Ndipo Ndikupephela Kuti bushili , chakwera ,Joyce Banda , ndi team yawo yonse ya satanic sindikuopa I don't follow politics , But am warning them , fuko Langa , mtundu wanga akuonongeka, because of them , Prophet bushili prophecy Kuti anthu omwe anagenda chakwela amwalila , and am here to warm bushili he must stop his nonsense...and alape .. akupha anthu kuvala chikopa cha nkhosa kuja nkati Ali mkango .. prophet wa bodza am also a woman of God and am trying all my best Kuti ma message amufike bushili Ngati amapha anthu , ineso am ready to dies for God's work ..my life is useless if mfuko Langa , mtundu wanga , akuonongeka , let me warn dziko lamalawi , tilape anthu akuonongeka chifukwa of lack of knowledge, I send this to all bushilis followers, Ngati mulibe mzimu wachidziwitso you are following Satanism people...my heart bleeds ...
There are so many people who don't know that Bushiri is afake prophet.Joyce Banda,Chakwera and many others they are in plot and may malawians are suffering because of these people.
Tikupephela ma plan awo akumidima satheka .. ndipo i stop all the evil altars that wants blood mu dziko langa ..sindisatila ndale ayi , koma zikundiwawa zedi mtima wanga kusweka. Mulungu wathu atikhulukukile , tilapile malawi ndipo fear not , kudziko lakumidima , akupanga ma meetings okhesa mwazi pa zitsakho koma i stand on the holy altar of God , amwa magazi awo , adya nthupi lawo , yesaya 54 vs 17 ku dziko langa .mtundu wanga
Marry Chilima To come out Can Shake the Whole Nation She Is Neutral last Minute MALAWI Could become Canaan. We are afraid to push her due to big loss, A Husband , not A joke But her response Can Raise The nation to EXPECTED CANAAN AS HER HUSBAND VISION MANY REFORMS WERE DONE BY SKC Looking forward to This proposal.
Ine si Mngoni koma tsiku lina tilalamulidwa ndi mayi wa Chingoni Hee heee sindikuseka koma kusekerera UTM Doctor Saulos chilimaaaà Tonse amalawi pambuyo pa U TM nyomiiiiiii
Mai Mary Chilima Ambuye akuona kulira Kwanu ndipo Mulungu woziwa Chilungamo ndiye amene ayankhe mafoso anu ndi a Malawi pa ifa ya anthu amene anatisiya pa ngozi ya ndege imeneyi the DC Boooon Kalindo the truth of Malawi
Chilima anaphedwa alindizoyankhula zambili koma palibe wina aliyese amene amadziwa kuti amafuna kuyankhula kuti chani koma mary chilima akudziwa zomwe mamuna wake akafuna kuyankhula ndiye tiyeni timulimbikise apange ndale coz mamuna wake anali wandale
Justice for SKC and all fallen heroes who were in that plane💔
Nkhani yoti Mary Chilima alowe ndale sindinagwilizane nayo koma iyi yokha yoti akusakasaka chilungamo pa imfa ya mwamuna wake, I support her 100 %
Akukasaka kuti
Iye uja ndi wa ndale kale inu mukungomuoopa coz mai uja akadzuka nkupangisa mtsonkhano chingachitike nchiani we need mama mary to rise up
Mutanthauza chani poti Mary Chilima ndi wa ndale kale sadalengezepo zoti adasiya ndale
God of vengeance, please intervene for us. Be strengthened Madam Chilima
Ndipo Ndikupephela Kuti bushili , chakwera ,Joyce Banda , ndi team yawo yonse ya satanic sindikuopa I don't follow politics , But am warning them , fuko Langa , mtundu wanga akuonongeka, because of them , Prophet bushili prophecy Kuti anthu omwe anagenda chakwela amwalila , and am here to warm bushili he must stop his nonsense...and alape .. akupha anthu kuvala chikopa cha nkhosa kuja nkati Ali mkango .. prophet wa bodza am also a woman of God and am trying all my best Kuti ma message amufike bushili Ngati amapha anthu , ineso am ready to dies for God's work ..my life is useless if mfuko Langa , mtundu wanga , akuonongeka , let me warn dziko lamalawi , tilape anthu akuonongeka chifukwa of lack of knowledge, I send this to all bushilis followers, Ngati mulibe mzimu wachidziwitso you are following Satanism people...my heart bleeds ...
There are so many people who don't know that Bushiri is afake prophet.Joyce Banda,Chakwera and many others they are in plot and may malawians are suffering because of these people.
Bon Kalindo 🔥 sukunama. Mcp yamutukwanadi mary
Rest in peace SKC. Mary Chilima osaopa, osafooka, osatopa.
Commission of inquiry ndiyosafunikira,zikuoneka kuti Winiko ali kale ndi umboni choncho akuyenera akatsegule mlandu wa murder ku court
Tikupephela ma plan awo akumidima satheka .. ndipo i stop all the evil altars that wants blood mu dziko langa ..sindisatila ndale ayi , koma zikundiwawa zedi mtima wanga kusweka. Mulungu wathu atikhulukukile , tilapile malawi ndipo fear not , kudziko lakumidima , akupanga ma meetings okhesa mwazi pa zitsakho koma i stand on the holy altar of God , amwa magazi awo , adya nthupi lawo , yesaya 54 vs 17 ku dziko langa .mtundu wanga
Mai Mary chilima akuyenela kulimbika mtima , Ndi njila yokhayo imene ingapangitse Kuti chilungamo Komanso chipambano chioneka . Ambuye amusogolele Mai wathu ..
