If it is that soldier talking then he must be careful as chakwera and his gang are mafia they are now playing games they are out to kill so brother be careful
Black board??, Benzene (this is just a small component in gasoline) how did they suck it? , Every pilot before flight makes a check list. We need real facts gents. We are with you but we need facts.
Olo ngati driver amapanga check ma tyres, engine coolant, engine oil. Galimoto likalila amaonso all warning ⚠️ lights pa dash board and levels of fuel. Should we say gage ya fuel mu ndege inali yokufa. If at all they use a dip stick, sanapange zimenezo? Facts are really supposed to be laid osati trying to trigger unnecessary riots.
nkhaniyi ndiyabwino kwambili ndipo zikomo..koma mwafurumira kuibweretsa pa air before kumalidza kafukufuku wanu.chifukwa anthu awawa atha kukumangani or kukuphani before kubweretsa zomwe muli nadzo
Our Ibrahim Toare the likes of Bokinafaso President. Thanks my Fellow Wasili
Ulemu wanu munthu wankulu ndiinu nzelu mukuimila amalawi asati zinazo zikungozinenepela ngati njovu chilungamo kumachiona koma kuchibisa akufuna udindo Allah adzakukhaulisani tsiku Lakiyama lnshaallh 🙏🙏🙏🙏
Mulungu akutetezeni Big man
Ooowooo ngat mukufufuzabe nde mukutiwuzilanji maumboni okwanilira musanapeze why phuma nanga
Big up to you brother may almighty God protect you
May God protect you brother man till chilungamo chifike pa ground
We need something like this sir ayalukedi
❤ Malawi ndidziko laufulu Koma galuyu akutiphela ufuluwathu
God bless you and protect you 😢😢😢😢
😢😢😢😢 mlungu simuthu chilungamo chiziwika Soon in sha Allah
. allah Akbar 😮😮
Inshallah
Tikukhulupilira mulungu my brother akuteteza
Thanks so much. More fire osawopa
Sitikufuna kuvaso zimenezo ayi zilibe tchito ikakwana yakwana basi Mulungu analemba anafa atumiki amene amalankhulisana ndi Mulungu ndye mukanene achilima
Osaopa mulungu akutetezerani ululani ndithu galu ameneyi sawina 2025
Commando wathu iweye big up kuyimila chilungamu
❤❤❤❤ sangakuchoseni ntchito bwana 😢😢😢. Tilinanu pamozi
Kodi ulikuti ukuoneka bwanj😂😂
Big God bless you 🙏
Thanks bwana kulidi mulungu kumwambaku
May Good Lord protect you🙏
Its Bwana Mumandinyasa ndisakubiseni 😂😂 for me
Aaa koma ndiyetu asilikali ake ndiopoilatu, ndiye kuti apha nao ngati anachita kuphedwadi
Or utafa ukaona ufumu wa Mulungu pot kulibe wambeu ku dziko lapansi God bless u soldier 🙏🙏🙏
Thanks alot my brother good Messnge Chakwela you mast go
Big up!!!
God bless you 🙏🙏
Thanks u so much solder for good reporting Allah continue bless you 🙏🙏
❤❤❤ zilibwino kumayankhula chillungamo tchimo ndilachakwera yekha. Mulungu akudaliseni bro 😢😢
A Malawi ndinu oputsa osandipsetsa mtima mwamva ngati ndizoona bwanji osamunyanyalira Chakwerayo kuti atule udindo 😢
Bwanji simunaulure Ngozi isanachitike . Tipinduranji panopa a Vice president athu Ali Mmanda . Mkanaulura Ali Moyo bolani
Mbusa Chakwela wapha Chilima.............
Thank you brother polankhula chilungamo mulungu azikudalisani komaso akutetezeni pa choipa chilichose 😢
Thank you very much???
Inshallah mulungu akutetezani mpaka chilungamo xhiziweke
Good job sir
❤ kukanakhala olo plan yabwino ya asilikalinu kwa nonse amene simuyanjana nane kuphatikizapo ineyo kunyomushuta bas galu ameneyo
Ukutsutsawe do your audio dzitchule dzina nafeso tikumve fundo zako on public. Simple.
Zimawawa kwa wina aliyense zoona kwa obadwa ndiponso wobhereka@❤
Ndipo inu inu
Ulemu wanu munthu wankulu apa ofunika audio muilengeze mu English kuti imveke ziko lonse lapansi
mumaziwa ndiye simudaiteteze ndege bwanji ........inuso mwapha nawo chief
Mbwerera za anthu aku Malawi ndi zimenezo akufuna kuoneka anzeru pano.
The son of MCP stupid
Ine chetee waiting for mapenalty monday kutcheu chakwera ngopusa
Mmmh zovuta bwanji, I pray for your protection
Big up chief❤❤❤ ndipo mizimu yao yimusowese ntendere naye asowe
Aaaaah thank God chilungamo chixiwike
Thanks so much our good brother . We really need the truth on this matter .
GOD BLESS YOU
We're crying all as a nation 😭 but this is totally nonsense!!!!
Ndipo akanangokhala osaululanso nanga simunthuyo wafa kale 😂😂😂
Big up aise pambuyo pako
we are behind you comrade, we don't fear anyone.
😢😢😢 mulungu alipo sakumangani ndithu
Mulungu sateteza anthu amabodza ngati uyu!
