koma nkhani yolimbana ndi obwelayo sinkhani yabwino,tiyeni tikondane ngati tonse tili ndi red blood cells ngati achakwela muli ndi connection yopangila nkhaza obwela from Ruanda please khalidwe limwnwli silothandiza mukanasintha
Thanks bosses stay safe and warm continue with the good analysis of data collection I hope the these videos reaches the president so that they can become a turning point into practical mind set change on actual development Continue with these
Chakwela mmutu mopanda nzelu south Africa ikupita pa sogolo chifukwa cha anthu obwela muzapite ku bellvell ku capetown amalawi azazako kugulisa tomato kuotcha nyama ndi zina za mbili munangotengela boma msanje mmutu mopanda nzelu
Ndikuganiza kut emission imeneyi sichotsedwanso pa youtube. Pali emission yinayake pa nkhaniyi yamalefujizi imene inachotsedwa. Sikupezekanso ndithu!! Fortunately, anthu anaipanga kale download before being removed!!
Kagame walitola dziko lathu ndi boma la chakwela mpaka kulowa asilikali achilendo kumanda malawi inazolowela kupempheza mafano esh amalawi made mistakes to voted congress party chipani chanyazi
Our main challenge is Bakili muluzi here .. akungolekelera anamupanga bribe ..tikuvutika freedom that he gave to us akungoyang'anira wina wake akutizuza
azikhale alindivuto ngati zinthu zikutelo nanga anthu athawila kuti sibwino kungopanga zokomela munthu modzi bwanji akanakhala ndi iwo ali kumozambiki ndiye anthu aziwatelo so sad. zipani zinazi ndiye ayi bola dzana lija timadandaula za kudala kwa zinthu ndi mafuta osati zopusa zoika moyo wa anthu ena pachiswe ayi.
😭😭😭😭...ife monga a malawi tonsefe ndife athu opusa kwambili ndipo tilibe nzeru or pang'ono athu inu munkampanga mademo ku DPP 2019 mpaka kutseka misewu kuti peter muthalika asaduse kulibwanji mademo omwe aja mutawabwelezaso kuti satano-yo achoke pampandopo kapena tinene kuti ulamuliro wake wa satana-yu ukukusangalasani bwanji mwangoti ziiiii or mademo ayiii tawonani satana-yi mene akumawaphera athu osalakwa sizama refugees okha ayii even a malawi akufu simasewe tawonani njala zithu mene zikukwelera tsiku ndi tsiku koma iyee sizikumukhudza aliduuu basi chimutu thasalala kuma office-ko😢😢😢.. sindikudziwa ngati kuti ma video's Anu ndi ma comment awathu amawafikila koma ngati nkutelo ine ndikuti iwe chakwera panya pako pamodzi ndi nduna zako zonse,,ndipo ine ndine muthu modzi amene sindimakufunira zabwino pa moyo wanga ayiii ndipo sindimafuna even nditava dzina lako likutchulidwa near by me ndipo ndimangolaka laka kuti mulungu atangobwela ngati tsiku la lero kuti adzachitenge chitsilu chukula mutu ngati matako a mayi ake atangochiponyera pakati pa moto kuti chipyi chi nfiti ngati chimenechi fuck you chakwera....😭😭😭😭😭
Brother don't worry, the spirit of God show me a vision that chakwera and chilima their leadership is over! Dk is coming in next election he will change Malawi for better.
koma nkhani yolimbana ndi obwelayo sinkhani yabwino,tiyeni tikondane ngati tonse tili ndi red blood cells
ngati achakwela muli ndi connection yopangila nkhaza obwela from Ruanda please khalidwe limwnwli silothandiza mukanasintha
Thanks bosses stay safe and warm continue with the good analysis of data collection I hope the these videos reaches the president so that they can become a turning point into practical mind set change on actual development
Continue with these
Thank you very much bro 🙏🙏👊👊!! Umakwana ndithu!! Umafufuza kwambiri!!
Give them citizenship cz they need to stay in peace thank u
Thank you bg mn respect ndawi zonse appreciate your intelligent sir
Mmatimvetsa kukoma but mumatisiya mmalere....mmangosiya kulakhula osasazika
I need to see you face face brother u r the best guy
Bakili tv u r a legend
Ur de 1 👌big boss💥💥
Ndalama ikuononga dziko lathu
Koma kanyoni analakwanji guys 😢🥺😭
Keep up brother manyazi amugwila chakwela
Who burned Quran in Sweden 🇸🇪 give us updates
Tiwapemphelere ma refugees
God provide this channel Aman.
