Limpopo FM wafikayi ndi Comrade Ntanyiwa akuti asilikali omwe anaulula zambili za ndege ija aphedwa

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 28 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 118

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b หลายเดือนก่อน +13

    Am not Malawian but I love my brother and sisters from Malawi chakwela must go

    • @FatimaAyami
      @FatimaAyami หลายเดือนก่อน +1

      Do you hear what he say

  • @ChildofGod_MjB
    @ChildofGod_MjB หลายเดือนก่อน +11

    Eeeeeeh koma Malawi nde wavundilatutu 🙌🏾😭

  • @NEBERTMVULA
    @NEBERTMVULA หลายเดือนก่อน +9

    CHAKWERA, ZIKHALE NG'OMA, MKAKA, CHIMWENDO BANDA, CATHERINE HARA, KUNKUYU be very careful Malawi is watching. MCP WILL COME TO AN END!!!!

  • @georgeaiwa8661
    @georgeaiwa8661 หลายเดือนก่อน +3

    Comrade Ntanyiwa ndinu amfumu ndipo we are in your favour. May God and ancestors protect you from MCP and it's corporates

  • @user-kw2do9wf3c
    @user-kw2do9wf3c หลายเดือนก่อน +7

    ulura zambiri ndimakunyadilani Mr Ntanyiwa

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q หลายเดือนก่อน +7

    Politics is a dirty game killing innocent people like that its very sad.

  • @Jafaliwathombo
    @Jafaliwathombo หลายเดือนก่อน +12

    Keep it up abraz,we are on your back and we know more from you

  • @user-hq6dq7zr1e
    @user-hq6dq7zr1e หลายเดือนก่อน +4

    Musationongele South Africa timadalira konkuno ife,monga Osauka nde mumuuze nyaniyo,apole moto

  • @user-lw9su5om5z
    @user-lw9su5om5z หลายเดือนก่อน +6

    Eeesh kma chakwera mmmm

  • @JummaSAmick
    @JummaSAmick หลายเดือนก่อน +3

    Malawi X mavuto plus mavuto oooh Malawi wanga

  • @IgnatiousFote
    @IgnatiousFote หลายเดือนก่อน +2

    A malawi tikakhl chete kwmbr Chakwela ayambisa nkhondo kuphanso asilikali atatu pamwamba pa ngozi ya ndege ija

  • @user-kw2do9wf3c
    @user-kw2do9wf3c หลายเดือนก่อน +4

    utipase ma video onse angozi Mr Ntanyiwa plz

  • @LonnieGrem
    @LonnieGrem หลายเดือนก่อน +4

    Kma abale ufuluwo nde ndutio🤷🤷😭😭

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy หลายเดือนก่อน +4

    😂😂😂thawi dzina ngat useke Pena ngat ulire pena kungokwiya bas eeesh chigawenga cha chikhristu

    • @user-oc9vl9xz8e
      @user-oc9vl9xz8e หลายเดือนก่อน

      Ku malawi kuli anthu ozindikila oziwa kuyankhu komanso a nzeru

  • @GetrudeMseteka
    @GetrudeMseteka หลายเดือนก่อน +3

    Palibe chisisi pasziko lapasi. kungade kumachabe basi.. keep it up brother tidziwe zoona.

  • @agreementphiri5416
    @agreementphiri5416 หลายเดือนก่อน

    We are all with you mr Limpopo, Keep it up.

  • @dysonfysonchifundo2284
    @dysonfysonchifundo2284 หลายเดือนก่อน +2

    Mukutiyimilila inuyo 🤝

  • @InnocentBabyTurtles-iq4ok
    @InnocentBabyTurtles-iq4ok หลายเดือนก่อน +1

    no one lipopo fm with comrade mtanyiwa

  • @user-ku2fe8nb3j
    @user-ku2fe8nb3j หลายเดือนก่อน +1

    A christu okhaokha kuphana mesa mumati zigawenga ndi Asilamu. Zamanyazi kobasi

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 25 วันที่ผ่านมา

    Big up bro❤✊✊✊✊✊💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @HalimaDamiano
    @HalimaDamiano หลายเดือนก่อน

    Wabudula ndiwo zagulu. Keep it up bro

  • @veronicanyirongo1314
    @veronicanyirongo1314 หลายเดือนก่อน

    More fire limpopo we love u our brother for justice ❤❤❤❤

  • @ruthkundwe7448
    @ruthkundwe7448 29 วันที่ผ่านมา

    above all this,God is at work

  • @ThomsonNyirenda-df9io
    @ThomsonNyirenda-df9io หลายเดือนก่อน

    We really appreciate we know more things from you 😮😮😮

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli หลายเดือนก่อน +2

    Lord have mercy

  • @user-bi5lg8mg9y
    @user-bi5lg8mg9y หลายเดือนก่อน +3

    Best Radio

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws หลายเดือนก่อน

    Poti ku Malawi tilibe muthu odalilika a Malawi adzatsakha Peter Mutharika koma pamenepo pa Peter Mutharika ndimavuto okha okha.

