Ndinkangoti ngati muthu Ali Dr amakhala wanzeru koma awa u Dr wao ndi opanda mawo nzeru,apa bola osaphunzilafe mwina tikhoza kubwera ndi ma facts, alibe so manyazi, DPP fertilizer 20 MCP 107, fuel DPP 850 MCP 2750 ,dpp sugar 750 MCP 2500,chimanga 20,000 MCP 50000+, ngati alipo otsutsa anditsutse
@@beinhardkausiwa7107 dpp chinavuta ndi chiyani kukoza njajeyo or doko la msanje lidakukanikani kod simuyamika kungova kt ndinu otsutsa ndiye zilizonse
Fertiliser siwondula brain iwe alimi tikugulitsa 2bags ya chimanga kugula thumba la fertiliser koma 2020 timagula 21000 koma timagulitsa chimanga matumba 7 panopa kwa alimi fertilizer siondula
Brain boma agwesa yekha 😂😂😂😂😂😂 proud to Brian
Aziyakha fuso amaneo osamagoti Dpp
I think Brian banda is a blessing to malawi
Kma uyu akunama Dpp ikubwelera m'boma ndipo ulira sunati ife olo titavota lero Dpp ikhoza kuwina ndi 89 % osalawo mutha kugawana
Kudzivuta ndi mtima uku... DPP ikubwera ndithu m'bomamo😂😂😂
Sakuyakha ma fuso uyo
Tidzawonani pa mavoti
Nose a MCP machende anu😢😢
Achimwene Mudziwopa MULUNGU
Amakanika kuyankha mafuso awa 😂😂😂 kumangodziluma
Sangaloze zomwe current government yapanga..Chixungu chimaonesa ngati munthu akunena za mzeru..Garbage...
Tiwawonera amenewo akungwa chagada😂😂😂😂 njanjiyotu ndiyamozambique asatisokose ameneyo
Padziko lonss lapansi chsru choyamba kapen chidebe chophikira makata kusimba ndye ichi osamaiwal chitukuko cha 16tillion ijatu muitchule njanji ndye siyan Joyce Banda anatiuza kale
Alimi tasitha chifukwa cha chakwera fodya akugula chimanga tikugulitsa mitengo ya bwino
Kd angokamba za DPP bwanji ayankhe ameneyo nkhan ndiyokut akuba misonkho yathu ife Malawi
Zomwe mwapanga a mcp ndikubweresa njala komaso kugwesa kwacha zomwe anthu sazakuiwalani
Kunama kopanda Nako manyazi ineyo ngwa ku nsanje komweko koma zomwe akuyamkha akuluwa nzabodza zokhazokha
Iweyo udamwa nawo ndopa za anthu Aja mudaphera kuchikangawa
Taziyakhani mafuso bwanawe njanji ndi yamozabque.
Doctor kukanika kuyankha funso... Mediocre
Awa ndi achitsiru bwnj 4yrs azitiwuza zanjanji
Amariza bwanji njanji ndarama atagawana mkudya
Uyu ndising'anga akuoneka makani 😂
Uyu machende ake
Achisilu awa
Achisilu awa
Kkkkk DPP my vote
Koma Ka background sound always do touch my soul! Who did that sound
YT LIBRARY
Ndinkangoti ngati muthu Ali Dr amakhala wanzeru koma awa u Dr wao ndi opanda mawo nzeru,apa bola osaphunzilafe mwina tikhoza kubwera ndi ma facts, alibe so manyazi, DPP fertilizer 20 MCP 107, fuel DPP 850 MCP 2750 ,dpp sugar 750 MCP 2500,chimanga 20,000 MCP 50000+, ngati alipo otsutsa anditsutse
Kodi mbulutu ameneyi ndiye UTImuzitibwelesela athu oti atithandiza osati zozizila akukambazi mbava ndi chikangawa wakeyo
Iwe ukuzitcha doctor ndi zako chikangawa ndinu dzisilu,mbuzi ya munthu MCP palibe chomwe akuchita zisilu za anthu DPP 2025 boma ovota ndife tiona
Km akuthawamafuso bwanji ngat akut dziko akuliendetsa bwino muwudzen ayankhe nkhan ya fetelezayo asathawe
Iwe kayuni ndi fisi wamva mmene zikuvutila ukafanizile ndi nthawi ya DPP kma umaganiza
Anthu sitidya njanji komanso ntchito zikusowa komanso zinthu zinakwera kwambiri ndiye umoyo wa anthu ukuyenda bwino bwanji
Munthuyu ndi opanda nzeru chakwera walephereratu iyeyo akuziwa zimenezo ndipo an thu ndi okwiya akuvutika koopsa anthu sadya njanje
Kod njanji yake yaku Mozambique akunyadilayo ????