Live live 🔥🔥🔥
Reality exposure
Ngakhale Ku South Africa ma foreigners ndi omwe akupanga zitukuko
Musaiwale kut ndi MCP olomutaiwuza mutavula pant singamve ndipo ndiyosamva
👏👍2much jzy MW wa2.Brah taday you most am appreciate 2.
Kulankhula momveka bwino bro big up keep it up be safe
Makwana
Chakwela mmutu mopanda nzelu south Africa ikupita pa sogolo chifukwa cha anthu obwela muzapite ku bellvell ku capetown amalawi azazako kugulisa tomato kuotcha nyama ndi zina za mbili munangotengela boma msanje mmutu mopanda nzelu
Inu ndiye number one basi kwa history
Timakunyadilani big man
Thanks bro
Respect brother man❤❤❤❤
You are doing grt job Mr man, keep it up
Chakwela Ndi mbuziiiii yomwa Madzi ometela NDEVU,iye akuti waipeza nzake nkunena Kagame.That's why akumawapatsa ndalama ma Bulutuuuuuuuu ena kuti azisokoneza DPP Bwantasaaaa Nyawu Gule wankulu kwawooooo.Agalu inu muziwanso pa 2025
Kaaya🤔
Mulungu azikutetezani brother
Vuto la Malawi timatengeka ndizirizonse zimenezi tikuvutika ndiife osati a president Thanks for your information
Ayi bakili tv palibenso😮😮Ingwileni ntchito bwana
You are saying Truth brother 👍👍🇲🇼 🇲🇼
I learn a lot from you broh.keep it up
Ine ndimafuna anthu angati inuyo muzilowa ndale mukhoza kutithandiza E.g Manganya akugwila ntchito kuposa chilima nd chakwela pano.
Ulamuliro umenewu ukapitirira ndiye kuti kuMalawi kudzabwera revolution and Iwill be one of them. We are tired of this nonsense now.
That's true
Mulungu achite nawo azikhale ng'oma pamodzi ndi chakwera
Anthuwa ndichimodzi mozi Ife muyisiye free
Thanks to give us history God bless you
Kkkkm😂 indeed chakwera nd nd young brother of id amin 😂😂
Salute to our own explorer yool
Idi amin criterion all the time, for example raising texes
You are doing great job
Ndikuganiza kut emission imeneyi sichotsedwanso pa youtube. Pali emission yinayake pa nkhaniyi yamalefujizi imene inachotsedwa. Sikupezekanso ndithu!! Fortunately, anthu anaipanga kale download before being removed!!
Nduna imeneyi ikufunika imangidwe chilungamo chiwoneke ndi chigawenga chachikulu
Following
Well articulated sir.
Kagame walitola dziko lathu ndi boma la chakwela mpaka kulowa asilikali achilendo kumanda malawi inazolowela kupempheza mafano esh amalawi made mistakes to voted congress party chipani chanyazi
Chanel No 01 here in Malawi
BIG 👍
Nkhaniyo ndiyowona bro munthu wakuda kuzuzika mu thaka ya mu Africa
Am agree with u y bakili muluzi is quiet ? He is the one who bring democracy but he is quiet y
A best analyst
Chakwala usatinyatse
Never give up bro
Our main challenge is Bakili muluzi here .. akungolekelera anamupanga bribe ..tikuvutika freedom that he gave to us akungoyang'anira wina wake akutizuza
Mbale zikhale ngoma, please siyani kudzudza anthu otsalakwa, mwabera ndalama yokwana 6milion, lero mukuwadzudza is it fair, mulungu akuone pamodzi ndi chakwera anthu oipa inu, mulozedwe mudzakapangitse mnsokhano kwa goliati mudzaonanso ndalama zonse zomwe mwaba mudzadzitsandza, chakwera munthu woipa iwe
Chakwera ndi Zikhale ng'oma ndiwanthu osafunika m'dziko lamalawi anthu achabechabe
Chakwera needs God to deliver him from evil spirit
azikhale alindivuto ngati zinthu zikutelo nanga anthu athawila kuti sibwino kungopanga zokomela munthu modzi bwanji akanakhala ndi iwo ali kumozambiki ndiye anthu aziwatelo so sad. zipani zinazi ndiye ayi bola dzana lija timadandaula za kudala kwa zinthu ndi mafuta osati zopusa zoika moyo wa anthu ena pachiswe ayi.
First to comment
Well spoken, wokuda ndi wokuda ma burundi akuzuzika mu nthaka yawo fukwa cha zoba uyu opembeza azungu he doesn't deserve to be called a brother
Yonse madala madala keep it up 💕💕💕
Awesome bro
Kodi Mr Michael Sauka yemwe anapeka Nyimbo yafukolathu,kwao kudalikuti???..ai ndithu Big timadziwa zambiri kwainu ndi fire!!!!!
