Imeneija inali plan ndipo anayiyambila patali, angakhale imfa ya Kasambala ija anachitaso kuphedwa, anapanga plan yopha Kasambala podziwa kuti anali Lawyer wake wa Chilima komaso anali pachimzake kuyambila kale, so anati tiphe kaye Kasambala ndipo Chilima timupangile chiwembu akamapita ku maliro a Kasambala, ndi mmene anapangila, so pakali pano sikuti iyi ndi commission of Inquiry no, apa ndikukaniza kuti ma Demostration asapangike, chifukwa zikanakhala za chilungamo sibwezi atapanga exclude aku banja komaso azipani zina za ndale.
Kuyakhula kwa chidunji inutu Mulungu adzikubisani ngati Bakili muluzi TV, ndi. COMrade NTanyiwa ,komadi Chakwera sakuyenera kuyima upulesidenti because ALLIANCE inja ndi Zomwe anangwirizana iwe tsolongo ,Ulendo uno unakakhala wa Chilima unfortunately he no longer there may his soul continue to rest in peace Atati Chakwera wavora kuti sayima ndekuti ayima ndi Manganya😅😅😅😅 Dzimvete mutolo❤
Mmene mulili mmalawi muno,panopo tilibe a opposition kutereko tiyamike anthu ngati aawa akumabwera pa social media wa ndikumalankhula zomwe sizikuenda bwino coz a opposition angokhala chete....
Anthu anachosa manthongo mmaso, 1964 inapita Ngati palibe Cha kabisila ku State House, Ndikuti kwina kungabisike china chilichonse muboma limeneli Babulo agwe basi Kaya Ali pa Swindi Basi agwe pansipa 😢😢😢
Everyone must have not accept this to happen, no enquiry should start and nobody must not accept the positions, the ball is gonna be in your court and the Malawians will tare you apart believe you me
Tikati titsatile malamulo , a Chakwera anasankha a Maiko Ussi potsata chilungamo chamgwirizano ndi Malamulo. Koma a Ussi ndi a UTM Di? Ngati sali a UTM ndiye mwaphwanya malamulo
Musatiyambitsire zinthu za chabe .you are in China and you feel you can speak your mind that's your constitutional right. Chakwera has also his own constitutional rights as well. If you have evidence come in the open rather than talking nonsense . Nkhondotu itha kukhalapo but know that no one will be spared .
Bon kalindo adanena kale kuti kupha ine kubwera Ena mafana omwe ndi a chabe kwambiri uyu ndi namanyonyolo mm bravo brother ❤❤
I love this guy 🎉🎉🎉🎉 his reasoning on the agreement is very perfect.
Commission of inquiry yanga ndi iyi kamlepo kalua,born kalindo,anamiwa,lyton mangochi,Norman chisale,Rv kambiri comrade mtanyiwa, bakili tv,Elizeyo mtalika,a njawala wakubanja kwa achilima senior kapeni munthu mmozi wa onse oferedwa comrade cliff chinyama,Timothy mtambo,Sameer Suleman
🎉🎉🎉🎉
Iwetu ndiye wasankha bwino komit imeneyo ndiyeingabwelese chilungamo chenichen
😂😂😂😂🔥
@@thomaswyson-e2q nanga apanga release commission of enquiry opanda kalikukumwe kamenekaka
True@@thomaswyson-e2q
Comrade Chinyama ndi namandwa sure ndipo akukamba zoona zokhazokha... salute ❤❤❤❤
Komatu munthu walankhula chilungamo uyu guys. Ndipotu wanena zinthu zomveka kwambiri. Ee uwunso ndi mtunda okwera ndizikhadabo simasewera. Akulankhula live mopanda mantha💪💪💪
Ndipo live imfa imene inja imandiwawa zed choipa chisata mwini
This man has an organised brain, I love this guy
150% mau awa ndioona ndithu ndipo chonde aMalawi mau awa tiwatenge serious aChakwera nthawi yawo yakhala president inatha ndithu. Mgwirizano unatha nawo aChakwera anayenela kutula pansi upresident
Ambuye akubiseni mmapiko mwake malume, cz chikangawa safuna kuzuzulidwa ngati pena pake sipakuyenda bwino, anthu oterowo akumasowesedwe
Uyu ndiye sakuopadi coz ndiza live ❤
Uyu ndiye sanyengelera akung'alura eeee
Akamangidwa palibe omusata a Malawi comwe timadziwa ndikungocemelera tili kumastand akagwa ground tonse balala nde conde tiyeni timpatse munthuyu sapoti cz akuankhula zikungamo zonkha zokha ,monga ndli kumbari yanu akulu olo mukumane ndi zofinja ndli pa mbuyo panu
Zoona
Amamgidwa chifukwa choyankhula vaai
Chakwera wabararika mix achina ntanyiwa bakili tv bon kalindo
Ndipo amagofuna atawapha kma alibe kuthekera😢
Khokhokho samala mmbale iyi ndichikangawa asakupeze bravo ❤❤❤
Zoonatu
Kachilumamo aka Koma bola asakusowese bro❤
Yeah, exactly,,.Koditu Ndi sikusinja.....
