Ndizovuta kuti oyipawa kuti akupange chipongwe Ntanyiwa.coz mulungu wadzusa inu bigger kuti mupulumuse dziko lamaliwi all the best God bless you with more protection 🙏 🙌 anthu oyipa sasukunika ku malawi 🇲🇼
Akangopita Ku German nkhanira imeneyo pibwerera Army mulande dziko ndikuzamangira pa airport akalowewe kundende life in prison kukanakhala Ku chilembenzo kwanthu chachisilamu tikanapanga sharia law aphedwe ,Koma asilikaliy dzukani musagone izi zachitikadzi zausatana ooopsa ndipo anandinyasa mene anali Ku chikokobe kumangochi kumanena kuti ati abale anthu akuziwa kuti anawapha lero siizi chifunga chapita dzuwa latuluka zaulira nde ati bwanji pamenepo☹️
Choyambilira tiyamika mulungu maka chifukwa cha Team iyi tikuti Limpopo Fm. Ndipo mulungu emweyo apitikire kugwira nanu ntchito imeneyo Tikowa mu Bible psalms 54 vs 17 Ves ilili ligwire ntchito pokutetezerani pogwira ntchito yanu Sir Comred
Ndalama akugawazo ndi za eni wake Amalawi kuzidya basi Koma Chidziwe mchipande powomola Maumboni ayambe kuoneka pa kusankha Ma khansala. Chikangawa boys you Will pay for what you did. Mwazi wa anthu 9 mwausamba thupi lonse. COMRADE NTANYIWA keep it up, keep moving🏃🏃
Mulungu amve ma pemphero athu.. ulendo akupita Ku Germany aziwone mudzina la chiwanda chakecho. Amalawi chonde tiyen tizuke ngt ma Kenyan. Tiyen pa nseu😢😢😢😢😢😢
Nkhani iyi yikundiwawa abale anthu kuchita kukhapa ndi zikwanje zoona? MCP what are you doing us? 😭😭 MCP ndi president wanu chakwela are you a Malawians? Why are you doing this? Because of money? Your position? Fokofu! God will punish you 😢
Ine nili ku Zambia koma nkhanga zaona sinipeza bwino ngati sininainvere.Comred ntanyiwa ni best
A Mcp ankawona ngati akamudzimitsa Chilima nde kuti Mcp idzalowanso osadziwa kuti mpamene akutero po akudzichotsera mbvoti Pena tikhonza kumanena kuti Mulungu analora dala kuti zimenezi zichitike
Muli boooh Mr mtanyiwa. I love you so much all team for Limpopo fm
Ndiliphe kuno ku Pretoria ndi ntanyiwawu Kaya ena amamuda koma ine nde ummmmm I like this guy ndingot malawi first yonse
Antanyiwa inuyo Mulungu anakonza mumatiyimilira lemu wanu❤❤❤❤❤
Chakwera pokupha Chilima amkaona ngati azawina koma sizitheka apa anadzikalasila makala amoto heavyyyyyy
More fire ntanyiwa mumatiyimilira keep it up
Mulungu samaoneka ndimaso koma pamene ife tikuyenda or pamene takhala timakhala naye limodzi,
Moti onse amene anapanga chipongwe chimenechi MULUNGU awaika pampalanganda.
