Kodi za nsewu wa kumakanjila adzikawodza anthu aku BT chabwino ena anachokela komweko ku mangochi chipitile patenga nthawi amva chani amenewo nde mabodzwo ngati mufuna kunena za ku zomba pitani komweko mudzikalodza minsewuwo atsati muli ku mulanje kumanena za ku salima AAAA ANTHU SANGAKUMVELENI AYI UCHISILU WA MCP UYU ANTHU OLEPHELA AWA AKUDALILA KUBELA VOTE KUMATU KUDZACHEMA KU MALAWI CHIFUKWA ANTHU AMBILI SAKUFUNANI A MCP NDE MUSAMALE
Mangochi ndiwe one ❤❤❤
Zikomo big man ulemu wanu MCP yatikwana iyi
Amangochi osafookatu chifukwa pano nde muli ndi nzelu za bwino kwa mbili❤
Mbambande 🔥
Menya brother amvetse, Chakwera palibe chimene akuchita
Chimwendobanda uzafangati galu
Comrade true.
Chonde musanyengedwenso ndi ng'onazi chonde
AMangochi takunya dilani m b tv tanyuwa A D C teyenawon zatikwana ng'ona zimenez
Kodi za nsewu wa kumakanjila adzikawodza anthu aku BT chabwino ena anachokela komweko ku mangochi chipitile patenga nthawi amva chani amenewo nde mabodzwo ngati mufuna kunena za ku zomba pitani komweko mudzikalodza minsewuwo atsati muli ku mulanje kumanena za ku salima AAAA ANTHU SANGAKUMVELENI AYI UCHISILU WA MCP UYU ANTHU OLEPHELA AWA AKUDALILA KUBELA VOTE KUMATU KUDZACHEMA KU MALAWI CHIFUKWA ANTHU AMBILI SAKUFUNANI A MCP NDE MUSAMALE
Apa ndiye mukuyimilira amalawi osati kumabakira boma loyipa la MCP
Panotu tinzeru tikubwera
🔥 fire lyton mangochi ❤❤
Mcp mulibemo utsoreri angakhare nduna zimene ndi mbuzi zokhazokha
Mutu wayamba kugwila ntchito tsopano
Koma lyton usapangeso zopusa Ngati umafuna zija Kuti utenge ndalama Ku MCP basotu
Mangoch umachedwapat kulankhula ndikumeneku
Apandiye bolani.
❤❤❤ mangochi 😂
Pitilizani amangochi kutisegula kumaso takunyadilani
Umatha
Hit the nail brother
Anapha track azimayiwa eeh
Nsampha waning'a MCP munya muona
Panopa amangochi tikukunyadilan
A Lyton tili pambuyo panu osaopa malawi ndiwathu zoona anyamata amenewa ife timawakonda ndipo mlungu awapatse moyo wautali akutimenyela nkhondo zabwino kwambiri APM oyee! DPP oyee! Mumakwana sendela sister tili tonse 2025 DPP boma
Mbuli yosaphunzira iwe palibe chomwe ukuziwapo tizithumwa tomweto munakakwima kwasing'anga anu aja mukunamatu inu
Kwachematu
Mbuzi yamuthu nachimutu
Ngati Pali chipani chaboza mumalawi ndi DPP chipani chinanamiza anthu kuti chisintha Malawi kukhala Singapore ,mbombera , zambili munalonjeza palibe chomwe munapangapo cholozeka ndimisonkho ya aMalawi
Wasowa chonena iwe chikangawa😅😅😅
Zowona mangochi umakwanira iweyo