Bon Kalindo Ndi Guru lake la Malawi first ayankhura izi pamene anapangitsa press conference lero

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 27 ส.ค. 2024

ความคิดเห็น • 172

  • @user-mg5yy5hk9t
    @user-mg5yy5hk9t หลายเดือนก่อน

    Anganga Alula malawi fist member all the way from mangochi mamatiyimilira mr big man keept up mangochi yosaopayo

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน +8

    Ndipo athu inuyo tchito mukuigwila mulungu azikusungani ndi moyo maka Mr boni kalindo simutopa mwamangidwa kambili mbili mukanakhala wina bwezi mutatisiya ife athu osauka sikuti ndinu Muthu ovutika ayi koma mumasiya pogona pabwino zakudya zabwino kukagona Malo onyasa chifukwa Cha ife aphawi kuzipeleka m,sembe pokhapo mulungu adzikudalitsani ❤❤

    • @RiyemaDomybusiness
      @RiyemaDomybusiness หลายเดือนก่อน +1

      Exactly 💯💯 bon amatiyimirila ampwawi

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน

      @@RiyemaDomybusiness sure tidziwapephelela ndithu athu amenewa

  • @VungaQueen
    @VungaQueen หลายเดือนก่อน +9

    Boni Kalindo munthu wotiyimilira 🔥🔥🔥

  • @Moses51
    @Moses51 หลายเดือนก่อน +3

    The Dc bon kalindo keep up update 💪💪🇲🇼🇲🇼💯 osawopa

  • @user-ez8uk7py8n
    @user-ez8uk7py8n หลายเดือนก่อน +3

    That is true it needs all Malawian to vote as long as he/ she is Malawian Mr president keep continue loving your poor people abd our country Malawi proud of you thanks

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj หลายเดือนก่อน +4

    I respect your Mr nkalindo together with Malawian fest and the cautrry everyone DC is so powerful as well and you are always welcome to our team of Malawi wholld my Allah bless you always about the what happened with Malawian

    • @esaMoha-dm4kj
      @esaMoha-dm4kj หลายเดือนก่อน

      I am a Malawi but now I'm in the sauth Africa estan about working on

  • @WysonJalamu
    @WysonJalamu หลายเดือนก่อน +8

    Big up the DC osatopa, osafowoka, osawopa malawi ndi wathu uyu, tili limodzi pa nsewu basi.

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g หลายเดือนก่อน +9

    Please please ife TIKUFUNA ufulu wathu wovota a MCP asauchotse ponamizira ma id, aliyense akuyenera kukavota popanda id

    • @Franklifo2217
      @Franklifo2217 หลายเดือนก่อน

      Nzelu mulibe enanu! Anthu omwe mumalephelesa malawi kutukuka🙌

    • @hudycorex1893
      @hudycorex1893 หลายเดือนก่อน

      Inu amzeru kwambiri?​@@Franklifo2217

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c หลายเดือนก่อน

      Anzeru ndinuyo? ​@@Franklifo2217

  • @MussaHassani-zg1hm
    @MussaHassani-zg1hm หลายเดือนก่อน +1

    This is our president kalindo thanks so much for your help Malawias

  • @DavieBinzih
    @DavieBinzih หลายเดือนก่อน +1

    More fire mr kalindo we proudly of you keept up we love you

  • @YousufMpunga
    @YousufMpunga หลายเดือนก่อน +3

    Ndine Yusuf wakumangochi kmnso amalawi amene Ali kumaiko akunja apasidwe mwai wovota kuchokera kunja konko kumene ali

    • @patrickmacheso5062
      @patrickmacheso5062 หลายเดือนก่อน

      That's true, we need to vote and choose the President that we want not this Manyaka Government, but the problem is Akazembe athu sathandiza or kuwapempha kuti atipatse mwayi ovota.

  • @WezzieChimuzi-ek7bk
    @WezzieChimuzi-ek7bk หลายเดือนก่อน +1

    Good job my people Ambuye azikutetezelani ndi mwanzi wawo nthawi zonse ..

  • @user-uf4db7im7d
    @user-uf4db7im7d หลายเดือนก่อน +1

    This government must go

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q หลายเดือนก่อน +1

    yaa wa mcp ngati akunyasidwa ni boni karindo asavere khani zake ayi chonde ife anthu osauka tiyeni tizimuvera boni koma uzayime iwe boni tizakuvotere

  • @user-uf4db7im7d
    @user-uf4db7im7d หลายเดือนก่อน

    Every malawian should be in a possession of ID, If the NRB is failing to reach all malawians for ID registration, you should expect Malawi to be on fire, because voting results will not be accepted, People have rights to vote for who they want not rigging.

