Limpopo Vuu Ntanyiwa akatele watulukila ndi chi program chija nkhani ya lipoti ili umu

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 5 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 309

  • @IsaaclBanda
    @IsaaclBanda หลายเดือนก่อน +16

    Ine nili ku Zambia koma nkhanga zaona sinipeza bwino ngati sininainvere.Comred ntanyiwa ni best

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b หลายเดือนก่อน +24

    A Mcp ankawona ngati akamudzimitsa Chilima nde kuti Mcp idzalowanso osadziwa kuti mpamene akutero po akudzichotsera mbvoti Pena tikhonza kumanena kuti Mulungu analora dala kuti zimenezi zichitike

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i หลายเดือนก่อน +5

    Muli boooh Mr mtanyiwa. I love you so much all team for Limpopo fm

  • @JuniorHala-vf9ov
    @JuniorHala-vf9ov หลายเดือนก่อน +6

    Ndiliphe kuno ku Pretoria ndi ntanyiwawu Kaya ena amamuda koma ine nde ummmmm I like this guy ndingot malawi first yonse

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b หลายเดือนก่อน +16

    Antanyiwa inuyo Mulungu anakonza mumatiyimilira lemu wanu❤❤❤❤❤

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d หลายเดือนก่อน +12

    Chakwera pokupha Chilima amkaona ngati azawina koma sizitheka apa anadzikalasila makala amoto heavyyyyyy

  • @Anni00Zungu
    @Anni00Zungu หลายเดือนก่อน +27

    More fire ntanyiwa mumatiyimilira keep it up

  • @HashimNyirenda
    @HashimNyirenda หลายเดือนก่อน +7

    Mulungu samaoneka ndimaso koma pamene ife tikuyenda or pamene takhala timakhala naye limodzi,
    Moti onse amene anapanga chipongwe chimenechi MULUNGU awaika pampalanganda.
    Shaaaaa ulemu wanu bigy potiziwitsa za lipotili Amen

  • @ListerBarsonBanda
    @ListerBarsonBanda หลายเดือนก่อน +8

    Ndizovuta kuti oyipawa kuti akupange chipongwe Ntanyiwa.coz mulungu wadzusa inu bigger kuti mupulumuse dziko lamaliwi all the best God bless you with more protection 🙏 🙌 anthu oyipa sasukunika ku malawi 🇲🇼

  • @user-hs4bm2yj8r
    @user-hs4bm2yj8r หลายเดือนก่อน +9

    Mtanyiwa the pangolin original, keep it up the good work brother man ❤

  • @RachelNkhoma-vn2jo
    @RachelNkhoma-vn2jo หลายเดือนก่อน +10

    mbambande padziko lapansi palibe chinsinsi mbali yakuno chinsaru Cha mkachisi chang'ambika tiyenazoni a Ntanyiwa ,wabisala mbatata msana ukuoneka aona moto a Mcp

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b หลายเดือนก่อน +8

    Kkkkk kkkk more fire man of God kumanga Mulungu asiyeni awakanthe😂

  • @HanaNyasulu
    @HanaNyasulu หลายเดือนก่อน +7

    Ndipo ine sindipuma bwino ndikapanda kunvera nkhanga zaona❤

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki หลายเดือนก่อน +9

    😂😂 😅😅😅😅 comrade inetu since morning ndakhala ndikufufunza nkhangabzawona osayipeza

  • @JohnChiwaya-ym5me
    @JohnChiwaya-ym5me หลายเดือนก่อน +4

    Mtanyiwa umakwana,,, We are proud of you!!,
    You are out and clear kuno ku BT , ku quarry

  • @SaidiAdamu-c6i
    @SaidiAdamu-c6i หลายเดือนก่อน +8

    Takunyadilanj a ntanyiwa mwatulukila coz m'bale wathu akasowa kwa 2 days tikumakhala ndi nkhawa coz agalu a mcp wa akutamangatu eeey

  • @HafsaAbwanali
    @HafsaAbwanali หลายเดือนก่อน +6

    Akangopita Ku German nkhanira imeneyo pibwerera Army mulande dziko ndikuzamangira pa airport akalowewe kundende life in prison kukanakhala Ku chilembenzo kwanthu chachisilamu tikanapanga sharia law aphedwe ,Koma asilikaliy dzukani musagone izi zachitikadzi zausatana ooopsa ndipo anandinyasa mene anali Ku chikokobe kumangochi kumanena kuti ati abale anthu akuziwa kuti anawapha lero siizi chifunga chapita dzuwa latuluka zaulira nde ati bwanji pamenepo☹️

  • @christinachikadza3760
    @christinachikadza3760 หลายเดือนก่อน

    Listening from Capetown South Africa.
    Keep the good work Mr ntanyiwa

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 หลายเดือนก่อน +9

    Big up yomweyo Chikangawa

  • @collinsbanda8024
    @collinsbanda8024 หลายเดือนก่อน +2

    More fire 🔥 ntanyiwa we love love you all the way from south Africa 🇿🇦 ❤️ 😊

    • @PeterMillimbo
      @PeterMillimbo หลายเดือนก่อน

      Timakunyadilani a Limpopo FM komano nchifukwa chiyani asilikari athu sakukhala mbali yowateteza anthu?

