Nduna Iyi Anzake Sakuikonda... Chifukwa Cha Izi .. (Amalawi Ali Akondwa)

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 1 ก.พ. 2025
  • #malawi

ความคิดเห็น • 89

  • @InnocentGomani-b9n
    @InnocentGomani-b9n 7 วันที่ผ่านมา

    Amumba continue doing a good work , indeed your were chosen to stand before us by God. May God keep on blessing you and give you healthy life. Osafoka, osasintha gear up and osatopa😂

  • @PeterMakaika
    @PeterMakaika 11 วันที่ผ่านมา +1

    Dunayi sikulakwitsa koma...anthu tikuzuzika dziko lathu lomwe...Mr Mumba keep it up ❤️ ❤️ ❤️

  • @MdalaBonomali
    @MdalaBonomali 11 วันที่ผ่านมา +1

    Ineyo ndikugwirizananawo anduna amenewa ndipo pempho langa anthuna musalole anthu ena kukupatsani chinbansi chifukwa nduna zinzanu zizikukondwa nanu chondechonde anduna pitilizani ntchito yabwino we love you so much ♥️ ❤❤❤

  • @JamesLeonardhowa
    @JamesLeonardhowa 9 วันที่ผ่านมา

    Ziribwino❤❤❤ yekayu borako

  • @tobymarshall1624
    @tobymarshall1624 10 วันที่ผ่านมา

    Excellent anduna !! A true Malawian citizen !!
    Amen.. & Amen !!

  • @FynessBotha-i5p
    @FynessBotha-i5p 10 วันที่ผ่านมา

    I love you Mr nduna good job

  • @JonathanChibaka
    @JonathanChibaka 10 วันที่ผ่านมา

    Samu ndakunyadilaso chifukwa suyang'ana mbali koma chilungamo like you first

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 7 วันที่ผ่านมา

    God bless you vitumbiko

  • @shabanLoleni
    @shabanLoleni 10 วันที่ผ่านมา

    He is a good examples of ministers who have nominated all these years

  • @enockrobert
    @enockrobert 11 วันที่ผ่านมา

    Bwana Mumba your doing a good Job......

  • @OwenBandh
    @OwenBandh 10 วันที่ผ่านมา

    Good

  • @ChilangizoKajiyabanda
    @ChilangizoKajiyabanda 11 วันที่ผ่านมา

    To be honest he is doing great job

  • @IvyKangwere
    @IvyKangwere 8 วันที่ผ่านมา

    this guy ili bho.ndipo ndizomwe zikufunika kt anthu obwerawa asamatizunze ife okhala amalawi.

  • @MwaleYankhoKatanga-w9h
    @MwaleYankhoKatanga-w9h 10 วันที่ผ่านมา

    May God enlarge his territory,ziiilii bwinoo kwambiri apitirizeee

  • @JosephMunthali-v8c
    @JosephMunthali-v8c 10 วันที่ผ่านมา

    We more of these leaders

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 11 วันที่ผ่านมา +1

    Chifukwa akupanga zokomela a Malawi one osati a MCP okha ayi anthu omwe akufunika pa Malawi ndi ameneyu Mumba keep it up..

  • @shabanLoleni
    @shabanLoleni 10 วันที่ผ่านมา

    We need strong ministers like him not poor ministers who are hunting the corruption

  • @jonathanmteko-vj1to
    @jonathanmteko-vj1to 11 วันที่ผ่านมา

    He is doing a good job. Keep it up honourable Minister.

  • @JafarFrank-u6q
    @JafarFrank-u6q 11 วันที่ผ่านมา

    Vitumbiko wayimba bho kwambiri please continue ❤🎉

  • @CharlesChibisa
    @CharlesChibisa 7 วันที่ผ่านมา

    This what Malawian's want

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b 10 วันที่ผ่านมา

    Mumba ntchito imene Mulungu anakupatsa ndiimenei Amalawitu tikuzunzika moti ena atenge chitsanzo pa inu mbiri yabwino iposa chuma

  • @GeraldBiliat
    @GeraldBiliat 11 วันที่ผ่านมา

    Nchito yabwinokwabiri osati ndunazinazi zogonazi zopondereza Malawi kukonda anthu obwera!!

