ไม่สามารถเล่นวิดีโอนี้
ขออภัยในความไม่สะดวก
ต่อไป
เล่นอัตโนมัติ
Ахбори Тоҷикистон ва ҷаҳон (19.08.2024) اخبار تاجیکستانOzodivideo
มุมมอง 31K
Zotsatila Za Chisankho Ku DPP Convention 2024 - MEC announces all winners OFFICIAL RESULTSAmuna Misso Tv
มุมมอง 4.1K
Mr Jokes, Performs live in front of a Minister! it was great!MR JOKES
มุมมอง 104K
#เชียร์krk #supungKRK SHORTS
มุมมอง 137K
เดินจากอยุธยาสู่อ่างทองกับพี่ตั๊กบริบูรณ์...จะถึงไหมครับKyutae Oppa
มุมมอง 1.3M
จิ้มฝั่งไหนกินอันนั้น (ซ้ายหรือขวา)CreamLike
มุมมอง 1M
เป็นพี่- ละครสั้น สอนใจ【 หนังดี เอ็มวีเพลิน 】หนังดี เอ็มวีเพลิน
มุมมอง 112K
TAONANI MPHATSO YOMWE A KU BANJA LA MALEMU CHILIMA APEREKA PA MISAMakosana
มุมมอง 96K
Pr Bujingo Atuuse.Asabidee Namwandu Namuwa Amabugo Ga (1 Million) Shillings.Tindi Files
มุมมอง 19K
MANGANYA VS AKWENI - KWAPHULIKASO INA KU UTMMakosana
มุมมอง 51K
CCAPYUM SERVICEMVAMA CCAP NKHOMA SYNOD (Rev. Yassin Gammah)
มุมมอง 208K
Zomwe Zinachitika Kut Ndege IsoweSam Malvitha
มุมมอง 229K
Charley Patache - Barman - Malawi Official Music VideoMALAWI MUSIC TV
มุมมอง 394K
JOSHUA VARELA KUDZUDZULA MKHALIDWE OIPA OKHUDZA IMFA YA SAULOS CHILIMAMALAWI TODAY
มุมมอง 82K
มายคราฟ แต่คุณ"แกล้ง"ผมได้!? #minecraft #minecraftbut #มายคราฟ #กดไลค์GOLF BACK HEART
มุมมอง 117K
[TH] VALORANT Champions Seoul - Playoffs Day 5 - FNC vs SENVALORANT Esports Thailand
มุมมอง 138K
นี่คือ Texture Pack ที่โคตรจะสมจริงที่สุด!!! #เกมกับshorts #minecraftMrWattana
มุมมอง 822K
"มนต์ชัย" ชนะขาดลอย นั่งนายก อบจ.พิษณุโลก อีกสมัยสํานักข่าวไทย TNAMCOT
มุมมอง 160K
Prank vs Prank #shortsMr DegrEE
มุมมอง 3.8M
เปิดหน้าพ่อแม่ครั้งแรก! ไม่เคยบอกใครมาทั้งชีวิตเพราะ?Ajumma Nammy
มุมมอง 551K
Musavutike umboni tinaupeza kale black box ilikuti nanga maphone alikuti anthu wonse anali ndimaphone ndichifukwa chiyani anali wovulidwa zovala
Kumadziwatu kuti Chilima wachita ku phedwa ndi a MCP,paja mwalandira ndalama a wonder
Ine wonder amandionekera wa mcp aaa
Chilima sangaphedwe chonchija!!🙆🙆🏽🤦.....we have nothing to lose....we are coming
Kodi ndege ndiyomweso inamvula chilima dzovala ?chilingamo mukufuna inuso ndiye chiti chionadi mukuchidziwa
Odziiwa salankhula zambiri amangoti Insha Allah kutanthauza kuti zonse akudziwa ndi mulungu ndipo ndi mwini zonse
Zoona mbale moti anthu wose adakaganiza choncho zikanakhala bwino
Agalu abodza ife chilungamu tachidziwa muzinamiza ana osati ife amalawi, mwapha anthu afiti inu
Ndege yagwera kutali ndi midzi ya anthu yeti it's not far from villegers ndiye iyeyu sanadziwe kuti amanama zosezi ngati alibe choyankhula akhale chete komanso zonsezo zikanati ndi zabwino zokhuza za zosatira za kuchipatala ko bwedzi abanja sanabwere poyera why delay yeti aziti angonenapo izi zokha zinazo azanenabe, presdent wanuyi has something to do ndi imfa ya chilima period
Report lachani umboni ife tilinawo jacket anamumvula ndani?? Nsapato anamumvula ndani?? Osawopa chakwela wapha chilima umboni ife tilinawo
Nose ndinu zinsiru kwambiri amene mukufotokoza maboza anu Chakwera wamupha muzake 😢😢