Zoonadi brother chilungamo. Osaopa osafooka osatopa. Brother Mulungu Zikutetenza we are supporting you
Cliff ndiwe superpower asee
Pano anthu atopa bas ndipo alimba mitima akungoswa chilungamo mopanda mantha 💪💪💪
A Wilson Jackson,mumutu mwanumo ,anthu akumukayikilani ngati,ulibwinobwino,zinthu zikuchita kuwonekelatu ,kapena ndikuwuzilenitu bwino kwambiri mwina mundimva,Awilson Jackson,Muli ombwambwana kwambiri,umboni ukuchita kuwonekelatu,mukufunilanji umboni wina
Born Kalindo sali yekha. Ng'alulaisation group yabwera kuzakhala.
A Chakwera chifukwa cholephera kupanga ziganizo mopanda kudalila owazungulirawa,apwetedwa pa zinthu zoti sanatengepo gawo nkomwe MOTi chimene akachita after the incident nduna zonse zokhudzidwa akanazichotseratu maudindo kuti Iwo akhale clean!
True man Chakwera kaya akuganiza bwanji? Munthu uyu wadusa pa nebukatinezala or herodi kuzimva anthu amene asankhidwa asapite ku State kukawalumbilisa kuri chimuzimo choyipa kumeneko. Amalawi mukuziwa kuti kumalawi tili ndimutumiki wa Mulungu wamoyo yasini gama chakwela ndi kabineti yake apite kwayiye akalumbire pamaso amutumikiyo ngati sanachite chiwembu akambwera ndimoyo koma ngati anachitadi aliyese muzaona chimene chizamuchitikire.palibe oposa Mulungu ngakjale akhwime bwanji kumbukirani eliya ndi ambala eliya anapambana
😮
@MeddyN🎉🎉🎉🎉dalama
Amen ambuye akudariseni achimwene
That's true Brother. But this World hate the truth
Best one ❤❤❤❤ koma chinkhumba chaona haha😅😅
Imeneija inali plan ndipo anayiyambila patali, angakhale imfa ya Kasambala ija anachitaso kuphedwa, anapanga plan yopha Kasambala podziwa kuti anali Lawyer wake wa Chilima komaso anali pachimzake kuyambila kale, so anati tiphe kaye Kasambala ndipo Chilima timupangile chiwembu akamapita ku maliro a Kasambala, ndi mmene anapangila, so pakali pano sikuti iyi ndi commission of Inquiry no, apa ndikukaniza kuti ma Demostration asapangike, chifukwa zikanakhala za chilungamo sibwezi atapanga exclude aku banja komaso azipani zina za ndale.
Kuyakhula kwa chidunji inutu Mulungu adzikubisani ngati Bakili muluzi TV, ndi. COMrade NTanyiwa ,komadi Chakwera sakuyenera kuyima upulesidenti because ALLIANCE inja ndi Zomwe anangwirizana iwe tsolongo ,Ulendo uno unakakhala wa Chilima unfortunately he no longer there may his soul continue to rest in peace Atati Chakwera wavora kuti sayima ndekuti ayima ndi Manganya😅😅😅😅 Dzimvete mutolo❤
Kuyankhula mwa chilungamo our brother❤❤❤
Maliro aja munapita nawo ku Parliament ndiye Pano akalumbile ku Parliament.
Mwana wa chikangawa
Respect bro kuyankhula chilungamo
Zovuta....koma olo atatani izi zidzaululika....zizezakhala poyera koma a MCP ayasetsa kuphimba chilungamo koma awawa alephera.....A Malawi siopusa ayi ndipo timaona
All the way from former capital city of Malawi
Achakwela kodi ndimunthu ,oganiza bwanji? Kodi adaphuziladi awa? Kapena anangophuzila chizungu kunja?
Mau koma amenewo 🎉
Mdala ameneyu wasavuka, akufunanso adyenso secretary general, Dzuwa likuswa mtengo Kaliati.
I love the courage boss bg up🎉🎉
Apa ndiye wabaya ndipo panalibenso chokhazikitsira inquiry.
Mmene mulili mmalawi muno,panopo tilibe a opposition kutereko tiyamike anthu ngati aawa akumabwera pa social media wa ndikumalankhula zomwe sizikuenda bwino coz a opposition angokhala chete....