  • @BishopEdward-n9k
    @BishopEdward-n9k 11 วันที่ผ่านมา

    Ameneyo ayamba bwino ndithu apitilize kutero kuli nyasi kuja kuno mulungu amupase mphamvu ndi nzeru vitumbiko Mumba

  • @GeoffreyElias
    @GeoffreyElias 11 วันที่ผ่านมา

    Well done an continue

  • @mayahIntias
    @mayahIntias 7 วันที่ผ่านมา

    Time up mwachedwa nazo mukanayamba 2020 komaso mupite ku migration ndi road traffic tapangani zimenezo

  • @brianuladi9549
    @brianuladi9549 6 วันที่ผ่านมา

    🎉

  • @LuciusKhudze
    @LuciusKhudze 10 วันที่ผ่านมา

    Aa mmene ndaganizira ine ngati M"MALAWI a president akanapangitsa cabinet meeting awaphunzitse ma ministers ena mmene akuyenera kugwilira ntchito. 85% yanduna atati azigwira ntchito modzipeleka chonchi ayindithu bwezi lDziko lathu lilipena pake. Pomaliza ndingoti Enginer v, Mumba pitirizani ntchito ya bwino, Aliyense amene angabwere kwayinu kufuna kukupatsani chiBANZ MANGENI BASI.

  • @RoseMchenga
    @RoseMchenga 11 วันที่ผ่านมา

    Ambuye anutsogolere asafooke a Malawi tikuzunzika chifukwa cha umphawi

  • @PaulVictory-m5o
    @PaulVictory-m5o 11 วันที่ผ่านมา

    the best minister ever in chakwera administration,tikanakhala ndi nduna ngati izi chakwera could have delivered.

  • @innocentmaloya8348
    @innocentmaloya8348 11 วันที่ผ่านมา

    Nzeru zikubwela chifukwa tikupita ku chisankho

  • @MaxwellKantondo
    @MaxwellKantondo 7 วันที่ผ่านมา

    Uyu akutha

  • @WillyDUX
    @WillyDUX 11 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤❤❤

  • @ConradccjSokoSoko
    @ConradccjSokoSoko 9 วันที่ผ่านมา

    Minister MUMBA apitilire ku onetsetsa anthu ogwira ntchito peze zofuna zao

  • @BrainsLastain
    @BrainsLastain 11 วันที่ผ่านมา

    He is fit. May God comfort him

  • @AHAMADUJRAminie-c6q
    @AHAMADUJRAminie-c6q 11 วันที่ผ่านมา

    Congratulations to him😊

  • @PatrickHalineck-n8q
    @PatrickHalineck-n8q 10 วันที่ผ่านมา

    Angokhala president wa malawi basi

  • @AkwendaKelemesi
    @AkwendaKelemesi 11 วันที่ผ่านมา

    Iyi...ndiye..nduna ..tikufuna

  • @kenkelunkybanda
    @kenkelunkybanda 11 วันที่ผ่านมา

    Akuchita bwino kwambiri ,dziko ndi lathu anthu obwera asamatizunze pamene tikuwapangira ndalama ma company mwawo

  • @kelvinwilliam960
    @kelvinwilliam960 11 วันที่ผ่านมา

    Good work, koma kutengela ndi umphawi ku malawi akuyenera kupanga consider Anthu ogwila ntchitoyo kamba koti anthuwo ngakhare kukumana ndi zovuta pa ntchitopo koma amapezabe cholowa after payment.

