We always supporting you all freedom fighters in malawi , You encouraging us as Malawians to know our freedom without scare anyone We will fight our freedom together with you . We will continue to blame the stupid things from any government
A Vice President athu Dr Michael Bizwick usi I like ur speech iwe umandiwaza komano bola Lazaro waumphawiyo asakutume pa Ndege mkudutsira ku Chikangawa Forest
Please Bon Kalindo do not associate with Timothy Mtambo, he is a devil 👿 just like Chakwela, please do not trust him, please, please. He is MCP do not be cheated.
VP zimene ukunenaz ndizoona km usatipusitse ai Ubwino wake the dc ndizako wenewene bola menyan nkhondo chakwera achoke Malawi abwerere pakale osat manyakawa
Michael usi as our vice president pamenepo ulemu wanu kumeneko ndiye kuyankhula kp it up.aboni kalindo akungonena zinthu zomwe akuziona ndimaso zomwe boma likuchita samaonjezera koma poti iwowo akulankhula chilungamo that's why amcp ndizimene amadana nazo .koma l love your speech 🎉🎉
Koma a vice president panepo mwaikocha, Bon Kalindo akumanena zinthu zeni zeni zimene anthu akudandaula. I like that Mr. VP.
More fire VP usi mwaya bwino ntchito koma ndi mawu amenewo mudana ndi MR PRESIDENT
I like your speech mr vp 🎉🎉🎉
We always supporting you all freedom fighters in malawi ,
You encouraging us as Malawians to know our freedom without scare anyone
We will fight our freedom together with you .
We will continue to blame the stupid things from any government
bwinotu michauel usi. usowatu
The Dc bon kalindo tiyeni mademo Chakwela you mast go
A Vice President athu Dr Michael Bizwick usi I like ur speech iwe umandiwaza komano bola Lazaro waumphawiyo asakutume pa Ndege mkudutsira ku Chikangawa Forest
More fire 🔥🔥🔥🔥 kalindo ..... Michael usi ulemu wanu vice president pamenepo mwaonesa chikondi zikomo kwambili ❤❤❤❤
Please Bon Kalindo do not associate with Timothy Mtambo, he is a devil 👿 just like Chakwela, please do not trust him, please, please. He is MCP do not be cheated.
He knows bro.... The DC he is another story baba😂
True
Mulungu akudalisen iweyo polankhula mau amenewo timoth asamukhulupilile kwambili
@@JamesManjawira-yz4ji❤❤❤❤
Ai zikom a vice president tikuona ngat tili limodzi ndinthu ndikuvana nazo bon kalindo it's the best ❤❤❤
Thambo sindumukhulupila Ine carefully born
I like manganya's speech keep it up bro
Mr Ussi well put keep it up.
So Mr VP mutathauza kut a Malawi ndi amisala mwana wao kalindo ngwabwinobwino 😂
Nkulu wachimimbayo nde utinso😅
Good point Mr Vice President
VP zimene ukunenaz ndizoona km usatipusitse ai
Ubwino wake the dc ndizako wenewene bola menyan nkhondo chakwera achoke Malawi abwerere pakale osat manyakawa
I like to see mutambo and bon kalindo together
Usi Michel nice one
Kkkkk naye manganyatu wabwelapo
Chakwera olo lero anakamwalira tatopa naye
Adala chemanganya twanyadire awechete chenene
Abon kalindo pathako panu mwava
The DC pangorin mwana wovuta kwambiri kwatuluka
A vice president mwayankhula bwino osati angangawo yawo ndiyomanga anthu 😂