Shaaaaa ulemu wanu bigy potiziwitsa za lipotili Amen
Ndizovuta kuti oyipawa kuti akupange chipongwe Ntanyiwa.coz mulungu wadzusa inu bigger kuti mupulumuse dziko lamaliwi all the best God bless you with more protection 🙏 🙌 anthu oyipa sasukunika ku malawi 🇲🇼
Mtanyiwa the pangolin original, keep it up the good work brother man ❤
mbambande padziko lapansi palibe chinsinsi mbali yakuno chinsaru Cha mkachisi chang'ambika tiyenazoni a Ntanyiwa ,wabisala mbatata msana ukuoneka aona moto a Mcp
Kkkkk kkkk more fire man of God kumanga Mulungu asiyeni awakanthe😂
Ndipo ine sindipuma bwino ndikapanda kunvera nkhanga zaona❤
😂😂 😅😅😅😅 comrade inetu since morning ndakhala ndikufufunza nkhangabzawona osayipeza
Even me ase
Mtanyiwa umakwana,,, We are proud of you!!,
You are out and clear kuno ku BT , ku quarry
Takunyadilanj a ntanyiwa mwatulukila coz m'bale wathu akasowa kwa 2 days tikumakhala ndi nkhawa coz agalu a mcp wa akutamangatu eeey
Akangopita Ku German nkhanira imeneyo pibwerera Army mulande dziko ndikuzamangira pa airport akalowewe kundende life in prison kukanakhala Ku chilembenzo kwanthu chachisilamu tikanapanga sharia law aphedwe ,Koma asilikaliy dzukani musagone izi zachitikadzi zausatana ooopsa ndipo anandinyasa mene anali Ku chikokobe kumangochi kumanena kuti ati abale anthu akuziwa kuti anawapha lero siizi chifunga chapita dzuwa latuluka zaulira nde ati bwanji pamenepo☹️
Listening from Capetown South Africa.
Keep the good work Mr ntanyiwa
Big up yomweyo Chikangawa
More fire 🔥 ntanyiwa we love love you all the way from south Africa 🇿🇦 ❤️ 😊
Timakunyadilani a Limpopo FM komano nchifukwa chiyani asilikari athu sakukhala mbali yowateteza anthu?
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.
Km chakwera mpak kumupha chilima chifukwa cha kufuna kuimas upulezitent km chakwera ambuye akuchitire chifundo chifukwa uli chabe ulibe zelu ulipo ndipo iwey uzafa ngt mbalame sure ndakwiya nawe chakwera shem on you, chakwera must go 😭😭😭😭😭😭😭💔💔💔💔💔💔
Mr Ntanyiwa koma mumaseka mopweteketsa moyo😂😂😂😂😂 Chakwera akamavera Limpopo i think thukuta limayenda kuchokera kumapazi kupita kumutu😂😂😂😂
Mbambande comred ntanyiwa 🔥
Ntanyiwa mumakwana, ndipo Limpopo FM ndi radio mbambande, No.1
Osamvela nkhanga zaona mtima umawawa ngat chibwenzi Chako chatha 😂😂😂
😅😅kungozuka timafikira Popa ntanyiwa oyeeee😅
You are the best ❣️❤ Limpopo FM ndi radio yokha imene amalawi wonse amayikonda and we need report from black box ✊
chilungamo chiyende ngati madzi opha mzake nayenso aphedwe watching from jhb
Mtanyiwwa ulemu wanuw km ndili ndi fuso bwanji ashankwela ankuyenda ndi amey yonkwana 4000 km shikangawaw anatumisa andu 8 onka bwanji sinankalla bwanji
Mumakwana keep it up
Mfiti za mcp, asilikali akanangowalandapo dzikoli agalu amenewa miyezi yatsalai
Ndipo inuyooo!!!
Asilikali akumalawi sangalande boma ngati momwe anachitila azimbabwe iwalani zimemezo
@@viennasamuel2976 Ndipo mukunena zoona Asilikali aku Malawi mmmmmmmm ndi amantha koma kuzunza anthu mu njira zina ndiye amatha.
Omenyela ufulu a original akumalawi ❤😂😂 Ntanyiwa ❤
Ut reminds me of king Nebuchadnezzar...anazionatu ulemerero wa Mulungu utamuchokera.... from King to nobody kutchire mmmmhu
Km nyimbo ya kayin ya kumapetoko ndiyoopsya kwambiri ndiyokhudza ngakhale mfiti imene ikhoza kufa ndi chikumbumtima.
Comrade Ntanyiwa akubwela mwa coming 😂😂😂😂😂
Kkkkkkkkk😂😂😂😂 chikangawa woyeeee satana achite manyazi sure more fire 🔥
Choyambilira tiyamika mulungu maka chifukwa cha Team iyi tikuti Limpopo Fm.
