Bon Kalindo watuluka kundende. Chakwera ndi Dictator.

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 27 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 82

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 หลายเดือนก่อน +6

    Koma a vice president panepo mwaikocha, Bon Kalindo akumanena zinthu zeni zeni zimene anthu akudandaula. I like that Mr. VP.

  • @ChaibishuSwadck
    @ChaibishuSwadck 3 หลายเดือนก่อน +3

    More fire VP usi mwaya bwino ntchito koma ndi mawu amenewo mudana ndi MR PRESIDENT

  • @RabeccaMpunga
    @RabeccaMpunga 3 หลายเดือนก่อน

    I like your speech mr vp 🎉🎉🎉

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 3 หลายเดือนก่อน

    We always supporting you all freedom fighters in malawi ,
    You encouraging us as Malawians to know our freedom without scare anyone
    We will fight our freedom together with you .
    We will continue to blame the stupid things from any government

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 3 หลายเดือนก่อน +3

    The Dc bon kalindo tiyeni mademo Chakwela you mast go

  • @KondwaniNguleti-x1q
    @KondwaniNguleti-x1q 3 หลายเดือนก่อน

    A Vice President athu Dr Michael Bizwick usi I like ur speech iwe umandiwaza komano bola Lazaro waumphawiyo asakutume pa Ndege mkudutsira ku Chikangawa Forest

  • @NoelLangwani
    @NoelLangwani 3 หลายเดือนก่อน

    More fire 🔥🔥🔥🔥 kalindo ..... Michael usi ulemu wanu vice president pamenepo mwaonesa chikondi zikomo kwambili ❤❤❤❤

  • @YoungMwacho
    @YoungMwacho 3 หลายเดือนก่อน +4

    Please Bon Kalindo do not associate with Timothy Mtambo, he is a devil 👿 just like Chakwela, please do not trust him, please, please. He is MCP do not be cheated.

    • @JamesManjawira-yz4ji
      @JamesManjawira-yz4ji 3 หลายเดือนก่อน

      He knows bro.... The DC he is another story baba😂

    • @JoshuaNyirongo
      @JoshuaNyirongo 3 หลายเดือนก่อน

      True

    • @AngolanChinga
      @AngolanChinga 3 หลายเดือนก่อน +1

      Mulungu akudalisen iweyo polankhula mau amenewo timoth asamukhulupilile kwambili

    • @AngolanChinga
      @AngolanChinga 3 หลายเดือนก่อน

      ​@@JamesManjawira-yz4ji❤❤❤❤

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 3 หลายเดือนก่อน

    Ai zikom a vice president tikuona ngat tili limodzi ndinthu ndikuvana nazo bon kalindo it's the best ❤❤❤

  • @petermajor-mb2rb
    @petermajor-mb2rb 3 หลายเดือนก่อน

    Thambo sindumukhulupila Ine carefully born

  • @VictoriaWilliam-ms2ft
    @VictoriaWilliam-ms2ft 3 หลายเดือนก่อน +3

    I like manganya's speech keep it up bro

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 3 หลายเดือนก่อน

    Mr Ussi well put keep it up.

  • @SteveSangwa-tb7lk
    @SteveSangwa-tb7lk 3 หลายเดือนก่อน

    So Mr VP mutathauza kut a Malawi ndi amisala mwana wao kalindo ngwabwinobwino 😂

  • @Dee01papa
    @Dee01papa 3 หลายเดือนก่อน

    Nkulu wachimimbayo nde utinso😅

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 3 หลายเดือนก่อน

    Good point Mr Vice President

  • @amontchuwa6876
    @amontchuwa6876 3 หลายเดือนก่อน

    VP zimene ukunenaz ndizoona km usatipusitse ai
    Ubwino wake the dc ndizako wenewene bola menyan nkhondo chakwera achoke Malawi abwerere pakale osat manyakawa

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 3 หลายเดือนก่อน

    I like to see mutambo and bon kalindo together

  • @RadsonTimoteo
    @RadsonTimoteo 3 หลายเดือนก่อน +1

    Usi Michel nice one

  • @LuciasSimione
    @LuciasSimione 3 หลายเดือนก่อน

    Kkkkk naye manganyatu wabwelapo

  • @IdahKadewere
    @IdahKadewere 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwera olo lero anakamwalira tatopa naye

