Grace chinga was a true servant of the Lord and a prophetess. Whatever she prophesied many years ago it has come to pass. May God destroy the wicked rulers I hate chakwera and bushiri big time
Kalata iyi I atuluka ndikale Grace atangotisiya kumene ndithu izi ndi Zoonadi kwamene simunamve nthawi imeneyo zinangokudusani koma kunena moopa mulungu kalata inatuluka chaka chomwe chinatisiya Grace the same wk
Ndimunthu yenkhayo odzazidwa ndizimu wadziwandi yemwe agayime ndikunena kuti kalata iyi sikuphelezela pazose zomwe zikuchitika ndinthu ndiyenkhayo nayeso akusowekela mamasulidwe nkunthekaso nayeso Ali mugulu limeneli ndamene agabwele ndikutsutsa chifukwa izi zikuchitikazi diso nkhuti lilirose lakuuzimu wamulungu likuwona komaso likuva tiyeni amalawi koooooose muli tipephele kwa mulungu kumwamba achitile atimenyele nkhondoyi
Vuto amalawi ife ndiokanika.kungotipatsa Gayiwa 50 kg basi .bushir bushir .kumuchemerera
Mutumizeni bushiri ku south africa azikayankha milandu yake mwina tipumeko kuona imfa zaabale athu iiii ntundu wamalawi ukutha kaziko kake komweka kamanjaka koma zochitika pwilikiti mmmm tisalekelele izi amalawi titha ndithu
Ziko la malawi mulungu amalikonda koma ife ena ambilife sitilikonda chifukwa chadyera tikukakamirabe anthu omwe akulitha ziko lathu pamodzi ndiife tomwe tikuona ndikumati sazachoka pampando amalawi olimba tiyeni tipemphere chikhululuko kwa mulungu kuti alowelerepo chifukwa anthu ena adakalibe ndi khungu ndichifukwa akuti chakwera yemweyo
Lelo chipani chake ndichimenechi cha chakwela chamwanzi mix bushiri mulungu achite nanu mukumphetsa anthu osalakwa
Grace chinga was a true servant of the Lord and a prophetess. Whatever she prophesied many years ago it has come to pass. May God destroy the wicked rulers I hate chakwera and bushiri big time
Chili chose chomwe chinanenedwa umu chikuchitika chabe anthufe kumvetsetsa zimatimvuta
Grace chinga mzimu wanu uziusa mumtendere lelo ndiizi chakwera ndinzake bushil akungopha anthu ngat nkhuku zimenezi ofunika mumtumizile azinvere ekha bushil 😢😢
Amene akuti sakukhulupilirayo ndi mwana wake wachikagawa
Ulosi ukukwanilisidwa magazi daily akukhesedwa kuchoka pakhomo nkubwelelanso wamoyo ndi chisomo
eee sukunama ase ukamachoka khawa biiii kut ndikafika kma ulendowu
May heavenly father remain my lawyer...eish chonena chagwera mkati.
Vuto la anthufe ndi kusakhulupilira.
Grace chinga sadaname
Joyce Banda milomo ngati odya nyama za kuufiti
Let's pray for our nation Malawi God will answer our prayers
Amen ukukayikilawe abambo ako ndi chakwera mfiti yokutha ntchito mutu wako dziko mmene likuyendelamu ungamanene zimenezo umbuli eti ukumvera kukamwa kapena
Ndizoona ananena kale grace chinga
I pray that Malawi be safe against evil plans
Rero ndiizi zikuchitikati
Mau ako aphelezera grace...lero zikuchitikadi kuyambila pa june mpaka pano magazi okhaokha Amalawi muno
Ndipo live thaw yake nd yomwei chakwera wakwanilisa😮
Chipani chake ndichimenechi tilimochi abale ngozi kumalawi chonchi mmmm why god😢😢😢😢 ambuye tilanditsen ife ana anu tathodwa tasowa nzeru
Wow khani wozwizwista MHSRIP,ambuye mulungu azititeteza ameeen
Everything happen so fast but we can connect grace was a gift from God...when dpp loose 2019
Zililokutu ndipo za malodza 😎🇲🇼
Malawi
Kalata iyiyi eeeeish
Ndizoona
Nditangonva dzina la bushir ndi skeffa chimoto ndayamba kukukhulupililan
Sopano akulankhurai ninda😮
Ndizowonadi zikuchitika ndithu
Izi ndizoona zokhazokha mulungu landitsani dziko la Malawi kudzanja la woyipayo
Malawi flash back
Joyce Banda ndi Bushiri akukunamizirani ngati
Amen
Ulosi wakwanilitsidwa
Koma mulungu atithandiza ndithu dziko lathu
malawi wafikapo iiiish
Zooonadi
Mulungu salakwitsa kalikose apanga jira ina
Mzimu wako uuse muntendere ndipo uzitimenyera nkhondo anafe kuti nafe tizalowe mu umfumu wakumwamba
Esh skefa wandikhumudwitsa kan zoonad 😢😢😢
Ndipo Inu aaaaaa
Apadi ndiye zayamba kuoneka ndi maso
Zoona zake
Ndizaulula
Koma guys moyo ukuwawa
Pope vs malawi
Mulungu atipatse maso auzimu
Agiling'ande yalakwatu pamenepo basi kkkkkkk
Zikukwanilisika sopano
😂😂😂😂😮
Ndukayikira ngati zili zoonaa
Ndizoona kalatayi tinaimvera grace chinga alimoyo bwana and ananena zambili anantchula Maina ambili Koma athu ena amatha anaidula kalatayi
@@LamieTiger ya full ilikutiko tiyimvere nafeso
Kalata iyi I atuluka ndikale Grace atangotisiya kumene ndithu izi ndi Zoonadi kwamene simunamve nthawi imeneyo zinangokudusani koma kunena moopa mulungu kalata inatuluka chaka chomwe chinatisiya Grace the same wk
Mmene ndinayumvera ine inalekezera pomwepo chifukwa owerengayo anauzidwa kuti asiye koma imapitilira ndithu komabe nthawi imeneyo inalekezera pomwepo
Ananena kale izi grace chinga
Zoonad
Ndizoona