Dziko lathu lili ndi atsogoleli wovetsa chisoni mmaganizidwe awo ngati ana koma chonsecho ndi anthu wophunzila bwino thu kaya vuto ndi chiyani kaya, chimanga mmalo moti chipite kwa admarc aliyense adzikagula yekha, ali busy kugawa kwa anthu wowadziwa okha okha ndiye ena mukuwamanawa akagula kuti huuuu! More fire 🔥🔥 Born Lap ndo
Bwana Honorable Kalindo,
Mumatha and you represent Us.
Big up DC never stop fight for us
Abale timpange sapot bon kalindo uyu amayankhula zoonad
Kungoti Amalawi timadana ndi chilungamo
Boss DC your the best solar of malawi 🇲🇼
Wina Mr DC azapite azakhulupilile kuti inuyo ndimwana oopsa
Boom kalindo u is de best than MBC TV
The DC❤❤❤
More fire mr Bon Kalindo 🔥 🔥 🔥
Kamandiwaza komati MA kape aku area 30 😂😂😂😂😂 eeeee koma the DC ayi zikomo
Kkkkk bon kalindo ase
If all Malawians were Bon Kalindo,Malawi would be a paradise on earth!Where are
You my heavenly Father ???
🙏🙏🙏🙏
Dziko lathu lili ndi atsogoleli wovetsa chisoni mmaganizidwe awo ngati ana koma chonsecho ndi anthu wophunzila bwino thu kaya vuto ndi chiyani kaya, chimanga mmalo moti chipite kwa admarc aliyense adzikagula yekha, ali busy kugawa kwa anthu wowadziwa okha okha ndiye ena mukuwamanawa akagula kuti huuuu! More fire 🔥🔥 Born Lap ndo
Chief chief
Ulemu wanu mr Dc
Apiteso ku chiradzulu hospital utsiku magesi sayaka utsiku😂😂😂😂
DC ❤❤❤❤
❤ Congratulations Mr bon kalindo respect 🙏
😂😂😂😂😂😂😂 amwene bon kalindo ndaseka kwambili mwati winawake akufuna kukapepesa manyumba awathu ochita bwino 😂😂😂😂
DC 🎉🎉🎉🎉
Good your point
chesaopa the DC akatundu 🔥💪💪🔥
Anthu awawa sadzamva ayi kuuzidwa xochita Koma osasintha kachitidwe ka zinthu,KP it up B. Kalindo
Our 2 an' half Man, The most Dangerous
komatu lero M'mene zilirimu Mmalawi Muno palibe akupanga mademu Koma likangolowa M'boma la Dpp muzingot pang'ono pang'ono mademu
Ndiconco kumene cifukwa dpp ndi ya democrancy ndichifukwa anthu akuifuna kuti ibwelele kuti adzipanga dzomwe akufuna 💙💙💙💙💙
Fire the Dc kuyakhula kosaopa auzeni aziwe chimene akupanga ndizauchitsilu ndiye ine ndilipamodzi ndizimene mwayakhula lero God bless you
❤
The best bon kalindo
Kkkkkkk osat akupita kukapepha ameneyo 😂😂😂😂😂
Dziko silamunthu modzi km ndi lamalawi dziwani kt kunja kumada ndipo kumacha lamulo la dziko ukalitengela manja mwako ndi chimodzimodzi kumwa asidi samalani pakamwapo malawi ndiokwiya kwambiri zonse za padziko tinazipeza ndipo zotsala tidzasila ena ndibwino tingoyang'ana kumwamba chomwe atipatse yehova mulungu chikhala chomwecho cz tikapezerana zifukwa pano tingazuzike kutsogoloku komaso mwina kuzizitsa ana athu kapena abale athu kumene tiyeni tikhale anthu odzichepetsa ndi omvetsetsa masiku athakale awa zikomo
Kkkkkkk kma bon iwe anakonza
Boon kalindoooo😂
First viewer
VP nde ali busy kugawa ufa tima 2 kgs 😂😂😂😂😂😂😂🙌🏻🙌🏻🙌🏻🙌🏻🙌🏻
Kkkkk ali busy kuphikilira mphala ana mhuuuu kumalawi tiziona
Kkkkkk munthu yemwe sanaimepo pawindo la video show sangamuuze bon chochita 😂😂😂😂
Thawi ya kamuzu athu amachita zoipa mbiliyoyipayi imamuyipisa kamuzu zithuzina kamuzu samaziwa ndizomwe zikuchitkaso lelo ku mcp komweko athu akuwononga mbili zomwe zimugwese chakwela ndipo agwa ndithu omvesa chisoni
Mumatiimilira boss
😂😂😂😂😂😂 koma ndaseka chimodzimodzi Muthu kutunga madzi musinje kukanthira munyanja.
