Chakwera is refunding the money through blood to Bushiri ,as he is killing people who are not supposed to be killed whyy,kupha munthu satelo ,what you plant you will grow you must know that everyone shall test death ,ndee iwe kupha nzako pachifukwa cholamula ,uzaona polekera mfana iwe ,chakwera ndimunthu opusa kwambir kupha anthu oti amuthsndiza,look how he killed sidiki Miaa
Uyitana bwanji anthu akunja kusiya maiko amene ali pafupi? Kma ubusawo umayendadi kapena mumangosocheletsa n'khosa? Dziko ndi anthu ake May the Lord Almighty help us🙏
Ambuye mutetezele miyoyo ya anthu omwe Ali mu ndegeyo chifukwa pa ife tokha sitingakwanise kitelo ndi pemphelo lathu ndipembedzelo pa zoopsa za chitikazi amen
Wowona Za nyengo ,munalola bwanji Kuti ndege yinyamuke ? And yinanyamuka bwanji Ku Mzuzu mukudziwa Kuti nyengo siyilibwino?? Usatana uwu. Kodi Chi MZIMU cha Kamuzu Banda chiliso mwa inu bwana ??
God have mercy all those people they have responsibility You are the one who knows the truth about that missing We have many question but only God knows everything
Sakanamupha chifukwa ife timadik ra kuti 2025 tikawachosa pampando alowe jere chuma chao chonse chilandidwe chibwelere iu boma apa ND ye kuti case ya chilima pansi pano yasekedwa pano kumwabako akuyankha mafunso awoononga malawi ndi kuba
Wasalayo iwe uziona satana wen wen , kaya umaziwa kaya koma I think suziwa mmene umapangila zinthu zako , and unakakhala oziwa akele lomwe unakatula pasi udindo koma kuipa ntima bsi, bola yona anavomeleza nsanga kuti anthu ake asamwalire . Koma iwe walimba ntima kuti tifele limozi ai zikomo Mulungu akupase moyo wautali ndi kuipa ntima kwakoko.
Mr chakwela where is vis president, you doing noses.you exactly what was happening because don't ask people that story, this is the your plan you are div
Aliyense azafa osatsogoza anzanu chifukwa chofuna kulamula dziko, zitsilu inu a MCP ndimatsenga anu a nyau
Ndipo Zoopsatu anthu oipa zedi awaaa mmmm
Iwe chakwera tangonena komwe kuli chilima simoyo umenewo
😂😂😂😂😂 koma guys oh simyo wabwino et?
Ndpo anfufuzetu ameneyo fast
😂😂😂😂😂
😂😂😂😂
Mfiti chi president chokupha😢
Inu ndege yasowa 10am inu ngati president mwadziwa Chama 3pm ugalu okhaokha
Ine ndadandaula kut Chakwerayo sanakwele nawo naye akanakwera nawo afele limodz agalu amenewo😢😢😢
Akwera bwaj mwini wake chiwembu Mcp ntchito zake ndkupha koma amalawi mumavota Dara izi aaaa
Chonde chonde chakwera usandichimwitse wamva chimene ukupangira chibwibwi ndi chani?? Uzalipira mwadzi umenewu
Iwe cakwera wamutani chilima kutero iweyo umangoganidza za magazi basi abusa assembles mmmm mulungu akuyendereni
Achakwela speech yawo sikumdimvekela bwino bwino
Palibe wabwino apa asewa akanakwela ndege limozi ndikufaso limozi mesa ndi m mene amabera ndalama zathu zamisonkho
Inu ndi achitsiru kwambili
@@petertaulo8014 zako zimenezo wapita basi akabela ndalazo kumanda
Lord have mercy.
Achakwela ndi nduna zanu mukuziwapo kanthu ndipo mukayankha mulandu siku lomaliza
Tipeza amene atapulumuke?? Akutanthauzanji??😢 Iye akudziwapo chani? Kusinyeza kuti yagwa? Or yapsa ?or yira ? Or yakatera dziko lina?
Osapulumuka ndiye sawaoeza?? Soeach iyiyu mmmmmmmmm🇲🇼🇲🇼🇲🇼👀👀👀👁️👁️👁️👁️
Mr president??????
