ไม่สามารถเล่นวิดีโอนี้
ขออภัยในความไม่สะดวก

kwagwanji wa report lomwe achipatala atulutsa lokhudza Imfa ya Dr Chilima 😢

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 28 มิ.ย. 2024

ความคิดเห็น • 116

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw หลายเดือนก่อน +3

    Musavutike umboni tinaupeza kale black box ilikuti nanga maphone alikuti anthu wonse anali ndimaphone ndichifukwa chiyani anali wovulidwa zovala

  • @SymonNamalomba-sh3fu
    @SymonNamalomba-sh3fu หลายเดือนก่อน +3

    Kumadziwatu kuti Chilima wachita ku phedwa ndi a MCP,paja mwalandira ndalama a wonder

    • @TheresaKuluwemba
      @TheresaKuluwemba หลายเดือนก่อน +1

      Ine wonder amandionekera wa mcp aaa

  • @frankjolijo
    @frankjolijo หลายเดือนก่อน +2

    Chilima sangaphedwe chonchija!!🙆🙆🏽🤦.....we have nothing to lose....we are coming

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma หลายเดือนก่อน +4

    Kodi ndege ndiyomweso inamvula chilima dzovala ?chilingamo mukufuna inuso ndiye chiti chionadi mukuchidziwa

  • @JiyaWilliam-g8y
    @JiyaWilliam-g8y หลายเดือนก่อน +3

    Odziiwa salankhula zambiri amangoti Insha Allah kutanthauza kuti zonse akudziwa ndi mulungu ndipo ndi mwini zonse

    • @user-kt5bq2wg6v
      @user-kt5bq2wg6v หลายเดือนก่อน

      Zoona mbale moti anthu wose adakaganiza choncho zikanakhala bwino

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 หลายเดือนก่อน +2

    Agalu abodza ife chilungamu tachidziwa muzinamiza ana osati ife amalawi, mwapha anthu afiti inu

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl หลายเดือนก่อน +2

    Ndege yagwera kutali ndi midzi ya anthu yeti it's not far from villegers ndiye iyeyu sanadziwe kuti amanama zosezi ngati alibe choyankhula akhale chete komanso zonsezo zikanati ndi zabwino zokhuza za zosatira za kuchipatala ko bwedzi abanja sanabwere poyera why delay yeti aziti angonenapo izi zokha zinazo azanenabe, presdent wanuyi has something to do ndi imfa ya chilima period

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h หลายเดือนก่อน +3

    Report lachani umboni ife tilinawo jacket anamumvula ndani?? Nsapato anamumvula ndani?? Osawopa chakwela wapha chilima umboni ife tilinawo

  • @MatthewsJohn-kv8fj
    @MatthewsJohn-kv8fj หลายเดือนก่อน +1

    Nose ndinu zinsiru kwambiri amene mukufotokoza maboza anu Chakwera wamupha muzake 😢😢

  • @ShabaniKuswere
    @ShabaniKuswere หลายเดือนก่อน +2

    Ine zikundidabwitsa Kuti mchifukwa chani akubanja akuti satulutsa report lonse,akubisa chani????? Apatu zangoonetseratu Kuti zomwe anthu ambiri akulankhula Kuti a Chilima anachita kuphedwa,zomwe akupanga a boma kumamanga anthu chifukwa choti akulankhula molira komaso kufusa mafuso pazodabwitsa zomwe zinachitikaso kutsatira ngozi imeneyi

  • @user-zo3bf3ec3g
    @user-zo3bf3ec3g หลายเดือนก่อน +1

    Times chichitikileni malilo achilima chinachake pakatipani chachitika ma program anu sakukoma mukuyeneya muzikonze mukuonesa mbali muzochitika zanu
    Kanakonda ndalamazo mulandile ndipo mudye koma muzima pachilungamo ndipo muzitiuza zoona😔😔

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm หลายเดือนก่อน +1

    Nkhan ndyakut chakwera anamupha chilima ndi anzake mcp ndiyakupha kd chakwera chiyambire kulamura kumalawi ndi ngozi zingat,nanga anamuvura zovara chilima ndan samalani mulungu akukanthan nonse muli pambuyo pa chakwera

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of หลายเดือนก่อน +1

    Kachilungamo aka ena sakondwa nako kuzolowela kunamizidwa times mwapamba kugwila tchito yeniyeni thanks

  • @iangondwe6857
    @iangondwe6857 หลายเดือนก่อน

    thank you for teaching us guys i agree with we must use our brains

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj หลายเดือนก่อน +2

    Chachikulu akubanja afotokoza okha zilibwino ndiye makape ena azitengela za ndale chilungamo akubanja achiziwa

    • @stevezulu2108
      @stevezulu2108 หลายเดือนก่อน

      Abanja awophyedwa ndi Boma. Zoona zidzadziwika boma likadza sintha.

