LIMPOPO FM 20 JUNE 2024NDI COMRADE NTANYIWA CHIGAWO CHAKU MADZULO

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 27 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 296

  • @originalblack100
    @originalblack100 3 หลายเดือนก่อน

    Comrade you are the best. Investigative, informative and truth. Tikuyamika boss.

  • @MorrisMapiri
    @MorrisMapiri 3 หลายเดือนก่อน +1

    God is coming soon to judge this world, this is reminder to everyone who has hunger for power.

  • @BrandonThomas-le8eb
    @BrandonThomas-le8eb 2 หลายเดือนก่อน

    Ntanyiwa moto moto timakukondani❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ Allah akupase moyo wautali ichala

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl 3 หลายเดือนก่อน +6

    Ngati sinina vere program iyi sindimakhara mosangarara chifukwa nimava zenizeni

  • @daviebrasil4480
    @daviebrasil4480 3 หลายเดือนก่อน +3

    Ntchito ilipo ku malawi ndipo yehovah ana muuza kain kuti ndamva kufuula mwazi pomwe pagwera mwazi wamunthu sipanama

  • @spargomw
    @spargomw 3 หลายเดือนก่อน +5

    Ntanyiwa🎉🎉🎉🎉🎉 muzibwera kawiri patsiku mokupemphan😂😂😂😂😂

    • @EllinaBitto
      @EllinaBitto 3 หลายเดือนก่อน

      Kawiri patsiku kakuchepa mthanyiwa❣❣❣❣❣❣❣❣❣❣❣❣uzibwera after 2 hours

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 3 หลายเดือนก่อน +2

    Everyday ndizikhala pa limpopo fm😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @Happ2y
    @Happ2y 3 หลายเดือนก่อน +4

    Kkkk kma guys limpopo fm and bakili muluzi TV and Mr born kalindo ndi MA akulu akulu apa malawi ndinu MA big 😂😂

  • @twavysibale4751
    @twavysibale4751 3 หลายเดือนก่อน +4

    Koma mtanyiwa becaréful,..dnt trust anyone...we value you bro, you're our eyes,..ena akhoza kumatumidwatu...just be careful,..

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg 3 หลายเดือนก่อน +1

    Apatu Chilungamo chioneke basi çause its painful mene mwachotsera moyo wanzanu ujaaa so sad so painful 😭😭😭😭😭 Mulungu alowererepo

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 3 หลายเดือนก่อน +2

    Kalikonse tikaona. Following from BLK

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 หลายเดือนก่อน +1

    The best Radio station in southern Africa.

  • @BrandonThomas-le8eb
    @BrandonThomas-le8eb 2 หลายเดือนก่อน

    Thanyiwa umakwana mulungu azikusogolera

  • @MussahNamalomba-e3p
    @MussahNamalomba-e3p 3 หลายเดือนก่อน +3

    Likangolowa boma Lina likubwelali limpopo fm izakhale yaboma basi

  • @TonyOkoibedi
    @TonyOkoibedi 3 หลายเดือนก่อน +2

    Ndipo live Ntanyiwa tikungodikila kuulutsa mavot tinavota tsiku loikadi chilima M C P inakwililidwadi

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 หลายเดือนก่อน +2

    Ntanyiwa woyeeeeeeee usadzafe ntanyiwa Mulungu adzangokutengani mlenga mlenga. Ayaluka anthu amenewa. pa dziko lapansi palibe chinsisi Mulungu akukantheni ndithu anthu nonse munapanga chiwembu chimenechi ndipo mizimu ya anthu wonse munawaphawa idzakhala ikukusowetsani mtendere kulikonse mutadzapiteko idzakhala ikukusowetsani mtendere moyo wanu wonse

  • @Amgwagwa
    @Amgwagwa 3 หลายเดือนก่อน +3

    Kkkkk koma alimpopo umafufuza aiseee😮😮😮

  • @lazarusluciano6916
    @lazarusluciano6916 3 หลายเดือนก่อน +1

    We've been waiting for it❤️🌹

  • @UzeChongo
    @UzeChongo 3 หลายเดือนก่อน +2

    Welcome my brother ife chete kuno, ,from south africa De deur

  • @BisonJackson
    @BisonJackson 3 หลายเดือนก่อน +2

    Mulungu akutetezeleni anthu Ngati inu mutakhalapo angapo mumalawi muja chakwela mukhoza kumuchotsa 2025 isanakwane mmmn galu aneneyi wawonjeza

  • @FrancisGama-qb7ze
    @FrancisGama-qb7ze 3 หลายเดือนก่อน +2

    MCP zoti nd chpani chokupha ife tikangonvatu pno takhulupilira ndthu

  • @AnaLourencokan
    @AnaLourencokan 2 หลายเดือนก่อน

    Mulungu ..akudalitseni. Antanyiwa

  • @HopesonMkomaula
    @HopesonMkomaula 3 หลายเดือนก่อน

    Limpompo fm you are the great radio master
    I salute you my people

  • @JohnsonMaulana
    @JohnsonMaulana 3 หลายเดือนก่อน +1

    Wathu wathu comrade more 🤜🤙😍💥

  • @ThokoMakaika-o5u
    @ThokoMakaika-o5u 3 หลายเดือนก่อน +2

    Dzulo mwatiudza za Malunga...lero Manganya...