Ambuye mulungu tikupepha kuti mutichosera mcp mu boma, satanic awa chonde chonde achoke
Osatenga anthu oti mutu ndiwozungulira amawona ngati ndiwochenjera kupusisa amalawi ayiwala kuti akuzipusisa okha koma Mulungu akuona
Osayakhula mwamwatama mcp si chipani chafuko fuko lake liti. Ndipo ndikunenesa kupanda chilima ndi zipani zina mcp abwezi simunalowe muboma. Mcp yazaza ndimbuli magesi akuzimazima kunu ku mzuzu akulamula ndindani Brian banda uziona anthu owaika pa times chimene ukulankhula nacho chili ngati sikizi. Ngati dpp mavoti anakubwera inu akambwe bwanji chisankho chachiwili munabwera mugwirizano ndi zipani zina.umbuli tikunena kuti ku mcp kuli ziwanthu zoti mumuto muli ambuye tengeni. Ngati dpp inakuberani kachiwili aliyese akanayima payenkha ndipamene tikanaziwa kuti ddp inakuberani koma zipani 9 zimene munabwera nazo muchisankho chachiwiri pano munene mopumbwa mcp yinawina ndizoona kuti munthu wopanda zeru saziwa chimene chamufikisa pamene ali. Shame mcp muziweni Mulungu osanena mochachalika motumbwa mwamatama
Kunena zoona palibe kusiyana mcp ndi DPP onse ndimbava anthu awa ndiamozi
Brian mumatha akukanika kuyanga galu ameneyo angamuvotere ndani mbuzi yamuthu chakwera ndindani
Akulu muli mpingo wanji koma mmapemphela inu kunama olo mwana wa zaka zitatu akhoza kukugwilani bodza lanulo mukunama kuti chichokeleni kamuzu njanje kunalibe Iyaaaaaaa ndinu abodza kwambiri ndipo DPP ndi boma lomwe anthu mukuyidayo ndiye boma lomwe china chilichonse chidali chotchipa koma inu ndi umbava wanuwu komanso kuyipa mtima muli nakoko kosaganizila anthu amdziko mmmmmmmm chokanipo tatopa nanu mwamva muuzane
Koma abale tikuziwa kuti ana anu akusangalala muziyankhulako zoopa mulungu plz plz ulendo wanjanji ife tizipita nazo kutiko
Ndimaganiza kuti Dr amakara ndi nzeru koma pano zadziwika kuti ndi opsa
Brian doctor uyu akusepa mafuso😂😂😂😂 dpp 2025 boma
Aaasaa athu awa ndi about ndithu njaji ku Malawi kulibe
Aaaaaaa akukanika kukuyakhani mafuso ndi mbuli ya muthu sitidya jaji
Mwamuna wadzeru sabrama mwamuna wakare mukaone oterewa dziwani banja lamumvuta basi
Inu. M. C. P kwanu nkunama basi tidzakutchotsani m boma inu dzitsilu inu
Chabwino njanji ikugwila vepi koma zasintha moyo motani?
Mumuziwe yesu ndi ophunzira ake 12.