    • @SaidiMbawa-st6bj
      @SaidiMbawa-st6bj หลายเดือนก่อน

      @@stevezulu2108 naweso ofoyilatu mene adaliri chilima uja anthu akwawo angaope boma ali ndi masapota ambili adafotokoza chilungamo palibe amene angachite naye matha chilungamo ndichimenecho Mulungu akuziwa chilichose

  • @AlfredNazombe-me2ly
    @AlfredNazombe-me2ly หลายเดือนก่อน +2

    Ndipo ine uyuu wandebvuyi amandiyelamo kobs amazimva nzeru kom ndimbuli yothelatu

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma หลายเดือนก่อน +2

    Chakwera anapha chilima musatinyase munachita kuwakhapa

  • @RabeccaMpunga
    @RabeccaMpunga หลายเดือนก่อน +1

    Zoona zeni zeni tizaziziwa MCP ikazachoka pampando ndipo sikale.

  • @ZakaliyaAlick
    @ZakaliyaAlick หลายเดือนก่อน +1

    Abusa akudziwawonkha kuti kugwa ndzanja la Yehova ndikowopsa akonda chinyengo asiyeni adzaziwona chimwemwe chawo adyelatu.

  • @augustMag
    @augustMag หลายเดือนก่อน +1

    I am waiting 2025 all Malawian tikazavota amene azawineyo ndikukhala president boma limenero ndi lomwe lizachete kafukufuku wa ifa ya anthu amenewa amene anamwalira pa ngozi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere osatha 😭😭😭😭

  • @user-hq8yn8tl1h
    @user-hq8yn8tl1h หลายเดือนก่อน +1

    Koma osayiwala Kuti mphekesera ili pawiri;
    Kukhala yoona
    Kapena...
    Kukhala bodza😢😢

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x หลายเดือนก่อน +1

    Ife sitikupanga nawo zinamizanani nokha nokha munamaliza amcp ndi kukhapa

  • @MosesSolomoni
    @MosesSolomoni หลายเดือนก่อน +1

    Awanda amzanu munalinawo pa program wa sanati waze asadzabwereso mwamva?

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias9972 หลายเดือนก่อน +1

    And mukazilowetsa ndale mukulakwisa because muona ngati lamulo ndi loyipa

  • @HaliJana
    @HaliJana หลายเดือนก่อน +1

    MUBISE MUNENE IFE TIKUDZIWA KUTI CHAKWERA,ANACHITA PLAN YOPHA CHILIMA MUKUCHWDWA NAWO UMBONI WANU NDIPO CHAKWERA UFA OSANYELA IWE UWONASO

  • @AishaChipande
    @AishaChipande หลายเดือนก่อน +1

    Wander ukungonena chakwela mwina kt alindimamina mumutu

  • @Doreen-yl3qm
    @Doreen-yl3qm หลายเดือนก่อน +1

    Mboni yayikulu ndi Mulungu amene anali ku chikangawa amene amawona zonse,la 40 likadzakwana zizaulirika

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of หลายเดือนก่อน +1

    Anthu kumalawi kuno amasangalala ndimabodza gwelo LA zonsezi ndiumbuli basi

  • @user-hq8yn8tl1h
    @user-hq8yn8tl1h หลายเดือนก่อน

    Azanena akazakhumudwisana 😢😢zitapanga xpire😢😢😢😢

  • @mathewsmakina7845
    @mathewsmakina7845 หลายเดือนก่อน +1

    Andevu zamwayi zanu munadya kale simunganene zoipa za Mcp ayi

  • @MosesSolomoni
    @MosesSolomoni หลายเดือนก่อน +1

    Tidzingo koment zachina JB zachina ntanyiwa bakili muluzi TV ndi ena akunjawo bas ife sitidzilemba km ma koment kwaolemba akunjawo bas

  • @AyandaPhungula-bg9ql
    @AyandaPhungula-bg9ql หลายเดือนก่อน +1

    Zawusilutu zoti tidzinamizana 😮😮

  • @EsnartMartin
    @EsnartMartin หลายเดือนก่อน +1

    Atolankhani achinyengo awa tonse tikudziwa kuti ndalama za magazi zilizonse ponse

  • @user-sz6bi3tw5y
    @user-sz6bi3tw5y หลายเดือนก่อน

    Pitani mukatenge black box ya ndege tinve kuti inapanga record zotani pamene ngodzi inkachitika pamenepo ndipu tipenze umboni basi.