  • @MuhajirAnusa
    @MuhajirAnusa 3 หลายเดือนก่อน

    Chilungamo chinenedwe basi Limpopo Radio station number one the whole Malawi more fire ❤❤❤

  • @MackdBanda
    @MackdBanda 3 หลายเดือนก่อน +1

    Comrade ing'aluliren afiti amenewa ayaluke akakhala chakwelawo diso ngat makilere afune asafune 2025 APM bomaaaa munyanafe agalu inu

  • @WinfordGondwe
    @WinfordGondwe 3 หลายเดือนก่อน

    Keep it up please 🙏 you are opening the eyes of the Malawians

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 หลายเดือนก่อน +2

    Koma anthu alibe chisoni munthu anawapangila kampeni kumuphanso, sadik miya anapangila kampeni kumuphanso
    Gwenembe ndithu anapha m, bale wake chisoni ndithu shame

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 3 หลายเดือนก่อน

    May God protect you all the time Mr Ntanyiwa. Thanks for all your info, big up.

  • @sheila5812
    @sheila5812 3 หลายเดือนก่อน +2

    Ntanyiwa usakhale wapereka number kwa Soldier yo,akumangitsa atha kukumanga mwina watumidwa ameneyo.

  • @nellikkmwenda7087
    @nellikkmwenda7087 3 หลายเดือนก่อน +3

    Ulemowanu a limpopo

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy 3 หลายเดือนก่อน

    Zina zmne amanena mind you zmakhla estimated zina Nd zoti zachtka km zina amanena kut tiyembekezere zmnezozo but to say the truth LIMPOPO FM si ya masewera🔥🔥🔥🔥

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 3 หลายเดือนก่อน +3

    Sikisinja anapha mu bale wake chifukwa cha dyera ng' ona iwe

  • @DonaldPonda-p2q
    @DonaldPonda-p2q 3 หลายเดือนก่อน +2

    Ndipo mizimu ya anthu 9 amenewa ifinye chakwera

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet 3 หลายเดือนก่อน +3

    Yipase Moto ntanyiwa

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kafukufuku wamaliro achilima sitikufuna nyau kuti zigwire ntchito imeneyi, tufuna mabungwe oziyimira pawokha komanso mabungwe akunja agwire ntchitoyi, asatana nonse muwonekera ng'amba chaka chake ndichino cha 2024

  • @HalimaShafie
    @HalimaShafie 3 หลายเดือนก่อน +2

    Yomweyo galu iwe chakwera kukonda ndalama

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 3 หลายเดือนก่อน

    Where there is lack of philanthropy and patriotism, cupidity prevails.

  • @StellaCharles-dq8db
    @StellaCharles-dq8db 2 หลายเดือนก่อน

    Km abale inu chakwera mutu ukugwiran kd bwanj angofuna kuchosa miyoyo yanthu chonde bon kalindo samalan kmso mulungu akhale pasogolo panu 😭😭😭😭😭😭😭

  • @SymonZemben-gd3ne
    @SymonZemben-gd3ne 3 หลายเดือนก่อน

    More ffffffffiiiiiiiirrrrrrrrreeeeeee🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 I m behind you Limpopo FM akanganyawa aziwona sanati ana achepa😂😂😂😂😂🤸🤸🤸🤸🐐

  • @mirriamwilliam-nq9wg
    @mirriamwilliam-nq9wg 3 หลายเดือนก่อน +2

    Bodza akupanga trace akupeza usapereke #

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 3 หลายเดือนก่อน

    Umakwana bwan😊😊

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 3 หลายเดือนก่อน +2

    chakwera ndichigawenga pamtumbo pa make ndithu

  • @PatrickSamu-kp2xf
    @PatrickSamu-kp2xf 3 หลายเดือนก่อน

    Mumatha comrade Mthanyiwa, yomweyo galuiwe,

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkk more fire palibe chobitsika pansi pa thambo,kuli Yehova kumwamba sagona kapena kuwodzera

  • @AnimalproductionandVeterinarys
    @AnimalproductionandVeterinarys 3 หลายเดือนก่อน +2

    Aaaaa wabodza uyu akumatiphulitsa nalo bodza. Dzulo watipatsa dzina lina la vice president

