Chawez ukufuna mp ku blantyre city east uzitenge bwino coz anthu aku bt akukumva ukudzipanga wekha de campaign,,, uzibaya mmaso wamva uzitenge bwino kuno sikwa mcp,,, deusi nawenso ukufuna mbali yomweyo play ur cards well OK??? Museseleka muona
Chawez iwe sukuziwa kuti ku MCP kulibe ufulu waiwala kuti ku MCP ukangoyakhula kuti mundisiyile nane ndiyimileko anafa ndichikangawa waiwala iwe bolani ku dipipiko anthu sakufa amasiyana bwinobwino
mutharika atupele muluzi adatiuza ife amalawi kuti mukasanga mcp mavuto siizi kodi amalawi manyi akutinyela achakwera palibe chimodzi akudziwa pangani yoyendetsa dziko ndiye chifukwa chake chinachilichonse mmalawi muno chili upset down because we choose arearner to drive along distance that was abig mistake we have done
my vote MCP 🗳 ❤❤❤
I will vote for mcp
Agree or not...there are some grains of biasness here..
Achisiru achaweziwa.
Chawezi amalakhula ma wise okhaokha more 💥💥💥💥
Onse DPP and MCP had no opposition to leadership. No Democracy.
Program ya makape sadic miya mesa munaphaso ndye mukulubwalubwa chan apa ana agalu inu
Ngati Pali program ndia zisilu ziwili zimenezi
Kuphunzila kwa kuno ku Africa ndi memory chabe saziwa kupanga zinthu koma amasungila zomwe anaphunzisidwa kuchoka ku America
Chawez ukufuna mp ku blantyre city east uzitenge bwino coz anthu aku bt akukumva ukudzipanga wekha de campaign,,, uzibaya mmaso wamva uzitenge bwino kuno sikwa mcp,,, deusi nawenso ukufuna mbali yomweyo play ur cards well OK??? Museseleka muona
Kodi program imeneyi amene amapanga sponsor ndi chipani cha mcp eti mukutinyasa kwambiri
Chawezi uzinverako mzakoyo,,ukumafotokoza kwambili wekha
Victor amayankhula bwino kusiyana ndi uyu wa Chikangawa party
Za zii
Zot Chawezi awina ndakaika,kamunthuka ndka MCP,komanso program iyi ndadana nayo
Zoona munthu kukhala Dr koma saziwa za mankhwala kapangidwe kale koma kukumbukila kapelekedwe ka mankhwala basi
Chawezi Get out
Usova dpp boma 2025
Wadya zambiri za MCP
Chawezi ndimamuwona ngati ndi mutumbuka wa nzeru koma ayi chisilu cha chabe chabe wozikonda basi
Amafuna azikusangalatsa Iweyo ? Kuti Iweyo wagwira ntchito yanji . Chokhacho chongotchula kuti Mtumbuka , Iweyo waonetsa kuti ndiwe watsankho , komanso wopanda nzeru
Mcp idabwela kuzakhala ndiposo palibe zoluza ndiposo tidakoza kale zobera ngati mene amabera a dpp
Osamamvera program yi
Ndipo ndasiya, nyasi
Zikubeba
uyuyu chawezi banda ndi wa mcp mboloyako chitsilu galu ife amalawi taonetsetsa for sure kuti mau akulu amakoma akagonela
Nanga angapikisane ndi Chikangawa ndani?
Koma chawezi u can talk the truth ,times television inaluza munthu
Victor chipofya alikuti
Boma ndilomweli coma president tikusitha
Osamuopsyeza chawez Mwamva Chawez ndi munthu ophunzira vwino amaziwa zomwe akuyankhula
Kodi iwe ukulimbana ndi muthalika bwanji chakwela bwanji kunalibe ofuna kupikisana naye
Chawezi 2030 uzagwila ntcĥito mu state house ntchito ija Brian banda analepherà
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Chawez iwe sukuziwa kuti ku MCP kulibe ufulu waiwala kuti ku MCP ukangoyakhula kuti mundisiyile nane ndiyimileko anafa ndichikangawa waiwala iwe bolani ku dipipiko anthu sakufa amasiyana bwinobwino
Chawezi iwe umalandila ndalama Za MCP kape iwe
Koma buns imene wadya Chawezi kodi yellow buns kapena chani? Achakwera analephera kumusoyira mnyamata Chilima, ma buns akuwononga atolankhani.
