Bwana Boooon Kalindo president Chakwera mwamuyankhula mokwanira koma kusava kuli ndi president Chakwera Ndipo munamukonda kumuongolera koma mmmmmmm palibe chichitika palibe chositha awa sindikuuziwa kuti potenga boma la Malawi amaganiza chani? Ndipo ine sindikupeza yankho Leni Leni koma Mulungu sakutitaya atiombola Malawi panopo 😭😭😭😭😭😭😭😭 the DC Boooon Kalindo president wa aphawi 🔥🔥
Andale awa sangakwanitse kusintha zinthu,kuyambira kukhala m'boma nthawi ya a Kamuzu kufikira pano..amangotsatira,alibe change for the goodness n better world..🎉
Kkkkk ambassador wà ku Malawi anaba katundu wa ku zimbambwe eèee zoòsyatu izi .kodi ndi a zikhale Ng'oma olo a cĥmwendo Banda !!, koma kusaukaku. Kùangitsà mànyàzi boma ndi dziko lomŵe
Andalewa sakhaniza bwino, uyu vuto anaipisisa kwambili ndi gulu lake lonse amene amamusatila , koma aaah Mulungu ubwino wake alipo akuona ikakwana nthawi yake yoti at least osauka azapezako bwino basi
Boniiiiiiiiiiii kalindooooooooo the DC 💪 ♥ ❤ ❤❤❤
Kom ndiye khutukuved iiiih 😮
😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊@@SueWahna
Thé Dc Bon kalindo number one ❤ good message
Truth shall prevail. Love u DC.
The Dc umatiimirila keep it up
Our best TV
We do hv president in malawi,
Atsogoleri athu ziwanda zinawatseka mmaso komanso makutu maso alinao koma sakuona makutu ali nao koma sakumva ndi chifukwa malawi ali mmavuto opsa
Booooooni kalindoooooo the DC
Bwana Boooon Kalindo president Chakwera mwamuyankhula mokwanira koma kusava kuli ndi president Chakwera Ndipo munamukonda kumuongolera koma mmmmmmm palibe chichitika palibe chositha awa sindikuuziwa kuti potenga boma la Malawi amaganiza chani? Ndipo ine sindikupeza yankho Leni Leni koma Mulungu sakutitaya atiombola Malawi panopo 😭😭😭😭😭😭😭😭 the DC Boooon Kalindo president wa aphawi 🔥🔥
Booooooon kalindooooooo kkkkk machine bigy
Andale awa sangakwanitse kusintha zinthu,kuyambira kukhala m'boma nthawi ya a Kamuzu kufikira pano..amangotsatira,alibe change for the goodness n better world..🎉
Kkkk karindo moto kuti mbu!!
ABoni Kalindo Mulungu azikudalitsani.Kunena zoona kuyankhula ndipo mukuyesetsa,ndipo ine ndakhulupilira kuti chipani cha MCP ndichoipa kwambiri.Ndipo amalawi sindikudziwa kuti tithawira kuti.Boma iri likawinaso amalawi tiziifa ndi nkhaza.Ndinabadwa 1990 koma simnaonepo umphawi wa malawi ngati panopa.CHONDE AMALAWI TIYENI TIVOTERE CHIPANI CHINA OSATI CHI MCP AYI PLS😩😩😩😩💔💔💔😢😢😢😢😢
❤❤❤❤❤karido Dc
The DC, Boma ili litipha ,dongosolo lothandiza amphawi lilibe
😢😢😢😢 kma malawi eeeeee ndipite kuti abale ine kma
The Dc Boni kalindo ❤❤❤❤
I would wish to join you guys,the strong Malawian
Dangerous child keep it up good working
Ku Malawi tilibe strong opposition 😢😢😢😢
K a m u n a 💪💥
😂😂😂😂
Ati today here tomorrow there kkkkk
Siku transport😂😂
Big up kalindo
Koma chakwera 😮😮😮 what kind of president is this 🤔🤔🤔🤔
Andale akumalawi ndagalu
Ndi zomvesa chisoni zinthu zomwe zikufotokoza DC wina lero lomwe nkumati boma ndi pomweli. What a shame.
DC mumatimilira ulemu wanu
Ambassador kusesa chilichose cha mnyumba kkk
Thats very true...
