Mai chilima abwelepoyala ndikudziwitsa ntudu wa amalawi KT atsogolera chipani cha UTM ndinjila yokhayo tingazadziwe chilungamo cheni cheni chatsogolo la chipanichi km chonchi ai sizoona nkhope ya biyeni izasowa pansalu paja God bless you Mai Chilima
Bwana DC ulemu wanu ndipo ndimakunyadilani mukung"alula kwanu koma ya Mai Chilimayi Mmmm, ndakaika. Tisawakakamize ku Ndale isali mbali yao komanso akulirabe, amantha ndipo patenga nthawi kuti mtima wao ukhale pansi. Mwina asintha maganizo uthenga wanuwu akauganizira bwino...
Chilima MHS continue.. To RIP opposes the idea of family succession politics he wanted change. Kalindo is of the view of old politics. I second the idea of Chilima that chipanichi ndachanu a Malawi sizakunyumba kwanga. The genius new that he will not be there forever.
The DC, this is what exactly happening in Malawi😢 I v Come from MHG and kwathu ku Liwonde kumakhala ngati ku Mangalande ife eni dziko kumayenda ndi mantha but our leaders 😢😢💔
Zoona amalawi tikanazuka tose kuchosa pule ndinduna zake . Akanakhala maiko ena bwezi nduna za Chakwera ndi iyeyo atathamangwisidwa kale. Ifa ya ngozi ilipo koma wosati ya anthu 9 yoyesa kukoza ndichifukwa akupereka statement zosiyana Mulungu wamoyo akuwaseka kumaso
Musiye Mary azilira mamuna wake wafa imfa yowawa chifukwa cha ndale ndiye iyenso apita pa mpando wa upresedent aaaaaaa Bon pena umayankhula zoduka mutu
Ndipo ndizoonadi Mary Chiloma ndipo atha kulamulira dziko la Malawi mosayang'anila Mtundu wamunthu Amalawi let's vote Mary Chilima kukhala President wa dziko LATHU
Kalindo akuyankhula zoona koma vuto zipanizo zikatengera kuphya mtima ndicholinga achotse MCP pa mpando nde ndi izi tikuzunzika lerozi adapangira kuphya mtima a tonse including himself anali gulu limodzi kumamunena mutharika kuti osanva
Bon kalindo ukutanthauza chani za kuti Legacy ya Skc ndi kubanja angayikwanitse mu chipani cha UTM,,,,, ? Sitikufuna ndale zodalira kubanja komwe kunali President wa Chipani,,,Mary can support the party osati kukhala President as now ,,,,This is not Family Party,,,Maganizo opusa amenewo
Ndimakuvera zoyakhula zako koma izi zomati mary chilima utm wadeya ndipo utm ndi chipani cha amalawi osati chakubanja. Akafuna akubanja abwele athandize utm not tisakhe wakybanja ayi. Mzeru zimafuna anthu a mzeru. Utm ndi ya malawi zipani za ku banja zilipo
Ayi inu a winiko .mmayesa inuyo munali limodzi ndi skc. Bwanji inuyo osaimirira kukhala pulezidentyo? Koma mzimayi yu ayi.mukufuna kuti adzaphedwe moopsya ngati mamunake? Mmene wafers mamuna wake.ndi andale ena a mcp? Musatero a baba
Mmmm ndipovuta kut angakhale akupitiliza, i hope atha kukhala ndimantha pazomwe zinamuchitikira mwamuna wakee
Mai chilima abwelepoyala ndikudziwitsa ntudu wa amalawi KT atsogolera chipani cha UTM ndinjila yokhayo tingazadziwe chilungamo cheni cheni chatsogolo la chipanichi km chonchi ai sizoona nkhope ya biyeni izasowa pansalu paja God bless you Mai Chilima
Exctry good idea
I support this idea....Mary chilima the game changer.
Bwana DC ulemu wanu ndipo ndimakunyadilani mukung"alula kwanu koma ya Mai Chilimayi Mmmm, ndakaika. Tisawakakamize ku Ndale isali mbali yao komanso akulirabe, amantha ndipo patenga nthawi kuti mtima wao ukhale pansi. Mwina asintha maganizo uthenga wanuwu akauganizira bwino...