Akulu nkhani ndi usogoleri osat zanuzo
Chawezi mukulakhulira izi chifukwa cha kwiyo yoti anakuchotsa ntchito ku mbc............zako izoo
Chakwela alindizaka 65 wapangachani chothandiza amalawi chawezi uzingonyopola ndalama zaku MCP ufune usafune APM akulamula next year
Chawezi wa MCP
Chawezi wa Mcp galu uyu
Ndipo ine amandinyasa ndale zake amafuna kampando kena kake
Ndalama za MCP zikukoma Achawez 😢
Nanga peter akachezera sakagona uku anthu akanva mikonono ya munthu wamkulu
Chawez ndimbuzi yamunthu
iyeyo chakwera ngati ankanenadi zimenezo ndiye kuti ngwabodza nanga bwanji wamupha chilima mnyamata amene amalawi ambili timamudikilila mmalo mwake amalawi ambili taonakuti chakwera ndi mutharika it's better mutharika abwelele pampando akonze dziko limene agalu akuba amcp aliwononga
Inu mavizi amanu
Chawezi machende ako
Achawez nd a MCP
mutharika atupele muluzi adatiuza ife amalawi kuti mukasanga mcp mavuto siizi kodi amalawi manyi akutinyela achakwera palibe chimodzi akudziwa pangani yoyendetsa dziko ndiye chifukwa chake chinachilichonse mmalawi muno chili upset down because we choose arearner to drive along distance that was abig mistake we have done
What is MCP then 🤷
Mutharika ndi wamtendere
Programm yonse kunthera nkhani yofoira ngt imene ah or kuika nkhani zoti zitukule dziko ah
Inu simunaphe chilima chifukwa champando wa president
Chawezi tikudziwa zonse kuti ndiwe wa MCP, ndipo mmutumwako munazadza mwazi nde palibe ungatiuze .zaku DPP zisakukhudze iwe ndi mbuzi .zoti APM analengeza kuti wapuma pa ndale ,npomwe enawo ankaonesa chidwi sudziwa? Koma anthu atamupempha APM kuti awaphule pa moto wa MCP nde enawoso akanakaimila chifukwa chani? Munya muyankhatu milandu mukuopayo tikakuchotsani pampando
Chomwe achawez mmawaikira pama problem sindimachidziwa chifukwa amayankhula zofoira always
achawezi bambo anu atakalamba ana siya kukusamalani ndinu achitsiru
Dzadziii,dzotsakoma
ndiwa mcp
I like this program chawez mulungu akusunge
Ndiye mwati mudziyankhula kuti adapita, adaona, adali, tidaona, etc kuti mysanduke achewa kuti akukondeni? Heeede!😂
Vote for MCP ❤️🔥❤️🔥❤️🔥❤️🔥 2030 woooooo!!
Pansana pako ase
Ndipo ndiwe opusaaaaa aise abale Ako sakuvutika iwe
Sikupusa koma ngati ndizopangilana ngati opusa ndiweyo kaya
Iweyo ulibe sana eti
Ambuyakoo
Kachilingamo kamabaya moti ena akutukwanani mmalo molakhula fundo mungodziwa kuti chalungamo kabaya
Munthu ukakalamba you lose memory.Zinthu azichita kukumbutsa.Ndiye wina wozongulira mutu kumati Apm 2025 boma.Akagwere uko.Dyera basi.
