DR MICHAEL USI AKUNGOLANKHULA KUMENE ZA MGWIRIZANO MCHIPANI CHA UTM |

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 10 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 99

  • @Thembokatuli
    @Thembokatuli 24 วันที่ผ่านมา +13

    Tidya nawo ndalamazo koma palibe vote kwa chikangawa group

    • @user-qo3kg6rv9f
      @user-qo3kg6rv9f 24 วันที่ผ่านมา

      Chikapusa chidyereni!!!! Inu

    • @owenmoses9434
      @owenmoses9434 23 วันที่ผ่านมา

      Koma zkumaperekedwad dollar zo?.😢😢😢😂 Agalu a wa

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 23 วันที่ผ่านมา +2

    Kodi Dairy kumangoti a President anandisankha, inu ndioyamba kusankhidwako. Kodi imfa ya Chilima ija simakupasa mantha etie????

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 24 วันที่ผ่านมา +4

    Akuwombera m'manja wo ndi akachasu, zikuchita kuwonekera masekedwewo😂

    • @lacksonsiyadi943
      @lacksonsiyadi943 16 วันที่ผ่านมา

      Izo nde zoona zake ambuye mtengeni

  • @brainsmkumbwa6267
    @brainsmkumbwa6267 24 วันที่ผ่านมา +7

    Masapota oyenda nawo amenewo,mene malawi alili palibe angawombele manja Michael Usi Kumpoto

  • @leonardmalirana7423
    @leonardmalirana7423 24 วันที่ผ่านมา +1

    SKC ANAGWIRIZANA NDI MCP KUTI TERM INO NDI YAKE NANGA INU A USI ZILISO MOTERO KUTI 2025 MUIMA NDINU

  • @user-wb9ji3oe5o
    @user-wb9ji3oe5o 24 วันที่ผ่านมา +2

    Landirani ndalamazo muzidye ndipo chisankho charity mumtima mwanu. Adali kuti zaka zonsezi 4? Idyani ndipo voti iri kwa inu.

  • @user-ru1mm7bf4p
    @user-ru1mm7bf4p 24 วันที่ผ่านมา +2

    Munanena zonse palibe chomwe mwapangapo mu 4 year ndiye mungapange Chaka chimodzi? Akulu inu dyela mukumva kukoma ndi Chakwela koma nthawi mkachitsilu posachedwapa tikuiwalani

  • @user-hl1jt6eo3d
    @user-hl1jt6eo3d 24 วันที่ผ่านมา +4

    ndalama tidya nawo zaulelezo 😂 we gonna accept your gift ..after eating money vote 2 DPP

  • @nelsonnkhambule6292
    @nelsonnkhambule6292 23 วันที่ผ่านมา

    Mukupusika waka wana. Kwali tipeni waka ndrama tilyepo nase ku mzimba kulinje wa mcp

  • @OsmanOsher-sh6gp
    @OsmanOsher-sh6gp 23 วันที่ผ่านมา

    Awa akufuna atimangise tiyankhula bwanji mutasema kachanyau ka Ceiba crime

  • @MakabaBauleni-c2i
    @MakabaBauleni-c2i 22 วันที่ผ่านมา

    Kma Mr Usi sakutha kuona patali cz udindo uwu ngwa chaka cimodz chabe nde sakudziwa kt president yemwe akuwatuma leroyu pamene convention yacitika ya mcp iwo chawo palibe kmanxo sakudziwikatu pano kt ali cipani chanji mapanga awiri avumbitsa mwacidziwikire apa Mr usi avumbidwa

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 23 วันที่ผ่านมา

    Bwinotu koma kumenyela nkhondo ndiolose nkakutafunile pasidya...

  • @bisweckchimphamba8497
    @bisweckchimphamba8497 15 วันที่ผ่านมา

    Kodi ngongolezo umakongoletsa ndi iweyo?ndimayesa kuti kuli bungee laketu!iwe tangopita ku MCP basi usapussise anthu,munthu wachabe chabe iwe

  • @KennedyKanyama-ce8lb
    @KennedyKanyama-ce8lb 22 วันที่ผ่านมา

    Palibe mungapange pepani. Kudya katatu athu tikudya katatu pa week. Tikudikira passport yotsika mtengo. Tikudikira univesal subsidy. Tikudikira kuthesa ziphuphu now corruption is mission of this government us u can see. That is no sense. Nde inuo mwaima pamenepo ndikumanena zotsathekazo. Sikufuna kamwa yanuyo ndi chakwera wakoyo zimene tikufuna mungopanga zomwe munalonjeza osati kugawa ndalama sintchito yako imeneo. Za neef zikukukhuzani bwanji? Vice presdent kumanena za neef kkkkkkk. Upite kwa chakwera passport, fertilizer, kudya patsiku katatu, kutheza umbamva omwe a mcp akubazo. Osati zanzii ngati zimenezi sitimadya ndare.

