Very true mwana wakwathu yu mmh ndimwana ovesesa ozichepetsa komaso olimbikira he is teaching me alot,he is special and talented Ambuye akufikitse komwe ukufuna iweyoo🙌❤️ Extraordinary Yahweh he is God
I respect you my brother islael munthu oleredwa ndi agogo ake sakhala munthu wamba pitiliza kukhala ndi moyo ozichepesa ndiwe munthu okonda aliyese ndipo supasa anthu Bluetik 😂😂😂😂😂 mulungu apitilize kukusamalira kuti uzafikile pomwe iwe ukufuna much love from this side 🎉❤🎉🎉
He dint do anything zinangobwera atayamba kukula so please mind what you say mungotenga nazo sambi chifukwa palibe zimamuwaza so the face will be ok with time mind you thank you
@@miraclechinga5407Thanks wayankha bwino coz Israel wafotokozatu bwino bwino kale nkatimo akuti sanafune sanachiteyi kupanga Koma zilonda Ndie Ku studio ko anangopanga okha mwina amafuna achotse sunguzo. Ndie uyoyo Kaya bwanji vuto kunva ena kumawavuta zedi
Very true mwana wakwathu yu mmh ndimwana ovesesa ozichepetsa komaso olimbikira he is teaching me alot,he is special and talented Ambuye akufikitse komwe ukufuna iweyoo🙌❤️ Extraordinary Yahweh he is God
Zikomo kwambili ndathokoza sister
God bless you
Mwana uyu eeeeeeeeeee anakoza ndi fire zedi ndiozichepetsa, wanzeru komanso ochezeka, keep it up bro
I have learnt alot on this interview.
Keep good work Israeli
Adha awa muli nzeru ndipo amaziwa chochita analeledwa bho❤❤
Appreciate to you mwana wa ng,ono km uli ndipotetial and vision
I respect you my brother islael munthu oleredwa ndi agogo ake sakhala munthu wamba pitiliza kukhala ndi moyo ozichepesa ndiwe munthu okonda aliyese ndipo supasa anthu Bluetik 😂😂😂😂😂 mulungu apitilize kukusamalira kuti uzafikile pomwe iwe ukufuna much love from this side 🎉❤🎉🎉
Zikomo kwambili ndathokoza
Mwanayi amasogozedwadi ndi mzimu oyera.. pitiliza kuika mulungu patsogolo young man
Ndipo ndendendedi Amai ake zedi eeeeeee thank to God anatisiira mphatso yabwino zedi ndithu
Munthu wanzeru heavy; God bless you.
Thats my brother❤️ ndiwe dolo
Thanks alot sister yo so supportive and a loving sister
This guy is really amazing and he's blessed and God got more nlessings for coz he's hamble🙏🏿🙏🏿
Munthu wokula ndi agogo amakhala wanzeru ngati mumene ulili iweyo ndiwe mwana koma uli ndizeru pitilizani kuwakonda agogo aja nose mumawakonda pitilizani kukondana mulungu akudaliseni
Ndipo koopsa zedi, Agogo ndi deal zedi or utati wakura ndi amama okhanso ndi deal
I can't wait 😊
I support ur desition,it happens also to me focus with your life brother
Keep being a humbled guy israel u r sensitive 🎉
Keep up young talented boy
This is great I like this boy he is so talented
In this interview i have learn a lot and thanks guys for organising this ❤❤❤❤❤❤
Very intelligent guy I like you bro, may God bless u
❤fanai ndiozichepesa
Mfana woganiza bho
Much appreciate to you big up uli ndi good vision and potential
Mama akodi palibeyi angawakwanitseyi Koma ndikanakonda Miracle akanalimbikira kuti azafikepo, ndikhumbo langa
Ambuye apitilize ntchito ayambayi kwa iweyo
Amen
Ndipo ndiozichepetsa koopsa zedi ndiosiyana ndi azibale ake onse ajaa uyuyu ndiwina eeeeeeeeee Mbambande zedi brother Israel iwe ndie ndiwathuwathu Mbambande zedi brother
❤❤❤❤❤❤❤❤❤ I love you so much my brother
Keep it up my boy timakunyadila always
Zikomo kwambili ndathokoza
The guy is so humble
Kwabasi I like him
God be with you Israel
Humble guy
Mwana wa agogo kkkkk grace mzimu wako upitilire kuusa my mtendere
Ndipo koopsa zedi
The guy z amazing
Ine pheee mundipeza pamenepo
Nde nde nde a mako mwanawe kudzichepetsa ambuye akutsogolere mwanaweee
Cool guy
Koma nde kuchedwatu yakwana mesa
Nfana odekha
He is very hamble
Thanks alot
Your ginius adha
Thanks alot
Nzathu
🙏
❤️❤️❤️❤️🔥
Mulungu apitilize kukutsogolera ndikukupatsa nzeru zodabwitsa mwana wanga. Pitiliza kudzichepetsa ndikudalira pa Mulungu. Kupemphera patsogolo.
@@EllamariaKaliya-tc2es Amen
But what ever happened to his face anazilakwira ...
He dint do anything zinangobwera atayamba kukula so please mind what you say mungotenga nazo sambi chifukwa palibe zimamuwaza so the face will be ok with time mind you thank you
@@miraclechinga5407 alright noted with thanks and now tadziwa
@@miraclechinga5407Fact boss
@@miraclechinga5407Thanks wayankha bwino coz Israel wafotokozatu bwino bwino kale nkatimo akuti sanafune sanachiteyi kupanga Koma zilonda Ndie Ku studio ko anangopanga okha mwina amafuna achotse sunguzo. Ndie uyoyo Kaya bwanji vuto kunva ena kumawavuta zedi