A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 7 ก.ย. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Lyton Mangochi says that the Right Honourable Dr. Michael Usi is not a true member of the United Transformation Movement.
Pa Nyasa VoiceBox, Lyton Mangochi wati Wolemekezeka Dr. Michael Usi si membala weniweni wa United Transformation Movement.
#malawi
Iwe mangochi umandibowa pazambiri koma leroli wakamba chilungamo ❤❤ the spirit
😂😂😂
This is straight forward talk and advice
Munthuyu nthawi zina amalankhula zoduka mutu koma lelo walankhula chilungamo ndakukonda Mr mango hi for this audio.
Galu ndi gula manganya siwa utm komaso anamupeleka chilima
Uthenga opanda chigamba, apa ndiye chilungamo.
Bwana Lyton mangochi lero mwakambako mfundo zomveka bwino ulemu wanu
Apapa ndiri mbariyako or mntaniwa atanva audio yakoyi akunva kukoma mot utamatero anthu akukonda kwambiri the fact u hv say to day congrats Mr Layton big up tufuna chirungamo choncho
Ndipo bwana Mangochi mwang'alula ulemu wanu akulu awa eeeish atipepelesa sure
Mr. Mangochi awuxeni abambo amenewa chifukwa ndiye akupanga. Zinthu zobowa kwabasi.kasatana kachabe chabe kauzeni kamvetsese
@@TheresaNtodwa exactly
Ine umandinyasa heavy kma lero Mutu wako wayamba kugwila ntchito ❤zanzeru
Someone hit Like for me
Iwe Lyton Mangochi apa wanena mfundo osati yamasewera. Ndamvera each and every sentence looking for a mistake koma mwalankhula zaufumu weniweni.
I love you
Apa pokha Usi avomereza chilungamo kuti anthu alindi maso ndipo amaona ndithu iiiii
100%. Usi si wa UTM. Angofuna kusokoneza UTM yo.
Tilitonse mau olawura asiye.
Ngati zolankhura alibe angosiya. zamadirama ife sitikufuna.
Ine ndili wakwanu. Kumwitu koku Karonga. Komam'sasiye kudziwitsa anthu choonadi, monga m'nachitira pakatipa.
Tinali kuganiza kuti nanutso mwagudwa.
I think you are coming back to your senses Mr Mangochi.... Keep it up.
Ndakuombela mmanja mangochi apa pokha chilungamo chimamasula usi ndi wa MCP
Chilungamo chimawawa koma izizi ndi zoona..Malumewa SI a UTM
Apa nde wang'alula zeni zeni momveka bwino dziko akulitengela chibwana
Bwanji osakayendera ma office a NRB ku southern, eastern and northern regions kuti anthu alandire za unzika mu nthawi yabwino?
Akanangopanga za tikufzlanji asamasokoneze anthu
AMangochi,apatu mwaonesa umunthu.ndipo mukukhala ngati siinu a Mangochi,koma zikomo. coonadi ncofunika
Uku tu nde kuyankhula kopanda chigamba mau mau. pena nso atipeperetsa a Usi wa Aaaaa inu
Mr Lyton Mangochi ulemu wanu mwayankhula chilungamo God bless you Mr Mangochi
Lyton Mangochi apa walankhulatu ngati munthumuuzeni usi akutitenga ngati ife zitsilu hule wamunthu
Madala madala tsopano, munasowatu😁💗💗
Well composed speech keep it up Mr Mangochi. Teach him a lesson
Apa ndiye wayanbapo kumeneko zanzeru
Mwayankhula chilungamo malumee,May God bless you!!! Ameneyu adzazunzika nao mzimu wa Chilima
Apa wayankhulatu za nzelu even BON Kalindo ajuyamikila
Lerotu Mr Mangochi mwakambatu mfundo zomveka bwino. Ulemu wanu manganya komwe aliko amve. Chipan chathiko Ife ayi.
