BRIAN BANDA KUPHAPHALITSA ZIMAFUSO -🤔🤔🙌🙌21 July 2024

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 5 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 55

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff หลายเดือนก่อน +15

    Akayamba choncho dziwani kuti mulungu wamakamu ayamba kuwakantha inu mulungu awavula zovala onse akuimila MCP ife chete ndi umasiye wanthu amen 🙏🙏

    • @moosasinoya3307
      @moosasinoya3307 หลายเดือนก่อน

      May Soul Rest In Peace SKC😭🔥💪

  • @MervinMwambinga
    @MervinMwambinga หลายเดือนก่อน +1

    He can be a youth, well educated, good passions and visions but our constitution does not give power to Vp to decide and implement ideas. We have evidence, our lovely late VP SKC. He was our only hope for this country and no one else. Tiye tizinamizana chonchi basi.

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 หลายเดือนก่อน +1

    Mtsukuluzi simunampatse mpata kwambiri ngati mmene munachitira ndi Ndebvu za mwayi. Muzipanga balance a Brian Banda. Mwaonetsa tsankho

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn หลายเดือนก่อน +4

    Skeffa chimoto wathadi eti mpaka afika apa kkkkk

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili หลายเดือนก่อน +7

    Mcp ndiyakupha

  • @PriscillaKhumbanyiwa-i1d
    @PriscillaKhumbanyiwa-i1d หลายเดือนก่อน +3

    Satana amayenda ndi asatana azake amalawi wosazindikila kumasapota anthu akumpha amcp

  • @macmsiska2937
    @macmsiska2937 หลายเดือนก่อน +3

    Mbava yayikulu iyo yikamayankhula m'maso muli gwaa

  • @user-wx5fq7gg7d
    @user-wx5fq7gg7d หลายเดือนก่อน +1

    Mayi Chikata my neba from Mzuzu

  • @user-el8to1te3l
    @user-el8to1te3l หลายเดือนก่อน +2

    N'gona zen zen

  • @NelsonMarley-m6p
    @NelsonMarley-m6p หลายเดือนก่อน

    Zimayi opusa chinkhope ngati mtengo wamulambe mxiew

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 หลายเดือนก่อน

    AAAAAAAAA nthawi Yotani monse muja??? Mumba ndi chakwera amabera limodzi agalu amenewa shupitiiiii

  • @user-un4pm4yt5i
    @user-un4pm4yt5i หลายเดือนก่อน

    Dzitukuko dzompha anthudzo alamulira inuyo

  • @PriscillaKhumbanyiwa-i1d
    @PriscillaKhumbanyiwa-i1d หลายเดือนก่อน +1

    Anthu andale makonda kumuchula mulungu pafupipafupi mulungu akukantheni bava za mcp

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi หลายเดือนก่อน +3

    Koma siteniwe muganise bwino sachakwela muiwale

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 หลายเดือนก่อน

    Big up brother man!!

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di หลายเดือนก่อน +1

    Botolo la madzi okumwa muziliika kusogolo kwanu a Brian osati ku mbuyo or ku mohepete kwanu muziliona or mulibuzy

  • @user-el8to1te3l
    @user-el8to1te3l หลายเดือนก่อน +2

    Mbava

  • @LloydMkula
    @LloydMkula หลายเดือนก่อน

    Akufuna kutumikila a chakwera not a Malawi ma delegates mazimvelatu

  • @joeljere4385
    @joeljere4385 หลายเดือนก่อน

    Onse aku North okhaokha

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 หลายเดือนก่อน +2

    Nyero yako mzimai iwe ndithu

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂 thiraspot paka 1 mita

  • @user-bi6pb5gc8t
    @user-bi6pb5gc8t หลายเดือนก่อน

    Mwamvatu nokha akuti eyeyu akufuna azizatimikila achakwela osati amalawi

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza หลายเดือนก่อน

    Ziyezekanani ku mcpkp uyaaa

  • @Betty-fe9ql
    @Betty-fe9ql หลายเดือนก่อน +1

    Koma ma comment a Brian mpake pena amankhoma 😅

  • @stevemtambalika
    @stevemtambalika หลายเดือนก่อน

    Chikangawayu watha basi kkkkk

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 หลายเดือนก่อน +1

    Mukupikisana kwambiri because you are in government now,, fact osati zinazo aaaaaah. We have also heads to reason.