😭😭😭😭...ife monga a malawi tonsefe ndife athu opusa kwambili ndipo tilibe nzeru or pang'ono athu inu munkampanga mademo ku DPP 2019 mpaka kutseka misewu kuti peter muthalika asaduse kulibwanji mademo omwe aja mutawabwelezaso kuti satano-yo achoke pampandopo kapena tinene kuti ulamuliro wake wa satana-yu ukukusangalasani bwanji mwangoti ziiiii or mademo ayiii tawonani satana-yi mene akumawaphera athu osalakwa sizama refugees okha ayii even a malawi akufu simasewe tawonani njala zithu mene zikukwelera tsiku ndi tsiku koma iyee sizikumukhudza aliduuu basi chimutu thasalala kuma office-ko😢😢😢.. sindikudziwa ngati kuti ma video's Anu ndi ma comment awathu amawafikila koma ngati nkutelo ine ndikuti iwe chakwera panya pako pamodzi ndi nduna zako zonse,,ndipo ine ndine muthu modzi amene sindimakufunira zabwino pa moyo wanga ayiii ndipo sindimafuna even nditava dzina lako likutchulidwa near by me ndipo ndimangolaka laka kuti mulungu atangobwela ngati tsiku la lero kuti adzachitenge chitsilu chukula mutu ngati matako a mayi ake atangochiponyera pakati pa moto kuti chipyi chi nfiti ngati chimenechi fuck you chakwera....😭😭😭😭😭
eti amalawi angoti ziii or mademo
man ukafuna kuziwa kut ndiwo izi mlisabola timalawa
Pipo timuoempherere kanyon zazikulu zichitika
Ambuye atithandize akanyoni komwe Aliko awoneni Maka chitetezo chamoyo
mumakwana big man from here Dubai
Komanso nkhanza (nkhanza ndi katangale)
Umphawi pamodzi ndi nsanje ndizomwe za manga bomali kotero bomali silikufunikanso term inayo.
Brother don't worry, the spirit of God show me a vision that chakwera and chilima their leadership is over! Dk is coming in next election he will change Malawi for better.
Ndunayanu ulibe zeru akupangisa kuti bomayambeso kumatingeira kuno akuwona zimene mukuchita kumeneko
Mumakwana big man !!
Komaso mutiuzereko kwa Chakwerayo kuti kampeni si yopangira ku msikiti
Kom ziko lanthu ndilomvesa chisoni kwambili, akupanga nsanje ndi ma frica azawo osati anthu a pink wa eshiiii so sad 😏😏😏☺☺
chilungamo ndichimene mukuyqngula ulemu wanu bro
Ati kungopita kunja kukapanga za umasikini😂😂
Nakha bwanji ndi takhala ine/inuyo mungave bwanji kuti ndinu refugees
Akaka naneso kandiseketsa nde anachita kutsindikiza 🤣🤣🤣🤣
I like you bro ndipo a Malawi ife nde tili dallow koopsa
Only God knows 🙏
Keep on updating bro mumatiimirira tikuchapika mmutu bro a Malawi these pple they are propagandas the (tonse).
Ndinu mbambande brother
Bakiri muluzi ndi number one
Uyu chakwera atipwetekesa
Munachita mademo omuchotsa presdent yemwe amapangitsa zinthu kuti zizitchipa. Lero mukulira koma mukulephera kumuchotsa.
Achakwela alephela kusunga dziko alichaba pa business yakumba ndala za amalawi
Inu ndawakulu ndipo Chanel yanu ndi 1
Tandipatseni number ya zikhale ndi nundwe komatso kagame ndilakhulane nawo monga lne Mmalawi olimba mtima komatso yemwe makolo anga anatungila madzi dzikoli madzi pomwe timalimanga
Azikhale matama komanso kuipa mtima
malawi is now lankin as a 3rd poor country in the world. poor governance, jelousy, oppression are indeed some of the factors that are killling malawi
Akulu inu muyenera kukhala president ndithu
Only God have mercy on us
Chilungamo chake
Koma ku malawi eeeeee ndilibe nako mau
it's sad to hear that for its my prayer so that very soon God must do something to those people who are doing this
Koma ine ndikamamva izi mtima kupweteka zedi kodi zimachende zaku mpandozi bwanji nkhaza chonchi ambuye chonde zulani mitima yawo
Osamu chosa bwanji kd
Mulungu akudaliseni amwene
Pokha pot tili amphawi kamba ka jealous ndi zoona100%
Koma mangochi ilembe sanje anthu gati ifetso timapedzera ndalama za mpindu
Continue kutipatsira nkhani❤
God help us 🙏🧎
Mumakwana bwana