    • @FarookHope
      @FarookHope 3 หลายเดือนก่อน

      iwe usamathe mau wava usamale

  • @AaronLilexMphangwe
    @AaronLilexMphangwe 2 หลายเดือนก่อน

    A Mtanyiwa munabwera inuyo

  • @futurekanjanga1290
    @futurekanjanga1290 3 หลายเดือนก่อน

    Nyimboyi ndaifira hvy

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 3 หลายเดือนก่อน

    More fireeeeeeeeeeeeèeeee waiting comrade ❤❤❤❤❤❤❤

  • @Imraanjafali
    @Imraanjafali 3 หลายเดือนก่อน +2

    Koma Malawi aaaa lelo Vice president ndi Michael usi akifuna tilitso or Uyu a Ali ku mcp

  • @StechelectronicsRepair-qh5jl
    @StechelectronicsRepair-qh5jl 3 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤we just waiting for the truth

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk 3 หลายเดือนก่อน +1

    May God guide you Ntanyiwa

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki 3 หลายเดือนก่อน

    Comrade nyimbo ija yatheka tribute ya a chilima the best tribute ever the most heart ❤️ breaking tribute ever please please send me a link to send this song to now

  • @KelvinJpchimphepo-sh6nc
    @KelvinJpchimphepo-sh6nc 3 หลายเดือนก่อน

    More fire

  • @Fanzo-h2l
    @Fanzo-h2l 3 หลายเดือนก่อน +3

    Komansotu Antanyiwa musamalensotu mwina uyu amutumanso kutiakufufuzeni ngati akufuna kukupatsani imfomationa akufuna kuti akupezeni mosavuta plz brother ife tikudalira inu

    • @cynthiakananji1608
      @cynthiakananji1608 3 หลายเดือนก่อน

      Aaaa uyu sangamupeze akunama awawa amunamiza kanyimbo kakeko angokasunga yekha kapena akapititse Ku zodiac 😂

  • @SangwaniThika
    @SangwaniThika 3 หลายเดือนก่อน

    Comrade wabwera

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 3 หลายเดือนก่อน +1

    Chilungamo chiyende ngati madzi amalawi koma comrade ntanyiwa Inu ndi akatundu ndikamavera programuyi ndimasiya zonse kuchita kwanga kumakhala kumvesera .ndiye ndizoona magalimoto a army alowadi muziko lathu 9😞

  • @YasmeenYalabi-b2c
    @YasmeenYalabi-b2c 3 หลายเดือนก่อน

    Kuyenda ndi Limpopo simudzasowanso kumva bodza Lili lonse ikakhile kwa kuyaaaa Comrade Ntanyiwa

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 หลายเดือนก่อน

    May God protect you Ntanyiwa together with all good and sound activists

  • @AslamCassim-b7n
    @AslamCassim-b7n 3 หลายเดือนก่อน

    Ipondeni fada inuyo mum antha Abro mtanyiwa more fire❤❤❤❤❤

  • @FredlillianMbuba-sx3dd
    @FredlillianMbuba-sx3dd 3 หลายเดือนก่อน +2

    Pitirizani kutipasila malipoti a imfa ya Chilima 😂

  • @MustafaAbdullah-pb5zv
    @MustafaAbdullah-pb5zv 3 หลายเดือนก่อน

    Mtanyiwa more fire LiLiLimpopo

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee 3 หลายเดือนก่อน +1

    Comrade inbox me I have a song ready, tribute to Late Chilima the hottest ever

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee 3 หลายเดือนก่อน +2

    Comrade could you please hit my inbox your song is ready

    • @clubjunta
      @clubjunta  3 หลายเดือนก่อน

      +27822885847 tumiza pa WhatsApp

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 3 หลายเดือนก่อน +1

    Limpopo FM NDI Bakili Muluzi tv alibeyi zibwana muyaluka nonse a MCP dziwani amalawife siopeperayi

  • @BrandonThomas-le8eb
    @BrandonThomas-le8eb 2 หลายเดือนก่อน

    Inu mumanena chilungamo

  • @timothyphiri2895
    @timothyphiri2895 3 หลายเดือนก่อน +1

    Koma apapa ineyo ndadabwa america soldiers kupita ku Zambia adakanirapo kalapotu

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 หลายเดือนก่อน +1

    Please comrades mtanyiwa, usamale ndi awa akumati alindi nyimbo yolilira chilimawa, enawa nda mthirakuwiri ngati malata, munlo, ben longwe, layitoni mangochi, agape, ana opusa kwambiri amenewa

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo 2 หลายเดือนก่อน

    Sadzawinaso mcp bora kuvotera UDF

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 3 หลายเดือนก่อน

    Mr Ntanyiwa ineyo sinditukwana Koma ndi mkwiyo Mr chilima RIP😢😢😢 chakwera chakwera chakwera sikulina udzaona ngelo USANA 12:30😢😢