Ife UTM sangatigulitse .... UTM yachilima ija ilipobe ija yachina Kaliati
Koma apapa zikumveka bwino kwabas Mangochi walankhula mwanzeru chifukwa Manganya samamukonda Chilima .
Mqngochi your right ukunena zenizeni congratulations bro
Mwanena zoona Mr Mangochi. Manganya akufuna Kuba Chipani!
Iweso ukuti musiyeni usi ndwe Galu team ya Mr chikangawa fiti agalu lnu
Mangochi apa nde wandilankhulila ndithu angofusa kutisokoneza ife a UTM
Ay Mr mangochi apa pokha mwayesesa kulakhula kwa nzeru
Mr mangochi took his time to recharge and came back stronger 💪
Lero wayankhula mwanzelutu a bro, more fire 🔥
Today it's ur best audio mr mangoch best audio ever muuzenidi achose kachiwanda ka ma drama kkkk
Well spoken.....
Amangochi mukafuna mudye za ausi .
mwayankhula bwino kwambili ngati zikadi wa Malawi❤❤❤❤
Well said big man,thumb up🔥
Anali ngati Petro yemwe amamuonera Yesu patali ali pakati pa adani kumfunsa uyunso anali waiwo amvereke akunama sindikumudziwa ine ameneyo.
Apo Nde wanena zoona a usi Sia UTM
Bravo, wayamba kuyankhula mfundo zenizeni, zamphamvu.
Good speaking mr Lyton mangochi
Well spoken 🔥🔥
Mr Lyton excellent spoken keepitup
Long live Impi Biyeni
Good Message Mr mangochi
Fundo zinazo za mangochi ndi zopoila, amalawi tikuyenera kudziwa kuti tonse ndi amalawi koma zinkhulupiro ndi zotsiyana,kutsapedzaeka a Micheal usi ku candle 🕯️ light sichifukwa choti anene kuti si wa utm koma anene zifukwa zina
Let the Vice President be please !!!
Manganya palibe akulakwitsa and zomamena kut sanali wa UTM kapena kut si wa UTM ndikulakwa chabe.Mvuto lomwe Malawi tili nalo ndi nsanje.Chilima anamutenga chifukwa chani Micheal usi ngat sanali ofunikila?.Amene akudzimva UTM kwambiriwo bwanj Chilima sanawaike pa vice president?.Nsanje kusavomeleza phunzirani makape inu
Apa mwayankhula big.
Osaka asowa poyambira.
Amanganya ayenela kugwetsedwa mmpingo chifukwa ana phwanya limodzi la malamulo khumi. (Bodza)Ndinamva akukamba bodza mu zoyankhula zao pa zokhuzana ndi UTM. Mwanyozetsa mmpingo.
For the first time I am happy with you Mr Mangochi pa zanzeru zomwe mwalankhula apa.
I'm sure kuti we're expecting more from you
Respect
very true mangochi
You. have said. the truth utsi. is not for utm
Powerful message
Mwayakhura fundo ❤
Apo wabaya
Powerful advice from Mr Mangochi.
Zangongore zakezo tilibenazotchito koma asamatinamizekuti ndi wa UTM ai sitikumudziwaife
Michael Usi the big man
Amangochi mwalankhula zanzeru kwambiri mu audio iyi
manganya watikwana kale.Mr Mangochi mwabwera
Manganya ndichisilu galu ndi mozi mwa anthu ogwesa ndege ameneyo😮😮
Ndinalutuluka kale koma yapa pokha wayankhula zazelu ngati siukufunaso kupepha kwa manganyayo
aLyton APO mwalankhu zoona avaice si a UTM ayi
Paja amalawi pomwe munthu akupadula muwombela mumanja. But utm be careful once a party is divided into two no matter mbali yona ndi yochepa the conclusion will be a big space. Believe me utm usi and kaliyati please just sit down together and agree united and peace and friendly....utm yitha kutha mosavuta pa dziko lathu ndi into Three no matter what.
