AKULU NDAKUVERANI CHISONI KWAMBILI MWAPULUMUKA KOMA MUSAYEREKEZE KUKUPUSITSANI KUTI WINA AKUYITANENISO AI MUTHERA KU MCP MWAVA SAMALANI MOYO ATALA NKHANI MUSAMANYENGEDWE NDI NDALAMAZI MOYO NFIWABWINO
Osamubvela ameneyi ndi odwala,iye amafunako chiyani akumatukwana ku ma Media?anganamupha kumene.angofuna, kuchuka,maso anthu ali pa utm UDF afford and dpp.matama,akuluwa ndi amatama, ndalama zache ziti,wachamba ameneyo.
What goes up comes down, you were arrogant telling Malawians not to protest in LILONGWE and you thought that the whole world owes you a living, remember you reap as you sow. You are harv what you planted.
Inu a UTM❤❤❤, DPP💙💙💙, Aford💙💙💙, ndi UDF💛💛💛, mumvetsere bwino audioyi mpaka kumapeto. Osatukwana msanga. Mwana otayikayu walapa.
MCP ndi ufiti weniweni inu mumasapoteranji MCP.
Amenewo ndiye ochewa a mcp mungawachitire chabwino chotani amabweza chipongwe
wausilu uyu akha manyi kkkkkkkkk appreciate 🙏 ndazikonda
AKULU NDAKUVERANI CHISONI KWAMBILI MWAPULUMUKA KOMA MUSAYEREKEZE KUKUPUSITSANI KUTI WINA AKUYITANENISO AI MUTHERA KU MCP MWAVA SAMALANI MOYO ATALA NKHANI MUSAMANYENGEDWE NDI NDALAMAZI MOYO NFIWABWINO
Akanachipambadza😂😂😂Mesa yekha amati amawadziwa nde amakataniko😅😅😅😅
Timukhululupire Amenei ? Amatelo akafuna kukupanga zinthu.Nanga mwadya zingati
😢😂😢😂😢😂😢 Akulu mwalira ngati Mkazi wosiyidwa Chibwezi mpaka wuwuwuwuwuwu 😂😂😂😂😂😂 Pamenepa Phanzi mthaandize thawani sipokhala.
PAJA UNANYOZA ASILAMU KUTI UTHETSA CHISILAMU MDZIKO MUNO. NDIYE LERO UKUTI BWANJI?
TULUKANI BRO, MWINA NDI MWAYI WANU. AWOWO SAFUNA CHILUNGAMO. Munthu kuyankhula chilungamo walakwitsa? Vuto la ndale za chi Malawi ndilomweli. ZIPANI ZONSE MUNO ZIMATERO NDITHU, KAYA ZINAKHALA BWANJI?
Iweo ndi kape alipo anatenga Colgate kumasuka nkamwa mwa mkango akutizimule kumene athu mukuzuzisa ziko lino ndinu tikutibulaso tokha akakusiya azakowo
Kd inu simukaziwa kuti mcp ndi manyi zedi muziona😅😅😅
sasamba lwe usatiuze nyasi ukufuna umve chani kwa malawi
Musatinyase phanani komko zanu izo
ndimaona ngati ndiwe dolo koma aaaaaaah za ziiiiiii
Takulandiran sunganimoyo,, masewera ndi mcp kkkkkkk
Akuchitani bwino kuti muziwe fisi saweta.
Musamuvere chisoni mkuluyu amayerekedwa kumayakhula motumbwakuopsedza azipani dzina kuti asacite mademo kulilongwe akanakutibula kukupweteka zikanatisangalatsa chisiru iwe eti manyiiiii ako
Ayitu ife yayi takukana khala komko
Basi sungani moyo wanu malume kkkkk
Pamtumbo pako. Osamangopita kunyumba kwako bwanji? Panyo pako
Amen asungani
Tulukani ma young generation ku MCP mutherako 😢
Muphana agalu Inu kkkkkkkkk panyero pano
Akufuna ndalama awa tangowapani1mta athese mavuto. Kulira mkkkkkkkk sono akazi anu nkumati akaona nkumati adadi akulira
Muthanako choncho 😂😂 chipani chokupha
Achimwene gwilani ntchito politics I'd zikhale chinthu chomslixila pa moyo wabwino
MCP ndikachani kut uzilira galu iwe😊😊😊😊
Iwe umayesa ndi chipani chabwino
Walira mokweza mwana mamuna pofikizana size iyiyi mtimad wang'ambika azipan zina khululukan ndithu wasweka mtima munthuyi wavomereza kulakwa kwake😊
Payanani uko..Ndinu Akupha Agalu Inu...How is what you are saying helping Malawi mxaa
Tchimo limabala ifa...Lapani Achimwene Kondani Mulungu osati chipani..Cjisomo chakugwerani..