  • @MosesMkandawi-e2v
    @MosesMkandawi-e2v 22 วันที่ผ่านมา

    Kno 1000000 job's kno vote mfundo mulibe munawanamiza 1 000000 job's
    Pano mwapeza mfundo yonamizila anthu
    Pakuti munawalonjeza feterizes 4500
    Zonse munalemphera no job's no vote

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq 23 วันที่ผ่านมา

    Manganya becareful where is cheap feteleza,iwe wapakamwa kwabasi,thawi ya mcp yatha,don't bring excuses pls

  • @user-ev6bi7jr7g
    @user-ev6bi7jr7g 23 วันที่ผ่านมา

    Ndalama tengani ndizomwe zija amaba zija koma osawavoteranso

  • @MadalitsoIbrahim
    @MadalitsoIbrahim 24 วันที่ผ่านมา +4

    Masapota oyendanawo mpaka kuwapasa mic kuti azimveka kkkkkkkkkkkkk

  • @ELLENZAPS
    @ELLENZAPS 22 วันที่ผ่านมา

    Alibe manyazi manganya kuwimbera mfiti mmanja chakweya anzako athawa Koma iwe Uli maso pyu komko unya uwona galu

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq 23 วันที่ผ่านมา

    Kodi ameneyi akuyendayenda ngati ndani,ndi kapeni kapena vichi

  • @user-ww9rj2wx8d
    @user-ww9rj2wx8d 23 วันที่ผ่านมา

    Za ziiiii zamanyi nthawi yonseyi munali kt monse tavutikila muzaka 4 panopa muziti nyu nyo nyo ukawawuze ana ako wamva unamagulisa chilima ukufuna utiguliseso Kwa chakwela wakoyo

  • @user-sh5wq4uf6r
    @user-sh5wq4uf6r 24 วันที่ผ่านมา

    Kamunthu aka akuti ka kamanganya aka ndikopenga

  • @connexlita2846
    @connexlita2846 23 วันที่ผ่านมา

    Zimene akupanga Micheal Usi , nchimodzimodzi kusongozera mawungu ovunda ....

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 24 วันที่ผ่านมา +3

    Kod daily uzingot chakwera anandisakha Ine vice president kod zachilendo et sudaonepo

  • @user-cb5gh9md4i
    @user-cb5gh9md4i 23 วันที่ผ่านมา

    Awa angoyambitsa mpingo

  • @AllanWyson
    @AllanWyson 24 วันที่ผ่านมา

    Nawo bambo a sikono 😮😮😮 daily kumangokhalila a Chakwera pondisankha ine,,, 🤣 🤣🤣🤣

  • @lingsonmitunda293
    @lingsonmitunda293 23 วันที่ผ่านมา

    Koma dziko la Malawi lapepetulidwa ndithu 😅

  • @georgengwira3152
    @georgengwira3152 23 วันที่ผ่านมา

    Mbuzi yamunthu gwape

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q 24 วันที่ผ่านมา

    Za ziiiiiiiiii asasokoneze anthu uyu ali nchipani chake osangopita kumene ko bwanji???

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg 23 วันที่ผ่านมา

    ukachimwa dziwa nyimbo

  • @SaidDayton
    @SaidDayton 24 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkkk sakuziwa chomwe akuyakgula aaata

  • @FrancisMazamba
    @FrancisMazamba 23 วันที่ผ่านมา

    Ngongole anthu amasauka nayo kapena mukufuna muwapatse zaulele ndalamazo

  • @user-kt5bq2wg6v
    @user-kt5bq2wg6v 24 วันที่ผ่านมา

    Komatu munthuyu akamba chilungamo.

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg 23 วันที่ผ่านมา

    wina wabuka kale kachaso wake uko kut apatsidwa ndalama

  • @AdamKay-q1l
    @AdamKay-q1l 24 วันที่ผ่านมา

    Shipisani katunthu basi osati zogawa ndalama ai mwagawila anthu angati?