The DC mwana ooooooophya kwambiriiiiiiiiiiiii ✊✊
I love you bon kalindo kuyankhula ndiye waesesa koma vuto ndiife amalawi
We love you DC,,ur really enlightening us
I support this advice
Ndili mbali Yako Bonie ( my young brother) ukuyakhuladi zoona cz mery ndamene akhonza kunyamula UTM pamwamba kwambili
Ngati muli wowona kuti chilima anaphedwa simungayankhulenso zoti Mary akhale president umenewo ndiwusatana,
Km kuyima kwa mery pa chipani kunthaso kuthandiza kuti okuphawo alandile chilango mosanvuta cz akankhala kunja kwachipani sangayakhule molimba ntima adaniwo antha kumupeza mosanvuta pamene akankhala nkati ankhala otetezeka kwambili
Kodiinuo mutaphedwa panyumba panu akazanu asiye nyumbayo kuthawa kuyikana kusiyila anthuwena atenge nyumba chifukwa choti mwafela amunawake
The DC booooon kalindooooooo mwana owopsyaaa kwambiri inenso ndikugwirizana ndi fundo yoti marry chilima is deal to stand for president
The DC Bon Kalindo km umatha okumva wamva osamva akhare choncho
Chilima MHS continue.. To RIP opposes the idea of family succession politics he wanted change. Kalindo is of the view of old politics. I second the idea of Chilima that chipanichi ndachanu a Malawi sizakunyumba kwanga. The genius new that he will not be there forever.
Mr DC mfundo ya lero mokupemphani muike mu English and muiponye pa BBC NEWS kapena pa WORLD NEWS Kuti ma doners adziwe zimenezi za chipatalazi
Ine ku queen Elizabet ndilibe nako mau
Pa 4 April mwana wanga ampanga oparation
Nditalipila 100 pin
Chipatala chaulele chija mhhhh kobelekatu,
Amati kulibeko siza akufuna akagule mhhhh
The Dc mwana woopsa kwambiri
I agree with you DC Kalindo. Honestly this guy is wise 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Wandisokosera mauling utamva, chilungami ndie ndichimenecho😊
I agreed this statement mary nde deal koma sitikudziwa kuti mary angavomele
Chakwera watikwana kwambiri ndipo watitoradi ife amalawi.Mayi Chilima akuyeneradi kukhala mtsogoleri wa UTM.Lazaroyu popanda SKC anali yani.Kanyimbi amene akutizunza ifeyu munthu opanda chisoni kumupha mnzake yemwe anamuika pampando. Ambuye kumwambako tikanthireni Lazaroyu.
❤❤❤❤❤❤ Inu chilungamo simubitsa tiyamike kwambili boooon kalindo the DC president wathu
mary -Chilima is the Right candidate for UTM
100% and ndiozindikira
As member?
Never... is that not same for the Muluzi's and Muthalika's?
Amai Chilima tipulumutseni tikudikira Inu mama bwerani mutiyankhule
Mcp ikutuluka mbola basi afune asafune
Mcp ndi yakhaza yokupha ndiye pano malawi 🇲🇼 yaziwa za chipani cha mcp
Ndalama zingothera maulendo opusa basi ndiye namachende kunkuyu azibwera azitiyakhura zopepera, a Malawi anatiloza ife kaya ndi ndani? Anthu awa samayenera kubwelera boma mcp sichipani.
Ngat Panadol ku kamuzu central kulibe ndiye kumudzi akapezeke
The DC bon kalindo 🎉
The DC, this is what exactly happening in Malawi😢 I v
Come from MHG and kwathu ku Liwonde kumakhala ngati ku Mangalande ife eni dziko kumayenda ndi mantha but our leaders 😢😢💔
Ndipo live marry yemweyo pliz.