  • @PempheroAlufandika
    @PempheroAlufandika หลายเดือนก่อน +1

    Akukanika bwanji kuulusa .nde mabodzawo azinenambe anthuwotu

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga หลายเดือนก่อน +1

    Nde akubitsa chifukwa chani! Or asaneneso zilibe tchito so abitsa bwanji kunena uthenga wenweni 😡😡😡

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias9972 หลายเดือนก่อน

    Well come dont forget kuti every accident has acause,car ,motor bike,an aeroplane lets just calm we wiil have good answers dont talk things without umboni because its acrime

  • @HildaMbizi
    @HildaMbizi 22 วันที่ผ่านมา

    Nkhani ni 2025 pakuvota ndipo muzamumanyila kuti MCP tikukhumba yayi apa bwebwetani umo munga bwebwetele muzamumanya kuti Sono ndipo tavota mwakulira maliro Nadi njani wangakhumbaso wafwiti wakupemphera tikamuvoterani chifukwa Cha malemu

  • @user-bl6km6kx7n
    @user-bl6km6kx7n หลายเดือนก่อน +1

    mafuso ndiye ambiri choti muziwe vuto mphanvu tilibe bs mthaw yanu

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl หลายเดือนก่อน +1

    Kodi amene akupanga defend chakwelayi amupasa zingati akuona ngati akunamizatu mwana wakwaotu cz zokhuza ngozi zija msagwilise njira yowaseka pakamwa anthu kuti alankhule, komanso funso ndiloti kodi zomwe amapanga a silikali wo zoti tiyeni tikasake ndege uku osati kwinako amawalangiza ndi ndani komanso potumidza anthu nine akasake ndege zimenedzo ukudziona kuti ndi zazeru komanso kusiisidwa kwa kufufuza ndege basi nkhani zonsezo iweyo ndi ukadaulo wakowo sungaone kuti something was off here, let malawian explain there views malingana ndi momwe a presdent anuwo anapelekera uthenga wao unali osagwira.

  • @stevezulu2108
    @stevezulu2108 หลายเดือนก่อน +1

    Olo ingo zisiyani.

  • @user-dn6eg1xk7f
    @user-dn6eg1xk7f หลายเดือนก่อน +1

    mabodza ayamba osanena moopa ayi anafa ndi mabala ayi

  • @user-cr6if6tz6d
    @user-cr6if6tz6d หลายเดือนก่อน +1

    Achitsilu chamunthu a ndevu zatsoka mulungu akulangani inu agalu

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb หลายเดือนก่อน

    Ineso pang'ono ndayambaso kudanwa nazo mmmmm ndalamatu inapha yesu tisaiwale. Athuwa ...........????????

  • @user-ec4jo9cu4d
    @user-ec4jo9cu4d หลายเดือนก่อน

    Mukundisokosera mukanena zotsatira za kuchipatala mmalo monena zakugwa kwa ndege?!!

  • @user-ml2vw1dc9c
    @user-ml2vw1dc9c หลายเดือนก่อน

    Akubanja anena chilungamo ndipo tadziwa basi otukwanawa ndimowa ndifodya

  • @MatthewsJohn-kv8fj
    @MatthewsJohn-kv8fj หลายเดือนก่อน

    Chinachitikq ndichan kuti ndege igwe??

  • @FloridaMakwinja-eq2ek
    @FloridaMakwinja-eq2ek หลายเดือนก่อน

    Ndichifukwa chani akumanga wina aliyense woyankhura fir the whyy
    Later kumafufuza

  • @AufiThera
    @AufiThera หลายเดือนก่อน +1

    Mwapha Munthu

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona หลายเดือนก่อน

    Koma mwina achita bwino kusanena iwowo akubanja ndimtaya makoko .

  • @wonganichakakanyirenda3299
    @wonganichakakanyirenda3299 หลายเดือนก่อน +1

    Chilungamo chizaziwika basi

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb หลายเดือนก่อน

    Chakwera anampha chilima ndemukukamba chani nkunkuyu zikhare ngoma nose muzaziona analakwanji chilima

  • @NdamvaScnp
    @NdamvaScnp หลายเดือนก่อน +1

    Mcp yakumpha

  • @RobertCosmas-bo1uo
    @RobertCosmas-bo1uo หลายเดือนก่อน

    Posaikira kumbuyo chipani km malire a ufulu akalankhulidwe ndiofunika kwambri kuyambiri kuzako, makolo , pantchito ngakhale pa mudzi izi ndizofunika koma ndale zikutiyiwalitsa zosezi.

