HOT CURRENT LERO PA 25 AUGUST 2024 |

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 28 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 64

  • @SamboMaria
    @SamboMaria 2 หลายเดือนก่อน +8

    Burkina Faso ndye chitsanzo cha africa ndizotheka kukhara ndikutukuka opanda azunguwa.... Nthawi ndikachitsiru

  • @MosesMwachande
    @MosesMwachande 2 หลายเดือนก่อน +5

    This too much chakwera and his cabinet they r taking us for granted...but 1 thing...this thing don't last for ever....

  • @gumambalule7675
    @gumambalule7675 2 หลายเดือนก่อน +1

    Truth well told. The situation on the ground is pathetic, and we as a country are headed for disaster. Hot Current is really hot 🔥 🥵 🔥 🥵

  • @HenryManda-m9h
    @HenryManda-m9h 2 หลายเดือนก่อน

    A Brian Banda program yanuyi yalero ikanakhala album tikanangoti, the very best of Brian Banda Hot current because mwayankhula chilungamo, kaya nchifukwa choti IMF yavumbulitsa Bomba mukanakhala kuti m'mbuyo monsemo mumayankhula chonchi bwenzi mwina zinasintha komakayankhulidwe kanu m'mbuyomu mumanyengerera andale makamaka olamula achipani Cha mcp zimenezo ndi chifukwa anthu ambiri ngakhale kumamidzi amakonda kumvera pa social media , ngati kumamvera achina Limpopo , Ntanyiwa, Bakili Muluzi TV ,Bon Kalindo ndi ena amene amanena chilungamo mupotolize monga m'mene mwayambiramo thank you guys

  • @MaryNgola
    @MaryNgola 2 หลายเดือนก่อน +3

    Mumagaza bho,jessie kabwira akunyanya kudzitukumura akuona ngt anafika

  • @ChrissyBhima
    @ChrissyBhima 2 หลายเดือนก่อน +2

    Kkkkkkkk Jessei yemweyo,koma umbuli uli Ku a m c p iiiii chipani chochitisa manyazi Mai kabwira zomwe mukupangazi mudpitadi Ku school?mwasavuka Mai sinthani,mwabwera uyo, uve weniweni,sinthani

  • @victormbewe7462
    @victormbewe7462 2 หลายเดือนก่อน +1

    I like the word tipatsane ulemu 😢😢 otsamangoti boma ndilomweri ngati ndi ufumu

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 2 หลายเดือนก่อน +2

    Well done gyz kulakhuka moveka Bwino 💯💪

  • @SamboMaria
    @SamboMaria 2 หลายเดือนก่อน +3

    Tikadalibe muu kapolo. Mzungu akadatilamulira, akudawa ndizikwangwani...

  • @Vascomw
    @Vascomw 2 หลายเดือนก่อน

    We are with you from uk ❣️❣️

  • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
    @CHIFUNDOCHINA-lp9lg 2 หลายเดือนก่อน

    YES 👍👍

  • @ShadreckEliya
    @ShadreckEliya 2 หลายเดือนก่อน

    Mavuto onsewa sikulina Mulungu azatiyankha ndithu wawa❤

  • @HaleemaAllie
    @HaleemaAllie 2 หลายเดือนก่อน

    You guys God bless you

  • @stynessphiri
    @stynessphiri 2 หลายเดือนก่อน

    ❤ Mumakwana

  • @AubreymedsonMbewe
    @AubreymedsonMbewe 2 หลายเดือนก่อน

    Akuti nansonjola alipo m'bomamo kkkkkk😂😂😂

  • @HenryManda-m9h
    @HenryManda-m9h 2 หลายเดือนก่อน

    Akabwira ndimunthu wopita ku school, koma ndi mbuli ya munthu akakadayenderabe zomwe zija za Kamuzu ngati chipani chimodzi,sasiyanitsa ntchito za chipani ndi ntchito za boma ndichifukwa chake akufunanso kutengera dzikolli konkuja ku one party system ndiye za a Jesse Kabwira mbuli yophunzira

  • @arthurmakuluni6676
    @arthurmakuluni6676 2 หลายเดือนก่อน

    Speak truth to power Malawi

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb 2 หลายเดือนก่อน

    Tidakali pa thawi yakulila chilima mzimu wao uuse mmutende SK 😢😢

  • @IsaacAmiyele-w6y
    @IsaacAmiyele-w6y 2 หลายเดือนก่อน

    Well done

  • @LindaLimbe-fo1oy
    @LindaLimbe-fo1oy 2 หลายเดือนก่อน +1

    Job well done

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 2 หลายเดือนก่อน

    Inu ndinu ma journalists tell Malawians the truth for once….This govt is borrowing too much because it’s under pressure to deliver on its unrealistic promises

  • @LenardJames-j1n
    @LenardJames-j1n 2 หลายเดือนก่อน +2

    Nde kt Wa bakili mulizi TV uja amakamba chilungamo

  • @SteveChapola
    @SteveChapola 2 หลายเดือนก่อน +2

    Kabwira akufuna kudyanawo ndalama kuba basi

  • @MayesoBikefa
    @MayesoBikefa 2 หลายเดือนก่อน

    Bomali ose saziwa kathu

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 2 หลายเดือนก่อน +1

    🙏🙏🙏🙏🙏 All guys God bless you all

  • @FranciscoJendala
    @FranciscoJendala 2 หลายเดือนก่อน

    Jesse watengetsa anayenera kusiyanitsa ntchito zaboma ndi chipani

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 2 หลายเดือนก่อน +4

    Good message Jonathan

  • @FrancisLepu
    @FrancisLepu 2 หลายเดือนก่อน

    Brian take care asakuphe

  • @imraanJafal
    @imraanJafal 2 หลายเดือนก่อน +2

    Kkkk nose ulemu wanu lelo mwafika ndi truth

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn 2 หลายเดือนก่อน +1

    mcp ngakhale yitatani yitatani yikutuluka boma basi

  • @ChisomoChigaga
    @ChisomoChigaga 2 หลายเดือนก่อน

    Anyamata mwandiyakhulira bwino Maka apo akumati boma ndilomweli pa mwalasa, tipatsene ulemu di, ndinthu fukwa choza mawa sichidziwika asamale mayakhulidwe awo