  • @chipinkolola42
    @chipinkolola42 11 วันที่ผ่านมา

    Izi nde zofunikazo

  • @MACDONADLITIA
    @MACDONADLITIA 11 วันที่ผ่านมา

    Uyu ndiye Malawi akufunika

  • @JohnMosiwa
    @JohnMosiwa 8 วันที่ผ่านมา

    nduna koma vitu

  • @JonathanChibaka
    @JonathanChibaka 10 วันที่ผ่านมา

    Tiyeseko achinyamata maunduna awa mwina zingasintheko

  • @JaneMoyo-b7i
    @JaneMoyo-b7i 11 วันที่ผ่านมา

    Nduna iyi ikugwira ntchito yotamandika🎉🎉

  • @peterwadi1774
    @peterwadi1774 11 วันที่ผ่านมา

    Vitumbiko mumba my favorite,,,akugwiradi ntchito yake not zinazi

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 11 วันที่ผ่านมา

    Congratulations mumba

  • @ArafateDiquissone
    @ArafateDiquissone 11 วันที่ผ่านมา

    Anthu ife timadana ND usogolery umene suguira chito yake mokwanila mosangalasa Anthu amene ukuwasogolera,paVitumbiko zikutheka.

  • @StarfordDyton-n8u
    @StarfordDyton-n8u 11 วันที่ผ่านมา

    Akuchita bwino

  • @JonathanChibaka
    @JonathanChibaka 10 วันที่ผ่านมา

    Vuto lalikulu unduna amasankha nkhalamba yoti sangayendele company yayikulu mwina zimango nthela ku office basi

  • @ZiwaniKatita
    @ZiwaniKatita 11 วันที่ผ่านมา

    Akugwira ntchito bwino kwambili pasapezeke bora asalandile chi Baz

  • @WarriorKB-l3i
    @WarriorKB-l3i 11 วันที่ผ่านมา

    Eyaah nkhani njakuti ntchito yomwe akugwilayo anthu tikuyiona pamene acina chimwendo ndi nduna zi zake palibe cipanga iwo nde chifukwa cake

  • @ChifundoZibelu-v2f
    @ChifundoZibelu-v2f 9 วันที่ผ่านมา

    Ndikufuna DDP izakutenge paundunawo umaziwa kungwila ntchito tinakakhala ngati ameneyu zikoli bwezi likuyenda bwino koma muona ena opondeleza amupasa ndalama kuti asiye kuchita zabwinozi.

  • @gerladmoyah5525
    @gerladmoyah5525 11 วันที่ผ่านมา

    Komano vitumbiko akugwira nchito kuposa chakwera na ku mcp anayenera kukhara president ndi ameneyu osat mbuzi zinazo zinazo zikungoziwa kutukwana kumanga ndi kuba bas

  • @WillardChimimba-z4o
    @WillardChimimba-z4o 10 วันที่ผ่านมา

    Ukutima kugwila ntchito

  • @BiliatiJoâo
    @BiliatiJoâo 10 วันที่ผ่านมา

    Nyela ndi chibwadwidwe uyu alimbo apitilize kunyendela

  • @ThomasMGamah
    @ThomasMGamah 11 วันที่ผ่านมา

    Bodza iwenso nduna zanji zomwe zikumuda vitumbiko tchula dzina ka

  • @VeronicaSekobi-is6dk
    @VeronicaSekobi-is6dk 11 วันที่ผ่านมา

    ❤🎉

  • @GenialaChalera
    @GenialaChalera 11 วันที่ผ่านมา

    Uyu ndi munthu woti chakwera adakamusankha kale bwenzi zinthu Zina zili bwino

  • @SaniJonathan
    @SaniJonathan 11 วันที่ผ่านมา

    Vitumbiko wabwera bhooo hvy

  • @Bonisiwentamo
    @Bonisiwentamo 11 วันที่ผ่านมา

    Uyuyu amene kusatila Sulaiman tikuyamikila athu otelewo papa chakwer Ana yitha posakha mbumba Kukhala nduna