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm หลายเดือนก่อน +1

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer หลายเดือนก่อน +3

    Km chakwera mpak kumupha chilima chifukwa cha kufuna kuimas upulezitent km chakwera ambuye akuchitire chifundo chifukwa uli chabe ulibe zelu ulipo ndipo iwey uzafa ngt mbalame sure ndakwiya nawe chakwera shem on you, chakwera must go 😭😭😭😭😭😭😭💔💔💔💔💔💔

  • @spargomw
    @spargomw หลายเดือนก่อน +3

    Mr Ntanyiwa koma mumaseka mopweteketsa moyo😂😂😂😂😂 Chakwera akamavera Limpopo i think thukuta limayenda kuchokera kumapazi kupita kumutu😂😂😂😂

  • @PhilipMatolino
    @PhilipMatolino หลายเดือนก่อน +14

    Mbambande comred ntanyiwa 🔥

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w หลายเดือนก่อน

    Ntanyiwa mumakwana, ndipo Limpopo FM ndi radio mbambande, No.1

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy หลายเดือนก่อน +5

    Osamvela nkhanga zaona mtima umawawa ngat chibwenzi Chako chatha 😂😂😂

    • @TakondwaSaidi
      @TakondwaSaidi หลายเดือนก่อน

      😅😅kungozuka timafikira Popa ntanyiwa oyeeee😅

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h หลายเดือนก่อน +1

    You are the best ❣️❤ Limpopo FM ndi radio yokha imene amalawi wonse amayikonda and we need report from black box ✊

  • @james-zd2nz
    @james-zd2nz หลายเดือนก่อน +2

    chilungamo chiyende ngati madzi opha mzake nayenso aphedwe watching from jhb

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj หลายเดือนก่อน +3

    Mtanyiwwa ulemu wanuw km ndili ndi fuso bwanji ashankwela ankuyenda ndi amey yonkwana 4000 km shikangawaw anatumisa andu 8 onka bwanji sinankalla bwanji

  • @blessingcharo7669
    @blessingcharo7669 หลายเดือนก่อน

    Mumakwana keep it up

  • @FatimaBakali-v7q
    @FatimaBakali-v7q หลายเดือนก่อน +6

    Mfiti za mcp, asilikali akanangowalandapo dzikoli agalu amenewa miyezi yatsalai

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os หลายเดือนก่อน

      Ndipo inuyooo!!!

    • @viennasamuel2976
      @viennasamuel2976 หลายเดือนก่อน

      Asilikali akumalawi sangalande boma ngati momwe anachitila azimbabwe iwalani zimemezo

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os หลายเดือนก่อน

      @@viennasamuel2976 Ndipo mukunena zoona Asilikali aku Malawi mmmmmmmm ndi amantha koma kuzunza anthu mu njira zina ndiye amatha.

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 หลายเดือนก่อน +1

    Omenyela ufulu a original akumalawi ❤😂😂 Ntanyiwa ❤

  • @AliceJere-k9v
    @AliceJere-k9v หลายเดือนก่อน +1

    Ut reminds me of king Nebuchadnezzar...anazionatu ulemerero wa Mulungu utamuchokera.... from King to nobody kutchire mmmmhu

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole หลายเดือนก่อน +3

    Km nyimbo ya kayin ya kumapetoko ndiyoopsya kwambiri ndiyokhudza ngakhale mfiti imene ikhoza kufa ndi chikumbumtima.