  • @Joe-vf1ym
    @Joe-vf1ym 24 วันที่ผ่านมา

    Iwe chitsiru akutuma galu

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 24 วันที่ผ่านมา

    Manganya ndi bulutu amangobweleza speech 😅😅😅

  • @paulmanyamba5437
    @paulmanyamba5437 24 วันที่ผ่านมา

    Zopanda mutu idziii mwaziwa liti dzimenezo kapena ndi tikufelanji eeeti

  • @user-rk3gq7gd8f
    @user-rk3gq7gd8f 24 วันที่ผ่านมา

    Unya uwona ulibe chipani

  • @RaphaelAniva
    @RaphaelAniva 24 วันที่ผ่านมา

    Za ziii bas, koma awa

  • @JasonMailos
    @JasonMailos 24 วันที่ผ่านมา

    Opeleka chilima uyu galu wamundu

  • @RaphaelKweve-u5s
    @RaphaelKweve-u5s 24 วันที่ผ่านมา

    Bwanawa sakudziwa chomwetu akuyankhula ,,,,nanga akayamba fundo sakuyimaliza ,,mkuyamba ina osamayimaliza ,,mkubweleraso mbuyo palibe chimwemwe ndavapo ine

  • @user-un8yq1gg2i
    @user-un8yq1gg2i 24 วันที่ผ่านมา

    Musawanamizire anthuwa mwene, palibe amene wapempha apa inuyo ndiamene mukuwalonjeza, komansotu a utm wo avala dzanyuwanitu kkkkk anyway nyimbo ikamatha or ukweze volume imatsikabe

  • @YNOTGEORGE8
    @YNOTGEORGE8 23 วันที่ผ่านมา

    Nonses

  • @JeanBetha
    @JeanBetha 23 วันที่ผ่านมา

    Mbuz

  • @StevenBanda-f5g
    @StevenBanda-f5g 24 วันที่ผ่านมา

    Ulibe nzeru komanso ndiwe garu

  • @Kiyamachilipa
    @Kiyamachilipa 24 วันที่ผ่านมา +1

    Mwadziwa liti?

  • @kondwanichiwanda
    @kondwanichiwanda 24 วันที่ผ่านมา

    Zaziiii kape uyuu

  • @CassimMbalaka
    @CassimMbalaka 23 วันที่ผ่านมา

    Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pokuyikani nose wokhudxiwa pa ifa ya chilima

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk 24 วันที่ผ่านมา

    Chokhachi usi,,,ndimakudyadira...akumbutse ndare kumwamba kulibe....

  • @JosterNgalawa
    @JosterNgalawa 24 วันที่ผ่านมา

    Opanda dzeru iwe mr chikangawa

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 24 วันที่ผ่านมา

    Chitsilu iwe eti uyu amandinyasa

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 24 วันที่ผ่านมา

    Nifi yo tiyeni tilandire tidye koma osavotera chikangawa. Komaso akunamayo akuti akupereka nifi ku nkhota koto limenero ndi boza vp lamukunkuniza

  • @dennisbanda4751
    @dennisbanda4751 24 วันที่ผ่านมา

    Bwana usi mulungu azikutsogolerani mulindi umunthu

  • @CobratwaibYusuf
    @CobratwaibYusuf 24 วันที่ผ่านมา

    Chemanganya azanu ali ku convention inu simudapite bwanji kodi utm imene muli inuyo ndiiti ??????

  • @felixjoseph8161
    @felixjoseph8161 24 วันที่ผ่านมา

    Chitsiru uyu alibe nfundo anapha nzake kufuna mpando panyini pamake akuona ngati ndife ofoira ngati iye

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 24 วันที่ผ่านมา

    Kodi akuyimbira m'manjawa anawagulira aMbuye ntengeni?

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg 23 วันที่ผ่านมา

    komatu guys anthu ndiye Ali ziiiii 😂😂😂😂 akungodziwa kut bodza lawo lachepa anthu akungodziwa komwe akupita kkkk

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON 24 วันที่ผ่านมา

    😂😂kusangalarila mr yudasi yoooooo 😂😂😂😂😂😂😂😂 koma njara ili thoooo osamanama usiiiii iweeeee ukukakamira achakera ukugula mavoti kwawathu

  • @jazielbenford5881
    @jazielbenford5881 23 วันที่ผ่านมา

    Panja penipeni

  • @user-rz8qp8tj8e
    @user-rz8qp8tj8e 24 วันที่ผ่านมา +1

    Go and sleep mbuzi iweyo

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 24 วันที่ผ่านมา

    Akuyakhawo ndie mawu ngat Isaac ndi Jakob

  • @alexandermwandira2376
    @alexandermwandira2376 24 วันที่ผ่านมา

    No sense, u r not a public speaker

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o 24 วันที่ผ่านมา

    Galu iwe ife a UTM sitimakuwelengela wamva

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona 24 วันที่ผ่านมา

    Pelekani ndalamazo koma udzasowa mavoti ndi chipani cha MCP.