  • @robenallie6985
    @robenallie6985 3 หลายเดือนก่อน

    Adala chemanganya twanyadire awechete chenene

  • @FrancisKalinde-wz7yd
    @FrancisKalinde-wz7yd 3 หลายเดือนก่อน

    Abon kalindo pathako panu mwava

  • @NicholasJames-cb7du
    @NicholasJames-cb7du 3 หลายเดือนก่อน +3

    The DC pangorin mwana wovuta kwambiri kwatuluka

  • @BrunoChakukuma
    @BrunoChakukuma 3 หลายเดือนก่อน

    A vice president mwayankhula bwino osati angangawo yawo ndiyomanga anthu 😂

  • @DoricaGoweka
    @DoricaGoweka 3 หลายเดือนก่อน

    Children Chakwera walephera Achike basi sakutha ayi . Kalindo more fire the DC . Unatiimiliraaaaaa 😅😅😅

  • @louisemsowoya8235
    @louisemsowoya8235 3 หลายเดือนก่อน

    Ambuye bwerani mwachangu kuzatipulumutsa 😭😭😭😭

  • @JoyceBanda-k8t
    @JoyceBanda-k8t 3 หลายเดือนก่อน

    Takondwera ndikutuluka kwa aprezdent anthu cakwera manyazi bwanji umafuna utawapha ngati momwe wapher chilima mulungu wakusekatu aprezdent athu atuluka amoyo litamandike dzina la yehova wamwamba mwamba kuno ku thyolo thekerani

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 3 หลายเดือนก่อน

    A VP alankhula bwino komabe take care kulankhula kwawo kukonza kukhala pusi pusi a kalindo akuyenela kamasamala kwambiri

  • @PizoZopi-w2g
    @PizoZopi-w2g 3 หลายเดือนก่อน

    Apm my vote ✊

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 หลายเดือนก่อน +2

    Chakwera udzipita sitikukufuna

    • @Lifestyle-q4k
      @Lifestyle-q4k 3 หลายเดือนก่อน

      Azipita kuti. Chakwera is not going nowhere

  • @GodfreyTSAMDOKA
    @GodfreyTSAMDOKA 3 หลายเดือนก่อน

    Avice president mwalakhula bwino kwambiri ngati mungankhale ndi masompheya ameneyo dziko liyenda bwino zikomo kwambiri

  • @spargomw
    @spargomw 3 หลายเดือนก่อน

    Lawyer wa Born Kalindo nae akufunika kumamuikiza m'mapepemphero kut Ambuye azimutetezera😂😂😂😂

    • @isaihmagani5697
      @isaihmagani5697 3 หลายเดือนก่อน

      Lawyer palibe vuto lomwe angampinge nalo chifukwa lawyer ndi ntchito chabe amayimira munthu aliyese akhoza kumuyimira

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq 3 หลายเดือนก่อน

    Avice akuwona dzolakwa dza chakwela mbudzi imeneyi ukamuwudze chakwela yo osadula mboloyo

  • @williammenard48
    @williammenard48 3 หลายเดือนก่อน

    Amoya akwa Golden ayankhula bwino monga VP

  • @MexcoJepter-p5f
    @MexcoJepter-p5f 3 หลายเดือนก่อน

    Akuwonetsa ngati aUsiwa akudziwa kuti amalawi tili ndiufulu woyankhula bola asakhale pusi pusi yemweyo

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 3 หลายเดือนก่อน

    Ndipo chilungamo chokhachokha mr vp

  • @Uladimbwana-fr9ev
    @Uladimbwana-fr9ev 3 หลายเดือนก่อน

    Koma manganya apa ndiye wabaya ndithu

  • @ebenezerkamanga6016
    @ebenezerkamanga6016 3 หลายเดือนก่อน

    Manganya ikapitiliza izi iwe tigwilizana vice president azitero

  • @EdisonNakulenga
    @EdisonNakulenga 3 หลายเดือนก่อน

    Dasagalala Lelo diyako Sima potuluka Kumada adede kumwabakunenepe

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah 3 หลายเดือนก่อน

    We follow

  • @RashidRacc
    @RashidRacc 3 หลายเดือนก่อน

    Bhonikali ndo ulemuwanu 🦾🦾🦾🦿

  • @joicemumba3608
    @joicemumba3608 3 หลายเดือนก่อน

    Apo tageilizanananu

  • @robinfeb5684
    @robinfeb5684 3 หลายเดือนก่อน

    Mademo ayendeeee bas azaona ngat moyo ndi ophwekaaaa
    Timuziwe roya yo zina lake 💪💪💪💪💪

