Sizachilendo Nduna Kuona Nduna Ikupeleka Ndalama Kwa Delegate Kuti Awine Convention - Billy Malata
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 30 ก.ย. 2024
- On Nyasa VoiceBox Billy Malata says it is perfectly ok for a Cabinet minister to spend money on party delegates in order to win a seat at the party's convention. Being a minister and competing in a party convention is not a reason to subject the individual to smear campaign.
Pa Nyasa VoiceBox Billy Malata wati sizachilendo kuti nduna ya boma iwononge ndalama kukopa nthumwi za chipanichi kuti apexe mpando kumsonkhano wa chipanichi. Kukhala nudna ndikupikisana nawo pa msonkhano wa chipani si chifukwa chomuyipitsira munthu mbiri pa kampeni.
#malawi
Amalata simungakambe za MCP zokha osanenako za dpp chifukwa mukuoneka kuti mukulimbananaotu dpp chifukwa khani imene mukunenazo ndi za MCP koma inu mukukamba za dpp zikuoneka kuti mukuiopa dpp
Muphana sumunati nzimu wa chilima wakwiya
Abilly malata meafunsidwa za mcp osati za dop ndie zoyankha mopepelazi achitsilu inu pa
Komatu nkhani ndi komwe akutenga ndalama.chifukwa ngt kuli chimbava choipa kut mcp nde ndie chithyola...ngt anafika pogula magalimoto 30 amwana wake yekha,nanga akazake ,nanga iye mwini...nde izi nzopusa
Amenewotu akuwululana ifeyo amalawi tikusangalala kuti akuwululana
Mwasowa chokamba inu, inu nde zithumwazo mulibe? Musalimbane ndi Dpp siyinayambepo yagawa ndlama zimenezi tikuwonera kwa mcp
Galu wa MCP utu munawonapo nduna ya dzachuma kele kaja ikumwadza ma milion ngati mene mukupangila inu a MCP nde muwone KWACHA INATHA KALE KALE PANO CHIDZUDE CHA NDALAMA CHIFUKWA CHA UCHISILU WA CHAKWELA NDI MCP YAKOYO INU AGALU KWABASI
Try to do your own things dont mention Dpp kuulurana mukuulurana nokha a MCP ife tilibeko
Akugula iwe galu bweletsa masache kuno tisesere kuchimbudzi
Koma kugawa ndalama for campaign ndi mulandu azanthu a ACB akuti bwanji,.?
Wasowa zokamba iwe osangonena zaku mcp zakozo bwanji a DPP chikuwakhuza ndi chiyani mbwaaaa iwe
Amalata mukatelo mwadyapo zoyakhulula achitchola koma zilipo koma osalimbana ndi DPP akupanga zawo Nanu pangani zanu tangoyamika kuti mukuwululana nokhanokha komande mphanatu munadya olakwika SKC
Iwe uzikamba za mcp osati DPP ayi iwe ndi ngalu kwambiri et
A Richard chimwendo Banda akuphatu aise
This how you politicians play with taxes??? You are backing each other then by taking it as normal? Why not also rebuking misusing that money??
Billy malata is a motherless dog..unreasonable fool
Akupasa dzingat pano wasiya yogulisa masache
Onongoni ndalamazo pakuti nthawi yanu yatha.
Atamungwila ndimatumba andalam pa airport..
Komano ndalamazo sanamugwire nazo 😂😂😂
Ifemusatisokosereinu muona kutsogoloku
Iwe ndimbudz kwambiri kdmata ndindan?
Ken panyapako galu wachabe chabe
Mr malata anapengapo kodi?
Nthawi yanu dyeranitu
Machende ako iwe wagwa nayo
Amalata mwatani kd?
Chitsiru iwe mbuzi ya munthu maphwala ako wakudyesa ndalama simplex chithyola Banda
Choka iweee zaziiiiiiiiiiii
Malata mbuzi
Mbuzi iwe malata
Galu wachabe chabe