Utumiki wa a Twaibu - Kutambasula za pemphero losweka mtima, lomwe Mulungu sadzalipepusa
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 5 ก.พ. 2025
- Ku 1 Samuel 1 kuli nkhani ya Hannah yemwe anali ndi chosowa. Atapemphera mwachilendo, Hannah anayankhidwa ndi Mulungu ndipo anapeza chosowa chake. Kodi mukudziwa kuti malamulo ndi madongosolo a zipembedzo zathu akhoza kukhala chotilepheretsa kuti tipemphere mosweka mtima?
Mverani kutambasula kwa a Twaiba, womwe akhala ku chipembedzo cha satana kwa zaka 17.
Amen Amen kupephera mene Mzimu oyera wakuuzira osati zamalamulo ampingo
Munasowatu a Mr twaibu
Amen Mr twaibu pitilizani kutiphuzisa ndikutidyesa mawu abwino my GOD continue to bless you and your family amen!
Uthenga uwu wachoonadi ukulalikidwadi pa dziko la pansi, amen amen
Amen man of living God
Amen and amen
Amen
God bless u Mr twaibu ahmidi hamid alli....mwapulumutsa anthu ambiri muthenga wanu
Zooona
Amen that's powerful message
Ndipangeni add mma group anu A Twaibu ine Petro Kachingwe Brantley Lunzu
Koma pano ndili kuno ku South Africa Jbrk
Ine Mai matipa
Ameni mutumik
Mulungu akupase mabvumbunso ochuluka
Ngt pali group ndpangen add plz
Mau achoonadi awa
Ndipangen add ngat Pali whtsap group pls
chat.whatsapp.com/JCJdMsSiiRn3Tk4IXjyf8n
Amen