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon หลายเดือนก่อน

    PALIBE CHANZERU MUKUYANKHULAPO APA NDI ANA OMWE AKUDZIWA KUTI CHAKWERA NDAMENE ANAPHA CHILIMA, OSAMAYANKHULA MOZEMBA KAPENA MUKUOPA KUKUKWEZANI NDEGE NANU IYAAAAAA, MUKAONA KUTI ZOKAMBAZANU NDI ZOZEMBAITSA KUIKIRA KUMBUYO BOMA NDIYE MUTSEKE MA PROGRAM ANUO MUSATINYASENAZO , ANTHU ALI NDI UFULU OYANKHULA TIRI MU DEMOCRACY, MUKAKAMBA ZA POLICE KUMALAWI KULIBE A POLICE KULIBESO ACHITETEZO

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i หลายเดือนก่อน

    Komaso apolisi naonso akuyenera kuphunzitsidwa mokwanira,akuyenera kuti lamulo limeneli alimvetse,asangotumidwa ai

  • @Hellenistic109
    @Hellenistic109 28 วันที่ผ่านมา

    Chakwela killed his vice

  • @user-cr6if6tz6d
    @user-cr6if6tz6d หลายเดือนก่อน

    Agalu inu ngati simukuziwa chimene mukupanga kuli bwino mungokhala sibwino kuyiyimira MCP chipani chamagazi

  • @ThokozaniSaiti
    @ThokozaniSaiti หลายเดือนก่อน

    All of you one day you will pay one by one for what you did to Chilima and others

  • @user-dn3gp6yi4y
    @user-dn3gp6yi4y หลายเดือนก่อน

    Palibe Cha zelu chomwe mukukamba apa tiziwa kusogoloku a MCP akazagwa m,boma

  • @mphatsomonjeza4371
    @mphatsomonjeza4371 หลายเดือนก่อน

    Palibe chotukwana koma akubanja ndi anzeru siopusa koma wanzeeu sangamasure pano kumbukirani pa bingu anafotokoza chinapha bingu???? anthu amzeru amatero kuti mlungu awamenyere nkhondo popeza zachitika kale

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz หลายเดือนก่อน +1

    Zopusa chakwera ndiwakupha basi olo Mbiri yake ndinyasa wapha Mia, busa wake reason kufuna mpando

  • @HenryLaidon-pl9ly
    @HenryLaidon-pl9ly หลายเดือนก่อน

    NDALAMA MDANI WA CHILUNGAMO

  • @stevezulu2108
    @stevezulu2108 หลายเดือนก่อน

    Zoona zidzadziwika MCP ikadza choka Mboma.

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy หลายเดือนก่อน

    Paja madolowatu adya za MCP sizodabwisa

  • @MadalitsoTamayenda-ez5pj
    @MadalitsoTamayenda-ez5pj หลายเดือนก่อน

    Zitsiru Inu mwadya ndarama zochuruka thus why mukuyakhurah zopusaaa

  • @JTUPHIRI
    @JTUPHIRI หลายเดือนก่อน

    Guys Malawi wathapo basi tivomeleze, mpaka wonder kumayankhula moduka mutu
    chonchi! Ndiye amene angatiimile ndindani?

    • @RABSONSIKELO
      @RABSONSIKELO หลายเดือนก่อน

      Dziko silinathe vuto lilipo ndilakut mumakonda ma negative

  • @user-sf7sd1hb4g
    @user-sf7sd1hb4g หลายเดือนก่อน

    Uyunso wadya ndalama zaboma

  • @lacfunnytv1251
    @lacfunnytv1251 หลายเดือนก่อน

    Nonsese

  • @JacobTMarko
    @JacobTMarko หลายเดือนก่อน

    Umbuli ndikufa nanga kumafika pomagenda m'mdipiti wa galimoto zonyamula maliro pali umunthu pamenepo .

    • @MadalitsoTamayenda-ez5pj
      @MadalitsoTamayenda-ez5pj หลายเดือนก่อน

      Imeneyoo timayintcha aggressive ndizinthu zopusa mafunaaa tizisekererah inunso umbuli mulinawo cozi mukufusa funso lopusa kwambiri

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb หลายเดือนก่อน

    Inu achina wander dyani ndalamazo ndi chakwera zisiru lnu times palibe chazeru pano

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI หลายเดือนก่อน

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @Gautengstanzo
    @Gautengstanzo หลายเดือนก่อน