  • @lacksonsiyadi943
    @lacksonsiyadi943 2 หลายเดือนก่อน +2

    Azungu atigwira ufiti

  • @CaptainMillias
    @CaptainMillias 2 หลายเดือนก่อน

    Azibambo inuyo mumaona patali ulemuwanu

  • @ChifundoChibande
    @ChifundoChibande 2 หลายเดือนก่อน

    A malawi we dont know what we have to know!!! Dzik ili amalamula nda zungu, try to understand mmen dziko limayender la malawi kt anth muziwauza zachilungam coz pal zinth zambir zomw simaziziwa zimen mmaziona ngat ndiza normal coz munakula muzimenez km am telling you this organisation called IMF sindimaiona bwin.. try looking from the bottom of our mavut kt muth kuzindikira....
    Let me ask you, azungu amatipats ngongol even when tili ndingongol ina kal y?

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p 2 หลายเดือนก่อน

    Amereka akayetsemula Malawi imagwira chimfine. N’chifukwa chiyani timayembekezera kuti atiuze zimene tikudziwa kale?

  • @RexMwimba
    @RexMwimba 2 หลายเดือนก่อน

    Man in the middle is just a rumour monger and not an analyst.
    Let only analysts continue to participate, otherwise the program will loose its usual taste

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 2 หลายเดือนก่อน

    Iyii idali mbambande

  • @TamandaniMaseya
    @TamandaniMaseya 2 หลายเดือนก่อน

    Chitukuko chakechiti chokuba ndalamacho😂😂😂

  • @evathamanga1242
    @evathamanga1242 2 หลายเดือนก่อน +1

    Adayedzeka kaye

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mofaya
    Banda

  • @SteveChapola
    @SteveChapola 2 หลายเดือนก่อน

    Ndalamayo agoika matubamwawo akuba pamodzi ndiabaleawo

  • @PatrickKennith
    @PatrickKennith 2 หลายเดือนก่อน

    Boma silomweli tizasankha September 2025.

  • @BrightZionga
    @BrightZionga 2 หลายเดือนก่อน

    Tiyeni nazo ❤❤u guys

  • @JohnChinangwa-r2g
    @JohnChinangwa-r2g 2 หลายเดือนก่อน

    sangamuphe ase

  • @enowkayakadjtembwe4602
    @enowkayakadjtembwe4602 2 หลายเดือนก่อน

    Mpatseni traole dzikoli

  • @GiftMlinde
    @GiftMlinde 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂❤❤❤

  • @ernestphiri5507
    @ernestphiri5507 2 หลายเดือนก่อน

    Otsogolerayo ndiye olephela

  • @AubreyMwale-y7q
    @AubreyMwale-y7q 2 หลายเดือนก่อน

    Muze wa mcpyo

  • @SteveChapola
    @SteveChapola 2 หลายเดือนก่อน

    Amereka yanenazona agobandalama

  • @HaliJana
    @HaliJana 2 หลายเดือนก่อน

    Program ikukoma kobasi anthu inuyo mumakwana kobasi

  • @maxwellluciano4943
    @maxwellluciano4943 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kkk kwavuta

  • @AlinafeNafe-s8p
    @AlinafeNafe-s8p 2 หลายเดือนก่อน

    Palibe choyamikila

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo1441 2 หลายเดือนก่อน

    Hot current iyi ndiye inalidi hot hot😂

  • @khamakumasewera9283
    @khamakumasewera9283 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mwasowa zokamba a Chafumuka.
    Ngati munthu akupanga chitukuko osayamikira ndi chiyani?
    Ena akumati bomali palibe la chita. Zitukuko zomwe akupanga a Chakwera 2:15 ena anawonongapp.
    Pena ena anangomanga za substandard.
    Analysis apo pokha yakuvutani bwana

    • @BizweckMbwindinga-uh6fq
      @BizweckMbwindinga-uh6fq 2 หลายเดือนก่อน +1

      Program ikukoma kwabas bwana muzimangilitu pitani pa TV 📺 mukasuse

    • @BrightZionga
      @BrightZionga 2 หลายเดือนก่อน

      Kaoneleni MBC malume

    • @AlinafeNafe-s8p
      @AlinafeNafe-s8p 2 หลายเดือนก่อน +1

      Aaaaaaaaaa chitokukocho akupangila kwanu

    • @fortunekamdumli-xy5zn
      @fortunekamdumli-xy5zn 2 หลายเดือนก่อน

      Awanso nde achitsilu bwanji

    • @MosesMwachande
      @MosesMwachande 2 หลายเดือนก่อน

      Kape uyu akatero wadya nawo

  • @AshimayeGama
    @AshimayeGama 2 หลายเดือนก่อน

    Chilima analichi vhitsilu wachabe chabe galu opanda tchoto mavuto osewa chifukwa cha iyeyu

  • @HenryManda-m9h
    @HenryManda-m9h 2 หลายเดือนก่อน

    Akabwira ndimunthu wopita ku school, koma ndi mbuli ya munthu akakadayenderabe zomwe zija za Kamuzu ngati chipani chimodzi,sasiyanitsa ntchito za chipani ndi ntchito za boma ndichifukwa chake akufunanso kutengera dzikolli konkuja ku one party system ndiye za a Jesse Kabwira mbuli yophunzira