Zina zmne amanena mind you zmakhla estimated zina Nd zoti zachtka km zina amanena kut tiyembekezere zmnezozo but to say the truth LIMPOPO FM si ya masewera🔥🔥🔥🔥
Comrade nyimbo ija yatheka tribute ya a chilima the best tribute ever the most heart ❤️ breaking tribute ever please please send me a link to send this song to now
Comrade you are the best. Investigative, informative and truth. Tikuyamika boss.
God is coming soon to judge this world, this is reminder to everyone who has hunger for power.
Ntanyiwa moto moto timakukondani❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ Allah akupase moyo wautali ichala
Ngati sinina vere program iyi sindimakhara mosangarara chifukwa nimava zenizeni
Ntchito ilipo ku malawi ndipo yehovah ana muuza kain kuti ndamva kufuula mwazi pomwe pagwera mwazi wamunthu sipanama
Ntanyiwa🎉🎉🎉🎉🎉 muzibwera kawiri patsiku mokupemphan😂😂😂😂😂
Kawiri patsiku kakuchepa mthanyiwa❣❣❣❣❣❣❣❣❣❣❣❣uzibwera after 2 hours
Everyday ndizikhala pa limpopo fm😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Kkkk kma guys limpopo fm and bakili muluzi TV and Mr born kalindo ndi MA akulu akulu apa malawi ndinu MA big 😂😂
Koma mtanyiwa becaréful,..dnt trust anyone...we value you bro, you're our eyes,..ena akhoza kumatumidwatu...just be careful,..
Apatu Chilungamo chioneke basi çause its painful mene mwachotsera moyo wanzanu ujaaa so sad so painful 😭😭😭😭😭 Mulungu alowererepo
Kalikonse tikaona. Following from BLK
The best Radio station in southern Africa.
Thanyiwa umakwana mulungu azikusogolera
Likangolowa boma Lina likubwelali limpopo fm izakhale yaboma basi
Ndipo live Ntanyiwa tikungodikila kuulutsa mavot tinavota tsiku loikadi chilima M C P inakwililidwadi
Ntanyiwa woyeeeeeeee usadzafe ntanyiwa Mulungu adzangokutengani mlenga mlenga. Ayaluka anthu amenewa. pa dziko lapansi palibe chinsisi Mulungu akukantheni ndithu anthu nonse munapanga chiwembu chimenechi ndipo mizimu ya anthu wonse munawaphawa idzakhala ikukusowetsani mtendere kulikonse mutadzapiteko idzakhala ikukusowetsani mtendere moyo wanu wonse
Kkkkk koma alimpopo umafufuza aiseee😮😮😮
We've been waiting for it❤️🌹
Welcome my brother ife chete kuno, ,from south africa De deur
Mulungu akutetezeleni anthu Ngati inu mutakhalapo angapo mumalawi muja chakwela mukhoza kumuchotsa 2025 isanakwane mmmn galu aneneyi wawonjeza
MCP zoti nd chpani chokupha ife tikangonvatu pno takhulupilira ndthu
Mulungu ..akudalitseni. Antanyiwa
Limpompo fm you are the great radio master
I salute you my people
Wathu wathu comrade more 🤜🤙😍💥
Dzulo mwatiudza za Malunga...lero Manganya...
Chilungamo chinenedwe basi Limpopo Radio station number one the whole Malawi more fire ❤❤❤
Comrade ing'aluliren afiti amenewa ayaluke akakhala chakwelawo diso ngat makilere afune asafune 2025 APM bomaaaa munyanafe agalu inu
Keep it up please 🙏 you are opening the eyes of the Malawians
Koma anthu alibe chisoni munthu anawapangila kampeni kumuphanso, sadik miya anapangila kampeni kumuphanso
Gwenembe ndithu anapha m, bale wake chisoni ndithu shame
May God protect you all the time Mr Ntanyiwa. Thanks for all your info, big up.
Ntanyiwa usakhale wapereka number kwa Soldier yo,akumangitsa atha kukumanga mwina watumidwa ameneyo.
Ulemowanu a limpopo
Zina zmne amanena mind you zmakhla estimated zina Nd zoti zachtka km zina amanena kut tiyembekezere zmnezozo but to say the truth LIMPOPO FM si ya masewera🔥🔥🔥🔥
Sikisinja anapha mu bale wake chifukwa cha dyera ng' ona iwe
Ndipo mizimu ya anthu 9 amenewa ifinye chakwera
Yipase Moto ntanyiwa
Kafukufuku wamaliro achilima sitikufuna nyau kuti zigwire ntchito imeneyi, tufuna mabungwe oziyimira pawokha komanso mabungwe akunja agwire ntchitoyi, asatana nonse muwonekera ng'amba chaka chake ndichino cha 2024
Yomweyo galu iwe chakwera kukonda ndalama
Where there is lack of philanthropy and patriotism, cupidity prevails.
