa kumusiya okalambayo komaso kukalambako ayamba ndi mai ako ndi bambo ako

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh 2 หลายเดือนก่อน

    Peter wakula sangakwanitse kulamulira azalamulira ndi getrude ndi chisale yawo ija

  • @AnnastanziaMhango
    @AnnastanziaMhango หลายเดือนก่อน

    Sazalowaso mu boma awa nanji iwowa chaponda nde never mpaka yesu wize

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward 2 หลายเดือนก่อน

    Iwetu brain Banda ndikuwona umadana ndi dausi

  • @MahallaMinistries-fv1hw
    @MahallaMinistries-fv1hw 2 หลายเดือนก่อน +3

    Atolankhani athu suffers from a certain condition

  • @ConradccjSokoSoko
    @ConradccjSokoSoko 2 หลายเดือนก่อน

    Wadwalika ndi kutopa gogoyu.
    Siyirani anyamata. Alipo ambiri anyamatakumeneko.
    Milandu ya malibino yinathera pati, atatchulidwa ku kothi pamodzi ndi Ntaba

  • @RonnexNyezule
    @RonnexNyezule 2 หลายเดือนก่อน

    Brian ati get away tu😂 atero George 😂

  • @douglaskayira8362
    @douglaskayira8362 2 หลายเดือนก่อน

    Nice

  • @GiftBonomali
    @GiftBonomali 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂 koma Brian amanditsangalatsa❤❤

  • @violetkamvanthupi2443
    @violetkamvanthupi2443 2 หลายเดือนก่อน

    UTM my vote

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda 2 หลายเดือนก่อน

    This old party, with old experience

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 2 หลายเดือนก่อน

    Chapond sakuyankh funso mwaluz ndiy muzit ndil ndigalimot ndiy kt chiyan anthu akukanan

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 2 หลายเดือนก่อน +2

    Nothing is was wrong Muthalika posamaliza nawo zochitika..bola alemba babawo zoyankhula zawo

  • @RabeccaMkandawire-i9j
    @RabeccaMkandawire-i9j 2 หลายเดือนก่อน

    Akapume amenewa ndi amene anayambitsa quota system

  • @OwenDubbyflitz
    @OwenDubbyflitz 2 หลายเดือนก่อน

    Mbwerera zeni zeni

  • @MphatsoZintambila
    @MphatsoZintambila 2 หลายเดือนก่อน

    Mbuzi izi

  • @DavieChiwale
    @DavieChiwale 2 หลายเดือนก่อน

    Brain uzioona mikoko yogona iwe

  • @RABSONSIKELO
    @RABSONSIKELO 2 หลายเดือนก่อน

    Mr Maize gate ur wounded

  • @AlihIbrahim-s7v
    @AlihIbrahim-s7v 2 หลายเดือนก่อน +3

    Dpp yasankha bwino mipando yawo

    • @RiteRoderick
      @RiteRoderick 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo koopsa zed bro❤❤❤

  • @DjKingXuluMtenje
    @DjKingXuluMtenje 2 หลายเดือนก่อน

    Kumangoduladula mau zobowa

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 2 หลายเดือนก่อน +2

    Nice conversation

  • @MoreenSemu
    @MoreenSemu 2 หลายเดือนก่อน +1

    Akudwala Peter akungu mukakamiza

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o 2 หลายเดือนก่อน +5

    Kukalamba munthu uja ndi nkhamba

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga 2 หลายเดือนก่อน

      Kagwere uko pedegu iwe 😂😂😂 age is just a number

    • @HarrisonMwanga-xy4sc
      @HarrisonMwanga-xy4sc 2 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂😂😂 kodi 😅😅😅😅

    • @patrickmoffat9609
      @patrickmoffat9609 2 หลายเดือนก่อน

      Iwe suzakula

    • @DalitsoDjimo
      @DalitsoDjimo 2 หลายเดือนก่อน

      Zoona a mwene suti a piter niwoyipa ayi koma akamba nchito yi sangayikwanitse.