  • @FrankSpison-o7o
    @FrankSpison-o7o หลายเดือนก่อน

    The Dccccccc Booooooooon kalindo inu nde anthu oti mzika zamalawi tizikupemphererani kwambili 🙏

  • @NellieKabvina
    @NellieKabvina หลายเดือนก่อน +1

    Pa ziphatsopo ndie zikudabwitsa zikupezeka kuti anthu ambiri akumadziwa tsiku lokuti akumaliza kupanga ma ID,,,sakulengeza tsiku loyamba anthu ambiri akudandaula

  • @harrisonlowheat6569
    @harrisonlowheat6569 หลายเดือนก่อน +1

    My president

  • @RemaniNkhoma
    @RemaniNkhoma หลายเดือนก่อน +1

    boni karindo tingopita mawa bwanji pa sewu kuti agaru awa tiwakhawurise

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 หลายเดือนก่อน

    Lets presure dem evo!....aluta continua!

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e หลายเดือนก่อน

    Good move Malawi First ❤

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj หลายเดือนก่อน +1

    I respect your nkalindo bisid ashankwela and everyone else has been in the path of mcp I don't respect anyone anymore because the people who keep and keeling Malawian people 2025 mashall Allah bless you nkalindo 😮😮😮

  • @ChristopherMadulira
    @ChristopherMadulira หลายเดือนก่อน

    Congugulations Mr DC ntchito mukugwila anthu inu only God bless you ❤❤❤❤❤

  • @AnussaAlli
    @AnussaAlli หลายเดือนก่อน

    Big up the DC Bon kalindo continue timakunyadlan❤❤❤❤❤❤🎉🎉

  • @jogechawa6192
    @jogechawa6192 หลายเดือนก่อน +2

    Bon Kalindo and malawi first our hope basi

  • @dawsonwaya4722
    @dawsonwaya4722 หลายเดือนก่อน

    Za ziiiiiiiii munthu unalephera kuimirira constituency ndiye ukati amalawi osauka aaaa zangokuvutani Moya, .

    • @robenallie6985
      @robenallie6985 หลายเดือนก่อน

      Ndizako zimenezo dc number 1

    • @FatimaAyami
      @FatimaAyami หลายเดือนก่อน

      Vuto ndi bomalo iyeyo amangopanga imprement

  • @OdettaLowrence
    @OdettaLowrence หลายเดือนก่อน

    Ulemu wanu Mr Born 🙏🙏🙏🙏

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z หลายเดือนก่อน +1

    Boni karido ndikatundu

  • @SamKaposa-i5c
    @SamKaposa-i5c หลายเดือนก่อน

    Viva malawi first Richard mphepo umadziwa kuyankhula more fire dc

  • @Okalekale
    @Okalekale 25 วันที่ผ่านมา

    Tikufuna tidziwe kuti ndi ndani amapanga sponsor gulu lanuli Mr.Kalindo?.The nation should know if you claim to advocate for transparence.

  • @BacklinebwanaliBwanali
    @BacklinebwanaliBwanali หลายเดือนก่อน +2

    Akupatsen moyo was utali

  • @user-dq9oe8sp8k
    @user-dq9oe8sp8k หลายเดือนก่อน

    Ifetu though tilibe ma ID kma tikazavota
    Angoona kuzinamidza agwapewa
    Fireeee the DC❤

  • @KeftonChimaliro
    @KeftonChimaliro หลายเดือนก่อน

    Iyayi zonsezitu akupangazi akufuna ndalama mtambo samachitaso chocho anango kuwapatsa zochita ndikungokhala duuu osayakhulaso amalawi anthuwo ndi amodzi Lucia's. Anayimba kale

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer หลายเดือนก่อน +5

    Wa mcp ngt born kalindo amakunyasa usamaver nkhan Zak iwey ndy opanda zelu ife tikufuna dziko libwerer ngt kal osat mukumakambo shem on you 😢😢😢😢

    • @KhalidwePentani-c6q
      @KhalidwePentani-c6q หลายเดือนก่อน

      Iwe ndamene ukava ngat ine mbuz izi za duuu

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 หลายเดือนก่อน

    Well done guys kpt up

  • @YohaneChitapini
    @YohaneChitapini หลายเดือนก่อน +1

    Mumakwana ndipo ndinu nokha boss ndagwada ndikumvesela

  • @MikeKoloko
    @MikeKoloko หลายเดือนก่อน

    Mumatiimilira, big up

  • @usherjamson174
    @usherjamson174 หลายเดือนก่อน

    Mulungu azikhala namu guy's 💪💪

  • @MercyJohnsonkanchure
    @MercyJohnsonkanchure หลายเดือนก่อน

    Mr Kalindo Mulungu azikupansani zeru zakuya ngati Solomon ❤

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo หลายเดือนก่อน

    Never give up guys let's see what happens

  • @ShariffAbdul-m9t
    @ShariffAbdul-m9t หลายเดือนก่อน

    I salute you

  • @TiyamikeMakande
    @TiyamikeMakande 28 วันที่ผ่านมา

    Mumatiuankhulira ndinu bwana ,mutiyankhulireso za ndrama za masiye ku Capital hill Chaka chino nchachitatu ndrama sakutipatsa tikuvutika ndi ana