  • @LowanMasiye
    @LowanMasiye หลายเดือนก่อน +1

    Boma ndilomweli

  • @FaheemChipojola
    @FaheemChipojola หลายเดือนก่อน

    Amai awa nzeru alibe ndithu

  • @user-qd7sz1pf1i
    @user-qd7sz1pf1i หลายเดือนก่อน

    Akunama amayiwotu 2025 mcp mulibepo😂

  • @NthambiInvestment
    @NthambiInvestment หลายเดือนก่อน +1

    Ngati mukunamizana zowinaso muiwale,, vote ya 2025 tikavotela kuchikangawa ,, MCP Pachilani muzipita ,,,,,
    Nanunso a skeffa ndi a mlaka plz plz ziyalondolelani anthu koyenela pl

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo1441 หลายเดือนก่อน

    Amayi inu mmmm😢

  • @mussamapira801
    @mussamapira801 หลายเดือนก่อน

    Akuba okha okha

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i หลายเดือนก่อน

    Abambo idzoo za ku chipani kwanu siii zotandidza a Malawi

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn หลายเดือนก่อน

    Zaziii

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr หลายเดือนก่อน

    A Brian ndi a ndevu apatu tikudabwatu leroli kwabookatu Ku MCP money kkkkkk.eeeeee koma abaleeeee.

  • @andrewBwanaisa
    @andrewBwanaisa หลายเดือนก่อน

    Mwagwa nayo nonse a mcp

  • @kingnavitcha6243
    @kingnavitcha6243 หลายเดือนก่อน

    Angalephere kuchitsa chipani choti ndi chake

  • @alomuddin8801
    @alomuddin8801 หลายเดือนก่อน

    Mcp ya khanza yabweletsa njala mu dziko la Malawi chilichonse chinakwera mtengo,

  • @DavieMoyo-pe8vn
    @DavieMoyo-pe8vn หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂 nyamata WA vinyo Ku MCP Malawi ngosangaratsa

  • @samuelosman3215
    @samuelosman3215 หลายเดือนก่อน

    Aaaa simulaka uyu?

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 หลายเดือนก่อน

    Woiphonya ati akufuna kutumikila chakwela not malawians.

  • @user-iq5xk6ju7y
    @user-iq5xk6ju7y หลายเดือนก่อน

    A Mumba is very controversial, kudzikundikira too much. Ubwino wako amaudziwa ndi ena. Zikuonetsa kuti atasemphana nawo mwayi uwu atha kuukira chipani . He is too confident. He is not bigger than the party.

  • @user-rx1dj7kg8k
    @user-rx1dj7kg8k หลายเดือนก่อน

    Amayi opusa

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r หลายเดือนก่อน

    Kamat uku sizitha bwino uku mungot phee

  • @lupakishomalangaelix6606
    @lupakishomalangaelix6606 หลายเดือนก่อน

    Usi sakaimila uku?

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d หลายเดือนก่อน

    Anthu akewa sizothandiza ziko

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw หลายเดือนก่อน +1

    paja iwe dxina lako ndani

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkkkk oyimba akumalawi

  • @hopembendela
    @hopembendela หลายเดือนก่อน

    iwe wakhutatu kondole eti

  • @jamesmsonkho4830
    @jamesmsonkho4830 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkkkkkkkkk

  • @michaelzuze6516
    @michaelzuze6516 หลายเดือนก่อน +1

    I regret watching this shit

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalie หลายเดือนก่อน

    Ndiwe galu pamodzi ndi akwanu ose stupid guy gud man for nothing.