Mayankhulidwe akukayikisa galu uyu bwanji osapita iwe unyamuke ukasake nawo ndegeyo galu uyu
Akuti mcp inabwela kuzakhadzika basi munthu kusowa ayi zikomo
Chitsiru iwe chakwera umwarilanso Poti chilima akamaora iwenso kumaola
Mkulu wa bodza uyu
Tikukhululukira chani tsono
Mulungu azakulangani bambo lnu pamiyoyo yawanthu yimene mwayipeleka sembe
Salanjenso adamusowetsa
Bola mukhala inuyo achekwela chifukwa ifeyo sitimakufuna kuti bola chilima
Adzalolera kukhetsa mwazi kuti apitilire kukhala pampando. Amalawi munthu uyu ndi oipa. Msonkhano wathao analengezetsa kuti aimanso. Kumbukilani amalawi kuti uyu munthu anapha president wa assembly of God Kuti iye akhalepo. Uyu ndikathyali don't trust chakwera . Bon kalindo chilima ukusewera ndi njoka, ndiolotse kankutafune
Rip
Chakwera is refunding the money through blood to Bushiri ,as he is killing people who are not supposed to be killed whyy,kupha munthu satelo ,what you plant you will grow you must know that everyone shall test death ,ndee iwe kupha nzako pachifukwa cholamula ,uzaona polekera mfana iwe ,chakwera ndimunthu opusa kwambir kupha anthu oti amuthsndiza,look how he killed sidiki Miaa
Ndizinthu zopweteka Munthu mwango mumasula pamilandu
zikomuno mukungolowesa zingawenkha zipaso zake zayamba kuoneka
Anamumasulila zomwezo inu simukuona angapange bwanji titini atangonkhala
Mukulimbikila kufuna ndege mmalo miyoyo ya anthu
MCP ndiyoipadi zaoneka apa.they are behind this assassination.amadziwa kut awayabwa agaluwa.akut tingopha basi ngat tingamulephere tivutana naye pazagwilizano wathu uja.koma a MCP chomwe mungadziwe mulungu si james ayi.ufumuwanu tauyesa koma mwalephera muchoka basi m'boma and nthawiyi idzafufuzidwa.inu kamalawi kakang'ono ngat kameneka munthu akasowe zoona mwawabisa kut mmatsenga anuwo?anthu oipa awa maka achina ritchad banda,mkukuyu ndi ozungulira kamutu kaja ometa old fashion kujemera dazi uja mitima imamawawa kut tikuchokadi ife zoona.munapha sidik mia leronso ndizi.mupha angat kod?
Phanani Koma nzimu wuliwose uzalawa imfa
Pazuzudipafupi bwajisanakwele galimoto imeneyidipulani samalani tawaibilani akaziawo achilimativemeneagatifotokozele ayakuleniakazawipopanotive
Yehova mulungu wathu pulumutsani Achilima ndi anthu ena omwe alimu ndegemo🙏🙏🙏
Zovuta ndithu
Oputsa iwe mfiti ya munthu
Really President this massage is very stupidly n childish
Ine mene ndikumuonela chakwelayu kayakhulidwe kake ngat Akuziwapo kathu 😢
Aaaa Inu mukuona ngati chani aaaa
Inu inu sogozani Mulungu
Ukuziwa eti olo Wanda msisha dzuro chama 9 analindinkhope yachisoni
😂😂😂😂
Muthu wabodza amaduka dukatu kd mumuvele bwino bwino guyz
Ine ndamvera Limpopo FM mmene ndamvelera a Malawi defense force anaitulukira nthawi yabwino koma awawa ndi abale awo amene anagwirizana nawo anawawuza asilikali amene anaitulukira ndegeyo kuti achoke pamalo padachitikira ngoziyo anapanga dala zimenezo wakupha uyu
Uyitana bwanji anthu akunja kusiya maiko amene ali pafupi? Kma ubusawo umayendadi kapena mumangosocheletsa n'khosa?