Children Chakwera walephera Achike basi sakutha ayi . Kalindo more fire the DC . Unatiimiliraaaaaa 😅😅😅
Ambuye bwerani mwachangu kuzatipulumutsa 😭😭😭😭
Takondwera ndikutuluka kwa aprezdent anthu cakwera manyazi bwanji umafuna utawapha ngati momwe wapher chilima mulungu wakusekatu aprezdent athu atuluka amoyo litamandike dzina la yehova wamwamba mwamba kuno ku thyolo thekerani
A VP alankhula bwino komabe take care kulankhula kwawo kukonza kukhala pusi pusi a kalindo akuyenela kamasamala kwambiri
Apm my vote ✊
Chakwera udzipita sitikukufuna
Azipita kuti. Chakwera is not going nowhere
Avice president mwalakhula bwino kwambiri ngati mungankhale ndi masompheya ameneyo dziko liyenda bwino zikomo kwambiri
Lawyer wa Born Kalindo nae akufunika kumamuikiza m'mapepemphero kut Ambuye azimutetezera😂😂😂😂
Lawyer palibe vuto lomwe angampinge nalo chifukwa lawyer ndi ntchito chabe amayimira munthu aliyese akhoza kumuyimira
Avice akuwona dzolakwa dza chakwela mbudzi imeneyi ukamuwudze chakwela yo osadula mboloyo
Amoya akwa Golden ayankhula bwino monga VP
Akuwonetsa ngati aUsiwa akudziwa kuti amalawi tili ndiufulu woyankhula bola asakhale pusi pusi yemweyo
Ndipo chilungamo chokhachokha mr vp
Koma manganya apa ndiye wabaya ndithu
Manganya ikapitiliza izi iwe tigwilizana vice president azitero
Dasagalala Lelo diyako Sima potuluka Kumada adede kumwabakunenepe
We follow
Bhonikali ndo ulemuwanu 🦾🦾🦾🦿
Apo tageilizanananu
Mademo ayendeeee bas azaona ngat moyo ndi ophwekaaaa
Timuziwe roya yo zina lake 💪💪💪💪💪
Bon kalindo ndidolo
Waturka. Zikomo
God is good all the wlc the DC 🙏🙏
Kumeneko ndiye kuyankhula Mr vp of malawi
Kodi iwe ntambo ukutani ndi mzako trapezie,mudayiwala ntchito yanu kodi?mademo alone m'bwalo
Iiiii sopanotu akuthamangitsani mukayamba kuyankhula zimenezo Che manganya
Wakambako Za dzeru Koma ndiwe kazitape manganya
More fire manganya
Achakwela alimmadzi ndipotu a manganya muikoke nkhaniyi osaphweketsa ndikuti mutha kutenga moandowo
Chakwera chimene akuchita sakuchiziwa ayi
I love what I'm seeing.
Inu anthuwa akudziwana yawa😅😅😅😅
Powerful
Wayitha vp
A VP alankhula bwino komabe take care kulankhula kwawo kukonza kukhala pusi pusi a kalindo akuyenela kamasamala kwambiri
Michael usi as our vice president pamenepo ulemu wanu kumeneko ndiye kuyankhula kp it up.aboni kalindo akungonena zinthu zomwe akuziona ndimaso zomwe boma likuchita samaonjezera koma poti iwowo akulankhula chilungamo that's why amcp ndizimene amadana nazo .koma l love your speech 🎉🎉
The dcc mulungu alemekezeke basi, km chilungamo chizaziwikabe ine ndili pambuyo panu forever
Zoona zimenezo
Ndawakonda avice president keep it up muli ndi zeru kuposa chakwera zomwe akunena born kalindo ndimene anthu amadandawura
Vp wayankhula bwino,keep it up bon kalindooooo
Kodi Amanda munali kuti muphula dzikotu inu chilungamo mukuchiziwa
Thanks GOD for helping you Mr DC ❤
Mitsonkho ya amalawi kunsewera nayo
Chakwera achoke simtikuvuna
VS WAYAKUL KUT THE DC SAKULAKWISA TIYEN PASEW BAS GATI KUKENYA NO PAIN NO GAIN
AVP ndinu katundu ulemu wanu zikomo
Mr vp mwayamba bwinotu
Manganya mwayakhulatu
Asamale
Awesome,ndidzomwe,tikudikila