Rest in internal perfect peace Grace Chinga 😢😢😢😢 Munatisiyila mau, I just want to say zomwe munatiuza zija zikuchitika mom once again rest in peace 😢😢😢😢😢😢
Dan Lu, Nkasa Ndi anthu oti sanapite ku school amadyela mukuimba chonchi, Akufuna azithandiza mabanja awo kangachepe angapeze ndeosawaloza zala koma pachilungamo chakwela waononga dzikoli, Chakwela amabisalila kuti ndi m busa koma amamupanga chilima zija ndinkhaza komanso Ufiti.
Chikangawa party Chikapita chaka chamawa chino, uzangoyang'ana nsana wa njira ya ku South Africa uzikagwira maganyu, Chifukwa ndiye ife tizakuphiphita ndikukuphwasulila ting'oma takoto.
Ndichifukwa chake pa ndalama paja Pali anthu akufa awa after awafinya pakhosi ati atembenuka munali ndani a Dan lu apa ndiye mwangoononga mbiri iwe n'galu
Choka apa iwe mwana wovesa chisoni iwe anthu akwanu akuvutika kwa baluku uko iye ulipano kutambasula kuchikamwa kwako konunkhako mwana ovesa chisoni mulungu akuyendele mwapadela dela ukufunika yesu iwe moti asukuwona mavuto ali muno
Awa last week ija amalira kuti anthu sakukonda nyimbo zawo akuluwa alibe gud guidance and akupha carier
Shaaa koma wapala heavy kapeyu though money exchanged hands koma nde wapala wathera pomwepa.
Dpp my vote 💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙
Akuwapusisa achikangawa uyu mumuwonaa azatulukaso kuzapita komwe kul ndalama.
Dpp my vote 🗳❤🎉🎉🎉🎉
Rest in internal perfect peace Grace Chinga 😢😢😢😢
Munatisiyila mau, I just want to say zomwe munatiuza zija zikuchitika mom once again rest in peace 😢😢😢😢😢😢
Dan lu wapala ndinyimbo iyi, lozani zanu ndiye nyimbo broh
Manyaka, phala la nyimbo,
Lozani zanu is the best song osati manyaka iyi
Dan Lu, Nkasa Ndi anthu oti sanapite ku school amadyela mukuimba chonchi, Akufuna azithandiza mabanja awo kangachepe angapeze ndeosawaloza zala koma pachilungamo chakwela waononga dzikoli,
Chakwela amabisalila kuti ndi m busa koma amamupanga chilima zija ndinkhaza komanso Ufiti.
Dan Lu skeffa ndi agalu muziona 2025 sipatali gyz ndi chakwera chikangawa wanuyo paeazy
Ntayeni uyo bola anatisila nyimbo za boh ku dpp galu akagwele ameneyo nde amvatu nyunyunyu mene kwa khomela pa katoto akunamatu ameneyo dpp my vote
Apm my vote😊
After Jetu atawapambana aganiza zolowa ku ndale 😢😢
Kkkkkkkk apa wanya nayo, zake zada basi
Dan apa ndiye ayi.... Nyimbo zomwe mudaimba posapota DPP ndikawawa ndipo dziwani kut ndizomwe agwilitse ntchito pa kampeni osat iyi ayi...
Mukuziyalusiranji akulu, Malawi wa lero Simachakatu ay anthu anasukusula palibe angawanamize😂😂😂😂
Dan lu sanalakwisee iyeyu akangochemerera chipani chimaluza 😂😂 osadanda adadi boma 2025moto kut buu 🔥🔥🔥 DPP my vote
Ine nd mmozi ndmamukonda kapeyu zomwe wachita apa patumbo pake
Mxiiii nde bola lozan zanu iyi ndiyo cha 🏃🏃🏃🏃🏃🏃
Kudyetsa anthu chitedze feteleza Mk100.000 chikangawa mbola ya nyimbo!
MANYI amunthu
Ndipo Dan lu sikuti siiwe oimba ayi mwina sukudziwa
Mmm zaziii muzangofela zayeni inu 😢😢changa chisoni chabe pot ndi artist wathu
Lozani zanu ife tione imeneinja number one 🎉🎉🎉kma iyi zilo pa 10 😂😂😂😂😂ubwedza ndalama iwe chikangawa akabwerako ku America 🇺🇸 silibwino ata 😂😂😂😂
Ndiwe galu palibe chimene chikuveka apa APM my vote
Ukayambileso aise apa nde palibe wagodya ndalama 😂😂😂😂😂😂😂😂
I stopped listening to his music a long time ago when I heard about him About chakwela
Chikangawa party Chikapita chaka chamawa chino, uzangoyang'ana nsana wa njira ya ku South Africa uzikagwira maganyu, Chifukwa ndiye ife tizakuphiphita ndikukuphwasulila ting'oma takoto.