Dziko ndi anthu ake May the Lord Almighty help us🙏
Dege yakugwaa mamawa foll up kuyamba madzuro
You Chakwera wam'gulitsa mzako Chilima kwa asilikali a ku Israel 🇮🇱 I know u bwinobwino
Ambuye mutetezele miyoyo ya anthu omwe Ali mu ndegeyo chifukwa pa ife tokha sitingakwanise kitelo ndi pemphelo lathu ndipembedzelo pa zoopsa za chitikazi amen
Wasiwesa ndiwe chakwela boma lamanyadzi kulephela kusaka ndege koma ndamala zaboma zaziiii😊
chitsiru iwe ndi amene wamupha chilima asakuziwa ndani iwe chigawenga ndi zigawenga zimzako unazipanga order ku isilaeli iwe satana
chitsiru ndi iweyo wamva. Don't bring confusion pa kusowa kwa ndege wava
@@MACFARLANEMULENGA wasowesa ndi ambuyako achakwera chimbalangondo cha dzilo satana mbuzi ya muthu icruding iwe kape wadziko
@@MACFARLANEMULENGA am taling you mbambadi chakwera azamwalila ali chiimire i promes you
Fuso langa kodi mene ndegeyi imanyamuka ku mzuzu kubwera ku lilongwe nyengo kumeneko inali bwanji? Chabwino ngati a anyamuka nyengo ilibwino ngati nyengo inasintha mbuyo bwanji osayimba phone kuti musanyamuke kuno nyengo silibwino.
Ndi opusa président wa Amalawi
Poti Asilikali a Israel alikomko kale , m'malo mopempha maiko amuno mu Africa monga South Africa, Zambia,Kenya, Tanzania akutchula dzimaiko zakutali
Iweyo chekwela ndamene wamusowesa ndiwe galu kobas
Wowona Za nyengo ,munalola bwanji Kuti ndege yinyamuke ? And yinanyamuka bwanji Ku Mzuzu mukudziwa Kuti nyengo siyilibwino?? Usatana uwu. Kodi Chi MZIMU cha Kamuzu Banda chiliso mwa inu bwana ??
Chakwera akupanga chibwibwi sindikumukhulupirira uyu lord please help..
Kungoti abambo awa ndimuthu opanda chilungamo muthu wachabe chabe chakwela mmmm
God have mercy all those people they have responsibility
You are the one who knows the truth about that missing
We have many question but only God knows everything
Anthuoyipa a mcp mulandilachilango mulungu akulangani
Ee3 kutchula mulungu pachabe 🙌🏿
Ngati ndege inachoka ku mzuzu .ndiye ku mzuzuko mwadzizi nyengo ndikusitha chinamvuta ndichani kuwaudza kuti musanyamuke ku Lilongwe kubwera kuno ku mzuzu chifukwa kuno nyengo yasitha .
Nkhan imenei ikubalarisa zedi.
Ziko lachabe
Mkuluyi walongosola kumbali yake so sad pena pake pakukaikitsa zed😢
Kodi ku maliro ko bwanji nduna zodziwka za mcp sizinapiteko????
More over chilima anali so kuchokera ku ulendo wina!???? 💔💔
Munachita kugwiri zana wachita ngati m'mene ada chitira Putin ndi prighozin,koma Chakwera sudachite Bwino kumupha Chilima ana kula kwira chiyani Osamu khulukira Chifukwa CHOTI amafuna kuimirira usogoleri Kodi popanda Chirima ukada wina? nonsense
MCP basi yipakire asadzaloweso mboma anthu akupha kuba eeeeeeee mudziwapo kanthu Inu kuphana chifukwa Cha utsogoleri mukaramurireso kumanda.
Sakanamupha chifukwa ife timadik ra kuti 2025 tikawachosa pampando alowe jere chuma chao chonse chilandidwe chibwelere iu boma apa ND ye kuti case ya chilima pansi pano yasekedwa pano kumwabako akuyankha mafunso awoononga malawi ndi kuba
Wabodza uyu chakwera wamugulitsa chilima wafera chilungamo.born kalindo wakhalaakuyankhula komachilima kusamva mlongo wanga.ndipo akangofa anthuawa uwadziwa amalawi
Isowabwaji gatizikosilatu gatitilizijo lamozabiki dimayesa dimalawimomuno mapuamalawialukutiko mulidisabiinu mulunguakuoneni
Our Lord our King save our chilima
Wasalayo iwe uziona satana wen wen , kaya umaziwa kaya koma I think suziwa mmene umapangila zinthu zako , and unakakhala oziwa akele lomwe unakatula pasi udindo koma kuipa ntima bsi, bola yona anavomeleza nsanga kuti anthu ake asamwalire . Koma iwe walimba ntima kuti tifele limozi ai zikomo Mulungu akupase moyo wautali ndi kuipa ntima kwakoko.