  • @FakeAcc-mi4ko
    @FakeAcc-mi4ko หลายเดือนก่อน

    Aslikali waphaso chakwela!😮 Akufuna atithamangitse kuno ku south tinathawa kumalawi kamba ka iye,galu kobasi chakwela ndi chimonica chakecho

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk หลายเดือนก่อน

    Loud and clear ❤❤

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne 24 วันที่ผ่านมา

    Chakwera must go

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws หลายเดือนก่อน

    Kodi Peter Mutharika anali muboma athu amadandaula nayo Peter Mutharika plz audzeni a Malawi nfundo dzabwino,,a malawi atsakhe president wina otsati Peter Mutharika chifukwa analephela kale Peter Mutharika ndiponso Peter Mutharika ndi president otsakha mitundu kwambili.

  • @user-vb1iq5un5p
    @user-vb1iq5un5p หลายเดือนก่อน +2

    Komatu zoyankhulazi ma comrades mwachulutsa..mukutisokonezatu..timve ziti kodi?.. zuwoneka kt mukugoyankhula zinthu zomwe simukuuzidziwa, omwe simuli nazo sure.muvi wa chiponyeponye.. apa mukuti mundege munaikidwa spray amene anapatsa dizzy anthu anali mu ndege .😂😂 😂...mukachulutsa zoyankhulatu,,, anthu sakukhulupilirani...siine wa MCP koma ndangokulangizani ma comrade..

    • @FakeAcc-mi4ko
      @FakeAcc-mi4ko หลายเดือนก่อน

      Aaaa vuto ndiweyo,

    • @FakeAcc-mi4ko
      @FakeAcc-mi4ko หลายเดือนก่อน

      Spray anaikidwa kt ndenge ikamatsitsidwa anthu akhale atafooka

    • @MarthaPhiri-ze8ee
      @MarthaPhiri-ze8ee หลายเดือนก่อน

      Zoona Pena pake abambu inu sitikunkhulupirani payamba munati ndege inachotsedwa transponder Pano mukuti anaikamo spray chenicheni ndichti💁

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne 24 วันที่ผ่านมา

    Kodi asilikàli 3000 angàsunge chakwera moyo wawo wonse, infa yilipo siiwoneka ndi maso, asilikali nawonso ndiwonkhuzidwa àkulira akunyonga omwewo

  • @SimonMlangiza-mu9fg
    @SimonMlangiza-mu9fg หลายเดือนก่อน

    Uku ndie kupusa kupanga zosokineza athu Malo mo manga Zilibe phindu kazikambani zokonkholoka

  • @UsenLashid
    @UsenLashid หลายเดือนก่อน

    Congratulation mr limpopo fm dont be afrid

  • @PetroMatias
    @PetroMatias หลายเดือนก่อน +1

    Ndani ameneo angaiwale nzaifa imeneo zachambazo mcp yathabasi

  • @Elvin-dr8tv
    @Elvin-dr8tv หลายเดือนก่อน +1

    Timchotse chakwera bcoz tazanu tithera Kuno joni

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt หลายเดือนก่อน

    Live from Mozambique.

  • @desirebeseni6695
    @desirebeseni6695 หลายเดือนก่อน

    Ndiri kumbuyo kwako chitezo chokwanira will provide mau afikire onse

  • @user-dn3gp6yi4y
    @user-dn3gp6yi4y หลายเดือนก่อน

    Dziko lotse la lapasi likuziwa kuti chakwela ndi wakupha bs 2025 angosaka kokhala malawi achokemo ndi family yake

  • @CharlesBanda-pm2oe
    @CharlesBanda-pm2oe หลายเดือนก่อน

    Ichi ndiye chitsiru cha zitsiru zonse,anthu omwe amaombera m'manja zinena za uyu ndi achamba Okha okha

  • @SamseyHassan
    @SamseyHassan 11 วันที่ผ่านมา

    This is really sad 😢

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y หลายเดือนก่อน +1

    Eeee Chakwela you mast go plz

  • @erickkhoko
    @erickkhoko หลายเดือนก่อน +1

    Asewera game yopoira

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b หลายเดือนก่อน

    That was really bad chakwela never liked the vice president evil act mr president that is bad from Zambia