A mcp akudzikwata ndi chala ndipo akulu awawa akungoyankha za mmutu mwao
Njanji yake iti zoba ameneyu a Malawi angadye njanji chitsiru ichi
Munthu uyu wadya ndalama za mcp kuti alankhule za mcp
Kkkkkkkk. Ndiye ma indicators kuti zinthu zikuyenda bwino ndi ati?
Kodi amenewa amadziwa zimene akuyankha kapena akungoyayankha kuti akome kwa mabwana awo ?
Scandal after scandal...By the way which indicators , coz when we talk of inflation nde eeeeeehhh zosakambika
Galu uyu kwabasi machende ake pati...
Dpp itenga boma chikwangwan ndizinkhale ng'oma
Mcp simungawinenso😅😂 mukuziwanso ap
Akuluwa atichimwisapo apa bola ndisunde kaye aaaaaa
Anthu akuba awa akuzinamiza kuti awinaso kkkk koma MCP kkk umbava wakeo
Zoona Brian waona kuti udokitara wa uyu kulibepo
So angokamba za Dpp why malo moyankha mafutso? 🤔
We don't need information,we need delivery shupit
Khani ndi pa ground not on papers such as,he talks about minister of transport,what is that?
Iwe chimutu chako mcp yakoyo fwetseke
Ameyo ndiopusa kwambiri
Sukulu munachita Koma mulibe nzelu
Maboza basi tatopa ndizaboza a mcp azaona 2025
Vuto nd ndalama chitsiru ameneyu
Koma ma doctor aku mcp abale 😂😂😂😂😂
Uyu si Dr ndi mbuli yachabe
Ndipo dpp sindiyifunaso kuva
Uyu ndi mbuzi ya chitsilu
Akulu yankhani funso straight
Pamtumbo pako galu
AAA MCP ndi DPP bola DPP. Aaa
Uyo ndiwamisara
Abwana muli ndi wabodza
Anthuwa ndi oyipa awa
Yankhani chilungamo
Dpp 2025 boma
Awa ndiwupenga
Alibefundo
Achisiru awa
Chizilu inu
Jaji yake it?
Awa amatha mr brian
Kkk
😊
4 kilometer ya njanji koma mmisonkhano ya mcp nkhani ndiya njanji njanji njanji eeeeee mcp muzichita manyaziii
@@beinhardkausiwa7107 dpp chinavuta ndi chiyani kukoza njajeyo or doko la msanje lidakukanikani kod simuyamika kungova kt ndinu otsutsa ndiye zilizonse
@@kingsleyhopematchaya5184 tiyamikre 4 kilometers are u serious??
@@beinhardkausiwa7107 nanga dpp inapangako or 1km kod pa zaka 15
Fertiliser siwondula brain iwe alimi tikugulitsa 2bags ya chimanga kugula thumba la fertiliser koma 2020 timagula 21000 koma timagulitsa chimanga matumba 7 panopa kwa alimi fertilizer siondula
@@kingsleyhopematchaya5184 koma iwe udapita ku school? Chimanga ndi feteleza choyenera kudula ndi chani? Wekha ukuti umagulitsa matumba 7 chimanga kuti ugule feteleza, pano matumba awiri achimanga kugula fetereza
@@AndersonChinkwapulo ndipamene alimife tikusamgalala koma alesinu ndiye zikuvutani chifukwa mulibe chogulitsa kukwera kwa chimanga kwapangitsa kt tisaone kudula kwa fertilizer iweyo panga masamu
@kingsleyhopematchaya5184 iwe uli ndichimanga chongogulitsa nkugula feteleza osati mudziko muli chakudya chokwanila kuti anthu adzidya, komanso usayiwala ulimi umachokera patali, kuti ufike poyamba kumagulitsa chimanga ndiye nthawiyo udathila feteleza otchipa nkukolola chimanga chochuluka , pano ukufuna uwoneke dolo?