ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
I came across this guy when we were doing donations he really cares for the street kids. He is taking care of many young boys and girls. God bless him
ABale MULUNGU apose pa menepa this is really meaning of your GOD knows mmmmh
Miracle working God, Yahweh 🙏
First comment ndakhala ndikuidikira part 2 imeneyi
Ur name is something else ,eish this God ndagoma naye ine
Moyo Wanga ausunga nd cholinga ❤❤❤❤❤❤
Nyimbo ikhale ya Favoured cctas " moyo wanga akuusunga ndicholinga
WAY MAKER & MIRACLE WALKER.❤❤❤
Ambuye Ali Nanu cholinga ndithu mulungu ndiwadongosolo🙏🙏
❤❤❤ ambuye azikudalitsani a God knows
Chonena ndilibe ambuye mukule ndithu muzonse amen
I too need this God 🎉 I even tear 😢
I appreciate to you my brother this is my ambition ❤❤❤
Wow!we Thank GOD
Ambuye Mulemekezeke nthawi zonse Amen 🙏🙏
Mmmm ndagwidwa mantha.ziko lapansi kukuchitika zinthu zoophya
Almighty God
To God be the glory
God bless you
Eyiii koma mkuluyi wakumana ndizinthu Komabe Mulungu amamukonda kwambili
God is good
Groly to Almighty God 🙏🙏🙏🙏
Kodi atsikana awiri amene amagwira nawo ntchito aja anali ochokera dziko lanji
Mulungu aliko ku mwamba 🙏🙏🙏🙏
the Drug Cartels... thats true Bro
Koma tikapsa yoooo dzikoli kukuchitika nyasi Mulungu atithandize kwaazanthu omwe akuchitilidwa muchitidwe umeneu
GOD CARES
Zonse nkumwamba!!!!
GODKNOWS chonde udziwe kut Yehova Ali nawe ndi cholinga
Inali plan Mwanayo ndi bambo akewo cholinga kusokoneza umboni anthu ama deal ngati amenewo samusiya ndi moyo
Ambuye apitirize kukusungani ndi moyo wanthazi ndi wautali
Eish this world is full of evil
Zosezo anali ma plan A Mulungu kuti moyo wanu uphulumuke sizophweka ayi pokuza malile anu
Ziko lapasi 😢😢😢😢😢😢😢😢
Eeeee Koma kunja kuno anthu akuchitilidwa nkhanza mmmmm
I came across this guy when we were doing donations he really cares for the street kids. He is taking care of many young boys and girls. God bless him
ABale MULUNGU apose pa menepa this is really meaning of your GOD knows mmmmh
Miracle working God, Yahweh 🙏
First comment ndakhala ndikuidikira part 2 imeneyi
Ur name is something else ,eish this God ndagoma naye ine
Moyo Wanga ausunga nd cholinga ❤❤❤❤❤❤
Nyimbo ikhale ya Favoured cctas " moyo wanga akuusunga ndicholinga
WAY MAKER & MIRACLE WALKER.❤❤❤
Ambuye Ali Nanu cholinga ndithu mulungu ndiwadongosolo🙏🙏
❤❤❤ ambuye azikudalitsani a God knows
Chonena ndilibe ambuye mukule ndithu muzonse amen
I too need this God 🎉 I even tear 😢
I appreciate to you my brother this is my ambition ❤❤❤
Wow!we Thank GOD
Ambuye Mulemekezeke nthawi zonse
Amen 🙏🙏
Mmmm ndagwidwa mantha.ziko lapansi kukuchitika zinthu zoophya
Almighty God
To God be the glory
God bless you
Eyiii koma mkuluyi wakumana ndizinthu Komabe Mulungu amamukonda kwambili
God is good
Groly to Almighty God 🙏🙏🙏🙏
Kodi atsikana awiri amene amagwira nawo ntchito aja anali ochokera dziko lanji
Mulungu aliko ku mwamba 🙏🙏🙏🙏
the Drug Cartels... thats true Bro
Koma tikapsa yoooo dzikoli kukuchitika nyasi Mulungu atithandize kwaazanthu omwe akuchitilidwa muchitidwe umeneu
GOD CARES
Zonse nkumwamba!!!!
GODKNOWS chonde udziwe kut Yehova Ali nawe ndi cholinga
Inali plan Mwanayo ndi bambo akewo cholinga kusokoneza umboni anthu ama deal ngati amenewo samusiya ndi moyo
Ambuye apitirize kukusungani ndi moyo wanthazi ndi wautali
Eish this world is full of evil
Zosezo anali ma plan A Mulungu kuti moyo wanu uphulumuke sizophweka ayi pokuza malile anu
Ziko lapasi 😢😢😢😢😢😢😢😢
Eeeee Koma kunja kuno anthu akuchitilidwa nkhanza mmmmm