5 YEARS TIKUGWETSA NO CHITUKUKO CHILICHONSE...POLITICS EVERY DAY...FUCK THIS GOVERNMENT....A COUNTY WE CAN'T EVEN GET A PASSPORT..TWO PEOPLE ON ONE BED IN GOVERNMENT HOSPITALS.. NOT EVEN MEDICINE FOR POOR PEOPLE SHAME ON US A CURSED NATION.....
Kunkuyu mwatsika mu mitengo tu Allan witika munapha uja nanuso mupita ndi miyala njilamu musa male ndi zikhale ndi chithyola nonse ndi nkaka agenda mu ntcheu a kwa chilima nonse
Missed opportunity for MCP in the north. Vitumbiko was a perfect piece of jigsaw for Lazarus in next year's elections. Vitumbiko could replace the void SKC left in the north.
Zikhale ngoma umayerekedwa pomanga anthu ngati ndiwe mulungu kubera mabrund musaketu bakili muluzi tv
5 YEARS TIKUGWETSA NO CHITUKUKO CHILICHONSE...POLITICS EVERY DAY...FUCK THIS GOVERNMENT....A COUNTY WE CAN'T EVEN GET A PASSPORT..TWO PEOPLE ON ONE BED IN GOVERNMENT HOSPITALS.. NOT EVEN MEDICINE FOR POOR PEOPLE SHAME ON US A CURSED NATION.....
Mulikuti?
Uli ku south africa iweti
@@robertfrackson8814 it doesn't really matter kut ine ndili kut...???
@@WonganiKatchale what do you mean.....? ine ndi Malawi ngat iweyoooo
Ndipo ndizoona bro,ine chipani Ichi ayi ndithu chatizunza amalawi
Kunkuyu mwatsika mu mitengo tu Allan witika munapha uja nanuso mupita ndi miyala njilamu musa male ndi zikhale ndi chithyola nonse ndi nkaka agenda mu ntcheu a kwa chilima nonse
zikhale ng'oma zomwezo vinyo watha mujekete
Ambuye amatsitsa ozikweza ..nakweza ozisisa....tiyeni tilimbike kupemphera basi 2025 ...ambuye ayankha ndithu
Inshaallah ambuye atiwalitsa 2025 dpp ❤️❤️
@@YusufuUsumani❤❤❤
❤❤❤ DPP booomaa❤❤❤❤🎉🎉🎉
Kamajekete😂😂😂😂😂😂😂
Amchita bwino Zikhaling'omba😂😂😂😂
The DC tuluka komwe uliko uying'alule kuno 😂😂😂😂😂
😂😂😂😂🎉🎉
Wang'alula kale kkkkk
Zotsatila za chisankho ichi zitidziwitsa chilungamo cha zimene zidachitika ku Chikangawa pa 10 paja .
😂😀😂😂😂ndpodi aulura zisisi after kupsa mtima
Koma apo nde mwalankhuladi tzisitsi ziululika timva ku Limpopo fm 🎉🎉🎉
Apapa we can comfortably confirm kuti ukuku aulurana 😂😂😒
Kumkuyu uyangane kumwamba umuone mulungu mmene amamutsitsila munthu unaeina pomupha allan witika mzimu wake wakwiya nawe
Zikhale ng'oma mutu uphulika mizimu yakwiya 😂😂😂
Kkkkkkkkkkk kapangidwe
zikhaleyoo uyooo ,2025 muziona chikangawayo agwanso Malawi siyanyumba mwanu muziona
Anthuso avotera prezdent wa experience 2025 achina Chunga kumeneko kkk
Vinyo watha kamajekete
I'm very happy chaluza chigalu chimenechi chimatumbwa Kwambiri,ndikamwe Kaye mowa apa
😂😂😂😂
I like the idea "ndalama talandila Koma ife tisankha munthu oyenela"
Tikatere tayambspotu😂😂😂😂😂😂 becareful chikangawa 😂😂😂😂
Ndipo izitu asasangalale kwambili zikulosela zinazake chaka chamawachi😂😂😂😂😂😂
1.2.3 John wick excommunicado lol
The question is Ndalama zomwe amagawa amazitenga kuti? Alibenso mphamvu pano afufuzidwe....misonkho yathu izithera izi😭😭😭
Kamajekete woyeeer 😂 😂😂
18:10 Brother bakili TV anyamata amakusaka Aja onse alephela mayeso uku tiyenawoni tiwagende ndizidina zamoto zikhale woyee witika kunkuyu woyee
Mumba waberedwa ma vote
Manganya si wawona ,kugawa ndalama si udolo,bwelelan kwanu kwawen ndi kwawen
Who has won ?