Ine zikundidabwitsa Kuti mchifukwa chani akubanja akuti satulutsa report lonse,akubisa chani????? Apatu zangoonetseratu Kuti zomwe anthu ambiri akulankhula Kuti a Chilima anachita kuphedwa,zomwe akupanga a boma kumamanga anthu chifukwa choti akulankhula molira komaso kufusa mafuso pazodabwitsa zomwe zinachitikaso kutsatira ngozi imeneyi
Times chichitikileni malilo achilima chinachake pakatipani chachitika ma program anu sakukoma mukuyeneya muzikonze mukuonesa mbali muzochitika zanu
Kanakonda ndalamazo mulandile ndipo mudye koma muzima pachilungamo ndipo muzitiuza zoona😔😔
Nkhan ndyakut chakwera anamupha chilima ndi anzake mcp ndiyakupha kd chakwera chiyambire kulamura kumalawi ndi ngozi zingat,nanga anamuvura zovara chilima ndan samalani mulungu akukanthan nonse muli pambuyo pa chakwera
Kachilungamo aka ena sakondwa nako kuzolowela kunamizidwa times mwapamba kugwila tchito yeniyeni thanks
thank you for teaching us guys i agree with we must use our brains
Chachikulu akubanja afotokoza okha zilibwino ndiye makape ena azitengela za ndale chilungamo akubanja achiziwa
Abanja awophyedwa ndi Boma. Zoona zidzadziwika boma likadza sintha.
@@stevezulu2108 naweso ofoyilatu mene adaliri chilima uja anthu akwawo angaope boma ali ndi masapota ambili adafotokoza chilungamo palibe amene angachite naye matha chilungamo ndichimenecho Mulungu akuziwa chilichose
Ndipo ine uyuu wandebvuyi amandiyelamo kobs amazimva nzeru kom ndimbuli yothelatu
Chakwera anapha chilima musatinyase munachita kuwakhapa
Zoona zeni zeni tizaziziwa MCP ikazachoka pampando ndipo sikale.
Abusa akudziwawonkha kuti kugwa ndzanja la Yehova ndikowopsa akonda chinyengo asiyeni adzaziwona chimwemwe chawo adyelatu.
I am waiting 2025 all Malawian tikazavota amene azawineyo ndikukhala president boma limenero ndi lomwe lizachete kafukufuku wa ifa ya anthu amenewa amene anamwalira pa ngozi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere osatha 😭😭😭😭
Koma osayiwala Kuti mphekesera ili pawiri;
Kukhala yoona
Kapena...
Kukhala bodza😢😢
Ife sitikupanga nawo zinamizanani nokha nokha munamaliza amcp ndi kukhapa
Awanda amzanu munalinawo pa program wa sanati waze asadzabwereso mwamva?
And mukazilowetsa ndale mukulakwisa because muona ngati lamulo ndi loyipa
MUBISE MUNENE IFE TIKUDZIWA KUTI CHAKWERA,ANACHITA PLAN YOPHA CHILIMA MUKUCHWDWA NAWO UMBONI WANU NDIPO CHAKWERA UFA OSANYELA IWE UWONASO
Wander ukungonena chakwela mwina kt alindimamina mumutu
Mboni yayikulu ndi Mulungu amene anali ku chikangawa amene amawona zonse,la 40 likadzakwana zizaulirika
Anthu kumalawi kuno amasangalala ndimabodza gwelo LA zonsezi ndiumbuli basi
Azanena akazakhumudwisana 😢😢zitapanga xpire😢😢😢😢
Andevu zamwayi zanu munadya kale simunganene zoipa za Mcp ayi
Tidzingo koment zachina JB zachina ntanyiwa bakili muluzi TV ndi ena akunjawo bas ife sitidzilemba km ma koment kwaolemba akunjawo bas
Zawusilutu zoti tidzinamizana 😮😮
Atolankhani achinyengo awa tonse tikudziwa kuti ndalama za magazi zilizonse ponse
Pitani mukatenge black box ya ndege tinve kuti inapanga record zotani pamene ngodzi inkachitika pamenepo ndipu tipenze umboni basi.