Inu amenewo mwamasukatu
Ichi ndiye chilungamo chake👏💪
Commission of enquiry imakalumbira Ku Parliament osati Ku Nyumba ya munthu ayi
Chilungamo ndi chimenecho palibeso chilungamo choose apapa, amalawi ambili amaopa kumasula chichewa ngati ichichi ,palibeso kukamba nkhani chilungamo ndiichi malawi akudziwa koma matha kumasula kunena chilungamo
Kwambili aa akuona ngat ife sitiziwa ngat ? Asatiphimbe kumaso
Mbava, yakuba u leader, asiye akalape koma zinazo ndiye mmmm Mulungu zangamve, kupha.
Zoonadi Brother zikumveka
Wise man, may you be protected by the blood of Jesus anthu olimba mtima ngati inu ndiwochepa
Help Malawi God 🇲🇼 🙏 Rise people are anxious to see the truth of the plane crash
It's still paining to those that have humanity feelings eeeeeishhhh
Akulu inu mukunena chilungamo ndipo zoona Chakwera ayenela kuimitsidwa ndithu. Chilungamo chioneke mapepala atulutsidwe ndithu. Asakhale pa balot
Yes Uli boooo tonse inatha palibenso chifukwa copitilizila kulamula
Ameneyu ndiye anayenela asatenge gawo posankha anthu.
Awison Jackson,musamayankhule ngati mwina ,inu mukuziwapo kanthu pa Imfa ya Chilima
Anthu anachosa manthongo mmaso,
1964 inapita
Ngati palibe Cha kabisila ku State House,
Ndikuti kwina kungabisike china chilichonse muboma limeneli
Babulo agwe basi
Kaya Ali pa Swindi
Basi agwe pansipa
😢😢😢
Koma ndichofukwa chiyani boma rikumanga anthu oyakhura nzakukhosi?
Bwanji osamanga anthu amene akupha anzawo bwaji.pamenepa dziko ramarawi kuribe purenzident.
Anthu opanda mantha ngat awa ndi onwe akufunika mdziku mwanthu muno😢
Nanga iwe
Izo ndiye ndizoona ndithu
Chilima adapita chifukwa chidali chiphinjo kwa chakwera chifukwa cha mngwirizano
Eya Anthu onse asa vote.kufikira chakwera wachotsedwa pampando.waupulezident chifukwa chakwera anapha chilima.ndipo zisankho.zilephereke basi ..chakwera achoke basi malawi adzasankha pakalhala pulezident wina wosankhidwa bwino.amen
Ada inuyo ulemu wanu anthu amalankhula koma inuyo palibeso ndi 1 keep it up more fire God is in control ndnu otetezedwa
Anthu sakuopa Pano..chilungamo ndi chowawa
Eeee nkhani iyii man mwang'alura ngamo kwambri i❤ this one
Zoona zake zimenezo mofaya
Kodi Ndichifukwa chiyani Achakwela,pankhani ya kafukufuku,akuyikapo ,cholesa.
Everyone must have not accept this to happen, no enquiry should start and nobody must not accept the positions, the ball is gonna be in your court and the Malawians will tare you apart believe you me
Kodi Mr. Cliff Chinyama unali kuti nthawi yonseyi a Malawi tikufuna munthi wa mphamvu ngati zimenezi? Eish! Ukubaya penipeni osati masewela ayi. Ukukwana brother.
❤❤❤❤❤clif chinyama ndpo ndi zona athu ndi oipa
Big bro the truth is good ❤😂😂🎉
wakufa sakuziwika oroso iwowo ankhoza kufa achakwerawo ndipo ife amarawi atitora ngati ife ndife zisiru koma akunama murungu ariko kumwamba uku ayankha
Inu nde mwaloza point nde nde nde mchomwe anaphela nde azisankha anthu amu enquiries ayi sisatheke asankha achipani chake kuti abise chilungamo
Tikati titsatile malamulo , a Chakwera anasankha a Maiko Ussi potsata chilungamo chamgwirizano ndi Malamulo. Koma a Ussi ndi a UTM Di? Ngati sali a UTM ndiye mwaphwanya malamulo
Very good ndiye posunga malamuro pompo amulore MANGANYA aimiletu 2025 ngati president WA tonse alliance
Mau away chikangawa ndi gure
Kunali kusewelesa amalawi kumeneko tizingokhalila kuvota?
Brother ❤🙏💪🇲🇼
Awilson Jackson Kodi simudamve zoti Ndege yachilima idachita kucheledwa?simudamveso zoti vice adachosedwa lamba ndisapatonso zidachoka?ngakhale ,jombo za Asilikali adachosa ,simudamve izizi inuyo,Awilson jackson ,simukuona nokha,kuti President,sakukondwela ,ndikafukufuku wangozi ya Achilima?