  • @StanfordMNthali
    @StanfordMNthali 2 หลายเดือนก่อน

    Chaka chino tiona maroza akariyati akupanga ubale ndi dpp ayiwala dpp amunyoza Chirima ndiposo kariyati kumbukirani mumene dpp yinamphela banja raTambala ku Lilongwe kariyati uribe Kodi Chirima anakhala kuti arimoyo mukanapita kumeko Mai opanda manyezi iwe

  • @PreciousDzonzie
    @PreciousDzonzie 2 หลายเดือนก่อน +1

    Agogo agogo agogo 2025 kotsutsa boma woooooo

    • @giftsululu4274
      @giftsululu4274 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo nkhalamba izi

  • @LightonKamwana
    @LightonKamwana 2 หลายเดือนก่อน

    Abanda muziva chisoni ndi agogo.

  • @JacklineNiwahereza-ni3pm
    @JacklineNiwahereza-ni3pm 2 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkk koma nde mwamuwonjeza chaponda kkkkkkk

  • @MaikNkhoma
    @MaikNkhoma 2 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkk yadwala nkhalamba ija

  • @RabiaNotes-ql8cf
    @RabiaNotes-ql8cf 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂Dr George Chaponda

  • @peterwhite3782
    @peterwhite3782 2 หลายเดือนก่อน +1

    ❤❤❤❤ Dpp

  • @YusufMapata
    @YusufMapata 2 หลายเดือนก่อน +1

    amuthalika akuchita kukakamizidwa kuti ayime koma munthu uja mafupa atopa popeza mtima sukalamba

    • @thomaswyson-e2q
      @thomaswyson-e2q 2 หลายเดือนก่อน

      Mafupa akalamba ndiabamboako kapeonyozamakoloako iwe mboliyakonso

  • @Lingstone-r3z
    @Lingstone-r3z 2 หลายเดือนก่อน

    Brain that is issue to close covetion,

  • @ConlardNkhoma
    @ConlardNkhoma 2 หลายเดือนก่อน

    Chipani chamagogo kkkkkk

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 2 หลายเดือนก่อน

    Sindin wadpp kom ndakondw kwambir pomuchots chapond

  • @ishmaelimani3779
    @ishmaelimani3779 2 หลายเดือนก่อน

    Khangati mitu sikugwila amalawi chomwe timachifuna sitimachidziwa

  • @charitykalulu
    @charitykalulu 2 หลายเดือนก่อน

    Kusakhalapo osati chifukwa chokula kapena

  • @MaxwellChiwaya-i8q
    @MaxwellChiwaya-i8q 2 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkk Brian Banda usadzafe udzangosowa

  • @omicloans
    @omicloans 2 หลายเดือนก่อน

    Use proper internet

  • @gradsonmayira9336
    @gradsonmayira9336 2 หลายเดือนก่อน

    Brian banda😂😂😂😂😂

  • @GavanaradagarasiDagarasi-bu6le
    @GavanaradagarasiDagarasi-bu6le 2 หลายเดือนก่อน

    Wakomoka amenewuja akudwala

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkkkkkkkk koma yah😅😅😅😅

  • @solobertkamunga2826
    @solobertkamunga2826 2 หลายเดือนก่อน

    Next time Dont post video yot ikuduladulA, azungu azititseka

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh 2 หลายเดือนก่อน

    Tizakalamba koma ngati tizizakakamila mpando

  • @JamesMpinda
    @JamesMpinda 2 หลายเดือนก่อน

    wakulu uyu avomeleze

  • @LydiaManzy
    @LydiaManzy 2 หลายเดือนก่อน

    Sokhano watha bhooo what's wrong sanabweere iyaa nawe

  • @GreyMwanyimbo
    @GreyMwanyimbo 2 หลายเดือนก่อน

    Madala team

  • @DumisanPhiri
    @DumisanPhiri 2 หลายเดือนก่อน

    Wakalamba uyu

  • @JonesManyeka
    @JonesManyeka 2 หลายเดือนก่อน +1

    Iiiii musiyeni munthu akagone