Ndipo mulungu emweyo apitikire kugwira nanu ntchito imeneyo
Tikowa mu Bible psalms 54 vs 17
Ves ilili ligwire ntchito pokutetezerani pogwira ntchito yanu Sir Comred
Ntanyiwa moto kuti buuuuuu
Ifetu Moni taulandili ndithu timakunyadilani ntanyiwa kwambili 👍👍🔥🔥
Mbambande Limpopo FM ndi ntanyiwa
😂😂😂😂😂😂😂❤❤❤❤❤🙏🙏🙏🙏
Yomweyo chikangawa
Palibe chinsisiiii padziko lapansili
All evil plans back to the sender in Jesus christ name
Limpopo with Comrade nthanyiwa woyeeeee
Ine popanda kuvela comred mdimadwala kip de gud job God protect you en guide u aswel
Kkkkk koma kumeneko chikangawa kunotu kuzomba tamuonesamo ground yonse anangokhalapo ndizibwenzizawo basi anyela agalu amenewa
Ndipo ulemu wanu mwachita bwino galu ameneu ndipo mulungu amukathe
Zomba mumatha ndazikonda kobasi zomwe munampanga chikangawa@@user-eh1mg3ww6d
Mwaitha
Asilikali pangani njira zimene mumapanga dziko ndilofunika lilandidwe mmanja MWA anthu away ndi okupha
Ndalama akugawazo ndi za eni wake Amalawi kuzidya basi Koma Chidziwe mchipande powomola
Maumboni ayambe kuoneka pa kusankha Ma khansala.
Chikangawa boys you Will pay for what you did.
Mwazi wa anthu 9 mwausamba thupi lonse.
COMRADE NTANYIWA keep it up, keep moving🏃🏃
Ntanyiwa WOYEEEEEEE mukutiimilira ife olirafe, mcp yayaluka, amadutsa m'mbali
Akangonyamuka galu ameneyo kupita ku German kwakeko tiyeni panseu tonse mademo😊
Kulakwa chakwera,,,,Ku Germany komwe akupitako kwapitanso amalawi ena amagulu omenyela ufulu nde ka akukapanga chiyani
Inu Malawi fest mulengeze kuti pofika siku lakuti mupeleke 1 wiki kuti chakwera atule pansi udindo
Mmakwanira a mtanyiwa ulemu wanu onse❤❤❤❤❤
Ambuye apitilize kukudalitsani. Ndikukutsungani ndi moyo a Ntanyiwa. Ndimakunyadilani. Pitilizani ntchito yomwe mwayiyamba. Chilungamo chioneke. Don't give up.
Aziyenda ma midzi Mo sinanga anthuwo alibe ma fn sakuziwa zomwe zikuchitika😮Koma Muthu amene Ali fn data angamunamize
Antanyiwa....musatisiye...Mulungu..azikuyanganileni❤
Asilikali please akanyamuka galu ameneyu, please a silikali take the office of President please
Mulungu amve ma pemphero athu.. ulendo akupita Ku Germany aziwone mudzina la chiwanda chakecho.
Amalawi chonde tiyen tizuke ngt ma Kenyan. Tiyen pa nseu😢😢😢😢😢😢
Limopo FM Ntanyiwa imakuyenera kwambiri ❤, it suits you bro, keep it up bro
More fire mr, comred ntanyiwa iweyo ndikatundu waboma olopano Brain banda pa times akunamano pale pale fisianadyamkazake🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Tiyenda pa 31 pano pasewu
Komaditu nane ndimazifusa kuti kodi chazulo ntanyiwa bwanji
Osamaiwala bambo avick ku cape maclrear ku dwale muziziwaso kt amikonda kwambili amavela daily nyamata ameneyu
Come on mr muthwanyiwa bwela nayoni nkhani yonse timakunyadirani
Matiyimira Mr Mtanyiwa ulemu wako
Awawa antanyiwa penapake mutu wawo sugwira chifukwa pamene aku German amafika amati amene azapange kafukufuku saziwa chilichonse angowatenga ku butchery pano akut atulusa lipoti lenileni chifukwa chakwera akupita german kukakambanawo Kodi tinve ziti ,iweyo ndiwedi munthu waboza ndipo la 40 likukwanila chitsiru iwe
Chitsiru ndiwe wopanda mnzeru
Ulemu Wanu mumatiyimilira inuyo ndithu ❤
Morefire boss mtanyiwa mpaka amve kutentha afit amenewa
Ambuye pitilizani kusunga moyo wa antanyiwa ndiwose amenene akufunila ziko lomwe munatipasa zabwino musalole oyipawa kuti awononge myoyo yawo komaso atate langani athu amene akuwoneka ngati ndikhosazanu koma ilimimbulu yoyipa tikuziwakuti zosezi mukupangisa ndinu kuti satanayo ayaluke pitilizani kusunga mizimu yabaleathu ose amane anaphedwa kuchikangawa osayiwa SKC chilima tikulemphela kuvomeleza kuti munachoka pakatipathu 😭😭😭💔
We are proud of you ntanyiwa
Ntanyiwa usamasowe chocho ife kumango check ma phone ngati notification ya limpopo hahaha respect always president ntanyiwa
Palibenso kudikira 2025... Achoke ameneyo
Fellow Malawian tiyen pa seu this coming Monday please Please this president he must go
More fire 🔥 comliee!