    Akuyankhula apapa panya pawo ndithu

  • @russellsombwa1609
    @russellsombwa1609 หลายเดือนก่อน

    Mmalawi wina aliyense akudziwa chozachita 2025 sikuti azavota chifukwa cha mayankhulidwe anu koma nkhalidwe

  • @DafterChitema
    @DafterChitema หลายเดือนก่อน

    Kodi anthu Inu atakhara mbale kapena mwana wanu mukhoza kuyankhula zokhuta choncho

  • @OscarKJekapu
    @OscarKJekapu 27 วันที่ผ่านมา

    Chakwera anyoxedwabe asiye uchigawega

  • @user-dg5pc6rz1b
    @user-dg5pc6rz1b หลายเดือนก่อน

    Zao izo or cent sidadyepo nde worries what bisani

  • @DiversonChimenya-h2u
    @DiversonChimenya-h2u หลายเดือนก่อน

    Khoswe akakhala pa khate sapheka zikanakhala kuti Dr saulosi chilima sanaphedwe bwezi panopa zosatilazo zitawulusidwa kale kale chifukwa black box siyikanasowa koma kusowa ko ndikumwe kukupangisani kuti muziyikila kumbuyo boma limeneri

  • @phillipmphanda2163
    @phillipmphanda2163 หลายเดือนก่อน

    Tizakumana pakachele bola chilungamo tuchidziwa

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx หลายเดือนก่อน

    Anthu aku ena I inu so kuti mwadya buns ya mcp

  • @AceelectricalengineeringAEE
    @AceelectricalengineeringAEE หลายเดือนก่อน

    Pa... Pako

  • @Sophisticate230
    @Sophisticate230 หลายเดือนก่อน

    Izizi nde ndizopoila kuti tizinamizana

  • @AshlafHakimi
    @AshlafHakimi หลายเดือนก่อน

    Chinyengo ichi agalu inu

  • @BerthThomas-v9l
    @BerthThomas-v9l หลายเดือนก่อน

    Munagulidwa Ndi mcp agalu inu

  • @OscarKJekapu
    @OscarKJekapu 27 วันที่ผ่านมา

    Ndinu zitsilu malibe chazeru

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d หลายเดือนก่อน

    Zitsiru izi zinadya ndalama

  • @user-hq8yn8tl1h
    @user-hq8yn8tl1h หลายเดือนก่อน

    Chibanzi😂😂😂😂😂😂

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 หลายเดือนก่อน

    koma eee msova a dpp

  • @wonganichakakanyirenda3299
    @wonganichakakanyirenda3299 หลายเดือนก่อน

    Pano akutiuza zina kusongolokuso azatiuza zina akubanjayoo

    • @ChikondiLikapa
      @ChikondiLikapa หลายเดือนก่อน

      Man akubanjawo apasidwa chiseka pakamwa apapa zaoneselatu chifukwa palibe chobisila choona choti chimasule amalawi tathandiza kulila lelo akatibisile alibe chisoni nafe ata ine basi ndazituluka akubanjawo mwina alandila ma banzi

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt หลายเดือนก่อน

    Define assassination

  • @MadalitsoTamayenda-ez5pj
    @MadalitsoTamayenda-ez5pj หลายเดือนก่อน

    Taziyayakhurani zanzeruuu ngati ma citizens amalawi bax bzy talking foolish thing yr stupt you tow gys mukuwona ngati mwawinaaa time yovata ikubwerah muzarirah ng,weee😂😂😂😂

  • @TaweniChavulaKamwendo
    @TaweniChavulaKamwendo หลายเดือนก่อน

    Eee

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y หลายเดือนก่อน +1

    MCP ndi yakupha

  • @PeterKayuni-n2r
    @PeterKayuni-n2r หลายเดือนก่อน

    Yaaaaa

  • @chifundoKaluvi-ey5uw
    @chifundoKaluvi-ey5uw 16 วันที่ผ่านมา

    Y

  • @ZakariasintidomathengaMathenga
    @ZakariasintidomathengaMathenga หลายเดือนก่อน

    Lie statement isn't true

  • @JimsonChisi
    @JimsonChisi หลายเดือนก่อน

    Mwaononga kawailesi kanu takasika

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os หลายเดือนก่อน

      Indeeee awonongadi Wailesi yawo pano sitikumvetseranso tasiya kuwadalira

  • @iangondwe6857
    @iangondwe6857 หลายเดือนก่อน

    leave chakwera alone put the matter in the hand of God

  • @courageouslondo1986
    @courageouslondo1986 หลายเดือนก่อน

    Don't post this .who a u.

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba หลายเดือนก่อน

    Ufulu omwewu anthu akuphilira Za pa Social media in the end akupangidwa scam.