Ya Papa kumwera yikhala usi utm pakati chilima UTM kupoto ndidela lovutitsisa don't relax with people from north they are chameleons... You can't trust northern region
Walankhula zoona Lyton
Kodi Usi akamayenda m'mene akuyenderamu ndie kut ntchito ya nduna ndi chani? Akungofuna kupeza credit koma akutionongeranso misomkho yathu.
Mwayamkhula bwino sure
Mumafuna muzidya naye ngati achipani muziyenda naye mwauponda. Musiyeni zanu agwire ntchito ya boma mufune musafune president wa UTM ndi Usi
Lyton. mwalankhula zan,zelu. Kwambiri kwambjri. takuyamikila kunokuchitipa
Mangochi wandigwira mtima koopsa
Manga NDI Yudas weni weni munthu opanda manyazi opanda chifundo ngati uyu mizimu ya Chikangawa Ili pa mutu pake fiti iyi
Yudasi sikaliyoti Manganya siwa UTM angotaya nthawi yache pachabe munthu oipa
Leroditu alangula zaseru
Nkhani iyi ya Straight forward 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌 ulemu wanu uku kulakhura mwabnzeru manganya or tsiku limodzi lopedzeka pa mwambo oyasa ma candle yoooo or tsiku loyakhulapo zokhudza imfa ya chilimba mmmmm Ambuye akukhululukireni iwe ndi mpeni othwa konse konse iiiih Chilima Rest well tidzakulirani mpaka kale 😭😭😭😭😭😭
Very good Mr Mangochi good Message ❤
Zanzeru ndizochepa umu kuti mumumvele bwinobwino statement yakeyi yachoka kwa iye manganya mwini kuti awuze mtundu wa anthu kuti akazamati ndine wa mcp anthu asazazizimuke kwambili,
Ndipo chakwera ali mommu this is propaganda of mcp
Layton magochi lero wayesetsa utamatero mwina anthu ayamba kukukonda
Anatha awa 😂😂😂😂😂😂😂😂😂 boma ili silikufuna kukhala ndi opposition ai,kusafuna kukhala ndi opposition zimasonyeza kuti ndiwe otayilira and sufunaso kudzudzulidwa.
Wayankhula za nzeru koma awa itha kukhala njira yopemphera ndalama kuti awapatse kenakake akhale chete
Apatu Mangochi walankhula zanzeru, tikumudziwa Manganya kuti ndi betrayer wankulu ndipo ndi mthira kuwiri
Listening Keenly .....kambani ndithu
Kumva kumakuvutani amalawi manganya si wa utm anali ndi chipani chake anapanga ngwilizano ndi chilima amalawi mwatani kodi
Ngakhale Mangochi ndiwamisala koma apa ayankhulako zanzeru
Ndende ndende ndipaseni acount yanu mukatenge sweat muike mkamwa mwalankhula zoona zeni zeni ndipo inuyo mulungu alowele pa nzeru zanu
Wayakhula ndithu za zeru
Well spoken
Lelo mwayakhulana zazeru Mr mangochi ndalam zathano et
Nsokhano uliwonse ine nali wakut nali wakuti Inu anthu ambili anasinthika kuchoka ku umphawi kumene koma sikut ukachita bwino basi history yokha yokha pa nsokhano.
Akulipira zingati amene akutuma? Koma wayankhula mfundo zabwino. Zikuomeka ngati MCP yikufuna kuti Usi angopanga declare kuti walowa MCP osati zakabisalira ayi. Lyton Mangochi wapeza profession yabwino nawenso, yamalipiro abwino koma a temporary.
mangochi ulemu wanu
Mangoch wabwelanso ukufuna akupase ndalama zina mwatitola et😂
Colinga chake usi amuitane mwapadera apase ndalama kt asamu kambe
😂😂😂
UTM inatha guzy lero uyipa uja wasanduka wabwino lyton
Ndipo zoona zenizeni mzimu wa chilima uwakathe amanganya pazomwe akuchita posokoneza chipani cha UTM
Akatelo mangochi ndalama zamuthera akufuna Zina kuchokera kwa manganya koma wanena pakati aise