Km abale inu chakwera mutu ukugwiran kd bwanj angofuna kuchosa miyoyo yanthu chonde bon kalindo samalan kmso mulungu akhale pasogolo panu 😭😭😭😭😭😭😭
More ffffffffiiiiiiiirrrrrrrrreeeeeee🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 I m behind you Limpopo FM akanganyawa aziwona sanati ana achepa😂😂😂😂😂🤸🤸🤸🤸🐐
Bodza akupanga trace akupeza usapereke #
Umakwana bwan😊😊
chakwera ndichigawenga pamtumbo pa make ndithu
Mumatha comrade Mthanyiwa, yomweyo galuiwe,
Kkkkk more fire palibe chobitsika pansi pa thambo,kuli Yehova kumwamba sagona kapena kuwodzera
Aaaaa wabodza uyu akumatiphulitsa nalo bodza. Dzulo watipatsa dzina lina la vice president
iwe usamathe mau wava usamale
A Mtanyiwa munabwera inuyo
Nyimboyi ndaifira hvy
More fireeeeeeeeeeeeèeeee waiting comrade ❤❤❤❤❤❤❤
Koma Malawi aaaa lelo Vice president ndi Michael usi akifuna tilitso or Uyu a Ali ku mcp
❤❤❤we just waiting for the truth
May God guide you Ntanyiwa
Comrade nyimbo ija yatheka tribute ya a chilima the best tribute ever the most heart ❤️ breaking tribute ever please please send me a link to send this song to now
More fire
Komansotu Antanyiwa musamalensotu mwina uyu amutumanso kutiakufufuzeni ngati akufuna kukupatsani imfomationa akufuna kuti akupezeni mosavuta plz brother ife tikudalira inu
Aaaa uyu sangamupeze akunama awawa amunamiza kanyimbo kakeko angokasunga yekha kapena akapititse Ku zodiac 😂
Comrade wabwera
Chilungamo chiyende ngati madzi amalawi koma comrade ntanyiwa Inu ndi akatundu ndikamavera programuyi ndimasiya zonse kuchita kwanga kumakhala kumvesera .ndiye ndizoona magalimoto a army alowadi muziko lathu 9😞
Kuyenda ndi Limpopo simudzasowanso kumva bodza Lili lonse ikakhile kwa kuyaaaa Comrade Ntanyiwa
May God protect you Ntanyiwa together with all good and sound activists
Ipondeni fada inuyo mum antha Abro mtanyiwa more fire❤❤❤❤❤
Pitirizani kutipasila malipoti a imfa ya Chilima 😂
Mtanyiwa more fire LiLiLimpopo
Comrade inbox me I have a song ready, tribute to Late Chilima the hottest ever
Comrade could you please hit my inbox your song is ready
+27822885847 tumiza pa WhatsApp
Limpopo FM NDI Bakili Muluzi tv alibeyi zibwana muyaluka nonse a MCP dziwani amalawife siopeperayi
Inu mumanena chilungamo
Koma apapa ineyo ndadabwa america soldiers kupita ku Zambia adakanirapo kalapotu
Please comrades mtanyiwa, usamale ndi awa akumati alindi nyimbo yolilira chilimawa, enawa nda mthirakuwiri ngati malata, munlo, ben longwe, layitoni mangochi, agape, ana opusa kwambiri amenewa
Sadzawinaso mcp bora kuvotera UDF
Mr Ntanyiwa ineyo sinditukwana Koma ndi mkwiyo Mr chilima RIP😢😢😢 chakwera chakwera chakwera sikulina udzaona ngelo USANA 12:30😢😢
Musasiye kuyangulira amalawi tikuseguka mitu pano sitimaziwa zomwe zikuchitika boma
Nkhanga lero zinasowa😂
N'chewa weni weni ndiye munthu wina nkumati chakwera boma misala
Achakwelawa atopesa koma dairy ma programs sapuma kd ndikumacheza ndi banja lawo😂😂
😢😢😢
Mumayitha brother Ntanyiwa timakunyadilani
Pansi pathambo palibe chobisika chakwera wabisala m'mbatata nsana ukuoneka
Kodi mwa vota kare kukokera kumeneko sindie mphamvu yobera imeneyi
Kkkkk yomweyo garu iwe, iponde fadah wina asathawe😂😂😂😂
Abakili tidavapo zamilandu yawo koma apa wina azafera ndende ndithu plz akulu akulu ingoziphani kusiyana ndi ukaidi basi😂😂😂😂😅😅😅😅
Mkulu mmakwanila ndipo mmatimvesa kukoma kwambili ❤❤❤❤❤❤❤❤
More 🔥🔥🔥🔥
Best fm ever🔥🥳
Salute Limpopo fm
Akunama osampasa nambala uyu watumidwa akuphani ndithu be careful
Inu amene munagwira ntchito imeneyo pomwe munkadya ndalama imeneyo mumaimva kukoma
😂😂 Afiti amenewa nawonso aphedwe basi opha mzake naye so aphedwe
More fire ntanyiwa 😂 ndipo ayalukatu
Mtanyiwa sumaiphonya za chidanti umanena zoona
Respect comrade Mtanyiwa .
Timakunyadilani big
wodza nyegelela agaluwa atipela chilima
kkkkkkkk akut ngt vitsilu padzko lonse lapansi nd ochewa
Mthanyiwa keep it up😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Please amalawi tisagone Ayi dziko ndilathu silamuthu modzi ayi
Mapwiya mulupare, Ntanyiwa unobwera phama.
Mukulolenji anthu akupha kupitiliza e kuyendetsa dziko?
😂😂😂😂 ndipo slogan yake timangoti "wa Chiyao wangalusa".. paja mumati ayao ndiwosaphunzira, Koma zachibwana no
Umatha aise Nthanyiwa , tiye nazo tikutsatira zonse
Limpopo FM more fire ahhh