July 25, 2024

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 22 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 99

  • @JeanMkandawire-q7p
    @JeanMkandawire-q7p 26 วันที่ผ่านมา +3

    Glory be to the most high GOD ❤❤❤

  • @ArvinKankhuni
    @ArvinKankhuni 2 หลายเดือนก่อน +2

    This is so powerful song wawooo ...glory to the almighty father ...I have played this song 7times ...AMEN AND AMEN

  • @joycejacquelineholla
    @joycejacquelineholla หลายเดือนก่อน +1

    We glorify God for the grace which upon Daughter of Zion.
    This is one of the powerful songs. Amen Amen

  • @beatricenkhoma1109
    @beatricenkhoma1109 2 หลายเดือนก่อน +1

    Yes Lord, your no 1 palibe ofanana nanu baba ulemu,matamando kukwezedwa konse ,kwayenera inu🙏🙏

  • @GloriaMwaliunju
    @GloriaMwaliunju 2 หลายเดือนก่อน +5

    Eeee this song is very powerful glory to the most high God, the owner of everything, king of kings and lord of lords 🙏🔥

  • @EllahEllah-hu7hi
    @EllahEllah-hu7hi 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mwayenela kulandila ulemu ndi matambo,,bondo lililonse layenela kugwadila inu baba,,, powerful song

  • @Namaseko
    @Namaseko 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mai mumaimba, koma nyimbo iyi mmmmm 🙏🙏🙏 Ambuye apitirize kukugwiritsani ntchito!!! Tikulemekeza Yehova osati chifukwa cha zimene tiri nazo ayi koma CHIFUKWA CHA M'MENE IYE ALIRI!!!

  • @VanessaChisale-k2o
    @VanessaChisale-k2o หลายเดือนก่อน +1

    Am blessed with the songs. ... Munyimbo muli mphamvu yopoosa kwambili

  • @LizzieMalie
    @LizzieMalie 2 หลายเดือนก่อน +1

    ❤🎉🎉🎉powerful 😢alandiledi ulemu ndi matamando God bless u cct

  • @rabeccadytone8772
    @rabeccadytone8772 หลายเดือนก่อน +1

    Ooh yes chifukwa. Mene mulili landilan ulemu ndithu 🎉

  • @EsterNkhonza
    @EsterNkhonza หลายเดือนก่อน +1

    Almighty Lord your an equal
    There is nothing we can compare with you

  • @RK-xw1of
    @RK-xw1of 2 หลายเดือนก่อน +3

    Musadzasinthe Mama. Yehova wayeneradi Ulemu ndi matamando chifukwa Cha mmene Alili. Nyimbo yokoma kwambiri kwa ma Worshippers onse. Indiphe ndi sitepe ine kuno ,on repeat . Ooooooo Yesu landirani Ulemu Woyera wankulu wa Israel, opanga njira popanda njira, Alefa ndi Omega , Thandizo lopezekeratu, Moto Onyeketsa,Tate Osakwiya msanga. Tate wa Amasiye onse . Dzina lanu Lili pamwamba pa Maina onse. Otimenyera nkhondo, otiweruzira milandu yathu. Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah Hallelujah HallUpelujah Hallelujah 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🥁🎷🎵🎶🎺🎤🎻🎸🎧🎹🎧🎹🎻🎸🎷🎵🎶🎶🎶🎶🎶🎶🎤🎺🥁

  • @mirriamwilliam-nq9wg
    @mirriamwilliam-nq9wg 2 หลายเดือนก่อน +2

    Oh yes Hallelujah ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤I'm in love with this song

  • @marthangwira7961
    @marthangwira7961 2 หลายเดือนก่อน +1

    Amen daughter of Zion, Mulungu akuuze malire anu , mupitilize kutitsitsimusa ndi nyimbo zanu zabwino zopereka chiyembekezo🙏

  • @DorothyBurton-q4n
    @DorothyBurton-q4n 2 หลายเดือนก่อน +2

    What a powerful ministration remain blessed

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 หลายเดือนก่อน +1

    Ameeeeeeen!❤❤❤❤❤

  • @lindabanda408
    @lindabanda408 3 หลายเดือนก่อน +1

    Allelluya, Ambuye tikulemekeza, tikulambirani, pakuti ndinu woyenera ulemu kulibe wofanana nanu
    Ulemerero wanu ndi wosasanthulika
    Ha!! Yehova dzina lanu liposadi nanga Kumwamba ndi dziko lonse lapansi
    Nthawi yakwana kuti wolambira inu akulambireni mu Mzimu ndi muchoonadi
    Ndi mitima yokondwera, ndi yoyamika tiyimba kukulemekezani, Woyera inu🙌🙌

  • @MarthaMtenje
    @MarthaMtenje 3 วันที่ผ่านมา

    This song is so powerful and ndikulimbikitsikan ndi nyengo yomwe ife tukumanananO❤

