CHINSINSI CHAKUGWIDWA KWA KALIATI KOMA CHIMENECHI - UWU NDIYE TIMATI UMODZI💪💪

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 23 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 48

  • @DanielTwiscombewe
    @DanielTwiscombewe 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +2

    😂😂 apolisi mufela ndalama zot simukwanitsa kuzidya mufela kukakamiza kt dziko likhalebe lovutika ok tiyeninazon

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +2

    Mugwiri zano ndiomwewo ,dpp,aford 🎉🎉,watching from johnnsberg

  • @VioletMbale
    @VioletMbale 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +4

    Chi usi iwe ukutaniko kunyumba? Pa 17 iwe suuzakhala wa utm manyazi

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +3

    MCP kuti mupeze mtendere mumange aliyense osusa osaiwal inenso ndiosusa mukudziwa kale zimene mukupangazi palib chopindula koma minyama yokha yokha

  • @JosephHill-fy1bb
    @JosephHill-fy1bb ชั่วโมงที่ผ่านมา

    UTM, DPP, AFFORD bomaaaa!!!!!

  • @RoseChimbwefu
    @RoseChimbwefu 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    I see we are going to one party system Malawian we must be careful eshiii

  • @DigleDafter
    @DigleDafter 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Yooh yooh 😢 Malawi okomera tonse unja alikuti lero ndiolose ndikakutafune palibe chosatha 😢

  • @OwenchangnyaMkandawire
    @OwenchangnyaMkandawire 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Mcp ndizitsiru za anthu.anazolowera kupha anthu amenewo.mademo basi kuotcha tima police stations tonse.

  • @TelezaManyela
    @TelezaManyela ชั่วโมงที่ผ่านมา

    koma apolice ntchito yanu simukuyidziwa pano mwangolowa kutumikira chipani chomwe chikulamula,osati anthu koma mulungu akuwona zosezi tsiku ndi limodzi

  • @johnjoachim3820
    @johnjoachim3820 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Police 😊

  • @JamesChiphazi
    @JamesChiphazi 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ife kumalawi pheeeee kusuzumila pa zenela kuyang'ana siku lamovoti koma uyelekeze kibbela ndikudula mabatile

  • @GidionLufani
    @GidionLufani 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +4

    Palibeso kubisa mwanganya ameyo

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Eeesh

  • @TimothyKabumbuKendrix
    @TimothyKabumbuKendrix 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Nthawi yakwanatu yamademo guys more fire osaopa, osaopa komanso osafooka.

  • @YusufKazembe-po6qo
    @YusufKazembe-po6qo 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Iwe galu Michael Usi ndiamene wapangitsa

  • @ElsaMalunga
    @ElsaMalunga 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Amipingo mulikuti mukufuna mpaka muyakhule anthu atafika pakuphana aPac mwatani chani moti simukuona zosezi km ndarama guys snapanga aaaaa hiiiiiiiiiiiiii manja kt buuuu kalulu nkanyama kochejera km kamanyedwa ok

  • @WakisaNjeghenje-i2n
    @WakisaNjeghenje-i2n 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Wina sakuziwa kut akaluza kucovion akufuna asokoneze basi😅😅😅MMM koma

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Manganya ameneyo ndiyemwe akuziwa kanthu akuwopa kukaluza komvetion

  • @ClementMakasu
    @ClementMakasu 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Amasulidwe

  • @GetrduNamacho
    @GetrduNamacho 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Manganya ndiwe d
    Galu kwa basi

  • @Kelvin-hj5qv
    @Kelvin-hj5qv 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Km manganya AYI ndithu ukulakwa ukufuna uchiphwasuliletu chipani chaa UTM km ukunama SKC anapanga mistake kusakha iweyo bwanji

  • @VictoriaWilliam-ms2ft
    @VictoriaWilliam-ms2ft 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Manganya ndi chakwera mukutenga dzikoli ngati lanu eti

  • @DanielTwiscombewe
    @DanielTwiscombewe 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Apolisi ngat mulibe tiyegas okwanila ulendo uno mukatenge tiyegas ngat matumba achimanga ngat mukukagawa malawi yonse cifukwa eeeee,mwaojeza

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Walila mokweza mzimayi olalata uja kuno

    • @JeanKambala-gm1zr
      @JeanKambala-gm1zr ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Siolalata Koma chilungamo inu

  • @FlorenceBanda-w5s
    @FlorenceBanda-w5s 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Chomwe chikufunika tizigopephera bas marawi wayaka

  • @MACDONADLITIA
    @MACDONADLITIA 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Tinaziona kale izi nthawi ya Bingu atamangidwa Atupele Muluzi ku Lilongwe komweko athu anagona ku police

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma guys ulamuliro sumatengera mphamvu,,,asiyeni amalawi kuti asankhe zofuna zawo,,,azitsogoleri asiyeni amalawi apange zofuna zawo,,,felony ndichani?

  • @PhalesNotta
    @PhalesNotta 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma manganya ukuziwa kut ufti umene ukuchitawo skulina zizakuvwerera wekha ndi chikangawa wakoyo anthu oyipa kwambiri inu uzikumbukira kut chilima kut aphedwe una panga plan ndiwe wemwe apanso wapangisa kut mai kaliati amangidwenso ayi zkomo

  • @ColleenChidimba
    @ColleenChidimba 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Ndipo aka kayudasi sikaliyoti kamanganya mm sakuchita bwino ayi bwanji pa Malawi mm kwanyanya

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ine nkadakonda area 30 itangootchedwa bansi

  • @AbdulMalik-o7n1q
    @AbdulMalik-o7n1q 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Usi kapena kuti manganya timiyendo tatifito ukhale ku MCP komweko akutuma chakwelako waona kuti sakulephela kutenga chipani kupititsa kwa mfiti akoo

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Mzapita mzomwezo kwa Mulungu just because of world material ur busy for nothing

    • @WakisaNjeghenje-i2n
      @WakisaNjeghenje-i2n 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      @@ShamimuBisani sukuziwa kut yesu analila kamba kandale?

  • @Rose-wu5ef
    @Rose-wu5ef 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Kaotchen police pls

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Eti kudzangoiotchapo area 30 yo basi

  • @PetrusTlhokwane
    @PetrusTlhokwane 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Tiyeni titumize zinjoka zambiri zikazuze mumaofesi apolisiwo bwanji tiyeni afiti tose tigwile ntchito utsiku uno

    • @ShamimuBisani
      @ShamimuBisani 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      @@PetrusTlhokwane kkk osaiwal.mwala.ngt Goliat anafa chfukwa chmwal

    • @ElizabethMulinde
      @ElizabethMulinde 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂ayi zikomo

    • @HabrilMalaya
      @HabrilMalaya 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂

  • @VitumbikoKaunga
    @VitumbikoKaunga 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Nde mbuzi zina zizikavotera manganya ku utm please Malawi segurani maso

  • @martintivalenji320
    @martintivalenji320 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    This is very sad

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Manganyá kulibe 😂😂😂

  • @GriffinAziziSokoh
    @GriffinAziziSokoh 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma sikukhala kwa bwino kumeneko

  • @ChisomoSaiti
    @ChisomoSaiti 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Tikubwela komko kudzayamba mademo

    • @shadreckphiri1799
      @shadreckphiri1799 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Nthawi ya mademo yakwana

  • @JoshuaNyirongo
    @JoshuaNyirongo 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Comrade Timothy Mtambo... where are you?

    • @honmitrus
      @honmitrus 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ali komko