A Mutharika Alephela Kusunga Chipani - Fedrick Billy Malata
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 30 ก.ย. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Former DPP NGC Member says former President His Excellency Peter Mutharika has failed to lead the party, and under his leadership the DPP has no future.
Pa Nyasa VoiceBox, membala wakale wa DPP NGC wati mtsogoleri wakale wa dziko lino Peter Mutharika walephera kutsogolera chipanichi, ndipo pansi pa utsogoleri wake DPP ilibe tsogolo.
#malawi
Basi ntchito kumunyoza nzanu. Kagwereni uko Pana nde Mcp tikupanga Chan, sibolanso nthawi ya Peter muntharika anthu amadya samafa ndi njala
Mcp yadya ma billions angati, ndlama ikungokwera tsiku ndi tsiku
Anthu dyera ndichoncho
ADAD woyeeeeee❤
apms time Malawian poorest was able to buy maluwa soap sugar mchele mafuta opikila talking more about apm chimanga was almost everwhere in the country maganyu ankapezeka zinthu zinali bweinoko compire ndipanopa any poor Malawian can agree wat um talking here please dont ever come here and tell amalawi zakumtumbo chitsilu
Yeah koma nde kulalatatu Akulakwirani Chiyani Amunthalika my Vote goes to ADADI ❤AMP❤🎉❤🎉❤🎉❤🎉❤🎉❤🎉
Mukamaliza kulalata mutiuza 😂😂😂
Zopusa etiiii
Who billy malata? Mbuzi
chakwera ali ndi ma adivisers okwana 25 ndie akupanga chani.unya wadyazo uzisanza mu 2025
Garu wachabe musiyen apm
Iwenso ndi zoba bwanji nqati APM mukumudelera osamusiya bwanji azagwe yekha?
Iwe kupita ndipita kusukulu kwako ungamanene zopanda zeluzo ,2025 DPP M'BOMA ❤
Malata ndi mbuzi ya.munthu koma nde ulipa mavuto, ndiwe chitsiru kwambiri wamva munyasimunati agaru inu . 🔥🔥🔥🔥
A Billy Malatao ndikape kwambiri, Peter Muthalika won the election after the death of late Bing, and if Peter Muthalika can not Win who will win then???
Wamisara phawi garu iwe sungalimbane ndi apm iwe nkuwina or agaru amcp ako sangamuthe
Muthalika is a great leader no matter what??
Billy malata usatinyanse iweyo anakakuchotea kale iweyo palibe amwene angakumvele panonapa ingosiya usalowelele nkhani ya Dpp pita ukajoine mcp watikwana apapa iweyo wamisala ndithu musiye peter muthalika , iweyo ukulira chifukwa anakuchotsa
Bwanji billy malata mutumize ku zomba metal Hospital, wapenga wasowa choyankhula,, Ife watilamu anthu akuziwa kuti ndi wachitukuko okonda anthu.
Iwe peza zochita zina , wasowa kolowera....ukhaula fanz ikufuna APM.....😅😅😅😅😅
Mwati mudzuke cos of the interview. Anthu omvetsa chisoni kwambiri inu, and vuto lamunthu ngati uyu palibe chipani chingamunyadile kuti walowa kkkk
Akanakhala kuti ndi wolephera mukanachoka nokha osadikira kuchosedwa
China ndichakuti, inu a Malata mu audio yanuyi mukamati munthu akuyendesa bwino chipani ndiye kuti azigawa zinthu kwa atsogoleri. Komatu APM ndiye zimenezo samapanga nawo. Ntukula pakhomo ndi program ya anthu ovutika ndiye azikapasa regional governor?
Inu mukungoyenera kupeza zochita otherwise palibe amene adzakudyeseni moyo wanu wonse
Iweyo ulibe mphindu axe,,umatani iweyo dpp olo palibe amene amakusowa amwne akukupopawo akunamidza,,wakwela ya kumphwa axe uwona 2025.