  • @user-wp9js5vu6s
    @user-wp9js5vu6s หลายเดือนก่อน +2

    Zachison 😢😢😢

  • @frankkaipa8925
    @frankkaipa8925 หลายเดือนก่อน

    South Africa sikunama ma plan a achina chakwela ndiamenewo

  • @Aubiekenneth
    @Aubiekenneth หลายเดือนก่อน +2

    Kod Inu school yake munayimba kut achitsiru inu

    • @harrisbanda5891
      @harrisbanda5891 หลายเดือนก่อน

      Choka chizukulu cha ng'azi iwee, lucifa iwee

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e หลายเดือนก่อน +1

      Chisiru ceni ceni ndi ladzalo cakwera amene wapha chilima mopanda kumva cisoni

  • @Mphatso-jr1fb
    @Mphatso-jr1fb หลายเดือนก่อน

    Even maiko aluya akudziwa ine ndinakhumudwa abwana wanga akundiuza

  • @user-zg9se4rw6v
    @user-zg9se4rw6v หลายเดือนก่อน

    Muthanyiwa , Muthanyiwa

  • @user-wx7pw8xg6x
    @user-wx7pw8xg6x หลายเดือนก่อน

    A Mtanyiwa Ife timakukondani kwambiri

  • @peterlowole7841
    @peterlowole7841 หลายเดือนก่อน

    South Africa must react before, us Russia did kick out MCP

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon หลายเดือนก่อน

    Kodi bwanji angopanga risign akuluwatu atipweteketsa tiridziko lovuta kwambiri

  • @YatoRoy-kt4lh
    @YatoRoy-kt4lh หลายเดือนก่อน

    There is a massive American base in Botwana,what are they going to do about it?

  • @EuniceBauleni
    @EuniceBauleni หลายเดือนก่อน

    Exactly

  • @AudreyMwangonde
    @AudreyMwangonde หลายเดือนก่อน +1

    Makape mcp zawavuta

  • @user-qf7ko2dd5g
    @user-qf7ko2dd5g หลายเดือนก่อน

    Mumativetsa kukoma

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne 24 วันที่ผ่านมา

    Chakwera wapenga misala

  • @SolomoneWizimane
    @SolomoneWizimane หลายเดือนก่อน

    Koma ndye bola aphe tose iyeyu ndchisilu bwanji kan dzkoli nd lake

  • @kekeaufi9834
    @kekeaufi9834 หลายเดือนก่อน

    Magalimoto adusa pa ludzu achilendoo mmmmmmm mulungu atithandize,,,,, ateteze dziko lanthu iiiii abale

  • @REXCHARLESKAJAWO
    @REXCHARLESKAJAWO หลายเดือนก่อน

    Mmmmmm koma zopsa kwambili 😭😭😭

  • @leonwisikesmwkbyowner
    @leonwisikesmwkbyowner หลายเดือนก่อน

    Powerful

  • @jamesmnenula3568
    @jamesmnenula3568 หลายเดือนก่อน

    Signs of the time.

  • @HalimaDamiano
    @HalimaDamiano หลายเดือนก่อน

    Keep it up

  • @GanizaniManyamba-i6q
    @GanizaniManyamba-i6q หลายเดือนก่อน

    Umakwanila blather man tiyenazo😅😅😅😅

  • @fantesher
    @fantesher หลายเดือนก่อน +1

    😢😢

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg หลายเดือนก่อน

    A utm naoso ndi dzisilu 😢😢😢

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq หลายเดือนก่อน

    No chilima dzofuna ndamene anagwetsa dpp kuti afe ndidzimene amafuna mesa chilima anakhala ku dpp bwezi 2025 akulamula malawi koma lelo wafa wati siya tikuvutika ndi mcp

  • @AlinafeChimoto-pp7wp
    @AlinafeChimoto-pp7wp หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja หลายเดือนก่อน

    Zoonadi MCP yathabasi ndi Anthu okupha

  • @chikaonekarh
    @chikaonekarh หลายเดือนก่อน

    Ndipo true

  • @user-wx7pw8xg6x
    @user-wx7pw8xg6x หลายเดือนก่อน

    Umakwana Mtanyiwa

  • @MikeMwale-bw1xw
    @MikeMwale-bw1xw หลายเดือนก่อน

    Kachipani konunkha.
    This party must never exist again in Malawi,Chakwera must go we don't need dirty leaders,killers,murders God will punish.

  • @NelsonMalija
    @NelsonMalija หลายเดือนก่อน

    Mwadxiwika 😂😂😂😂

  • @ElizabethKalonga
    @ElizabethKalonga หลายเดือนก่อน

    😢

  • @HaroldJambo
    @HaroldJambo หลายเดือนก่อน

    Chakwera must resign now

  • @Bertha-p1e
    @Bertha-p1e 26 วันที่ผ่านมา

    Limpopo fm

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 หลายเดือนก่อน +4

    Chakwela asazunzitse abale athu ku South Africa chifukwa chandale zake zopusazo, leave malawians alone in South Africa, i beg South African government and Rusher government Mr Puttin to deal with chakwela with his crocodile party called mcp please.