Ndizowona wamisala anawona khondo HT DC🎉
Zomvetsa chisoni kwambiri, chakwera ndi anzake awononga dziko ndithu
Mary Chilima is the right Candidate ✅️,
The DC is always right ✅️
DC akunena zoona, a mary chilima tili pambuyo panu
Chilungamo ndithu koma chopweteka 😍😍
Mery mukasakha kukhala president nde akwatiwasotu nanga ore amakhala butcher kkkk❤❤❤
😮t
Kumene Mary Chilima nde joker, azinzake a SKC ofuna kudyadi zamasiye pano ayamba kuonekera poyera plus mma TV umu kufuna kuzigulira malo mxiiim
The DC ng'alula basi,mbambande
Zoona amalawi tikanazuka tose kuchosa pule ndinduna zake . Akanakhala maiko ena bwezi nduna za Chakwera ndi iyeyo atathamangwisidwa kale. Ifa ya ngozi ilipo koma wosati ya anthu 9 yoyesa kukoza ndichifukwa akupereka statement zosiyana Mulungu wamoyo akuwaseka kumaso
Mary Chilima ndiokwana, chifukekwa alindikuthekera.
Chilungamo our president boooorn kalindo 🔥🔥
Mary emweyoo🎉🎉🎉
Iiiiii Mary Chilima kungoti ayima aaaaa basi akanyimbiwa zawo zizadelathu
Uremuwanu the DC ❤❤❤👍🤝
Ndipo zoonadi I like it Mary yemweyo
I totally agree with you the DC . Mary can absolutely make it .
Bakili-Atupele. Bingu-APM. SkC- Mary...zakubanja ?
Chakufwa-Enock
Marry Chilima is key indeed
Ndizowona my chilima atenge uprasednt
Ndifedi opepela the DC sukunama
Ine ndimaona ngati asakhale koma kuli achinyamata enawa nda amene atasankhepo ngati tufuma UTM isathe merry ayi achikulire maso Ali pa iye nde mmm ayi
The Truth bravo
Dc amatuma...Kma zoonadi ADC
The DC mwayamba kukocha zipani?kkkkk
Iwe ndi machine
Chilungamo ndimwano
DC umakwana 🔥🔥💪 💪
Bwana DC. Tikupepha kut. Mwezi uno usanthe. tamuchotsani ameneyu chikangawa yu. Komwe wapita iyeko akawone kofikila pls mabugwe lowelelanipo umboni ndiwokwanila pls
Really the daddcccc
Mary sangakhare president coz zitha kumukakami kt akwatire coz president sakhala butchara
Sankhala mbeta ,musaiwale kuti mery ndi nkanzi 😂😂😂😂
Ndakunyadila kkkk
Chikomeni registered though amatenga amayi ake kapena abambo ake . Chikomeni anatenga amayi ake.
Nkhani ya Mary ndi yowona coz ndi amene Ali oyenera kusogolera UTM manga ndi azake ayi ngakhale Kuti manga akufunisisa akhalepo yekha
Koma izi mukukamba ndi zoonz zenizeni
Dziko ilili eeeeh
Musiye Mary azilira mamuna wake wafa imfa yowawa chifukwa cha ndale ndiye iyenso apita pa mpando wa upresedent aaaaaaa Bon pena umayankhula zoduka mutu
Inundinu osaganiza sadzafa ndani kuchipanga chipani mkufika pamene chilili cha UTM ndintchito yaikulu asaisiye atenge ndichawo palibe vuto
Ndipo ndizoonadi Mary Chiloma ndipo atha kulamulira dziko la Malawi mosayang'anila Mtundu wamunthu
Amalawi let's vote Mary Chilima kukhala President wa dziko LATHU
Totally agree Mary chilima should be come out and take party enawa abwera kuzangodyerera
Kumeneko ndiye kuononga ndale ...kungoti anali mkazi wa chilima ndiye basi atha kutsogolela dziko? Wafela chilima June yomwe mkazi wake mphavu azitenge kut zolankhulila?