Aaaaaa ndinsanje man ndikatundu APM malume kapezeni zochita mwasowa zochita
Kd iwe kugwa chifufu kuja sikunakuthele mankhwala siunawapeze mbuzi ya munthu
Billy Mayaya kodi misala yija umadwala unachila?
Billy kaidi wachabe chabe kumuopa apm kumeneko akupitilizabe kukutuma azako anja
Akulu inuso mwasowa nkhani bwanji,pezani Zina zochita achitsilu inu
Anakuchosabe mbuzi iwe 😂😂😂
Nzulu zangokuchepela APM muulamulilo wake sanamange munthu kambazina iwe chikamba😂😂
Anthu enawa amafunika kungodzinga ndiye asowe basi,zokamba zake mbwelela zokha zokha ngati ngopenga,achipatala chonde muyezeni ubongo wake uyu
Mukunama baba APM Ndidolo
Malata umangidwasotu upita Ku Zomba ukapitiliza misala yakoyo
Man malata kambani zanu but truth people knows whom to vote
Munthu uyudi ndiwamisaladi .....za zii zimene akuyankhula apa......chisilu cha munthu ....umasowa choyankhula .....osamangodya ndalama zokuba za mcp bwanji
Mwejo palunkundu lwenu pikene ana mwe wani
Pajatu amzako ako Aja anakumangisabe Galu iwe wadyera 😂😂😂😂😂😂
Sanachilape galu ameneyu
Please please please Father, kambani zothandiza kuti ngati dziko tiyende chitsogolo poti apa tabwerera ku 1964. Apa palibe tikutolapo.
Ine ngati wachipatala,,,Billy kaya mati garu ndamupexa ndi matenda aubongo😀😀😀😀😀Kapee mmene tikuvutikilamu ukusangalala?ndiwe chisatana ndithu!!!!!!!
Muzakhumudwa chaka chamawa dpp ikulowanso mboma muzachita manyazi baba
Kkkkkkkk, ku Malawi Kapena ku Mozambique? Iwalani zolowa mboma.
nonsenu mukupita ndipo munya
Iwe tangosiya takudziwa kale ukufuna poyambira chamba eti
Iwe Malata pamutupako sipakuyendabwino ndipo ndiwe Galu kwabasi ndipo iwe unatuluka pagalu kapena pamunthu. Usazalankhulenso manyiakowo. Anthu akuvutika mmalawi
Billy malata ngati umawerenga ma comment anthuwa. Udzimvere chisoni. Ngati sangawine ndiye chukukukhudza ndichani kahwere uko wamisala iwe waganyu wa mcp walandila half million ugule chimanga udzikadya ndi mabanja ako
Mbuzi iwe nanga inu mwapanga chani mwaziwa ndikupha athu ndikusamusa ipan inu tinakuvote chifukwa cachilimatu tikuwuzeni ndipo ngat akuganiza zobera achimwene kkkkkkk
mwana wa njoka iwe APM our vote
It's him who is a failure not Mutharika.
Iweyo malata ikunakhala nane pa fupi iweyo nde ndikanakymenyani aimasewera mwachidure machende ako
Kumalawi sikuzatheka kunyozana basi nde chakwera wapanga chani
Komatu anthu nde akulankhula koma kusamva basi ,kakaka kukakamila akuziwa kuti pamapeto kuchita regret
Km ayi kugwirisa ntchito ufulu molakwika esh Malawi wafikapo
Chamba chosuta mamawa galu iwe uzawanyambita apongozi ako za kusi iwe galu malata
Billy malata ndiwe chisilu cha muthu palibe muthu angakuyamike siiiii
Tchende lako osanena zomveka bwanji nkhope ngati mbolo
Gulu lopasidwa burn awaso asalowe kumozambik kwameleka kwatalika
Aaa kape iwe,,ndiye ngati Ali ku mbuyo mesa Ali mu mcp momwemo.