  • @crosbeygondwe5403
    @crosbeygondwe5403 หลายเดือนก่อน +2

    Comrade Ntanyiwa akubwela mwa coming 😂😂😂😂😂

  • @JessicaManda-zm1ug
    @JessicaManda-zm1ug หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkkk😂😂😂😂 chikangawa woyeeee satana achite manyazi sure more fire 🔥

  • @fedson2050
    @fedson2050 หลายเดือนก่อน

    Choyambilira tiyamika mulungu maka chifukwa cha Team iyi tikuti Limpopo Fm.
    Ndipo mulungu emweyo apitikire kugwira nanu ntchito imeneyo
    Tikowa mu Bible psalms 54 vs 17
    Ves ilili ligwire ntchito pokutetezerani pogwira ntchito yanu Sir Comred

  • @HalimaDamiano
    @HalimaDamiano หลายเดือนก่อน +5

    Ntanyiwa moto kuti buuuuuu

  • @user-yu4np2wq4s
    @user-yu4np2wq4s หลายเดือนก่อน +1

    Ifetu Moni taulandili ndithu timakunyadilani ntanyiwa kwambili 👍👍🔥🔥

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj หลายเดือนก่อน +1

    Mbambande Limpopo FM ndi ntanyiwa
    😂😂😂😂😂😂😂❤❤❤❤❤🙏🙏🙏🙏
    Yomweyo chikangawa

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg หลายเดือนก่อน +1

    Palibe chinsisiiii padziko lapansili
    All evil plans back to the sender in Jesus christ name
    Limpopo with Comrade nthanyiwa woyeeeee

  • @LindaMakalani
    @LindaMakalani หลายเดือนก่อน +1

    Ine popanda kuvela comred mdimadwala kip de gud job God protect you en guide u aswel

  • @user-bi6pb5gc8t
    @user-bi6pb5gc8t หลายเดือนก่อน +4

    Kkkkk koma kumeneko chikangawa kunotu kuzomba tamuonesamo ground yonse anangokhalapo ndizibwenzizawo basi anyela agalu amenewa

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d หลายเดือนก่อน

      Ndipo ulemu wanu mwachita bwino galu ameneu ndipo mulungu amukathe

    • @PaulineKamwana
      @PaulineKamwana หลายเดือนก่อน

      Zomba mumatha ndazikonda kobasi zomwe munampanga chikangawa​@@user-eh1mg3ww6d

    • @viennasamuel2976
      @viennasamuel2976 หลายเดือนก่อน

      Mwaitha

  • @AlexHenere-r6l
    @AlexHenere-r6l หลายเดือนก่อน +2

    Asilikali pangani njira zimene mumapanga dziko ndilofunika lilandidwe mmanja MWA anthu away ndi okupha

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona หลายเดือนก่อน +1

    Ndalama akugawazo ndi za eni wake Amalawi kuzidya basi Koma Chidziwe mchipande powomola
    Maumboni ayambe kuoneka pa kusankha Ma khansala.
    Chikangawa boys you Will pay for what you did.
    Mwazi wa anthu 9 mwausamba thupi lonse.
    COMRADE NTANYIWA keep it up, keep moving🏃🏃

  • @macdonaldkorea2928
    @macdonaldkorea2928 หลายเดือนก่อน +1

    Ntanyiwa WOYEEEEEEE mukutiimilira ife olirafe, mcp yayaluka, amadutsa m'mbali

  • @IgienacioPhiri
    @IgienacioPhiri หลายเดือนก่อน +2

    Akangonyamuka galu ameneyo kupita ku German kwakeko tiyeni panseu tonse mademo😊

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope หลายเดือนก่อน +1

    Kulakwa chakwera,,,,Ku Germany komwe akupitako kwapitanso amalawi ena amagulu omenyela ufulu nde ka akukapanga chiyani

  • @ThomasStephan-tg6ng
    @ThomasStephan-tg6ng หลายเดือนก่อน +3

    Inu Malawi fest mulengeze kuti pofika siku lakuti mupeleke 1 wiki kuti chakwera atule pansi udindo

  • @NoelBambala
    @NoelBambala หลายเดือนก่อน

    Mmakwanira a mtanyiwa ulemu wanu onse❤❤❤❤❤

  • @PollyLysonLutepo
    @PollyLysonLutepo หลายเดือนก่อน +1

    Ambuye apitilize kukudalitsani. Ndikukutsungani ndi moyo a Ntanyiwa. Ndimakunyadilani. Pitilizani ntchito yomwe mwayiyamba. Chilungamo chioneke. Don't give up.