  • @HusseinMoffatt-mi1fl
    @HusseinMoffatt-mi1fl 3 หลายเดือนก่อน

    Bon kalindo ndidolo

  • @francebanda-du9yk
    @francebanda-du9yk 3 หลายเดือนก่อน

    Waturka. Zikomo

  • @ChinombaElvin
    @ChinombaElvin 3 หลายเดือนก่อน

    God is good all the wlc the DC 🙏🙏

  • @GiftHaward
    @GiftHaward 3 หลายเดือนก่อน

    Kumeneko ndiye kuyankhula Mr vp of malawi

  • @samueljuma4452
    @samueljuma4452 3 หลายเดือนก่อน

    Kodi iwe ntambo ukutani ndi mzako trapezie,mudayiwala ntchito yanu kodi?mademo alone m'bwalo

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 3 หลายเดือนก่อน

    Iiiii sopanotu akuthamangitsani mukayamba kuyankhula zimenezo Che manganya

  • @SamsonSolomon-rc4ef
    @SamsonSolomon-rc4ef 3 หลายเดือนก่อน

    Wakambako Za dzeru Koma ndiwe kazitape manganya

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 3 หลายเดือนก่อน +4

    More fire manganya

    • @WezzieChimuzi-ek7bk
      @WezzieChimuzi-ek7bk 3 หลายเดือนก่อน

      Achakwela alimmadzi ndipotu a manganya muikoke nkhaniyi osaphweketsa ndikuti mutha kutenga moandowo

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwera chimene akuchita sakuchiziwa ayi

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 หลายเดือนก่อน +3

    I love what I'm seeing.

  • @LuciasSimione
    @LuciasSimione 3 หลายเดือนก่อน

    Inu anthuwa akudziwana yawa😅😅😅😅

  • @samuelmoyo2650
    @samuelmoyo2650 3 หลายเดือนก่อน

    Powerful

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 3 หลายเดือนก่อน

    Wayitha vp

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 3 หลายเดือนก่อน

    A VP alankhula bwino komabe take care kulankhula kwawo kukonza kukhala pusi pusi a kalindo akuyenela kamasamala kwambiri

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 3 หลายเดือนก่อน

    Michael usi as our vice president pamenepo ulemu wanu kumeneko ndiye kuyankhula kp it up.aboni kalindo akungonena zinthu zomwe akuziona ndimaso zomwe boma likuchita samaonjezera koma poti iwowo akulankhula chilungamo that's why amcp ndizimene amadana nazo .koma l love your speech 🎉🎉

  • @IbrahimDailes
    @IbrahimDailes 3 หลายเดือนก่อน

    The dcc mulungu alemekezeke basi, km chilungamo chizaziwikabe ine ndili pambuyo panu forever

  • @AbrahamLLoyd-xb2xc
    @AbrahamLLoyd-xb2xc 3 หลายเดือนก่อน +1

    Zoona zimenezo

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 3 หลายเดือนก่อน

    Ndawakonda avice president keep it up muli ndi zeru kuposa chakwera zomwe akunena born kalindo ndimene anthu amadandawura

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 3 หลายเดือนก่อน

    Vp wayankhula bwino,keep it up bon kalindooooo

  • @LawranceNkuliwa
    @LawranceNkuliwa 3 หลายเดือนก่อน

    Kodi Amanda munali kuti muphula dzikotu inu chilungamo mukuchiziwa

  • @augustMag
    @augustMag 3 หลายเดือนก่อน

    Thanks GOD for helping you Mr DC ❤

  • @JackMvura-ik2td
    @JackMvura-ik2td 3 หลายเดือนก่อน

    Mitsonkho ya amalawi kunsewera nayo

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwera achoke simtikuvuna

  • @cjaylucky
    @cjaylucky 3 หลายเดือนก่อน

    VS WAYAKUL KUT THE DC SAKULAKWISA TIYEN PASEW BAS GATI KUKENYA NO PAIN NO GAIN

  • @LawranceNkuliwa
    @LawranceNkuliwa 3 หลายเดือนก่อน

    AVP ndinu katundu ulemu wanu zikomo

  • @ElizabethKazambwe
    @ElizabethKazambwe 3 หลายเดือนก่อน

    Mr vp mwayamba bwinotu

  • @MemoryKaunda-js9qv
    @MemoryKaunda-js9qv 3 หลายเดือนก่อน

    Manganya mwayakhulatu

  • @enockdaisi1306
    @enockdaisi1306 3 หลายเดือนก่อน

    Asamale

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc 3 หลายเดือนก่อน

    Awesome,ndidzomwe,tikudikila