Za pension boma la chakwera ndi chiphinjo choopsa opuma ntchito mboma mpaka zaka ziwiri ena zitatu osalandila ndalama zawo shame on mcp government
Kkkkk ambassador wà ku Malawi anaba katundu wa ku zimbambwe eèee zoòsyatu izi .kodi ndi a zikhale Ng'oma olo a cĥmwendo Banda !!, koma kusaukaku. Kùangitsà mànyàzi boma ndi dziko lomŵe
Why malawi no action mu boma iliri why malawi wake up malawi and let's to do action
Thanks mumatiimilira Akalindo
Tamusiyrni yekha born kalindo yo aziyankhula kaye nkumaliza osamaikapo dziwe online tv inw mmandibowa bwaanjii
Vutoso ndi Amalawife tinagunata kwambiri chifukwa nkhalidwe lopusali timalionelera ndikumangodandaulira ma social media, uchisiru umwe umachitika kwathukuno mayiko ena anthu samayang'anira zopusazi
❤❤❤
Ndipo ndi owopsyadi that's why amaphana pa chibale
Ku Southern Region simulandila ntukula pakhomo chifukwa ndinu a DPP bwerani ku MCP
Koma a DC m'zipatalamu odwalaso akuzunzika kwambiri komaso ku NRB ku Blantyre eeeeh kuli mavuto anthu kumangobwererako
ADYERETU CHIKANGAWA KWAKE KWATHA
Boma lomvetsa chisoni kwambiri
Boni tamuona mdzako manganya pomwe Ali rero . Sidzimakupweteka mutima mwako ndalamatu zimadana ndi phokotso dzichepetse manganya akuthandidza apo ayi udzakalamba ulibe chilitchonse zivere chisoni zoona iwe udzigokhalira kuyendera ku Court thawi dzontse n
Kod ukamaona akuyankhula izi umaona ngati amangona ndi njala? Fufuzani kaye muzabwelenso
My Malawi kodi chenicheni ndichani?
Ana anjoka
Chakwera ndi mkozi yamunthu kwabasi
Ineyo Koma nkhawa zanga ndi zipanidi zotsutsa
M'chifukwa chiyani azitsogokeri athu omwe timati mwina atipulumutsa 2025 Ku Satana ameneyu angoti nziii!
De dc ndinu Katundu
Ndodo yasowa by mlaka 😢😢😢😢
Chakwera ndi president osanva kulangizidwa
Ankhutukumve😂😂
Mmene chikangaŵa wachokamu. Matsoka ake asiya kuti apweteke / alodze / aphe amalawi otsalafe mmalawi muno..komatu zisatheke .ndipo ku ungako asakatenge devaluation wakeyò. Amalawi tàkana devaluation ili yonse ..wamva iwe chikangawa!!?
Dziwe 1
Ah koma chakwerayu guys ndi munthu oyipa mtima kwambri
Akut screen yachombo 😂😂 Koma ziliko Chaka Chino
Chisoni Chamuna achakwera
Namayenda aona polekela
🎉🎉🎉🎉🎉😮😮😮
Koma aMalawi tidzadzuka liti ?? Kweni kweni mukufuna tichite kufika podya dothi Kuti mudzadziwedi Malawi akuvutika???? I wish ukanakhala Kuti dzimatheka munthu kudzigawa pa 100 times ine nkanadzigawa ndekha popanda ondithandidza nkupita pansewu ncholinga achoke chikangawayi
Malawi alipa moto
Tinkawona ngat m'busa atithandiza koma ayi manyakaaa eni eni amunthu!!🚮
Ife kuno ku mzuzu dzulo mafuta tinalibe
The DC
Kom ndiye khutukuved iiiih 😮
The dziwe tv inside the speech of kalindo is always distracting and boring
😢😢😢
Munalakwitsa ndinu amene lero mwazindikira tsopano
Kulakwa nde kwamunrhu
Zimenezo nde zoona
@@inessmsiyambiri8517 yaaa koma anachita mistake yaikulu pano akuzunzitsa amalawi
@@AngolanChinga azunzitsa amalawi
Auzen Dc
Chakwera sazava
Mr kalindo please number yanu perekani
Andalewa sakhaniza bwino, uyu vuto anaipisisa kwambili ndi gulu lake lonse amene amamusatila , koma aaah Mulungu ubwino wake alipo akuona ikakwana nthawi yake yoti at least osauka azapezako bwino basi
The DC