Kodi awilson Jackson,zonse zimene zikuchitika muno mumalawi,inu ndinu achilendo kapena tiziti ,mwamwa kadansana?
Muuzeni muuzeni anapha yekha anthu omwe wawasankha wawalowesera kale ndalama.
Bola akanva chakwela asakuphe chifukwatu BOMA ili limadana ndichilungamo
😢kafukufuku yese mwini wake akhale kamangila ndi asembe akatolika komaso brather wa saulosi ndi mwana wake baai ena oseo ndi boza
Munthu wankulu inuyo ndi azanu onse Antanyiwa, Bakili TV, the DC, bro sallo, Lyton mangochi ulemu wanu nonse
Kung'alura chilungamo chilungamo sichiwopsa ndipo chiziyenda ngati mtsinje Satanayo ndiwaboza ndipo kwake ndikupha ndikupha amen mpingo. Ambuye akutetezeni pamene mukuyakhula chilungamo
Tiye nazo muzasangarara masiku akubwwra
Anthu aku Malawi paokha saganiza amafuna kuti anthu ena waganizire. Ku nyumba ya president kumakhalanso office yake inu za mboma simukuzidziwa khalani chete chifukwa Bon Kalindo wanena male olumbiritsa ndiye aliyense osaganiza bwino angonena zomwezo.Baba mukanali mumadziwa malamulo adziko simukananenazi chifukwa inuyo muziauza anthu kuti mgwirizano siuli mmalamulo adziko ndiye popanga mgwirizano tichenjere ngakhale Chihana pamene akupita ku DPP akudziwa kuti chirichonse chikhoza kuchitika.
Eya kwambili chakwela ndi yemwe anapha chilima zopusa zanji zomwe qkuchita akuwona ngati sitimuiwa
Good boy ❤
Plan yawo yomupha Chilima inali yozama,ndichifukwa anayamba kupha Kasambala ndi cholinga choti afafanize umboni wazina ndi zina poti anali Lawyer wake ndiyenso amene amatha kudziwa zambiri even zokhudza Alliance yazipani zawo, so ndichifukwa chake pakalipano zinthi zikuoneka ngati pakusowa poyambira pofuna kupanga kafukufuku kunkhani yokhudza alliance yawo
Uganiza kwa booh zoona izi rest in peace legend of politics in malawi SKS
Sindinayambe ndamva chilungamo ngati chimene ndamva lero. Zukhala ngati zumveka ndithu.
Musatiyambitsire zinthu za chabe .you are in China and you feel you can speak your mind that's your constitutional right. Chakwera has also his own constitutional rights as well. If you have evidence come in the open rather than talking nonsense . Nkhondotu itha kukhalapo but know that no one will be spared .
Kugaza brother man
Ndipo ndiye ndizoonadi chilungamo chake ndichimenechi
Changanga wayowadyela
More fire
Ulemu wanu big man 🫡🫡🫡 iwe ndkatundu wenwen
Born kalindo watumat uyu kuti kaishoshe kuti tiiyambise yamanja ,nkuona choncho, sangalimbe mtima padera muona zowopsa Malawi ndipo a police azafa ochulula chifukwa mfut kuzaomba simuzatuluka chipolopolo muzatuluka utsi ndipo anthu azapha apolice ndimiyala komaso mikondo samalan amcp !!!
Nafe tudabwa kodi achakwela amalingalila bwanji pamodzi ndi mbava zinzao??? Malawi tagona kwambiri ndiye Kuti eeti?? Ma demo ankapanga kale aja anapanga nthawi yolakwika amafunikila panopa Koma dzuoneka ngati Kuti tuopa tonse tungolankhula pakamwa basi
Koma uyu😂 walimbadi mtima sakumuopa jezbell
Okha Mr chikangawa, okhanso ndikhesa mwazi
amalawi enanu ndinu omvetsa chisoni kwabc...zikuonetseratu kt cimene muli simukuchidziwa,may god help you
Iwe manyi ako mapwala ako kulankhula mokunya anthu onsewa opusa komaiweyo ndiwe galu kwabasi
Uyu nde bakili muluzi akunama uyu akuonetsa nkhope
Zimene. Zikudabwitsa ayika commission of equerely koma. Osanena ku mtundu was a malawiyangoikidwa. Mokakamizidwa
That's true bro
I love you brother ng'alula osaopa osatopa
Chilungamo osaopa brother 🔥🔥🔥🔥🇲🇼❤️
Exactly big man