Mudya ndithu
U know each other
Mukapanga masewela mumalizana mcp ndi chipan chakupha simukumva
Osamubvela ameneyi ndi odwala,iye amafunako chiyani akumatukwana ku ma Media?anganamupha kumene.angofuna, kuchuka,maso anthu ali pa utm UDF afford and dpp.matama,akuluwa ndi amatama, ndalama zache ziti,wachamba ameneyo.
Chonde mverani audio yonse musanatukwane
Wa usilu
Ukulira chiyani
Nde uzimukumba?😊
Sunganimoyo kkkk kkk uli booo
😂😂😂😂 ndinokhanokha kuthanakuthana basi iiiiii
Mwayamba kumenyanatu nokha nokha simunati. Khalani konko kwa bambo wanu ng'ona yodya anthuyo chakwera.
I hope uchila pompano 😂😂😂😂😂
Zikanakhala bwino ndiwe wamanyi kwabasi pamtumbo pako mesa ndiwe dolo
Samalani man MCP ikupwetekani komanso mukapanga masewera akuphani
Ukanati udzilire wekha ubale wake ndi mulungu ndiotani osati zomwe wachita apazi wandinyansa iwe galu kobasi
Ukufuna kum'bela ndani?
Propaganda yachabe iyi guyz, usatitenge a opposition ife ngati opusa wamvaa, akutumawo awuponda phwanga, DPP, UDF, UTM, AFFORD musamulore uyu please, wachita kutumidwa, muziwina malilidwe akewo ochita kulira ngati kamwana ka imbwa 🐕🐕 kaa
akuluwa ndi propaganda akunenai aaaa nde akuti samadziwa zimene amapanga?🤔🤔 okay any way paja ndeu yaeni savulira jeket
Akt nthima wake Wang,Ambika
Mwaona akulu bola isakhale ndale
Mudyana
Wanyatu anakakuponda umandinyasa
Uyu ndiofoila wamisala uyu
Zochitsilu zopusa ndiye ife chikutkhudza ndichani? Dziphanani ife tili pamalilo a chilima
Ndiy inu maganizo anu ali pati?😅😅
A dpp audf autm a afford musamalenaye ameneyo musatengeke mutola njaoka andale ndinu an' dede
Ndipo siunati
Kkkk km kumeneko
Awawa nde atiphadi😢
Ukunama ayise , kumene ukulowelera ine ndikuziwapo . Khalani ndi MCP yakoyo
Mcp ndi mbava Komatsu kupha anthu
😂😂😂 mulungu àmba kukukathani
What goes up comes down, you were arrogant telling Malawians not to protest in LILONGWE and you thought that the whole world owes you a living, remember you reap as you sow. You are harv what you planted.
Nkhosa yosochera yapezeka,,,ndee funso langa ndilakut muli kmwekobe ...?
Kkkkkkk woyikonda anayithawa .koma chachikhulu wamudziwa pano.
Za kubanja kwanu ife zisatikuze amwene musaipitse mbili ya mcp
Aaaaa ok 2025
Lchenjela
Yeah wuli be tchito mapwala amako iweyo ngakhale akanakuthimitsa
Kuli kanthu this is mcp brother
Iwe pita komweko ku MCP ko akutuma, tikuziwa kale, ma pran ako sagwila
Isandithere data langa nkhani yakoyi pankholo pako
No you love Evil thats period
Zaziiii akuthibule wazindikila mochedwa
Moti m paka pano simuziwabe kuti mcp ndiyapha
Iweyo kalowe Ku utm Ku MCP sitifuna anthu azibwanatu ai ndi we chisilu
Wamisala iwe
Now that God has rescued you mkamwa mwa Ng'ona think twice
Achitsilu inu Bola akanakuphani tikanasangalala a Thailand kuwili inu
Galu iwe
Ukufuna ulowe kuchipano china iwe akutuma kuti udzawonongeko
UPEPESENSO ASILAMU
Muyamike akusiya amoyo akolo
Bodza iliiii
Siyani ndale
Chipaniicho ndichokupha iwenso uli mugululo zakoizo
A brother ndi achisilu
Nde titani
Judas!
Simudapambane zisankho ayi
uli ndi thawi dala iwe
😂😂😂😂😂😂😂
Mphanani Ng,Ona zonkha zonkho
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Shem sorry brother
Kkkkkkkkkk zaugaki
V😂😂
Muphanako kkkkk
😂
Eya amakupha ndinzako kumene Chilima anamulakwila chani Chakwera zabwino zonse anamuchitila zija mphoto yokampatsa ikhala imfa
You have been castigating people who were talking about MCP.
Uwu ndi mchenga mu mpunga