  • @RanaQari-py4bd
    @RanaQari-py4bd หลายเดือนก่อน

    Mumakwana guys we love you all the time 🙏🙏🙏🔥🔥🔥🔥

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q หลายเดือนก่อน

    Malawi first all the best u are representing poor people. To be honest Malawi is the poorest country in the world our leaders are selfish we are going backwards.

  • @AlidWidon
    @AlidWidon หลายเดือนก่อน

    Wosawopa bon kalindo tili limodxi 💪💪💪🔥🔥🔥👆👆

  • @AndrewNyondo-ut3gk
    @AndrewNyondo-ut3gk หลายเดือนก่อน

    King David bon kalindo the DC❤

  • @lastonkandiyado4526
    @lastonkandiyado4526 หลายเดือนก่อน

    Respect 🎉🎉🎉

  • @HarrisonMangani
    @HarrisonMangani หลายเดือนก่อน

    They need to address those issues other wise Mmmmm panunkha mphira

  • @nelsonmhango7515
    @nelsonmhango7515 หลายเดือนก่อน

    Inu ndi king

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl หลายเดือนก่อน +3

    Pick up guys chilungamo ndimwano

    • @patrickmacheso5062
      @patrickmacheso5062 หลายเดือนก่อน

      Ndimayesa ngati mukhala kumbuyo kwa a name anu kkkkkkkk let's fight together, this country is belongs to all Malawians not MCP only.

  • @RanaQari-py4bd
    @RanaQari-py4bd หลายเดือนก่อน

    🙏🙏🙏🙏🙏 Thnx good work

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 หลายเดือนก่อน

    The DC ❤

  • @KhalidwePentani-c6q
    @KhalidwePentani-c6q หลายเดือนก่อน

    Zopanda ntchito izo akalindo mumangofuna udindo ngat mungakwanitse kutumikila dziko aaaa zawumbuli

    • @Mervic-vm8eo
      @Mervic-vm8eo หลายเดือนก่อน

      Wa MCP pamtu...

  • @ImanRashidi-so4oo
    @ImanRashidi-so4oo หลายเดือนก่อน

    Congratulations mr DC

  • @GodisoneNoel
    @GodisoneNoel หลายเดือนก่อน

    Asirikali achirendo muzikorathu zichepe mr DC

  • @GetrudeBanda-sd1yf
    @GetrudeBanda-sd1yf หลายเดือนก่อน

    Only GOd Bless you DC

  • @MuhammedNtaba
    @MuhammedNtaba หลายเดือนก่อน +1

    ❤❤❤ The DC

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r หลายเดือนก่อน +2

    Akumangeni ngati mwaphwanya malamulo dala mbuli

    • @kenmasta
      @kenmasta หลายเดือนก่อน

      Ndiye mmene akumamumangamo ndiye akumamupeza ndi milandu yanji,,,,..ndaletu zisakusokonezeni mchimwene andale amabwera amapita koma Malawi adzakhala yemweyu ndiye let's love Malawi.

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r หลายเดือนก่อน

      @@kenmasta mwanena nokha awa asiyeni koma akanalankhula zinthu zambili ndi za against popeza ine ndinapanga nawo compain ndiye sanandipatse udindo awona, zimenezo ndi zabodza,chikuwawe sichimanga dziko amwe awa ndi a ndale musokonekera sayamika ndi ankhwidzi amafuna zawo ziwayendere kalindo akudya makobidi inu mukudya nawo 🤗🤗 ayi so bola yesu

  • @user-dy5bj9ck5e
    @user-dy5bj9ck5e หลายเดือนก่อน +3

    The DCCC

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli หลายเดือนก่อน

    Good move bafethu salute you

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 หลายเดือนก่อน

    Point of correction not guru lake koma Born kalindo ndi guru la Malawi 🇲🇼 first

  • @YohaneChitapini
    @YohaneChitapini หลายเดือนก่อน +1

    Guys inu musazafe mulungu azikudalisani

  • @PempheroMoleni
    @PempheroMoleni หลายเดือนก่อน

    Firr the DC

  • @EliasMcray
    @EliasMcray หลายเดือนก่อน

    Go go ahead

  • @AnockyDavidd
    @AnockyDavidd หลายเดือนก่อน

    Congratulations to all

  • @gracetjomane-jj3ib
    @gracetjomane-jj3ib หลายเดือนก่อน

    Kutundu uyu the DC❤❤❤❤❤❤

  • @SueWahna
    @SueWahna หลายเดือนก่อน

    Big up Malawi first 💪💪

  • @Fridayasani
    @Fridayasani หลายเดือนก่อน

    Osawopha Bon kalindo tikukupembela kwamulungu Kuti anzikala nawe kwina kulikonse komwe udziyenda