Bon kalindo kunena chilungamo chene chen mulungu alinafe amalawi osadanda chakwela timuonesa nyekwe pa 2025 ndiboma lakelo lakumpa
Ine misozi imangotuluka ndikamaona zithuzi za achilima,analakwanji anthu awa
Kodi zomwe wayankhula Mary Chilima a mcp zawanyasa chifukwa chani
Vuto ayeni mtundu munafatsa nkhaniyi ikanatha kalekale koma inuyo munali duu ndie anthu sangachite kanthu popanda ayeni mtundu.Apapa ndie mwayamba kudzuka tsopano.
Amaonangati akhalachete
Marry Chilima To come out Can Shake the Whole Nation She Is Neutral last Minute MALAWI Could become Canaan. We are afraid to push her due to big loss, A Husband , not A joke But her response Can Raise The nation to EXPECTED CANAAN AS HER HUSBAND VISION
MANY REFORMS WERE DONE BY SKC
Looking forward to This proposal.
Bon Kalindo....... !!! the national speaker to the cursed country with the innocent blood of the late VP and other fallen heroes. Justice.... Justice
Ine si Mngoni koma tsiku lina tilalamulidwa ndi mayi wa Chingoni
Hee heee sindikuseka koma kusekerera
UTM
Doctor Saulos chilimaaaà
Tonse amalawi pambuyo pa U TM nyomiiiiiii
Mai Mary Chilima Ambuye akuona kulira Kwanu ndipo Mulungu woziwa Chilungamo ndiye amene ayankhe mafoso anu ndi a Malawi pa ifa ya anthu amene anatisiya pa ngozi ya ndege imeneyi the DC Boooon Kalindo the truth of Malawi
Koma. Nzoona. Mayi. Chilima. Muyimbe. Ntima. Ife. Tili. Pambuyo. Panu
Ife a malawi tikufuna Mademo a nyoooo...mpaka tikafika ku parliament konko..ndipo azakhala mathero a anthu amenewa..💪💪💪💪💪
Chikangawa party(MCP) mapwala awo ndithu asalowelelepo pa nkhani iyi coz nafedwa anawasiyila nkhani yimeneyi nthawi yayitali koma pali chomwe apangapo nde pano nafedwayo wabwela kuti apeze chomwe chinapha mwamuna wawo nde MCP yisalowelelepo apa....
Chilungamo chidziwike sure
The DC..More Fire 🔥..akatundu ❤❤❤❤
Zokuti wina sazapezeka pa ballot paper akhala atafa ndi mapemphero komaso kukwiya kwa mizimu ndizionadi
Kupita kukaona pomwe anafera Bale wako ndi kolakwika kapena kulira maliro abale wako ndikolesedwa ndiyakheni amalawi ndiyakheni
Mcp muona nyekwe chake chake ndi Chino
Ndipo agalu amenewa atitopesa. SKC rest in peace
Zoonaza abiye akalido mwayakulazo zichitika
Just for SKC AND VIVA MAI CHILIMA
Very good we need rotation ❤❤❤
Dipo akumanadimoto ahebili 12:29
All MCP members pa mtumbo panu
kma ikhale nyekhwe lizimu 😅
Sitisiya kulira mpaka wina agwe.
Bravo mayi Chilima
Nga'aluraaaaaaaa nthawi yathaa
Ine ndiiii Bonnnnn kalindoooooo
Wakupa chakwele😢😢
Wakupa chakwele😢😢
I follow you mam
DC woyeeeeeee motsoooooo kut buuuu
SKC🔥🔥
Zoonazake
❤
Onse amene sakugwilizana nanzo zoti mery chilima ayimire ndi a MCP andi alindimantha
@@LightwellMunthali-x7r sangawine mary ndale sangazithe ndi mwana maganizo opusa basi
Auzeni anyapapiwo agulugunyintha tizawadula mitu Peter akazalowa m'boma.mutisamale
Zopanda mzeru izi osamufunsa mwini moyo bwanji kuti munalileranji kuti chilima afe akuyankhani osati zanuzi anthu onsewa akufawa chilima apambane osewa kukomera kwake wakufa sadziwa kanthu biiiiii bible likunena osati munthu akutero ayi munthu ndi wabodza zazii musiyeni chilima lake anatseka nanga lanu mudzakhala mukutani
Kufa ndi kufu koma tikufuna tidziwe zoona chifukwa kufa ngati ifa yake ingakhale choncho tintha psweeti
Mpaka tizaziwe amene anapanga zimenezo...kaya ndinu amwene.....tizamva tsikulo
Aaaa koma MCP pena mudzikhala ndi dzelu mai chilima kupita kumawona pomwe anafela mamunake pamenepo pali mvuto iiiii kutsamvuatu MCP dziwani kuti mulungu simunthu dzotse akuwona kupanda chilima munali ndani inu a MCP aaaaa uchisilu basi
@@hanifahmponda8711 nanga ndi MCP mesa ndinu a DPP munagwetsa ndege?
@@alexandermeke6994achimwene tsekani kuchikamwa 🙏
@@HadijaKamwenendo yambani ndinu zikuphani ndale inu mumadya ndale inu umbuli ukuphani
Deliberate policy ndikugwilizana naye
DC woyeeeeeee ❤❤❤
Ife tili chete kudikila Mary Chilima kuti azayimere.
GOOD LET HER HEAR OUR PROPOSAL MALAWI CAN SHAKE HEAVILY