  • @BrandonThomas-le8eb
    @BrandonThomas-le8eb 2 หลายเดือนก่อน

    Musasiye kuyangulira amalawi tikuseguka mitu pano sitimaziwa zomwe zikuchitika boma

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk 3 หลายเดือนก่อน +2

    Nkhanga lero zinasowa😂

  • @DonaldPonda-p2q
    @DonaldPonda-p2q 3 หลายเดือนก่อน +1

    N'chewa weni weni ndiye munthu wina nkumati chakwera boma misala

  • @BonfaceMajawa
    @BonfaceMajawa 3 หลายเดือนก่อน +2

    Achakwelawa atopesa koma dairy ma programs sapuma kd ndikumacheza ndi banja lawo😂😂

    • @BonfaceMajawa
      @BonfaceMajawa 3 หลายเดือนก่อน +1

      😢😢😢

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm 3 หลายเดือนก่อน

    Mumayitha brother Ntanyiwa timakunyadilani

  • @DonaldPonda-p2q
    @DonaldPonda-p2q 3 หลายเดือนก่อน +1

    Pansi pathambo palibe chobisika chakwera wabisala m'mbatata nsana ukuoneka

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi mwa vota kare kukokera kumeneko sindie mphamvu yobera imeneyi

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkk yomweyo garu iwe, iponde fadah wina asathawe😂😂😂😂

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 3 หลายเดือนก่อน +1

    Abakili tidavapo zamilandu yawo koma apa wina azafera ndende ndithu plz akulu akulu ingoziphani kusiyana ndi ukaidi basi😂😂😂😂😅😅😅😅

  • @mustafailanga2585
    @mustafailanga2585 3 หลายเดือนก่อน

    Mkulu mmakwanila ndipo mmatimvesa kukoma kwambili ❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @dysonfysonchifundo2284
    @dysonfysonchifundo2284 3 หลายเดือนก่อน +1

    More 🔥🔥🔥🔥

  • @AuspiciousKalambula-hp7gj
    @AuspiciousKalambula-hp7gj 3 หลายเดือนก่อน

    Best fm ever🔥🥳

  • @GiftManuel-er7yh
    @GiftManuel-er7yh 3 หลายเดือนก่อน

    Salute Limpopo fm

  • @mirriamwilliam-nq9wg
    @mirriamwilliam-nq9wg 3 หลายเดือนก่อน +1

    Akunama osampasa nambala uyu watumidwa akuphani ndithu be careful

  • @DonaldPonda-p2q
    @DonaldPonda-p2q 3 หลายเดือนก่อน +1

    Inu amene munagwira ntchito imeneyo pomwe munkadya ndalama imeneyo mumaimva kukoma

  • @Carolynmzonde
    @Carolynmzonde 3 หลายเดือนก่อน +2

    😂😂 Afiti amenewa nawonso aphedwe basi opha mzake naye so aphedwe

  • @dontreybanda278
    @dontreybanda278 3 หลายเดือนก่อน +1

    More fire ntanyiwa 😂 ndipo ayalukatu

  • @chifundochitapa3663
    @chifundochitapa3663 3 หลายเดือนก่อน +1

    Mtanyiwa sumaiphonya za chidanti umanena zoona

  • @davidkadyakapita8836
    @davidkadyakapita8836 3 หลายเดือนก่อน

    Respect comrade Mtanyiwa .

  • @DavidPeter-e2o
    @DavidPeter-e2o 3 หลายเดือนก่อน +1

    Timakunyadilani big

  • @AlickJinamu
    @AlickJinamu 3 หลายเดือนก่อน +1

    wodza nyegelela agaluwa atipela chilima

  • @IgnatiousFote
    @IgnatiousFote 3 หลายเดือนก่อน +2

    kkkkkkkk akut ngt vitsilu padzko lonse lapansi nd ochewa

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 3 หลายเดือนก่อน

    Mthanyiwa keep it up😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 3 หลายเดือนก่อน

    Please amalawi tisagone Ayi dziko ndilathu silamuthu modzi ayi

  • @FunnyKatchenga
    @FunnyKatchenga 3 หลายเดือนก่อน

    Mapwiya mulupare, Ntanyiwa unobwera phama.

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela 3 หลายเดือนก่อน +1

    Mukulolenji anthu akupha kupitiliza e kuyendetsa dziko?

  • @wilsonali7890
    @wilsonali7890 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂 ndipo slogan yake timangoti "wa Chiyao wangalusa".. paja mumati ayao ndiwosaphunzira, Koma zachibwana no

  • @GeorgePatels-go7wj
    @GeorgePatels-go7wj 3 หลายเดือนก่อน

    Umatha aise Nthanyiwa , tiye nazo tikutsatira zonse

  • @ephraimphalawala4720
    @ephraimphalawala4720 3 หลายเดือนก่อน

    Limpopo FM more fire ahhh