Koma Carthy mpaka ena agula ma plot koma zilipo kwambiri
Zikhare ng'oma is strategically waluza ndithu
Vote ndimumtima
Wasala wamkuluyo 2025 akukagwaso
😂😂😂😂😂😂😂
Ndipo mmene zachitikiramu atsegule maso ake, Malawi wa lero siwipusatu
U always deserves bg
😂😂😂😂😂😂😅😅😅km zilibwino kwambiri chikangawa part
Anthu ari pokudya ndalama mavoti ari mu mitima kkk
Ambuye omva kulira kwa anthu imvan kulira kwa amalaw. Chaka cha mawa tisinthiren usogoleri bweresan mutharika ayang'anire dzikoli
Ambuye alemekezeke kuti a zikhale aluza anapanga mwano ndikudziva
Yomweyo galu iwe😂😂😂😂 uipemelereeeeeeee... Uipatse motoooooo💥💥💥💥💥
Akunkuyu mwano onse uja watha dikilani nanuso muzamangidwe kukubwelaku 😂😂😂😂
😂Kkkkk koma kumeneko wagwanayo zikhale nkhope Ngati popayi wakhaula
Kkkkkk koma ndiye vinyo wathaaaaa
Bakili TV is watching you zikhale😅😅😅
Ndipo pompano timunvera
Akukanika kukopa anthu 1400 akwanisa anthu 20 million
Convention iyiyi bola wina asaziphe yekha 😂😂😂😂😂
Zikhale zikomo udziwe kt Mulungu amamva nkhanza zija mukapangila ndan?anthu omwe umawasaka aja lero asaka iwe dziko umalitenga ngat lako
😂😂😂😂😂 asamuka ameneyo
Kkkkkkkkkkk choipa chitsata mwini
Ken zikhare ng'oma 93 votes 2025 boma😂
That is erosion package to ZikhaleNg'oma
Azikhale ng'oma ndi akumkuyu munatchukatu 😂😂😂😂 mwakhaula
Kmtu zikhale ng'oma ndisakumane nawe ndikuthira duka iwe galu mbuZi😂😂😂😂
Missed opportunity for MCP in the north. Vitumbiko was a perfect piece of jigsaw for Lazarus in next year's elections. Vitumbiko could replace the void SKC left in the north.
Very true and he could have come with a good vibe
A times mukulephera kutchula mayina bwanji?
