Sizachilendo Nduna Kuona Nduna Ikupeleka Ndalama Kwa Delegate Kuti Awine Convention - Billy Malata

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 30 ก.ย. 2024
  • On Nyasa VoiceBox Billy Malata says it is perfectly ok for a Cabinet minister to spend money on party delegates in order to win a seat at the party's convention. Being a minister and competing in a party convention is not a reason to subject the individual to smear campaign.
    Pa Nyasa VoiceBox Billy Malata wati sizachilendo kuti nduna ya boma iwononge ndalama kukopa nthumwi za chipanichi kuti apexe mpando kumsonkhano wa chipanichi. Kukhala nudna ndikupikisana nawo pa msonkhano wa chipani si chifukwa chomuyipitsira munthu mbiri pa kampeni.
    #malawi

ความคิดเห็น • 33

  • @GiftChitsulo
    @GiftChitsulo 2 หลายเดือนก่อน +3

    Amalata simungakambe za MCP zokha osanenako za dpp chifukwa mukuoneka kuti mukulimbananaotu dpp chifukwa khani imene mukunenazo ndi za MCP koma inu mukukamba za dpp zikuoneka kuti mukuiopa dpp

  • @patassonelucaszovuta3431
    @patassonelucaszovuta3431 2 หลายเดือนก่อน +2

    Muphana sumunati nzimu wa chilima wakwiya

  • @SurprisedDrumKit-ql7rj
    @SurprisedDrumKit-ql7rj 2 หลายเดือนก่อน +1

    Abilly malata meafunsidwa za mcp osati za dop ndie zoyankha mopepelazi achitsilu inu pa

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 2 หลายเดือนก่อน +1

    Komatu nkhani ndi komwe akutenga ndalama.chifukwa ngt kuli chimbava choipa kut mcp nde ndie chithyola...ngt anafika pogula magalimoto 30 amwana wake yekha,nanga akazake ,nanga iye mwini...nde izi nzopusa

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 2 หลายเดือนก่อน +1

    Amenewotu akuwululana ifeyo amalawi tikusangalala kuti akuwululana

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 2 หลายเดือนก่อน

    Mwasowa chokamba inu, inu nde zithumwazo mulibe? Musalimbane ndi Dpp siyinayambepo yagawa ndlama zimenezi tikuwonera kwa mcp

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 2 หลายเดือนก่อน

    Galu wa MCP utu munawonapo nduna ya dzachuma kele kaja ikumwadza ma milion ngati mene mukupangila inu a MCP nde muwone KWACHA INATHA KALE KALE PANO CHIDZUDE CHA NDALAMA CHIFUKWA CHA UCHISILU WA CHAKWELA NDI MCP YAKOYO INU AGALU KWABASI

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoy 2 หลายเดือนก่อน

    Try to do your own things dont mention Dpp kuulurana mukuulurana nokha a MCP ife tilibeko

  • @Fanzo-h2l
    @Fanzo-h2l 2 หลายเดือนก่อน

    Akugula iwe galu bweletsa masache kuno tisesere kuchimbudzi

  • @AdmoreSingini
    @AdmoreSingini 2 หลายเดือนก่อน

    Koma kugawa ndalama for campaign ndi mulandu azanthu a ACB akuti bwanji,.?

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo1441 2 หลายเดือนก่อน

    Wasowa zokamba iwe osangonena zaku mcp zakozo bwanji a DPP chikuwakhuza ndi chiyani mbwaaaa iwe

  • @CharityChirwa-t1e
    @CharityChirwa-t1e 2 หลายเดือนก่อน

    Amalata mukatelo mwadyapo zoyakhulula achitchola koma zilipo koma osalimbana ndi DPP akupanga zawo Nanu pangani zanu tangoyamika kuti mukuwululana nokhanokha komande mphanatu munadya olakwika SKC

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe uzikamba za mcp osati DPP ayi iwe ndi ngalu kwambiri et

  • @SymonNamalomba-sh3fu
    @SymonNamalomba-sh3fu 2 หลายเดือนก่อน

    A Richard chimwendo Banda akuphatu aise

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 2 หลายเดือนก่อน +1

    This how you politicians play with taxes??? You are backing each other then by taking it as normal? Why not also rebuking misusing that money??

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 2 หลายเดือนก่อน

      Billy malata is a motherless dog..unreasonable fool

  • @LuciusKazembe
    @LuciusKazembe 2 หลายเดือนก่อน +1

    Akupasa dzingat pano wasiya yogulisa masache

  • @SamuelMthengo
    @SamuelMthengo 2 หลายเดือนก่อน

    Onongoni ndalamazo pakuti nthawi yanu yatha.

  • @ChristopherMatemba-m4g
    @ChristopherMatemba-m4g 2 หลายเดือนก่อน

    Atamungwila ndimatumba andalam pa airport..

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoy 2 หลายเดือนก่อน

    Komano ndalamazo sanamugwire nazo 😂😂😂

  • @OswinDzama
    @OswinDzama 2 หลายเดือนก่อน

    Ifemusatisokosereinu muona kutsogoloku

  • @MarvGerald
    @MarvGerald 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe ndimbudz kwambiri kdmata ndindan?

  • @HamidMasamba
    @HamidMasamba 2 หลายเดือนก่อน

    Ken panyapako galu wachabe chabe

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 2 หลายเดือนก่อน

    Mr malata anapengapo kodi?

  • @MaxwellMbesa
    @MaxwellMbesa 2 หลายเดือนก่อน

    Nthawi yanu dyeranitu

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 2 หลายเดือนก่อน

    Machende ako iwe wagwa nayo

  • @MadalitsoChisale-j2o
    @MadalitsoChisale-j2o 2 หลายเดือนก่อน

    Amalata mwatani kd?

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa 2 หลายเดือนก่อน

    Chitsiru iwe mbuzi ya munthu maphwala ako wakudyesa ndalama simplex chithyola Banda

  • @WillamLawson-gk1lw
    @WillamLawson-gk1lw 2 หลายเดือนก่อน

    Choka iweee zaziiiiiiiiiiii

  • @MajiduMakiyi
    @MajiduMakiyi 2 หลายเดือนก่อน

    Malata mbuzi

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 2 หลายเดือนก่อน

    Mbuzi iwe malata

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc 2 หลายเดือนก่อน

    Galu wachabe chabe