  • @ambeweburton
    @ambeweburton หลายเดือนก่อน

    Timenyeleni nkhondo please mulungu imvani kulira kwathu

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e หลายเดือนก่อน +1

    ❤❤❤❤ guys

  • @PetroMatias
    @PetroMatias หลายเดือนก่อน

    Amarawig fct muri nbi mfunbo zabwini timakuyamikirani

  • @InnocentKavalo
    @InnocentKavalo หลายเดือนก่อน +1

    Zoona big umakwana dc

  • @Malambia
    @Malambia หลายเดือนก่อน +1

    Mr kalindo ulemu wanu

  • @ritchardchakuma5725
    @ritchardchakuma5725 หลายเดือนก่อน +1

    Apomwayikwanisa maiko enasaziwa Chichewa pakufunika ayaluke mbavazi 💯🔥🔥🔥🔥🔥

  • @kurhikhoza8298
    @kurhikhoza8298 หลายเดือนก่อน

    Tipiya pa sewu akapanda kuyakha

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z หลายเดือนก่อน

    Zikomo boni karindo umatiyimilila big Kom amalawi sitimayamika

  • @user-dy4gc2hr5e
    @user-dy4gc2hr5e หลายเดือนก่อน +1

    Good move

  • @AgnessChiwalo
    @AgnessChiwalo หลายเดือนก่อน

    Your good man bon

  • @LukaJaulanchirwa
    @LukaJaulanchirwa หลายเดือนก่อน +1

    You people you thinking harder that is good Diction thank chakwera is not thinking

  • @chikoko-uj2tt
    @chikoko-uj2tt หลายเดือนก่อน

    Salute 🫡 The DC

  • @ntandokazindzwana3083
    @ntandokazindzwana3083 หลายเดือนก่อน

    Fire fire tili pa mbuso pa malawi oyambirira

  • @JafaliAjusa-zg2xi
    @JafaliAjusa-zg2xi หลายเดือนก่อน

    Respect Mr

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm หลายเดือนก่อน

    The DC'S mwana woooopsa kwambiri chilungamo chiyende ngat madzi.

  • @AgnessChiwalo
    @AgnessChiwalo หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤ good news

  • @shephardlonex3371
    @shephardlonex3371 หลายเดือนก่อน

    Booooooooni kalindo

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo หลายเดือนก่อน

    Go konko bwana DC❤

  • @HajaSande
    @HajaSande หลายเดือนก่อน +1

    Zikomo kwambiri umawona patali

  • @PreciousKARINGANIZA
    @PreciousKARINGANIZA หลายเดือนก่อน

    Tilikomweko

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj หลายเดือนก่อน

    Following with all my chidwi

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 หลายเดือนก่อน

    I'm sure, the government you will grant our request

  • @MaryNgola
    @MaryNgola หลายเดือนก่อน +2

    Mmene wafikira Malawi alipodi amene akumamuona uyu kt akupanga zolakwika? Iweyotu wa MCP nkana akukubowa

  • @shephardlonex3371
    @shephardlonex3371 หลายเดือนก่อน

    Munene kuti ife ngati A Dpp

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤💯💯🔥🔥🔥

  • @RitaKainga
    @RitaKainga หลายเดือนก่อน

    Auzen anthu adyerawo amve ndithu

  • @JoshuaNyirongo
    @JoshuaNyirongo หลายเดือนก่อน

    Go konko..

  • @user-hr6dj4xc8l
    @user-hr6dj4xc8l หลายเดือนก่อน

    Koma mukuvutikatu kwambiri, munayambilira muja

  • @user-ru6fc3qy5n
    @user-ru6fc3qy5n หลายเดือนก่อน

    Zilibwino kwambili osaopa

  • @kashmirmohakashmirmoha8659
    @kashmirmohakashmirmoha8659 หลายเดือนก่อน

    Ulemu wanu DC😊😊

  • @ShadreckChimaimba-l9y
    @ShadreckChimaimba-l9y หลายเดือนก่อน

    Kunoso kwachitika zodabwitsa kunkhoma

  • @ShadreckChimaimba-l9y
    @ShadreckChimaimba-l9y หลายเดือนก่อน

    Osatopa big