Mkakawo ausungunula ndi mchere kuti usanduke madzi 😢😢
Matama onse aja Kamajeke,Kunkuyu ndiogawa money aja aluzaso🤣🤣🤣🤣🤣
Azikhare ngona mwachita bwino kuluza ndi akukuyu muli ndi mitima yo nyasa kwabasi
Iwe kamajekete mpaka 93 😅😅😅😅😅😅
😂😂😂😂😂dziko Lima zungulula
Ndi ka network kako ka 2G ko ndye wabowa😢
😂nde mwati nkhani ndiyazikhale
Ndengati anthu akuchipani sakukufuna umangoziwilatu pakaipa😂zikhale
Nde nyama zikuluzilulu pano mkumanati chani
Yes indeed
Zikhale sangawine wasala mbale wakeyo anthu okuphawo
Bakili tv naye zikhale ndi kunkuyu 😂😂 anya manyi uku
Mulungu amatsisa ozikweza ndipo anyamula ozichepesa
Kalandeni ndalama akuthyoleni miyendo anthu adakwiyati
Tili mu nthawi ya zikhale ngomaaaaaaaaaaaa waionatu
Ndpo Wina akadativuta akadawina ndthu stikadayenda Ai.azipta azikalima fodya ukoo😂😂😂😂😂
Chete watching from khotakota😂😂😂
😂😂😂😂 wamphwasamuka zikhare pathakopo kkkkkkk
Ndipo imfe timakhala tikunena kuti ndalama siyigula chikondi mamuna wabwino amaoneka ndi mtima wabwino awa azikhale ng,oma koma kulimbana ndi wa bakili muluzi uleke zimenezo
Mkaka ndi zikhale mmazimva uchi ngati mcp munayambitsa ndinu akuchotseni indiana lazalo vmyaluke ndi kunkuyu anthu akupha in ndll
Come 2025 another shock is coming
Mzimu wa anthu aku chikangawa uja osauphweketsa
Azikhale ng, oma achita bwino kuluza amazimbva kwambiri
Andevu za mwayi ali kuti?Amenewa amafotokoza bwino kwambiri....apit bull.
Osewa achita bwino osawina akupha wanthu ukachita choyipa uziwe kt chikudikila kumbuyo mizimu ya anthu 9 simasewela BP yikukomola nanuso
Yomweyo galu iwe😂 waluza mavot kamajaketi ng,oma
Munthu WA mayi unamulanda Malo uja apo ndiye umenyedwa ndi Ana galu iwe
Mulungu alipo ndipo alipo imfa ya chilima ikukathani😢😢😢
A mcp gawaniso ndalama ku tundu wa amalawi kaya ngongole gawaniso komano ziwani kuti chidikhodikho chili mu mtima
Ken zigone /ziyime/zikhare ng'oma/mabatcha/màmbilira walephera mongàso maudindo ake akulephelera 😂😂😂😂
Aviator 1.00x flex away 😢
Ife pheee kudikila wa Bakili Muluzi TV zikhale Ng'ona ndi Kunkuyu kuti akumva bwanji mthupimo
Check out aspairant mps next it's you moto umapita kwatsala tchire
93 keni zikhale ng'oma chimutu chikulile mwano😅😅😅😅
Zovuta kwambir 🤣🤣🤣🤣
Muudziwe moyo achina ujen 😂😂
Mulungu simunthu azikhale Ngoma mwanva muzifuse
Nanunso2 network yanuyi ndie ndi manyaka2 nanga ikungoduka duka ofunika muzitolere
Seems Brian Banda wakulira ku mudzi .Ali ndi moyo wa magemu
Zikhale Ngoma mulungu alemekezeke unapha Chilima ndi Kunkuyu .agalu ino
Oooooo mkaka😂😂😂😂😂
Mizimu ndiyokwiyabe mpaka 2025
Diesel watha
ankamwaza dala anali nd plan yokaba,ankadziwa kut akawina azakabwezeretsa kkkkk sorry kwammbiri koma
Zikhale Ngoma.
Who is this guest speaking?
Cathy Maulidi
Apa wabakili muluzi asakidwabe kapena zapita ndi kama jecket
Kkkkkkk aja amati ndi eni Malawi akhara pansi😂😂😂
Awa edzeka😅
Carthy iwe wawina takuona upange chitukuko kwwnu chamiseu osati kumadura anthu ziwaro yayi chepesani rekani kudumura virarowawanthu
Eeesh
Amuchita bwino kamajekete ndi satanaso kwambiri amuchita bwino
Chi network chake ndiye manyaka eni eni basi
Muziwe kut onse alepherawa nd oyipa mtima