    • @PatienceMphuche
      @PatienceMphuche 11 วันที่ผ่านมา

      Great Job a minister God bless you a Malawi azunzika nthawi yaitali

  • @BillyKondwerani
    @BillyKondwerani 11 วันที่ผ่านมา

    Muthu km amene ndamene angasithe zi2 zopusa zomwe zimachitika ma company

  • @AnipherChirwa
    @AnipherChirwa 4 วันที่ผ่านมา

    Ipatse moto

  • @SidreckRashid
    @SidreckRashid 11 วันที่ผ่านมา

    2025 akanayimila ameneyu

  • @DanielMjasten
    @DanielMjasten 11 วันที่ผ่านมา

    Nduna iyi ikudziwa chomwe ikuchitazi osati kimagokhala kunyuma ndikumadya ndalama za mphawi

  • @lindahgracesepeti767
    @lindahgracesepeti767 11 วันที่ผ่านมา

    Awawa akufunika kukhale a president unduna wawachepera

  • @hashimmtelera9536
    @hashimmtelera9536 11 วันที่ผ่านมา

    Vitumbiko ndi olemera kale,envelop yo azaikamo zingati zomupanga convince?

  • @andrewchimwaza6029
    @andrewchimwaza6029 11 วันที่ผ่านมา

    Uyu akugwila ntchito koma Bola asasiyile pomwepaa

  • @BrownMainje-sh7hj
    @BrownMainje-sh7hj 10 วันที่ผ่านมา

    Ndye matindi anduna kapena ai

  • @BiziweckThumpwa
    @BiziweckThumpwa 11 วันที่ผ่านมา

    Vitu ndi mbambande

  • @WittinessNkhokwe-q7h
    @WittinessNkhokwe-q7h 11 วันที่ผ่านมา +2

    Mumba pa pick

  • @judithStuwart
    @judithStuwart 4 วันที่ผ่านมา

    Or wangamutinkha mwana wakhwithu,wagwire waka ntchito yake

  • @ChrispinPhiri-x4l
    @ChrispinPhiri-x4l 11 วันที่ผ่านมา

    Zofunika

  • @OretarbadrBwanali
    @OretarbadrBwanali 11 วันที่ผ่านมา

    Munthu amene amadana ndichilungamo which means kut iyey ndiwanyengo

  • @standwellstaman3904
    @standwellstaman3904 11 วันที่ผ่านมา

    Engineer

  • @KenzoTrywell
    @KenzoTrywell 11 วันที่ผ่านมา

    Kumbali ya kawalazi yokha sanalakwitse 100%

    • @IanPhuka
      @IanPhuka 11 วันที่ผ่านมา

      Vitu. moto buuu wandikumbutsa nthawi ya Kamuzu Banda.

  • @cmsanyama200
    @cmsanyama200 11 วันที่ผ่านมา

    President Vitumbiko Mumba

  • @JessyChidanzi
    @JessyChidanzi 11 วันที่ผ่านมา

    Mulungu ndp aziwadalitsa abwana awawa

  • @ImranWyson-e9o
    @ImranWyson-e9o 11 วันที่ผ่านมา

    😊😊

  • @BoivybekingMh265
    @BoivybekingMh265 11 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂

  • @JafarKhalid-f6q
    @JafarKhalid-f6q 11 วันที่ผ่านมา

    Pazokhazi wandiwaza mumba

  • @liftedphiri2735
    @liftedphiri2735 11 วันที่ผ่านมา

    idiot's only will think his bad but anthu akwathu apindula so spot think like idiot's

  • @EvanceMaster-v5o
    @EvanceMaster-v5o 11 วันที่ผ่านมา

    A mcp onse akanakhala kuti amagwila ntchito bwino chonchi zikana beba koma osati kungokhuta nyemba kamangeni chisale wamwa thobwa ayi kamangeni gangata what is that stupid

  • @junasssabiwa1996
    @junasssabiwa1996 11 วันที่ผ่านมา

    Munthu woyipa

  • @ChimwemweIdanaMasiye
    @ChimwemweIdanaMasiye 11 วันที่ผ่านมา

    Lnduna izitelo a are aaaah avitumbiko Mulungu awadalise