Iwe uli ku soth Africa upite ukavote osamango kamba ayi dzoputsa basi utm yachani ife tili ku mbuyo kwa dpp basi chifukwa tikudziwa kuti ndiyachitukuko anawa ayi akuba anachoka ku dpp anapita ku mcp akubanawoso kumeneko uladi ndiena otele dpp motooooooooooooookutibuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuu2025 bomaaaaaaaaaaaaaaassaaaa
Chakwera zimuvuta yakwiya ndimizimu
Ndipo CHAKWERA wationesa amcp ndi oipa kwambiri ,Chilima amalakwa chiyani ndiy mfutso lathu daily mupephero lathu mulungu atiyakhe zatikhuza KWAMBILI tikulira kupha anthu 9 what is meaning of this? Ndale zophana zabwanji ? Achakwera MULIBE Muthu inu Santana iwe Chilima kukuikan Paule inu kubweza chipongwe chonchi AI mwaphadi tikuona APA ndipo YEHOVA sakhalat chete inuso mupita
Utm boma sange mnyamata utm yaphavu kwambili amandala akuti pusisa
CHAKWERA KUPHA ANTHU BASI KOMA AKUTI ANALI ABUSA KOMA KUMWAMBAKU AMBUYE AWAYENDERE ACHAKWERA
Jealous ndi ufiti zoona, Chakwera and mcp is evil to the core
Chakwera abwerere Ku Church galu ameneyi
Chakwela you mast go
Iwe uli ku soth Africa upite ukavote osamango kamba ayi dzoputsa basi utm yachani ife tili ku mbuyo kwa dpp basi chifukwa tikudziwa kuti ndiyachitukuko anawa ayi akuba anachoka ku dpp anapita ku mcp akubanawoso kumeneko uladi ndiena otele dpp motooooooooooooookutibuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuu2025 bomaaaaaaaaaaaaaaassaaaa
Nanuso munayamba bwino Koma zovotera nyamatazo ndiye ndimbwelera Nanu mukubaralika dziko ramalawi likufunika APM azayikonze then tizizasankha nyamatano otsati panopaso tibweletse ophunzira ayi kumeneko ndiye kukhara kuwononga dziko chifukwa or poyambira nyamatayo sangapawone
Aaaa inu ngati mukufuna APM nde mukuona ngati aliyense angakonde zokonda inuyo??? How???
Gud news
Abwana Ndikufuna Ndikuwuzeni dziko ra Malawi sitikufunika mtsogoleli wanyowani chifukwa dziko likakhara ndi atsogoleli ambili wopuma silimayenda bwino ,Coz atsogoleli wonse amarandirabe ndarama zaboma ndiye muganize Kuti tili kale ndi awili Chakwera Akhara wachitatu dziko lizayenda bwanji ?mayiko anzathu mtsogoleli wopuma amamutsakirq zufukwa amumange cholinga asamamulipile kuwopa kuwononga ndarama zaboma, ndiye chikufunika apa tibwelele Ku Dpp Ngati ayi basi timutsiye Chakwera Apange zofuna zake