Number one mtanyiwa
Inu ndi 1 basi iyaaaaaaaaaa😂 2 kuopa kuopa kupindika Shaaaaaaaa 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
More fire Mr ntanyiwa palibe chida chosulidwira iwe chidzapambana
UTM my vote
Mademo apa 31tikupita konko kuli chakwera konko tikufuna axipita azikalima kwawo antanyiwa yokhayi yapweyeka Malawi MOTi Malawi sitideka akuchoka bs isanakwane 2025 Malawi zukani tiyeni tiyeni Malawi pansewu
M'makwana bossman💪💪💪💪💪
Ulemu wanu Nthanyiwa more fire
Ntanyiwa iweyo ❤❤❤❤❤ ndiwe mfumu basi
Kuli bwanji ku Botswana, chikangawa yavuta pa nyasa🥱🥱🥱🥱
Mr Ntanyiwa we're together ❤💪
Through the blessings of God and God's Power One day Malawi First will Lead as Opposition Party representing Malawians
Keep it up Comrade.
Inu ndi fire🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥ana achepa❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
More fire big man
Moto kuti buuuuuuu aruta kontinyuwa comrade Ntanyiwa
Achilima anapita ifa yowawa ngati galu ophedwa ndigalimoto panjila koma mulungu anaona chilichose chinachitika kuchikangawa sizinakatheka ose kumwalila komaso inakakhala ngozi denge inakayaka
Amalawi tinagona kwambiri
Nkhani iyi yikundiwawa abale anthu kuchita kukhapa ndi zikwanje zoona? MCP what are you doing us? 😭😭 MCP ndi president wanu chakwela are you a Malawians? Why are you doing this? Because of money? Your position? Fokofu! God will punish you 😢
This so called president will rot in jail
Munthu kungophedwa just like that basi...
Stronger, so energetic and Courageous man SKC, gone just like that..
MCP mwanya..
Keep fire burning
Big up mtanyiwa
Antanyiwa Ambuye apitilize kuchita Nanu. Timakunyadilani.
Yoooooo abisala mbatata koma nsana ukuoneka Ambuye awakhululukire ndithu shaaaaaaaa 😭😭😭😭😭😭😭😭
I was asking the same kuti kodi nganga zaona kulibe
Mtanyiwa izi ndizimene timadikilira❤❤❤❤❤
Anaphedwadi anthu aja chief Justice akhala akuyimba nyinbo pompano yozuzula
U r number 1. Mtanyiwa timadalira iweo fire. Tifufuzireni pliz mutipatse zonse
Boom!!! Wathu wathu ntanyiwa
Musamasowe big man ❤❤❤❤❤
Mumakwanira mr Ntanyiwa !.Chikangawa yomweyo!! Galuiwe@. Kkkkkk timakunyadirani mr.🎉🎉🎉
Funso Langa kwa president chakwela,,,,,,kodi a vise President anapedzeka bwanji ovulidwa malaya??? Kodi tinene kuti ndege ndiyimene inanvula Malaya??