To develop Malawi it will require all Malawians to help build a mother Malawi. No one will come from anywhere else to help Malawians in building this country.
Wonder ndi mfana wopanda mantha, Brian mzake ndi George Kasakula, winayuso is in top form, keep up the good work guys, Hot Current ilibe inzake. Bravo. 😎
Keep it up guyz, Koma Apapa watsala Aubrey kusakara. Muitaneni adzaysukuluze Nawo naye. We respect you guys . Changalusa watching from Pretoria South Africa.
Please Brian we need Hot current like before. Like Dausi vs Kasakura. So you must ask ministers to come vs you people in Times TV it will be Good Hot current. Now it's Cold current.
Wonder ndi mfana wopanda mantha, Brian mzake ndi George Kasakula, winayuso is in top form, keep up the good work guys, Hot Current ilibe inzake. Bravo. 😎
I like u guyz mumatha
Keep it up guyz, Koma Apapa watsala Aubrey kusakara. Muitaneni adzaysukuluze Nawo naye. We respect you guys . Changalusa watching from Pretoria South Africa.
aubrey kusakala koma mutengeson kuti zizitsukuluzika bwino kwabasi.
Please Brian we need Hot current like before. Like Dausi vs Kasakura. So you must ask ministers to come vs you people in Times TV it will be Good Hot current. Now it's Cold current.
Brian's comments 😂nyontcholiiiiiii😅😅😅😅😅
I feel this panel is incomplete... tamutengeninso mtsukuluzi wamkulu kwambiri Aubrey Kusakala please please....
Mumatha guys
Anyamata mumakhwana
Kodi inu ndatola nkhani kapena adale?
Ma police ali ndi unyolo ochepa sangakwanitse kumanga malawi.
Mwina tifunse ma bilidala!!
Makhoti Amalawi. Ndi mitembo yokhayokha
Next week banda basi
Kkkkkkkkkkkkkkkkk.......🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼
Nthawi yanu muli muboma munakanika ku Manga boma for 27 years of democracy. Pano mwaona mwanayu Chakwela kuyesestsa kukoza dziko Shame on you.
Wakonza chiyani chakwela? Uli ndi maso koma suwona,uli ndi makutu koma koma suunva