Chawezi ngati wadyetsedwa badzi dzidya ndinkadziwako osatiife chilima alikuti katitengele chilima timvotele osati chakwerayo ife tatopa naye 50kg maize K55000 galu iwe ndithu😮
Tchende lako chawezi
Chawezi amayankhula chilungamo
Chawezi ukandiona utave. Ulibe nzeru ngati tate wako Kamuzu analysis kupha anthu nikuaponyera kung'ona. Choka apo mwana wam'fwiti. Palibe kanthu udziwa
Bro chawezi banda sure supsatila umafotokonza ngamo akwiye akwiye.
Ng'ona party
Idont like this program
Chakwera ndi wonama, ananama kuti achita resign after 2years
Chawezi ndi dolo
Mutharika ndi Ntaba amatafuna malibino sangawine misozi ya athu alibwino singalole
Iwenso unkadya nao ma alubinowo ndie kt
@@mercybiziweck pita ku court u will gate file of Ntaba and your APM not my Name
Chawezi ndiwe business ya muthu wadya za malawi kogolise iwe waziwa kuti ddp gulu wamuthu
Chawezi samandiwaza
this guy is very biased
Nanga Chakwera wachichepele apanga chani kumalawi?komanso dziwani kuti ngati panalibe wodzutsa zanja ku MCP kuti apikisane ndi Chakwera pa undindo wapulesidenti ndichifukwa choti amawopa kuphedwa ngati chilima,ngati iyeyo Chakwera amalola anthu kupikisana nawo bwanji sanasunge lonjezo la pakati pa iye ndi Chilima kuti wina aliyense azalamulira 5yrs?,pamwamba posasunga lonjezo wamuphanso,ndiye muziti Chakwera wabwino amalola anthu kupikisana naye pa upulesidenti?.Sadiki Miya anali wachiwiri kwa Chakwera ndipo anangomwalira mwazidzidzi,Chilima anali wachiwili wa Chakwera naye wangomwalira mwadzidzizi,pano pali Manganya,muzandifunse ngati manganya atafike 2029 ali moyo
Akupempha kuzakhala n'neneli ku state galu uyu
Chawezi amanena zowoona zokhazokha
APM akuladii alikuti achichepele at 85 next year is a shiiit
Akulu inu mulibe nzeru, omwe ali ndizaka zochepezo akupanga chan? Ndiomwewotu aliyika dziko pa moto. Iwe nde ulibe nzeru wadya zambiri za mcp galu iwe
Mutharika siwowopsa chakwera ndi satana wakupha
Chawezi banda mwana wakwithu ❤
Gati akupasa ndalama mcp igodya ndalamazo anthu akuvutika tikufuna iPhone mcp ndipo ddp ikalowa tizasiyila anyamata tingofuna kuchosa nyasi zilipozi
Machende ako chawezi mbole yako peter kod anakulakwira chani
Chawezi umakondera Congress
Alamulirabe mutharika ufune usafune
Chawezi ndiwe galu achinyamatawo akupanga chani kwawo ndi kupha ndi kuyendayenda ndi wumbava basi
Iwe machende amako wava cadet mboli yamako refugee
@@henryhenry6632 iwe Mavi yako na yakwadada wako chimbuzi chaminokusi
@@marryphili5419 panyin pamako kapolo, cadet machende ake peter munthalika nyelo zanu ma refugees
Pamusundu pako pavigawenga imwe munapha chilima ndiwe chikangawa
@@marryphili5419 chilima inamupha ndi nyin yamako
Ku mcp anthu sanafune kupikisana ndi chakwera kuopa kuphedwa chakwera ndi wakupha
Komatu Pali fundo mwa a nyamatawa muzawavomereza ku mtsogolo
Chawezi khala chete iwe suziwa kanthu
Iweyo usavote uvotere chakwera wakoyo
Chilungamo ichi
Chawezi ndiwe galu
Panyero pamanu
Chisilu cholezera pa program chi Chawezi zopusa basi ndisiyaso kuvera bwande
Chawez machende ako umalimbana ndi dpp bwaji panyelo pako
Dziko silingasunthe bcoz of zaka za munthu Mutharika might be old but his ideas are fresh and needed for Malawi's progression
True Malawi can become Singapore within a year lol
CHAWEZ WAYAMBA JUJIYA YA PAINIYA