Chikangawa Party Ayikwiira

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 4 ก.พ. 2025

ความคิดเห็น • 27

  • @LameckNgwangwa-g3p
    @LameckNgwangwa-g3p 8 วันที่ผ่านมา +1

    Koma , shot one , nkhumba , black box ndi chikangawa ziliko

  • @RichardSandfol
    @RichardSandfol 9 วันที่ผ่านมา +3

    Nkhaniyabwino kwambiri,, APM VIC KABAMBE

  • @HajjAmadu-e1u
    @HajjAmadu-e1u 8 วันที่ผ่านมา

    Kweni mwayankhulatu za nzeru kwen ulemu wani zimenezo ndie nzeru osangotukwanapo ai koma fundo ndi zimenezo

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 9 วันที่ผ่านมา +1

    Chikangawa party....tsongoleri wache mbusa dzina lake Chakwera......wationongera Mother Malawi 🇲🇼 😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @AlexKaunda-w7l
    @AlexKaunda-w7l 9 วันที่ผ่านมา

    M'busa uziwa kupakula nyemba

  • @MabasoMafa
    @MabasoMafa 8 วันที่ผ่านมา

    Boma ndilomweli sitisintha opposition ndiyomweyi sitisintha mpaka 32yrs woohoo

  • @InacioCement-t7n
    @InacioCement-t7n 8 วันที่ผ่านมา

    Mr Brack box chileka nkhumbe
    Zakeyu ,yudasi Mulanje
    Mr chikangawa lilongwe
    Namajekete
    lilongwe
    Mai kasikha lilongwe chikangawa
    Chikono banda chikangawa
    Masten yo......
    Valentine's soldier soldier chikangawa

  • @GonçalvesXavier-l3z
    @GonçalvesXavier-l3z 9 วันที่ผ่านมา

    Nanga kamadjekete aliposo😂😂😂😂😂

  • @MonCellphone
    @MonCellphone 9 วันที่ผ่านมา +1

    Plz tangotenga system yaku south Africa for example misonkho ya kumupoto yikhale konko yipange chitukuko konko, pakat choncho ndikumwela choncho Malawi akhoza kusintha

  • @MonCellphone
    @MonCellphone 9 วันที่ผ่านมา +1

    Blessings chilungamo ndichimecho mwina malawi angapulumke , koma so asiye zo pempha mayiko ena zopanda ulemu, siungayendese banja ndizopemphesa ayi, tizidalire tokha, taonani, Donald Trump waturuka mu (Who) world health organization, a Malawi mkalowa muboma siyan Kuba tukulani dziko lanu plz ndapaoata

  • @MartinNgoma-tp2jk
    @MartinNgoma-tp2jk 9 วันที่ผ่านมา +1

    Ndiye kulankhula koziwazasogolo 🇿🇲

  • @LameckNgwangwa-g3p
    @LameckNgwangwa-g3p 9 วันที่ผ่านมา +1

    Mbuzii za mcp

  • @AmandaConstance-fx8cr
    @AmandaConstance-fx8cr 9 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkkkk Mr Blackbox😂😂😂😂😂😂

  • @giftkayome3568
    @giftkayome3568 9 วันที่ผ่านมา

    Chikangawa government 😂😂
    Chilungamo wakamba mubale

  • @SaladeKimu
    @SaladeKimu 7 วันที่ผ่านมา

    Both APM and DK are lhomwes sikubalansa

  • @YusufMaulidi-b2c
    @YusufMaulidi-b2c 9 วันที่ผ่านมา

    Dziko la malawi lizasintha nthawi yomwe lizasinthe malamulo onena kuti president akalakwa he needs to step aside for investigation akapezeka osalakwa step in again apo bii aliyense aziba chifukwa akudziwa kuti sindingayimbidwe mulandu

  • @lovemorengwira
    @lovemorengwira 9 วันที่ผ่านมา

    Iweyo izizi Kaya wumazitenga Kuti. Ma President sangachokere mu region yimozi, uwu si ufumu. Mistake iyi ndiyomwe anapanga kusankha CHIMULILENJI.

  • @SimonBanda-b1f
    @SimonBanda-b1f 9 วันที่ผ่านมา

    Mugwirizano zipani zikuwopa chifukwa cha Chikangawa party inachita nkhanza kukana after atawina kuti panalibe mugwirizano.
    Koma Chikangawa party NDI a satana okha okha kaya akukatani Kuma church

  • @VictorBarratt
    @VictorBarratt 9 วันที่ผ่านมา

    You are talking on behalf of someone's interest.
    I suggest if there should be an alliance it would be good to the following party's to come together:
    UTM
    AFORD
    Nankhumwas Party
    This would be a powerful force.

  • @MeruMitha
    @MeruMitha 9 วันที่ผ่านมา

    😮😮😮😮😮😮😮😮😮😮

  • @shamechirambo
    @shamechirambo 9 วันที่ผ่านมา

    Ndiye walunkhula bwino,bola kusiya zakale zoyipa.

  • @WittinessNkhokwe-q7h
    @WittinessNkhokwe-q7h 9 วันที่ผ่านมา

    Si m'busa Inu anangovala chikopa cha khosa awa ndi mimbulu iyi

  • @ClemenceChavula-q3r
    @ClemenceChavula-q3r 9 วันที่ผ่านมา

    I recommend you Blessings in all you have said

  • @CharlesJames-f1w
    @CharlesJames-f1w 9 วันที่ผ่านมา

    Amanganya.sibasi.mwakala.pasi.mumati.mutani

  • @MonCellphone
    @MonCellphone 9 วันที่ผ่านมา

    Plz tangotenga system yaku south Africa for example misonkho ya kumupoto yikhale konko yipange chitukuko konko, pakat choncho ndikumwela choncho Malawi akhoza kusintha