Mwamupha inu zanu chifukwa chakufuna ulamulilo wa dziko km chomwe ungadziwe chakwala suwinaso pazomwe wachita kumupha chilima anthu aipa inu achipani cha mcp munazolowela kupha ndikusamba magazi anthu
Lazaro iweyo Mulungu akukanthe ndithu mumtima mwako ukusangalara ukudziwa kuti plan yako yatheka
Bodza lokhalokha, komatu olo musowese chilimu sikut muwinabe, afisi inu
Mumuone pa kamwa pakepo akuchita kuoneka kuti akunama uyu chakwera iwe utiuze komwe kuli chilima tatopa bro nkhaza zako satana iwe
Mmmm shame on you, kutereko a islael agwira ntchito mmmm Jan mumawaitanila kuti athane ndi chilima?
Chofunia thandizo maiko akutali ndichiyani pamene maiko apafupi kuthekera Ali nako
Mmmmm akuluwa tinataya chikhulupiiro ndithu kaya palibe okhalisa mmziko
athu musadandaule zosezi mulungu akudzuwa tingolilila payesu yekha basi
Chakwera mathero azanu ndamenewo iwesotu uzafa imfa ya chisilu
Koma Peter Muthalika? Nonsense, osalowetsapo ndale apa
Mulungu wo simukumuziwa kuma kuzunza anthu obwera ngati ndi obwera
Ndege yasowa mmawa, social media inanena kale koma boma kukanika ku Nena??
Kodi katundu anakagura satah uja panalibe ndege?????
Nkhani iyi Chakwera ukadyera nazo nsima pa window udziwanso
Kodi imakanizidwabwaji PA galaudikutiisikebwaji koma
Pepani utm sogoleleli amene yu kusava chilima
Iwe ndwachibwibwi ukuziwapo kathu galu iwe
Ngati nikutukwane kwambilitu nkamakumva ukuyankhula
Kuchoka mamawa koma malawi ziko lontembeleledwa
Sindikutha kuvesa ndizomwe ndikuvazi
Manyazi ulibe umudziwe yesu chakwaza
Funso imwe a MCP uyu ndiye mugwizano?????
Koma ngat samu yake ili iyiyi nde stigwilizanapo
Koma dziko lamalawi ndilomvetsa chisoni
Kuyakula samatha koma kuba bass pot alowa pitha
Zoonad awawa awonjeza kwambili amfit amenewa
E mwapanga not zimene zochitika iya
Sory chakwera wasala wekha zoona 😭😭😭
Mr chakwela where is vis president, you doing noses.you exactly what was happening because don't ask people that story, this is the your plan you are div
Osamgonena kt zomwe mumafuna zatheka bwanj....munthu wangobwera masiku omwewa ku ulendo.mukumtumizaso kumalilo osapita inuyo bwanj.mesa mumakonda kuyenda ndinu agalu achabe chabe
Ngati munthu amamwalira pangozi ya Njinga Chilima ndindani atakhale osamwalira pangozi ya NDEGE rest in peace Malume😂😂😂😂
Kwenako iweyo chakwera galu
Chakwera ndiwe mfiti yamunthu ukudziwapo kanthu,nzako wangobwera kumene kuchokera ku korea komwe unamutuma,lero nzako asanapume nkumutumanso kuti apite kumaliro asanapume bwanji sumapitako iweyo ndi nkazi wako? Galu wamunthu ukudziwapo kanthu
Wampha nzako ndiwe chakwera
Mwapedza potafunila drama
Galu wamunthu iwe mulungu akuone
Iwe chakwera usiye Kutchula Mulungu, machitidwe ako samagwirizana ndi za Umulungu. Umachulusa bodza ndie Mulungu sagwirizana ndi bodza.
Timati 3 o'clock not 3 kaloko
Ndege imachokera ku mzuzu komwe sikunali bwinoko , pomwe amanyamuka samawona nyengo kuti pobwela sitizatela bwino ayi zikomo