  • @TakondwaSaidi
    @TakondwaSaidi หลายเดือนก่อน +1

    Aziyenda ma midzi Mo sinanga anthuwo alibe ma fn sakuziwa zomwe zikuchitika😮Koma Muthu amene Ali fn data angamunamize

  • @user-eo2hl9ug1h
    @user-eo2hl9ug1h หลายเดือนก่อน +2

    Antanyiwa....musatisiye...Mulungu..azikuyanganileni❤

  • @user-hs4bm2yj8r
    @user-hs4bm2yj8r หลายเดือนก่อน +2

    Asilikali please akanyamuka galu ameneyu, please a silikali take the office of President please

  • @user-qq1uj7ct6n
    @user-qq1uj7ct6n หลายเดือนก่อน

    Mulungu amve ma pemphero athu.. ulendo akupita Ku Germany aziwone mudzina la chiwanda chakecho.
    Amalawi chonde tiyen tizuke ngt ma Kenyan. Tiyen pa nseu😢😢😢😢😢😢

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 หลายเดือนก่อน +1

    Limopo FM Ntanyiwa imakuyenera kwambiri ❤, it suits you bro, keep it up bro

  • @ganizanimanyamba
    @ganizanimanyamba หลายเดือนก่อน +1

    More fire mr, comred ntanyiwa iweyo ndikatundu waboma olopano Brain banda pa times akunamano pale pale fisianadyamkazake🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @SaidiAdamu-c6i
    @SaidiAdamu-c6i หลายเดือนก่อน +4

    Komaditu nane ndimazifusa kuti kodi chazulo ntanyiwa bwanji

  • @DonexNasenga
    @DonexNasenga หลายเดือนก่อน +1

    Osamaiwala bambo avick ku cape maclrear ku dwale muziziwaso kt amikonda kwambili amavela daily nyamata ameneyu

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona หลายเดือนก่อน +2

    Come on mr muthwanyiwa bwela nayoni nkhani yonse timakunyadirani

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji หลายเดือนก่อน +1

    Matiyimira Mr Mtanyiwa ulemu wako

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o หลายเดือนก่อน +2

    Awawa antanyiwa penapake mutu wawo sugwira chifukwa pamene aku German amafika amati amene azapange kafukufuku saziwa chilichonse angowatenga ku butchery pano akut atulusa lipoti lenileni chifukwa chakwera akupita german kukakambanawo Kodi tinve ziti ,iweyo ndiwedi munthu waboza ndipo la 40 likukwanila chitsiru iwe

  • @GoodsonfahardMaganga-qc2qk
    @GoodsonfahardMaganga-qc2qk หลายเดือนก่อน +2

    Ulemu Wanu mumatiyimilira inuyo ndithu ❤

  • @user-oj5ye6bj9q
    @user-oj5ye6bj9q หลายเดือนก่อน

    Morefire boss mtanyiwa mpaka amve kutentha afit amenewa

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i หลายเดือนก่อน

    Ambuye pitilizani kusunga moyo wa antanyiwa ndiwose amenene akufunila ziko lomwe munatipasa zabwino musalole oyipawa kuti awononge myoyo yawo komaso atate langani athu amene akuwoneka ngati ndikhosazanu koma ilimimbulu yoyipa tikuziwakuti zosezi mukupangisa ndinu kuti satanayo ayaluke pitilizani kusunga mizimu yabaleathu ose amane anaphedwa kuchikangawa osayiwa SKC chilima tikulemphela kuvomeleza kuti munachoka pakatipathu 😭😭😭💔

  • @blessingsnyalo-rp9ko
    @blessingsnyalo-rp9ko หลายเดือนก่อน

    We are proud of you ntanyiwa

  • @Atheeeefire
    @Atheeeefire หลายเดือนก่อน +1

    Ntanyiwa usamasowe chocho ife kumango check ma phone ngati notification ya limpopo hahaha respect always president ntanyiwa

  • @cynthiandekhakatundu6890
    @cynthiandekhakatundu6890 หลายเดือนก่อน +1

    Palibenso kudikira 2025... Achoke ameneyo

  • @Chisomo-dh2gq
    @Chisomo-dh2gq หลายเดือนก่อน +2

    Fellow Malawian tiyen pa seu this coming Monday please Please this president he must go

  • @AubreymjBanda
    @AubreymjBanda หลายเดือนก่อน +1

    More fire 🔥 comliee!

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw หลายเดือนก่อน +1

    Number one mtanyiwa

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 หลายเดือนก่อน

    Inu ndi 1 basi iyaaaaaaaaaa😂 2 kuopa kuopa kupindika Shaaaaaaaa 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @NizigiyimanaChantal-c2p
    @NizigiyimanaChantal-c2p หลายเดือนก่อน +1

    More fire Mr ntanyiwa palibe chida chosulidwira iwe chidzapambana

  • @ruthkundwe7448
    @ruthkundwe7448 หลายเดือนก่อน

    UTM my vote

  • @ThomasStephan-tg6ng
    @ThomasStephan-tg6ng หลายเดือนก่อน +3

    Mademo apa 31tikupita konko kuli chakwera konko tikufuna axipita azikalima kwawo antanyiwa yokhayi yapweyeka Malawi MOTi Malawi sitideka akuchoka bs isanakwane 2025 Malawi zukani tiyeni tiyeni Malawi pansewu