  • @jameskachulu8141
    @jameskachulu8141 หลายเดือนก่อน +3

    Zimenezi ndiye zoona koma sangakwanise brics siyamasewela Russia

  • @foradelinofara1382
    @foradelinofara1382 หลายเดือนก่อน

    Nizowona zimenezi

  • @afritouch4660
    @afritouch4660 หลายเดือนก่อน +1

    Muthalika ankangogona uja.? Mwayiwala kale? CHIHANA VICE ATUPELE

    • @SuzgoMkandawire-ss4kh
      @SuzgoMkandawire-ss4kh หลายเดือนก่อน

      Nanga awa osagonawa ndiye skutani

    • @harrisbanda5891
      @harrisbanda5891 หลายเดือนก่อน

      ​@@SuzgoMkandawire-ss4khwandifunsira bwino, ogalamukawo akupangapo chiyaan pazankhanza zomwe crocodile party akuchita popha anthu ?

    • @afritouch4660
      @afritouch4660 หลายเดือนก่อน

      That’s why I said Chihana & atupele not chakwera & grandpa.! 👴

    • @afritouch4660
      @afritouch4660 หลายเดือนก่อน

      No MCP no DPP..!! Waste of time.!

  • @SamuelbonifacioBonifacio
    @SamuelbonifacioBonifacio 13 วันที่ผ่านมา

    Eu

  • @EuniceBauleni
    @EuniceBauleni หลายเดือนก่อน

    Aponyedi

  • @AndasoniWikisoni
    @AndasoniWikisoni หลายเดือนก่อน

    Kkkkkk eeeee kwachematu

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w หลายเดือนก่อน

    AMALAWI UMPHAWI TILINAWO ,KOMA BWANJI WOSAGWIRANA MANJA ,MMATI DZIKO NDI ANTHU ,KOMA NO ACTION . IT'S NOT ONLY DEATH OF CHILIMA ,NO!!!!! ,KOMA IYI YINALI NTHAWI YOTI A PRESIDENT ACHOKE BY FORCE . KOMA KULI ZIIII. TIKUZUNZIKA KUKHALA MAYIKO AKUNJA KAMBA KOTI MALAWI AKUSOWA MTSOGOLERI WOTI ATITSOGOLELE

  • @IssaKapalamula
    @IssaKapalamula หลายเดือนก่อน

    That English is not for a South African citizen 😂😂😂😂

    • @MichaelWilliamsNyirenda
      @MichaelWilliamsNyirenda หลายเดือนก่อน

      Is for who ?

    • @IssaKapalamula
      @IssaKapalamula หลายเดือนก่อน

      @@MichaelWilliamsNyirenda Zimbabwean, and it’s a Shona guy

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2cz หลายเดือนก่อน

    Chakwela mbolo yako wamva

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d หลายเดือนก่อน +1

    Following

  • @user-ml9fm2wm1o
    @user-ml9fm2wm1o หลายเดือนก่อน

    🍇🍇🍇🍇🍇🍅🍅🍅🍅🍅

  • @SolomonAmon-bu5qc
    @SolomonAmon-bu5qc หลายเดือนก่อน

    Even in Kenya people are talking

  • @HassanKareem-ck2qj
    @HassanKareem-ck2qj หลายเดือนก่อน +1

    Mumakwana

  • @Aubiekenneth
    @Aubiekenneth หลายเดือนก่อน +3

    Iwe makutu amako wanva machende ako

    • @joebrown1158
      @joebrown1158 หลายเดือนก่อน +1

      Mwana wa njoka wakusaweluzika mwana wa chiwonongeko ulendo ku Gahena

    • @LamieTiger
      @LamieTiger หลายเดือนก่อน

      😂😂😂uvayanayo MCP ada zikolonse lamuoodza chakwera iweyo wekha ndi athu akwanu mudzamuwinitsa chakwera 2025
      Bola chakwera akanangokhala abusa m'mene analili kale lija coz apapa nde or kupepherera athu sangakhulupilire

    • @blessingsbanda1031
      @blessingsbanda1031 หลายเดือนก่อน

      Chitsilu chamunthu iwe

    • @joebrown1158
      @joebrown1158 หลายเดือนก่อน

      @@blessingsbanda1031 mwana Waipa kwambilri kusangalara ndi M C P MAKOLO ANGA ANA BVUITIKA NDI M C IWEYO NDIKUMASANGALALA CHOTERE MWANA WOIPA KWAMBIRI

    • @blessingsbanda1031
      @blessingsbanda1031 หลายเดือนก่อน

      @@joebrown1158 ndigulu la dzitsilu mwene pomwe yafika mcp pano.wina munthu oti wabwino bwino angamaiikile kumbuyo

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg หลายเดือนก่อน

    Chakwera pathako pake sure 😢😢😢😢 why this

  • @FelixKazembe-wi5zb
    @FelixKazembe-wi5zb หลายเดือนก่อน

    😢