  • @EmmanuelFinias
    @EmmanuelFinias 24 วันที่ผ่านมา

    bwana august akutha ngongole anthi sanayambebe kutenga

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt 24 วันที่ผ่านมา

    Kom mene ukuyanguliramo ziteka poti thawi yata kare dpp ikulowe boma koma mene chakwera afomerese bs areperela

  • @jamiajafali6619
    @jamiajafali6619 24 วันที่ผ่านมา

    Uwawuze aMCP kuti asiye kukapa antu..naweso

  • @brainsmkumbwa6267
    @brainsmkumbwa6267 24 วันที่ผ่านมา

    Galu wa chabe chabe iwe Michael Usi

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 24 วันที่ผ่านมา

    YUDASI KUMVETSA CHISONI KWAMBIRI

  • @JoycieMbaya
    @JoycieMbaya 24 วันที่ผ่านมา

    Koma ndiye sewero Leni leni

  • @KondwaniBanda-ul8sj
    @KondwaniBanda-ul8sj 24 วันที่ผ่านมา

    Aaaa zazi munayiwala kuti chilima anakuchitilani wabwino mumangokamba zachakwela basi kuyiwala kuti pali wina amene anakufikitsani pamaso pachakwelayo tiwona ngati ukhalepo paka 2026

  • @Kiyamachilipa
    @Kiyamachilipa 24 วันที่ผ่านมา

    Kulibe chulungamo, mwaluwa

  • @JoycieMbaya
    @JoycieMbaya 24 วันที่ผ่านมา

    Ka speech aka katikwanano. Kodi akuchemelerawo akuchita sewero?

  • @wisdomchilanga723
    @wisdomchilanga723 24 วันที่ผ่านมา

    Bwanji mukanaseva Biyen inu ausi

  • @user-kq6rp6hn7y
    @user-kq6rp6hn7y 24 วันที่ผ่านมา

    Business iyenda bwanji anthu alimbe ndalama

  • @PhillipHendre
    @PhillipHendre 24 วันที่ผ่านมา

    Anthu omvekawo kaya angati kkkkkk usi kwako kwatha tachita manyazi anthu angati akukululutira manyazi bwanji kale lonse zaka 4 za neef munali kuti 😊

  • @IsmaelBilal-lh1pi
    @IsmaelBilal-lh1pi 24 วันที่ผ่านมา

    Zidakwa zalezela zaulele 😅😅😅

  • @user-wl7xn3or6d
    @user-wl7xn3or6d 24 วันที่ผ่านมา

    Ndalama mosemuja simunayambebe kugawa mungowapusitsa Athu kkkkkk dzinenakuti tili busy tikupanga ndalama kkkkk ndalama zakeziti

  • @HanifaAdam-tm9yv
    @HanifaAdam-tm9yv 24 วันที่ผ่านมา

    Kma ma comnent wa mmakhala ndi nthawi yowerenga mr nthiko? anthu akukuitanani bambo a sikonooooo... anthuwatu ali ndi njala

  • @BlessingsMikeyasi
    @BlessingsMikeyasi 24 วันที่ผ่านมา

    Zamakommedy ine ai Keanu konko Pusey

  • @thulambale2836
    @thulambale2836 24 วันที่ผ่านมา

    Owina wina

  • @isaacimmantambala5294
    @isaacimmantambala5294 24 วันที่ผ่านมา

    Anyamata ama two sawu akutinyasa ma backing opoila...zilizose avekele eyaaaaaaaaaa bwanaaaaaa eyaaaaaaaaaaaaa kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e 24 วันที่ผ่านมา

    Chikangawa

  • @Kiyamachilipa
    @Kiyamachilipa 24 วันที่ผ่านมา

    Pepani chepetsani bodza bwana mthiko

  • @user-wl7xn3or6d
    @user-wl7xn3or6d 24 วันที่ผ่านมา

    Athu ake aka chasutu kkkk angofuna ndalama

  • @HappyBirchForest-zy8nq
    @HappyBirchForest-zy8nq 24 วันที่ผ่านมา

    A utsi ulemu sumakuyenelanitu muziona ma comments awanthu 😢

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb 24 วันที่ผ่านมา

    Galu lwe palibe chadzeru pa lwe galu manganya nonsense

  • @ShadreckAustin
    @ShadreckAustin 24 วันที่ผ่านมา

    Kape

  • @user-nt9go2fz3k
    @user-nt9go2fz3k 24 วันที่ผ่านมา

    Nyopakeee

  • @EmmanuelFinias
    @EmmanuelFinias 24 วันที่ผ่านมา

    zazii awa apenga

  • @MikeKanyaza-bm5tp
    @MikeKanyaza-bm5tp 24 วันที่ผ่านมา

    Mbuzi

  • @Kiyamachilipa
    @Kiyamachilipa 24 วันที่ผ่านมา

    Wabodza mthiko

  • @EmmanuelMoyo-hy5ni
    @EmmanuelMoyo-hy5ni 24 วันที่ผ่านมา

    Useless comedy man

  • @user-nt9go2fz3k
    @user-nt9go2fz3k 24 วันที่ผ่านมา

    Fusek