Iwenso mutu mwako simmayenda bwino fortsek
Pitani mukalowe ufumu wache mkwanda mulibe mfundo
Akutuman iwe alirata achakwera machende ako alirata
John tembo adawinpo achitsilu inu
Chakwela is a truely a thief
Malata iwe galu
Billy ......ndi we mbalame basi shut up
Iwe ukutaya nthawi yako kamba Zina bigy timve
Malata jelasi😂😂😂😂😂
Kagwele uko kape wopanda nzeru, who are you?
Galu ndiwe abille wakumba panyopako
Koma awinabetu ukha madzi sunati
Anthu adpp samabva asiyeni peter awamalizile chipani chakwela 2025 boma
Mukulira naye APM bwanji, mukhaula ife timuvotera osati mbuli zolepherazi
Chitsilu uyu kukamwa ngati wadya manyi
Ukachita mutu ngati gulo wamva 😮
Billy malata thongo lako
Machende ako ndi chakwera wakoyo
Munthu walankhula chilungamo, ndiye uti, Anthu amaiwala,mosabvuta.ndikukumbukila,kazi wache wa muthalika yo,amangopita ku Bank kumangolamula,kuti,ndikufuna, ndalama mwakuti.komwe,kuli kulakwila, malamulo aziko lino.peter,watha,olo,awine olamula si iye ayi.olamula,ndi kazache, ndi security wache ujayo.tiyeni, tisankhe munthu odziwa mabvuto anthu.dpp,itha ngati makatani, chifukwa cha peter muthalika.
Ndiweso galu iweso
Mkamwa monukhamo Kwathu Malata
Umphawi sizinthu😂😂😂
90 % madness
Kuyankhula kwa bwanji uku
Who are you?
Hehehe chilungamo kuwawa ndizoona agogo apite ku malo opuma🤣🤣🤣
Mukhaula, ife tikufuna gogoyo, anyamata anuwo alephera ndipo awononga dzikoli. Mbuli zokuba zokhazokha.
Akutumawo akupwetekesa
A mbuz iwe
Malatayo wasuta chamba
Mapwarako iwe galu kkkkk
Maphwala ako dala iwe
Galu
Galu iwe kwabasi
M'busa wautsilu
Mkunena zoona mr .malata nkhalamba ngati iyi 85yrs aziti akufunaso upule ansaka akabambe wosewo alibe nzelu nzelu zikakhale gogoyo ayi adpp polani moto
Ife tikavotera nkhalambayo, achinyamata anuwo apnonga dziko mbuli zosatha kulanula. Mukhaula muona
Kkkkk
Aaaaa no sense speech
malata ndiwe chitsilu galu mboloyako akukunamiza anzanuwo munya chitsilu galu
Yes or not but u must nkow that APM again 2025 nde inu pamene ukaba pankomo pakwanu sanakuleleni mdala nde mukutinyasa APA mashende Anu iwe amapwala ngat muli ndi kuntekela tangoyeleke kubwela Kuno
ndipo ukawauze azinzanuwo onse kuti nonsenu mbolozanu machende maphwala anu zitsilu pamnyapako galu iwe mmene amalawi akutivutikila lelo iwe chifukwa choti iweyo ukudya ndi mcp ukuganiza kuti ife sitikuona machendewako 5 years ago malawi was not like this
pamachende ako ndiwe chitsilu galu kuntumbokwako
Iwe Malata machendeako ukuyankhula ngati ndani pantumbo pamako
Ndala sowa apartment wakhuta eti very stupid
Sono ngati alephela iweyo wakwanisa chani tapanga dzako
Panyero pamako
Waunsilu iwe galu wachabechabe mutu ngati papaya
Ma battery ako iwe
usazayambilenso kukamba manyi akowo
Ndiye chikukukhuza ndichiyani galu iwe
Wasowa chonena iwe nsanje basi mumuziwe Yesu
Billy malata ndi mbudzi