  • @BrendaBanda-ij9dl
    @BrendaBanda-ij9dl 2 หลายเดือนก่อน +1

    Nice mama mumantha ❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @owenkamwendo2196
    @owenkamwendo2196 2 หลายเดือนก่อน +1

    Amen Amen Ambuye alemekezeke koposa kwabasi kamba kamphaso ya moyooo kunooo

  • @MichaelMwale-m8o
    @MichaelMwale-m8o 11 วันที่ผ่านมา

    Nyimbo zoti ukamamvera thupi lonse nyesi kuzoza kwanyimbo AMEN

  • @CostantinoChirwa-t3r
    @CostantinoChirwa-t3r 2 หลายเดือนก่อน +1

    ❤❤Amen , great messenge

  • @janebuka
    @janebuka 2 หลายเดือนก่อน +1

    Glory ...chifukwa Cha mmene mulili landilani matamando Yehovah

  • @MofoloJustin-l7m
    @MofoloJustin-l7m 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤❤❤❤❤landila matamando Jehovah WOSAKWIYA sanga wosamala wosamala thawi zonse

  • @EdinaKaonjola
    @EdinaKaonjola 2 หลายเดือนก่อน +1

    Love you mama❤️

  • @WisdomMaseko
    @WisdomMaseko 2 หลายเดือนก่อน +1

    Nice songs momie❤❤❤❤

  • @MannessNkhata
    @MannessNkhata 2 หลายเดือนก่อน +1

    Hozaaaaaaaa 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 ayayaya God receive the glory , Mami I love u

  • @lytonmhango3631
    @lytonmhango3631 หลายเดือนก่อน +1

    Nyimbo yabwino kwambiri ❤❤

  • @MargretDyson
    @MargretDyson 2 หลายเดือนก่อน +1

    Powerful

  • @JoyceChibwana-p1i
    @JoyceChibwana-p1i 2 หลายเดือนก่อน +1

    🎉🎉🎉 Becoz of your nature receive all praises🔥🔥

  • @edithpiscitelli5248
    @edithpiscitelli5248 2 หลายเดือนก่อน +1

    Amen ❤🔥

  • @JosephKhonje-yp8jr
    @JosephKhonje-yp8jr 2 หลายเดือนก่อน +1

    Moto wonyekesa🙌🙌🙌🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
    Landilani matamato dzinalanuliri pamwamba pamayina wose.Amen

  • @ThokozaniJenala
    @ThokozaniJenala 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ambuye mulemekezeke nthawi zonse.

  • @AliceMzumara-ci3fu
    @AliceMzumara-ci3fu วันที่ผ่านมา

    Thank you Jesus❤

  • @LucyTesha-rl2fi
    @LucyTesha-rl2fi 2 หลายเดือนก่อน +1

    Alleluya zoonadi mulandile matamando yehova

  • @FannyChingaNyasulu
    @FannyChingaNyasulu หลายเดือนก่อน

    Mamie, I love u so much. Glory be to God

  • @NemaMoleni
    @NemaMoleni 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ooh yes,, powerful 🎉

  • @ThokoChimwala
    @ThokoChimwala 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ikanamvekanso mwamphamvu kwambiri mukanaimba ndi Thom Kachimanga Kapenga Joseph Chirwa.

  • @rabeccadytone8772
    @rabeccadytone8772 หลายเดือนก่อน +1

    Oooh yes ❤❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉groly groly groly

  • @kingsleymakwale6297
    @kingsleymakwale6297 18 วันที่ผ่านมา

    We love you daughter of Zion God bless you

  • @PaulineKamwana
    @PaulineKamwana 2 หลายเดือนก่อน +1

    Landiranidi matamando inu father of fatherless mukungoyeneradi inu wondichotsa mmatope nkundiika pa thandwe .cmunafunse munthu pondidalitsa ooh hallelujah ❤🎉

  • @tsankhulojamson6202
    @tsankhulojamson6202 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mulungu azikudalitsani kwambiri a Mai inu😭😭😭

  • @desirejosito6612
    @desirejosito6612 หลายเดือนก่อน

    Akungoyenera Matamando palibe wofanana naye🔥🔥🔥

  • @vivianjackson6540
    @vivianjackson6540 หลายเดือนก่อน +1

    Chifukwa cha mmene muliri Yahweh.. Landilani matamando

  • @LuskaMoses
    @LuskaMoses 2 หลายเดือนก่อน +1

    Eish landilani matamando Yesu .