  • @DanielSingano-bb7xq
    @DanielSingano-bb7xq หลายเดือนก่อน +1

    M'makwana bossman💪💪💪💪💪

  • @GertrudeLuciano
    @GertrudeLuciano หลายเดือนก่อน

    Ulemu wanu Nthanyiwa more fire

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg หลายเดือนก่อน +1

    Ntanyiwa iweyo ❤❤❤❤❤ ndiwe mfumu basi

  • @PaulDaka-dc3re
    @PaulDaka-dc3re หลายเดือนก่อน +1

    Kuli bwanji ku Botswana, chikangawa yavuta pa nyasa🥱🥱🥱🥱

  • @JamesManjawira-yz4ji
    @JamesManjawira-yz4ji หลายเดือนก่อน +1

    Mr Ntanyiwa we're together ❤💪

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona หลายเดือนก่อน

    Through the blessings of God and God's Power One day Malawi First will Lead as Opposition Party representing Malawians
    Keep it up Comrade.

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 หลายเดือนก่อน

    Inu ndi fire🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥ana achepa❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @peterlowole7841
    @peterlowole7841 หลายเดือนก่อน +1

    More fire big man

  • @patrickzembani4315
    @patrickzembani4315 หลายเดือนก่อน +1

    Moto kuti buuuuuuu aruta kontinyuwa comrade Ntanyiwa

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 หลายเดือนก่อน +2

    Achilima anapita ifa yowawa ngati galu ophedwa ndigalimoto panjila koma mulungu anaona chilichose chinachitika kuchikangawa sizinakatheka ose kumwalila komaso inakakhala ngozi denge inakayaka

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 หลายเดือนก่อน +2

    Amalawi tinagona kwambiri

  • @user-sh5wq4uf6r
    @user-sh5wq4uf6r หลายเดือนก่อน +2

    Nkhani iyi yikundiwawa abale anthu kuchita kukhapa ndi zikwanje zoona? MCP what are you doing us? 😭😭 MCP ndi president wanu chakwela are you a Malawians? Why are you doing this? Because of money? Your position? Fokofu! God will punish you 😢

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus หลายเดือนก่อน

      This so called president will rot in jail

  • @JosephHill-fy1bb
    @JosephHill-fy1bb หลายเดือนก่อน

    Munthu kungophedwa just like that basi...
    Stronger, so energetic and Courageous man SKC, gone just like that..
    MCP mwanya..

  • @cephasSainet
    @cephasSainet หลายเดือนก่อน

    Keep fire burning

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m หลายเดือนก่อน +1

    Big up mtanyiwa

  • @PollyLysonLutepo
    @PollyLysonLutepo หลายเดือนก่อน +1

    Antanyiwa Ambuye apitilize kuchita Nanu. Timakunyadilani.

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 หลายเดือนก่อน

    Yoooooo abisala mbatata koma nsana ukuoneka Ambuye awakhululukire ndithu shaaaaaaaa 😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @feranjifeza6802
    @feranjifeza6802 หลายเดือนก่อน +3

    I was asking the same kuti kodi nganga zaona kulibe

  • @MISHECKBANDAH-m3h
    @MISHECKBANDAH-m3h หลายเดือนก่อน +1

    Mtanyiwa izi ndizimene timadikilira❤❤❤❤❤

  • @chiefjusticie
    @chiefjusticie หลายเดือนก่อน +1

    Anaphedwadi anthu aja chief Justice akhala akuyimba nyinbo pompano yozuzula

  • @KennedyKanyama-ce8lb
    @KennedyKanyama-ce8lb หลายเดือนก่อน

    U r number 1. Mtanyiwa timadalira iweo fire. Tifufuzireni pliz mutipatse zonse

  • @MarkinaJohn
    @MarkinaJohn หลายเดือนก่อน +1

    Boom!!! Wathu wathu ntanyiwa

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w หลายเดือนก่อน +1

    Musamasowe big man ❤❤❤❤❤

  • @ThandoKunene-j9u
    @ThandoKunene-j9u หลายเดือนก่อน

    Mumakwanira mr Ntanyiwa !.Chikangawa yomweyo!! Galuiwe@. Kkkkkk timakunyadirani mr.🎉🎉🎉

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws หลายเดือนก่อน

    Funso Langa kwa president chakwela,,,,,,kodi a vise President anapedzeka bwanji ovulidwa malaya??? Kodi tinene kuti ndege ndiyimene inanvula Malaya??