Akukanika bwanji kuulusa .nde mabodzawo azinenambe anthuwotu
Nde akubitsa chifukwa chani! Or asaneneso zilibe tchito so abitsa bwanji kunena uthenga wenweni 😡😡😡
Etii angotipwetekatsa mtima
Well come dont forget kuti every accident has acause,car ,motor bike,an aeroplane lets just calm we wiil have good answers dont talk things without umboni because its acrime
Nkhani ni 2025 pakuvota ndipo muzamumanyila kuti MCP tikukhumba yayi apa bwebwetani umo munga bwebwetele muzamumanya kuti Sono ndipo tavota mwakulira maliro Nadi njani wangakhumbaso wafwiti wakupemphera tikamuvoterani chifukwa Cha malemu
mafuso ndiye ambiri choti muziwe vuto mphanvu tilibe bs mthaw yanu
Kodi amene akupanga defend chakwelayi amupasa zingati akuona ngati akunamizatu mwana wakwaotu cz zokhuza ngozi zija msagwilise njira yowaseka pakamwa anthu kuti alankhule, komanso funso ndiloti kodi zomwe amapanga a silikali wo zoti tiyeni tikasake ndege uku osati kwinako amawalangiza ndi ndani komanso potumidza anthu nine akasake ndege zimenedzo ukudziona kuti ndi zazeru komanso kusiisidwa kwa kufufuza ndege basi nkhani zonsezo iweyo ndi ukadaulo wakowo sungaone kuti something was off here, let malawian explain there views malingana ndi momwe a presdent anuwo anapelekera uthenga wao unali osagwira.
Olo ingo zisiyani.
mabodza ayamba osanena moopa ayi anafa ndi mabala ayi
Achitsilu chamunthu a ndevu zatsoka mulungu akulangani inu agalu
Ineso pang'ono ndayambaso kudanwa nazo mmmmm ndalamatu inapha yesu tisaiwale. Athuwa ...........????????
Mukundisokosera mukanena zotsatira za kuchipatala mmalo monena zakugwa kwa ndege?!!
Akubanja anena chilungamo ndipo tadziwa basi otukwanawa ndimowa ndifodya
Chinachitikq ndichan kuti ndege igwe??
Ndichifukwa chani akumanga wina aliyense woyankhura fir the whyy
Later kumafufuza
Mwapha Munthu
Koma mwina achita bwino kusanena iwowo akubanja ndimtaya makoko .
Chilungamo chizaziwika basi
Chakwera anampha chilima ndemukukamba chani nkunkuyu zikhare ngoma nose muzaziona analakwanji chilima
Mcp yakumpha
Posaikira kumbuyo chipani km malire a ufulu akalankhulidwe ndiofunika kwambri kuyambiri kuzako, makolo , pantchito ngakhale pa mudzi izi ndizofunika koma ndale zikutiyiwalitsa zosezi.