Manjanjawidi kkkk
Koma asamale Mary yo ngati angatenge udindo wa late chilima.boma lilipo PANO ndi Mafia government
Mmmm ayi munthu adakalila mamuna wake
You have nailed, Born, that's 100%
Iweyo ndi amene wabweretsa cancer
Mr DC mwayamba kupanga compane
Kalindo akuyankhula zoona koma vuto zipanizo zikatengera kuphya mtima ndicholinga achotse MCP pa mpando nde ndi izi tikuzunzika lerozi adapangira kuphya mtima a tonse including himself anali gulu limodzi kumamunena mutharika kuti osanva
Bon kalindo ukutanthauza chani za kuti Legacy ya Skc ndi kubanja angayikwanitse mu chipani cha UTM,,,,, ? Sitikufuna ndale zodalira kubanja komwe kunali President wa Chipani,,,Mary can support the party osati kukhala President as now ,,,,This is not Family Party,,,Maganizo opusa amenewo
You are saying truth
UTM is not a family party. Zomwe zikupha zipani ndi zimenezo zofuna akubanja azipitiliza chipani
The DC kuyakhula mopanda matha koma zopanda phindu
Ndimakuvera zoyakhula zako koma izi zomati mary chilima utm wadeya ndipo utm ndi chipani cha amalawi osati chakubanja. Akafuna akubanja abwele athandize utm not tisakhe wakybanja ayi. Mzeru zimafuna anthu a mzeru. Utm ndi ya malawi zipani za ku banja zilipo
Wasauka iwe ukufuna chi bans
Iweso mutu wako sugwila ntchito muntha akhala bwanji president munthu mamuna wake wafa pompano munaonako president opanda mkazi or mamuna cholinga chanu ndi chan makamaka ulibe nzeru kalindo
Anthu nose amene munatenga gawo popanga mgwilizano ochosa chipani cha(..) Boma ndi oti mundabadwa ma, 60s, 70s, and 80s... mukuziwa khaza zomwe chipanichi chimachita..... bwanji simunapange gwilizano ndi chipani cha (...)ndichomwej chinabwelesa Democracy? So yesesani chipanichi chichoke, coz chikazangowina 2025..chizagula anthu ose osusa Boma ndipo yemwe azakane azaphedwa... Ndipo ife Ana am 90s.....2000, sitizakwanisaso kuchosa chipanichi....chonde nose amene munasogoza chipanichi Boma...we need ur action sizomangolankhulazo, tatopanazo....pangani chimozmoz, Mene munapangila 2019,, Bakili analimbana ndi Fiti zimenezi ....inu mkuponyelaso komweko..... Munaganiza bwanji......😢
Cancer bola,tikutitu ozizilisa pofuna kukuchosa zino lomweli mzipatala mulibeee ati ukagule mkumati inu budget ija ku parliament mudaika ndalama kt zigule mankhwala zija zilikutiii?
M chilima zigamuvute akanakhala ndi mwana olo bro bola mai yu wawopsedwa ndi zomwe maunawake anapangidwa komanso Kodi Agathe kukwatiwa panopa? Mpovuta
Kuba no1 kubakuba
Try ma demos DC
The DC
Ng'ona party, wangakachi party
Mai chilima iloweni basi ...and tizavota tonse Malawi tizavotela inu pofuna kudziwa chilungamo pa imfa ya amuna anu ....tiyeni nazo ife pa mbuyo pano
💯💯💯💯💯💯❤️❤️❤️🙏
Zikhala bwino kwambili bola avomeledze chifukwa mmm
Ayi inu a winiko .mmayesa inuyo munali limodzi ndi skc. Bwanji inuyo osaimirira kukhala pulezidentyo? Koma mzimayi yu ayi.mukufuna kuti adzaphedwe moopsya ngati mamunake? Mmene wafers mamuna wake.ndi andale ena a mcp? Musatero a baba
😢
Ndpo live
Dc kuyakhula mwamphamvu
🔥🔥🔥🔥
Unakakhala ndi nzeru sunakalora kuti munthu wazaka 90 akhale Presidential Candidate,achinyamata are ukunenawo ndiye ati?nchifukwa anthu amanena kuti ndiwe wamisala
Mbuli iweyo nanga
Kuswakuswa