Ayimbileni basi koma simukuwinanso taaa,
Ayimba oooooonse kaloweni kwa chikangawako,koma 2025 muli kunja
Braza mwapala lozani ija munapha💙💙💙💙💙💙 ....ayi adyeleni ndalamazo pot APM ananena kut kukana ndalama nkovuta ...tiyeni tilandire vote yanu ili komwe mwachoka uja😂😂
APM my vote
Ndichifukwa chake pa ndalama paja Pali anthu akufa awa after awafinya pakhosi ati atembenuka munali ndani a Dan lu apa ndiye mwangoononga mbiri iwe n'galu
Ineyo si sapota wa aliyense koma akulu awa alira sadati ndithu a Dan Lu mwachidule angovomereza kuti nsuzi watha awa
Sure ndipo awawa ndachitsilu samayeneraso kumayakhula zamwano anakangokhala chete osat kumalubwalubwa zaziii
Dan luu ungofuna akupase ndalama bas ukatero utuluke bisines imeneyo aaa koma ikudula
Iye amati marilo akatuluka nyumba sabewelela nyumba iye kumeneko wapitako ndiye maliliwo chifukwa anamwalila kalekale mu 1994 abella bwanji tingot wonse amene akulamulapanowo ndianthu akupha skufuna azingopha anthu osalakwa
Dan lu mwana wanga Dan lu mwana wanga Chan ichi olomanyaz pakamwapo kd mwachita kupangila record PA 4ni kapena Sana ibalace
My vote is for Apm osati chisilu tili nacho lelo chopanda maplan
.....chisilu cha munthu .....ineyo ndiye chakwera toto ngakhale anthu atatha mu ziko
Munthuyi ndi zobadi bwanji kkkkk maluzi amuswa heavy😂😂
Adan Luu mwakwera yokuphwa matayala iiiiiiu palibet chikomapo kuposa tsonyani ZANU IJA ife tione .
DPP MY VOTE ❤❤
DAN LU WADYERA PASANA PAKO NDITHU NDI CHIKANGAWA PARTY YAKOYO ZOPUSA
UTM MY VOTE ❤
Tomorrow is a hope not a promise....
Oppressed will decide
Choka apa iwe mwana wovesa chisoni iwe anthu akwanu akuvutika kwa baluku uko iye ulipano kutambasula kuchikamwa kwako konunkhako mwana ovesa chisoni mulungu akuyendele mwapadela dela ukufunika yesu iwe moti asukuwona mavuto ali muno
Kunena molondoloza ndekuti Peter salinawo kumidimaku ngakhale Bible linanena kye kuti dima umadana nkuunika so sizingatheke Ana adima kukapanga spoti Ana akuunika so zinayenela kuti Ana adima akhale pamodzi Ana opembeza mlungu pamodzi aliyense apemphele kwa mlungu wake ndye mulunguyo ayankhe pemphelo kwa Ana ake tione kuti kd Bala ndi mlungu so izizi grace chinga ananena kye kuti akumenya nkhondo yapansi pansi enawo azizatuluka kumapeto so pomwe nkhondo ikukula iwe ndne tiye tipemphele kuti mlungu amenyele ife nkhondo kuziwike kuti yehova amamenya nkhondo
Yes chilungamo
Wayimba za ziii, komabe tikuziwa kuti wangoyimbila business koma vote Yako ili ku DPP same to me
Imba zosapsazo poti ukufuna ndalam
Dpp ija osazaiphwekesa ❤❤
Lozani zanu ija ndye nyimb awa ndopusa mkona nyimb zawo sizikondedwa iyaaa musowa nanu kuchikangawa kwayitana mukatero
APM our votes in Malawi now
Mwana wanga ngat akukuseka at zosabhebha😂😂😂😂😂
Mumakutu ndikukhala kwake mumalowa sosoyanasiyana zabwino zokha ndizimene zimasalamo ndalama paja ikalankhu chilungamo chimakhala chete
Dan luu iweyo ngat ukufuna dollar nde wanyika
Komad zowona makosana cha kwela wasintha zambir maka Maka kwa ife timadalira kulima zinthu zikuyenda.
