Uthengau upite kwa brother nthanyiwa auze boma la ku South Africa ko kuti dziko lawomo mwalowa zifwamba zochokera Ku malawi zabwera ndiupandu. Nde muziwauza madera. Omwe Ali azifwambawo apolice awangire akaponye chakulinderako azikalima masamba tizigula mashop mu asazatulukenso chifukwa akutengela phamvu kumanja powaona kupusa eni dziko nde anthanyiwa musankhale nchisoni ndi crocodile pple agwidwe basi komweko uthengau ugwirisireni ntchito kuti akamangidwa ena atengereppo phunziro
Anthu awa asatidanitse amphawi ife ndi dziko la south Africa mu south Africa ndikumene tikupezelako thandizo lathu tikumakwanisa kusamalila makolo ndi ana kumamiziku ndiye inu aboma chepesani za chibwanazo muzipanga ku mudzi Koko kuno ayi tikupondani tikakuziwa tikufinyani ndithu akunkuyu samalani chifukwa mwatulusa maso ndi chipani chanu mutha kufa ngati nkhandwe wokuba nkhuku musamale koma
DPP sikuti inalinso ya bwino mulakwisa kwabasi. Utsogoleri wa DPP kapena MCP sitikuufuna ata pang’ono koma utsogoleri wa masomphenya a Dr Saulos Klaus Chilima
AWAWA GUYS AKANGOFIKA MU JONZ MUNO AKAMABWERERA ABWERERE ATASINZINA , ASABWERERE AMOYO IFE TAGWIRIZANA NDI MA ETA TIKANGOWAPEZA TIKUWAVEKA MA TAYALA NKUOTCHA TIKANENA KU POLICE KUTI NDI ZIGAWENGA ZACHOKA KU MALAWI KUFUNA KUDZASOKONEZA DZIKO LINO, ASIYENI A BWERE TIKUMANA KONKUNO
Alemba mmadzi amenewo olo akamapereka R2000 ifekuno ku Johannesburg sitingachite za kanunduzo. Azibale athu kumalawiko akuvutika kaamba ka boma lonunkha mcp
Ndipo tikumva pain heavy
❤🎉 mbambande iweyo umakwana ntanyiwa keep it up
Tell them Comrade
Tipha kuno 💪💪💪
Uthengau upite kwa brother nthanyiwa auze boma la ku South Africa ko kuti dziko lawomo mwalowa zifwamba zochokera Ku malawi zabwera ndiupandu. Nde muziwauza madera. Omwe Ali azifwambawo apolice awangire akaponye chakulinderako azikalima masamba tizigula mashop mu asazatulukenso chifukwa akutengela phamvu kumanja powaona kupusa eni dziko nde anthanyiwa musankhale nchisoni ndi crocodile pple agwidwe basi komweko uthengau ugwirisireni ntchito kuti akamangidwa ena atengereppo phunziro
Ndipo azikalimadi masamba kunoko asabwele
🤔big up big♥️💪💪💪💪✊✊✊✊✊✊🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Tanguwawombela komweko afele komweko akuwononga ndalama za amalawi
Anthu awa asatidanitse amphawi ife ndi dziko la south Africa mu south Africa ndikumene tikupezelako thandizo lathu tikumakwanisa kusamalila makolo ndi ana kumamiziku ndiye inu aboma chepesani za chibwanazo muzipanga ku mudzi Koko kuno ayi tikupondani tikakuziwa tikufinyani ndithu akunkuyu samalani chifukwa mwatulusa maso ndi chipani chanu mutha kufa ngati nkhandwe wokuba nkhuku musamale koma
Akunama amenewo tikangowadziwa akumana ndi ma tsotsi kunoku
Zilipo njira zina zamwamuna zooneka zoongoka koma tsiliziro ake ndi imfa anzathu tsogolo palibe munthu ukamafa umayamba kugontha mkutu ndizo zikuchitikazi
Shaaaaa km ndaramadi iripaminga et
Tiwagwira kuno ayerekeze kuyambiya kuno Pretoria comrade #MCP must gooooo!!!!!!!
Man mukutiyimilila and tikudziwa zambili kuzela mwa inu pitilizani
Awomberedwako chabe kuno!! Asamaletu other wise apita opanda moyo!!
Great ntanyiwa
Ayitu Mr Ntanyiwa inuyo simugwidwa mulungu sakulola anyapapi amenewa kut akwanilitse zofuna zawo nthawi yawo yoyaluka yakwana mudzingowayang'ana
Mr Ntanyiwa mmatiimirira monga ife amalawi omwe tiri panchombo penipeni pa Johannesburg tikukupemphanikuti tazizutseni zipani zosutsa kuti zizipanga zochirimika pa ground kuti boma lokuphali lichoke
Mkhuku imeneyi mukiyifuna ?
Ndikuyidziwa pamene imakhala.
Ndikakuwonetani pamene imakhala
DPP sikuti inalinso ya bwino mulakwisa kwabasi. Utsogoleri wa DPP kapena MCP sitikuufuna ata pang’ono koma utsogoleri wa masomphenya a Dr Saulos Klaus Chilima
You are one of the wise, just & intelligent people.
Ndipo sitikwanitsa achepaaa
Palibe chochitika mulungu ali nanu cholinga
AWAWA GUYS AKANGOFIKA MU JONZ MUNO AKAMABWERERA ABWERERE ATASINZINA , ASABWERERE AMOYO IFE TAGWIRIZANA NDI MA ETA TIKANGOWAPEZA TIKUWAVEKA MA TAYALA NKUOTCHA TIKANENA KU POLICE KUTI NDI ZIGAWENGA ZACHOKA KU MALAWI KUFUNA KUDZASOKONEZA DZIKO LINO, ASIYENI A BWERE TIKUMANA KONKUNO
Timakondwera nanu a bwana
Kod anthu akunyamuka ku malawiwo ayenda pa bas ? Ngat ili bus tiziwisen kut ndi bus yanji
Mr Ntanyiwa Kodi ifeso timaika ma comment zikhale ng'oma atigwilaso😢😢😢