Muthu was mzeru wake kumatenga ndalama kumakapeleka Ku Amelikano 😂😂😂😂 izizi ndizashupiti zokhazokha ndinthu
Apapa boni kalindo akapanga kukumangani ndekut inu ndi mcp mukuziwana
Auzen the DC we are together
❤❤❤
No fear the DC
The DC
Mbuzi ya chabe chabe chakwera😂😂😂😂😂
THE DC😂😂😂😂😂
Makwana big 😂
Big kalindo pitilizani kutimenyela nkhondo osaukafe ..No more mcp 2025
Koma mpaka kukapepesa 😂😂😂 koma kumalawi kwakomatu
😂😂😂😂😂😂😂 mpaka makape
Our own pangolin
Kayambe masero ako aja
Ukali
Apm analosera kt 5years yamakape Mcp awa nyekweeee tiziwa bwino lelo hehedeee mai kokhwa ine
Bon kalindo machende ake
Boma la Mcp likupenga misala tikuona ndi Maso..liri stranded bomali it has nothing to deliver.what it does is kumanga anthu on political grounds
Koma ichichi chitivuta ndi2 hahahah 😂😂😂😂😂
Ndiye mbuzi zina nkumati boma ndlomweli mwina chilipo amakupasani kumbali
The DC president of poor people 🔥🔥🔥🔥
Yaaa bwana bon kalindo osafowoka nd mbuz za mcp ndi galu wawo chakwela
😢😢😢
Fire kalindo🔥🔥🔥📢 adad pamalo pawo 2025
Pangolin wa boma uyu kkkkkk 😂😂😂
Kkkk
Ndimakape ausilu bazooka iyendepo bwana kalindo commander ndikhara ine tingotenga boma president kalindo zatikwana kwambili
Nthawi ndiye yatha yatha auzeni komatu inu a opposition ku uzidwa zofunika ndiye muku uzidwa
Dc
Zomvesa chison kwambr 😢😢
The Dc mwana oopsa kwambili🎉🎉
Chitsiru cha president akukapepesa chani kufuna kuba misonkho yathu
Koditu olo mutabvula maliseche kumayankhula anthu awa alibe zomvera anakhalira zomvera zawo . Kkkkkkkkkk ndi mgaiwa wasowawu mwina kundendeko kulimsima eti
😂😂😂Bon Iweyo AYI udzangosowa basi
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Kuyankhula kotere kunayamba nthawi ya Chakwera ndi Chilima ndiye panopa zisawabowe. Mbewu iyi anabzala okha.
Tiwauzeso kt eya boma ndilomweli we called Malawi komatigositha mtsongoleli basi
kkkkkk koma bon kalindo
Wina uyu kuno mmangeniso !!!
Kodi iweyo akukusiya chifukwa chanid kwenikwen😅
Kuno ku Blantyre madzi lero one week madzi sakutuluka,eeeeeee chipanda mvula yomwe ikubwerayi kaya ndipo kaya
Auze bon umakwanatu
Iiiiiiiii awawa awa eishhhhh
Dc tiyenawo mpaka moto kt buuuu
wina azafa naye uyu, nditokuuzani kk
Kkkkkk Koma Winiko iiiiiii.
Chikangawa waluza bas okupha uja kkkkk
live
Zikomo ndi lokondera Mangochi mwamusiye yekha no sapoti
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Ukuti kamuromwe Kati kambewa
Kkkkkkkkk chalakwe
th-cam.com/video/o0g35X9MOE0/w-d-xo.htmlfeature=shared
Kkkkkkkkkk
Umakwana biggy
Bon kalindo ndikatundu bas
Kkkkkkkkk koma abale
Zoona makape enieni
chakwera wangokula mutu km,mzeru alibe boma lamukanika ndinyani ameneyo
Kkkkkkkkkkkk
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Mumakwana inuyo mesa
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