Chabwino nthawi ya DPP economy simayenda bwino koma nanga Sugar ndi Fertilizer zinali pa mtengo wanji?? Leroli munthawi yanu Sugar ndi Fertilizer zili pa bwanji??
anthu ambili akunthawa ma koma mulibe chakudya ana akuwavutisa mwina angapeze zakudya zakudya zonse zinapita ndi munthalika ndiye uyu zakudya zonse wayika nyumba yake
A aaaaa inu a chikangawa mulibe mfundo, mamina mmutu Ali thoo ooooh, makape
Amalawi Ake womwe agwilizanawo NDI akum'nyini kwakoko
Chimangacho chikugawidya kuti kkkkkk koma malawi will never change
Chabwino nthawi ya DPP economy simayenda bwino koma nanga Sugar ndi Fertilizer zinali pa mtengo wanji?? Leroli munthawi yanu Sugar ndi Fertilizer zili pa bwanji??
MAYI MWAKALAMBATU MUKULANKHULA MOBANIKA
Mcp sikungona tulo chifukwa cha DPP ndipo muziwe kuti simungamake mwachepo ndinu ana kwambiri
Mwandikumbusa adadie mulilongwe town ataima pa mzikiti eee kunali gurutu size 😢
Chikangawa party mmmmmm ulendo wanu obera amalawi ukutha chaka chino
Nkhani ya ku chikangawa siinathe mzikumbukira msaiwale
Ndachitsirudi awa dpp sikukugonetsani tulo
Ndipo mufunemusafune DPP ikuwinaso ife ndi ana adadi chakwela simuthu wabwino ayi wamupha chilima tikuona ife
Moti zoona wina lero nkumati nthawi ya DPP economy siimayenda bwino koma pano ndiye economy ikuyenda bwino eti? Mwina mbali imeneyo ikuyenda bwino koma kuno ndiye sikuli bwino.
Ngongole bwanji yachuluka, amai inu ndi chitsiru kwambiri
Mmai iwe panyini posasapo
shemed and shemed
anthu ambili akunthawa ma koma mulibe chakudya ana akuwavutisa mwina angapeze zakudya zakudya zonse zinapita ndi munthalika ndiye uyu zakudya zonse wayika nyumba yake
Tikufuna commission of enquiry osati nyasi zanu a mcp muziona 2025
Kodi nyamata okuvotela inuyo asisadikila chani kwainuyo kwacha yongogwa dayile
Kodi Kani ndi athu aja mumawatenga mmagalimoto
Mcp ndiyomwe ikulamula ndiye sikugona bwanji.DPP ndiyomwe sikugona ndi zitukuko za Chakwera.DPP mfundo nje nkhani chirima basi
Manyazi mulibe mai Mulungu akuona ndithu. Mukachoka pamenepo muzikaonetsa maliseche .
Athu okuphaa
Mbuzi za amalawi.....i hope onsewo akhuta....panya panu
Kupusa dziko mmene likuwawilamu Inu mkumayankhula choncho
Likuwawa kwa alesinu omwe mumafuna zolandira
Mcp boma ndipo yasitha dziko ndipo zozembetsa ciment zimatha chitukuko chimakhala kimwera kokha pano sakusakha
Koma amalawi muli ndi nzeru?
Zautsilu zamanyi
Jese kabwira Mai onunkha kumatako komaso mavuzi sadziwa kumeta
Palibepo chanzeru pa chakwera
Akazachoka pampando onsewo ku prison bas atitora kwambiri panyero panu anyani 😜😜
Uzavota wekha mbuz iwe uzaziwona kuwawa thaw ikazakwana 90mis pa ground
Dikirani 2025 you will be ashamed
Eweyo yako idzathana ndi ya mdzukulu wanga koma yanga adzawinira
Zopusa kungotithera bundle.tingadye musewu kapena magesi ? .pangani kale. Za omwe akudya chitedze uko
Akulu awa ndioyipa kwambili
Dziko la anthu odzindikila ochepa
Nanga njala
Zaziiii
Mudzadziwa Chaka chamawa
Inu nde mulibe mabodza
Zauchisiru basi
Pamtumbo panu anthu a mcp nonse mulibe nzeru