  • @ResperBanda
    @ResperBanda 3 หลายเดือนก่อน +1

    Amen amen zilibwino kwabasi ife tili busy kuvina kosalekeza

  • @EdythGloryNamponya
    @EdythGloryNamponya 3 หลายเดือนก่อน +1

    Chifukwa cha m'mene muliri Yehova❤❤❤❤

  • @QueenSimukonde
    @QueenSimukonde 2 หลายเดือนก่อน +1

    Amen and Amen

  • @JacquelineMatewere
    @JacquelineMatewere 2 หลายเดือนก่อน +1

    Zoonadi landilani matamando chifukwa cha zabwino zokoma zimene mukumandichitira yaweh🎉🎉❤

  • @JoyceChibwana-p1i
    @JoyceChibwana-p1i 2 หลายเดือนก่อน +1

    🎉🎉🎉🎉🔥🔥🔥

  • @pemphokatembe443
    @pemphokatembe443 3 หลายเดือนก่อน +1

    Oooh Yes🎉🎉 Hallelujah ❤❤💃💃💃💃

  • @robertmphulanya5978
    @robertmphulanya5978 2 หลายเดือนก่อน +1

    So amazing

  • @MofoloJustin-l7m
    @MofoloJustin-l7m 2 หลายเดือนก่อน

    Landilani matamando ❤❤❤❤❤❤

  • @Lyn-c4m6s
    @Lyn-c4m6s 2 หลายเดือนก่อน

    Beautiful song

  • @beatricelimbanga850
    @beatricelimbanga850 2 หลายเดือนก่อน +1

    Amen

  • @MarthaMtawale
    @MarthaMtawale 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mandidalitsa mama mnyimbo zanu muli za mphamvu

  • @EvelynKarreta
    @EvelynKarreta 2 หลายเดือนก่อน

    Ooooooh yes keep it up

  • @Gloryphiri-pl1wn
    @Gloryphiri-pl1wn 2 หลายเดือนก่อน +1

    Amen so powerful

  • @blandinabonaventure
    @blandinabonaventure 2 หลายเดือนก่อน +1

    Amen mulandire matanda yahweh

  • @IsobelMughogho
    @IsobelMughogho หลายเดือนก่อน

    Hallelujah powerful

  • @Jessy-wh6wt
    @Jessy-wh6wt 2 หลายเดือนก่อน +1

    Amen 🎉

  • @AnnieChanansi-gc5hq
    @AnnieChanansi-gc5hq 17 วันที่ผ่านมา

    Amen Amen

  • @georgekchimwaza6838
    @georgekchimwaza6838 3 หลายเดือนก่อน +1

    Amen❤

  • @Lyn-c4m6s
    @Lyn-c4m6s 2 หลายเดือนก่อน +2

    Oh yes chifukwa chammene mulili baba I dont know why am singing this song with tears 😢 Jesus

  • @IreenMisinde-m8b
    @IreenMisinde-m8b 27 วันที่ผ่านมา

    Mai mumandidalitsa kwambiri ndi nyimbo zanu

  • @DorisLupiya-wh9mi
    @DorisLupiya-wh9mi 2 หลายเดือนก่อน +1

    Hallelujah

  • @SusanChirwa-c6q
    @SusanChirwa-c6q 3 หลายเดือนก่อน +1

    Halleluyah 🎉🎉🎉

  • @chimwemwenchocholo9033
    @chimwemwenchocholo9033 26 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤

  • @GiftGntl
    @GiftGntl 2 หลายเดือนก่อน

    Oooooh yes landirani matamando🧎🙏

  • @MemoryEdwin-q8j
    @MemoryEdwin-q8j 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye chifukwa cha mene mulili palibe wina inu mukule ife tichepe

  • @MarthaMtenje
    @MarthaMtenje 3 วันที่ผ่านมา

  • @gracekandodo6162
    @gracekandodo6162 21 วันที่ผ่านมา

    Zoona la ndirani Matamando Yehova chifukwa cha mmeene

  • @MaryZgambo-p5m
    @MaryZgambo-p5m 3 หลายเดือนก่อน +1

    Amen. Mama keep prays and worshiping the true GOD

  • @LydiaZibamagombo
    @LydiaZibamagombo หลายเดือนก่อน

    Matamando akukuyenerani baba

  • @MercyMaloya
    @MercyMaloya 5 วันที่ผ่านมา

    muli kudzodza munyimbo iyi

  • @chimwemwenchocholo9033
    @chimwemwenchocholo9033 26 วันที่ผ่านมา

    Chifukwa Cha mmene mulili......

  • @Edith-q2g
    @Edith-q2g 2 หลายเดือนก่อน +1

    𝕟𝕕𝕚𝕡𝕠 𝕒𝕜𝕦𝕪𝕖𝕟𝕖𝕣𝕒 𝕜𝕦𝕝𝕒𝕟𝕕𝕚𝕣𝕒 𝕦𝕝𝕖𝕞𝕦 𝕪𝕒𝕙𝕨𝕖 ❤❤

  • @MonicaKusamale
    @MonicaKusamale 14 วันที่ผ่านมา

    Amen❤

  • @EmmaJemitala
    @EmmaJemitala 2 หลายเดือนก่อน

    Powerful

  • @victoriamunthali8283
    @victoriamunthali8283 2 หลายเดือนก่อน