Well done sir continue fighting for your country
Akanakhalapo asilikali onga inu 10 zinthu zikanatha kulongosoka Lazaro ndi wakuphadi
Bwana kunyansa zoona, you're heartless chakwela
Appreciate
Mr Chirima 😭😭😭😭😭😭😭
Ulemu wanu m'fumu ❤
If it is that soldier talking then he must be careful as chakwera and his gang are mafia they are now playing games they are out to kill so brother be careful
Panyini pamake chakwelayo ndipo imfa yake idzankhala yogendedwa ndi miyala ameneyo
Iwe ndiye chitsilu chothelatu udziwe. Komwe uliko
There's no secret on the Earth
Good boy😢😢😢😢😢😢
Kubisala ku South Africa mkumati wabisala akupeza
Black board??, Benzene (this is just a small component in gasoline) how did they suck it? , Every pilot before flight makes a check list. We need real facts gents. We are with you but we need facts.
Olo ngati driver amapanga check ma tyres, engine coolant, engine oil. Galimoto likalila amaonso all warning ⚠️ lights pa dash board and levels of fuel. Should we say gage ya fuel mu ndege inali yokufa. If at all they use a dip stick, sanapange zimenezo? Facts are really supposed to be laid osati trying to trigger unnecessary riots.
Guy's let's work up fighting for chakwera go
Nanga bwanji samauulula zisanachitike
Zabodza izi unatani kunena zisanachitike
Eti eti
God be with you brother
God could not be with this brother!
Mpaka pano mu chaka cha 2024 ,tikanaganizabe kuti Otilamulira ndi milungu, kuti iwowo imfa singawakhudze.😢 whether assasinated or not its all death😢
You are more than a Christian Saint in the paradise.
Good job
Mvuto Malawi timankhulipira social media 😅
Timakhulupilira ndikumene cz sizonse zimakhala zabodza. Kachilungamo kamakhala in one way or the other
Nzimu wake uwuze muntendere 😢 our yourng vice president
nkhaniyi ndiyabwino kwambili ndipo zikomo..koma mwafurumira kuibweretsa pa air before kumalidza kafukufuku wanu.chifukwa anthu awawa atha kukumangani or kukuphani before kubweretsa zomwe muli nadzo
Umbuliu ndimatenda pena.kodi who chose the plane as veep transport to mzuzu
umbuli ovesa chison tu
Uyuyu amutuma ndipo amutumawo ali chete. Satana akafuna kusokoneza dziko amalisokoneza. Muganiza kuti anthu akulionera kukondwa ndikoli? Olo mutasintha atsogoleri ambili mbili muganiza kuti zinthu zidzasintha? Poti wina pamenepa akumenya campaign kuti adzadyerenso aMalawi, tsegukani mmaso watumidwa uyu. Munthu wachilungamo sabisala apite direct akafotokoze kuti aMalawi asiye chiwewe.
Chambaaa chakwera ameneyu
Ndipo munthu akuyankhulani bodza limene kaya mukuti ndindani, koma ndi opusa kwambiri! Bwanji samanena asanakwele ndegeyo
Ndipo ndi galu kwabasi ameneyu
Ndipo olo kumuuza mwana wazaka 7 akhoza kudziwilatu kt ndi bodza ili aaa mkayidi ndiye kt chiyani
Respect
Big up Mr Wasir
Mno mu Malawi ngatimli anthu ngati awawa bwedzi dzikolathu likanakhala lachilungamo tsangakuphe mdzanga amalawi ose akuimililani bwana opepela okha ndi amene adzvotera mbuziyi
Anthu ambiri kumalawi adayaluka mitu sigwira ntchito zoona kuthiradi ndamanga pazinthu zoonekeratu kuti munthuyu akukamba zabodza Malawi ovetsa chisoni
Iwe auze amalawi zoona coz olira sasekedwa pakamwa ngat tikuziwa kt kafukufuku wawoyo saphula kanthu agalu amenewa dziko la Mulungu ili
Zikomo m'bale chilungamo chidziwike, komaso a Mbuye akhale mbaliyanu
Osaopa ,osafooka kulimba mtima basi mmakwana inuyo mulungu azikutetezerani
Mulungu akudaliseni potidziwisa
Ine phe ku capetown za Malawi ndinayiwalako
Apa sipakuyenera kuwopa chifukwa zikatero mawa zizachitikira kwayena ndiye tizivomeleza zimenez mpaka liti apha anthu asogoro lawo angat pangani zomwezo bwana anthu ali pambuyo panu, tima dikira anthu ngat inu ndipo izi zowawa kwabasi, titeteze dziko osat kuphana tokha tokha ngat ndife anthu ndife obwera zoona
No comment
Mulungu akumenenyeleni nkhondo sir
koma yaaa anthu muli ndi mtima oyipa yooo😭😭😭
Chilungamo ndichofunika ake atinyatsadi uyu presdent kupha anthu chochi fuseki
Mmmhm kuzuza mizimu yosalakwa mhm
zabodza izi umbon mwadziwa bwanji kut fuel anali ochepa osatinamiza apa ayi asilamu pajad mtopola vuto mulowetsa ndale
Izii ndiye zowona osati zomwe akunama chakwela
Timva zambiri chirungamo chidziwikepo apa akumanama kuti akufufuza Fiona apeto ake
Koma ngati zili zoona analakwa ndithu 😢😢😢
Timenyana ndi boma basi ndukanguliratu gan yanga gyz
Chilungam chiyende ngt madzi ndili kumbuyo kwako bro..... zikom pa luntha lko
Chakwera lamulo limutsate 😭😭😭😭😭🙆🙆
Imeneyo singozi ai masewera
Ambuye amulange munthu ameneyu kupha anthu 9 because of money mzimu ukutsata ndipo usowa mtendere
Vuto ndinu asilikali simufuna kugwilizana ndizimene akulira anthu chifukwa zmene zikupangidwaz mawa zizachitikira kwa asilikali ena chifukwa akamatero akusonyeza kut alibe chikondi ndi ogwira ntchito azawo