Kod amapanga record amapanga ndani ngat ti ma studio ta mma kwalala
Mposooo😂😂😂
Tulani pasi ijatu eee munaphatu bgy
DPP 🔵💙 yomweyo next year m'boma
Iwe dziko lakutula pansi, watha basi aise. Ife timadana ndi anthu adyera.
Chakwera woyeeeeeeeee 2025 boma.
Iyi ndiye phwala LA nyimbo
Waipa zedii panyimbo imeney😂😂
Tikuona komwe ukathere ndi dyera lakolo
Mbola my vote Apm ❤❤❤
Manyazi bwanji ma cadet a DPP.
Mwanyika mabwana
Km dan luh kumpusitsa chikangawa kkk kumudyera ndalama kutulutsa manyakawa😂😂😂 kkk umatha APM WOYEEEE
Mumati ndinu wachiayao president wanu wavomela kut azanu achiyawo azipedwa uku aaaaa
Kape den lu mavuto onsewa matatuu phwi onsewo ndiwedi wasatanik wasatira anzako
Za ziii Dan luu hiyaaa
Km kumalawi ndalama patsogolodi nanga ndikulotadi mwamva aaaa
Unakati nyimboyi uzingovela wekha ase wava
Kujoyina MCP zimangofanana ndikujoyina UFITI
DAN LU NDIYE CHANI MANYAZI ULIBE
Dpp my vote
Manyaka anyimbo ndipo iwe ndiwe kape zedii ngati kuli kufuna ndalama mmmmm!!!!! Wapala zedii koma choti uziwe adad ndi moto ndipo ife tikhala tikusewela nyimbo monga izi. Lozani zanu ife tiwoneee komaso winaso ayiiii!!!!! Eyetu osati manyaka anyimbo iyiyi ndipo kumeneko udikilile iwe ndi skefa chimoto kupeleka nsembe
Km many amenewa ndiy ayi
Bolas kumavela mishion
Kumaimba ukuziwa kuti u need money koma not zoti Chakwera wawinaso
Ziwoneka pothela galu wamuthu ameneyo
Dpp my vote 😂😂😂😂😂😂😂 wapala galu💙💙💙💙🩵🩵🩵🩵🩵🩵🩵🩵🩵🩵🩵🩵💙💙💙💙💙
Za ziii,koma ndalama ndisatanadi ndithu.mboli yanu man apa mwatha basi
Kod nde kuti ma commet osewa sindipeza yomuyamikila eeet
Chopanda nthandauzo mkomwe zaziiiiii lozani zani woyeeeeeeee iyiyi mwapala bambo
Odi ndikamvele nyimbo za Jetu
Manyaka enieni.
😂😂😂😂😂😂😂zachison ndi 2 🙌🙌
wamisala dun luu
Nyimbo unayimba kale
Chikangawa party 😮
DPP my vote adad
AAA zapamtumbo zeni zeni palibe chikunveka
Eeeh kumalawi😂😂😂🎉
Anantha uyu anayesa kulimbana ndi onesimasi mbuzi yamuthu😂
Zaziii mbola ya nyimbo
Gays enawa ndi amalonda nyimbo zawo
Aona kutulusa chibale kumaposedw ndi jetu ali bola ndiimbe za ndale kkkkkkkkk
Koma kwanyimbo iyi ngati amupasa ndarama abesa kkkkk
Inetu maonangati Iposa lozani zanu ija osadziwa ndi manyaka anyimbo kkkkkkk apapa pamene ndadziwa kut sendera sister's ija imatha kuimba
A dan lu mwayamba kupita kuma studio ama 2500? Zamanyaz kwmbil😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂😂km lozani zanu ija adakwapula iyi wayaluka nayo ndimayesa mzakupsyatu APM 💙💙💙💙💙
Simene kulili kumalawi maluzi anyanya
Zaziiii mphala leni leni
Wapala zedi. Ndimaona ngat muzinena zitukuko zomwe wapanga ngat nyimbo yalozan zanu ija. Apapa ndimanyaka
Uzivele chison imeneyo ndinyimbo
Kachiken Dan lu kumbuka mene nyimbo zako unayimbila za DPP ndizimenez zikufanana kkkkkkkk chimene ungaziwe ndichi kukanakhal kut boma limenel ambuye akulifuna bwedzi ambuye atayikapo zanja panyimbo imen wayimba k mcp km chifukwa ambuye sakondwela nazo uthenga wako wanyimbo ukufalisa ndchifukwa aliyes kukomet akungot za ziii😂😂😂😂