PALIBE CHANZERU MUKUYANKHULAPO APA NDI ANA OMWE AKUDZIWA KUTI CHAKWERA NDAMENE ANAPHA CHILIMA, OSAMAYANKHULA MOZEMBA KAPENA MUKUOPA KUKUKWEZANI NDEGE NANU IYAAAAAA, MUKAONA KUTI ZOKAMBAZANU NDI ZOZEMBAITSA KUIKIRA KUMBUYO BOMA NDIYE MUTSEKE MA PROGRAM ANUO MUSATINYASENAZO , ANTHU ALI NDI UFULU OYANKHULA TIRI MU DEMOCRACY, MUKAKAMBA ZA POLICE KUMALAWI KULIBE A POLICE KULIBESO ACHITETEZO
Komaso apolisi naonso akuyenera kuphunzitsidwa mokwanira,akuyenera kuti lamulo limeneli alimvetse,asangotumidwa ai
Chakwela killed his vice
Agalu inu ngati simukuziwa chimene mukupanga kuli bwino mungokhala sibwino kuyiyimira MCP chipani chamagazi
All of you one day you will pay one by one for what you did to Chilima and others
Palibe Cha zelu chomwe mukukamba apa tiziwa kusogoloku a MCP akazagwa m,boma
Palibe chotukwana koma akubanja ndi anzeru siopusa koma wanzeeu sangamasure pano kumbukirani pa bingu anafotokoza chinapha bingu???? anthu amzeru amatero kuti mlungu awamenyere nkhondo popeza zachitika kale
Zopusa chakwera ndiwakupha basi olo Mbiri yake ndinyasa wapha Mia, busa wake reason kufuna mpando
NDALAMA MDANI WA CHILUNGAMO
Zoona zidzadziwika MCP ikadza choka Mboma.
Paja madolowatu adya za MCP sizodabwisa
Zitsiru Inu mwadya ndarama zochuruka thus why mukuyakhurah zopusaaa
Guys Malawi wathapo basi tivomeleze, mpaka wonder kumayankhula moduka mutu
chonchi! Ndiye amene angatiimile ndindani?
Dziko silinathe vuto lilipo ndilakut mumakonda ma negative
Uyunso wadya ndalama zaboma
Nonsese
Umbuli ndikufa nanga kumafika pomagenda m'mdipiti wa galimoto zonyamula maliro pali umunthu pamenepo .
Imeneyoo timayintcha aggressive ndizinthu zopusa mafunaaa tizisekererah inunso umbuli mulinawo cozi mukufusa funso lopusa kwambiri
Inu achina wander dyani ndalamazo ndi chakwera zisiru lnu times palibe chazeru pano
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Akuyankhula apapa panya pawo ndithu
Mmalawi wina aliyense akudziwa chozachita 2025 sikuti azavota chifukwa cha mayankhulidwe anu koma nkhalidwe
Kodi anthu Inu atakhara mbale kapena mwana wanu mukhoza kuyankhula zokhuta choncho
Chakwera anyoxedwabe asiye uchigawega
Zao izo or cent sidadyepo nde worries what bisani
Khoswe akakhala pa khate sapheka zikanakhala kuti Dr saulosi chilima sanaphedwe bwezi panopa zosatilazo zitawulusidwa kale kale chifukwa black box siyikanasowa koma kusowa ko ndikumwe kukupangisani kuti muziyikila kumbuyo boma limeneri
Tizakumana pakachele bola chilungamo tuchidziwa
Anthu aku ena I inu so kuti mwadya buns ya mcp
Pa... Pako
Izizi nde ndizopoila kuti tizinamizana
Chinyengo ichi agalu inu
Munagulidwa Ndi mcp agalu inu
Ndinu zitsilu malibe chazeru
Zitsiru izi zinadya ndalama
Chibanzi😂😂😂😂😂😂
koma eee msova a dpp
Pano akutiuza zina kusongolokuso azatiuza zina akubanjayoo
Man akubanjawo apasidwa chiseka pakamwa apapa zaoneselatu chifukwa palibe chobisila choona choti chimasule amalawi tathandiza kulila lelo akatibisile alibe chisoni nafe ata ine basi ndazituluka akubanjawo mwina alandila ma banzi
Define assassination
Taziyayakhurani zanzeruuu ngati ma citizens amalawi bax bzy talking foolish thing yr stupt you tow gys mukuwona ngati mwawinaaa time yovata ikubwerah muzarirah ng,weee😂😂😂😂
Eee
MCP ndi yakupha
Yaaaaa
Y
Lie statement isn't true
Mwaononga kawailesi kanu takasika
Indeeee awonongadi Wailesi yawo pano sitikumvetseranso tasiya kuwadalira
leave chakwera alone put the matter in the hand of God
Don't post this .who a u.
Ufulu omwewu anthu akuphilira Za pa Social media in the end akupangidwa scam.