PA DZANA - ZOSAYIWALIKA ZOMWE ANALANKHULA LATE DR SAULOS CHILIMA KU SALIMA, KAMUZU ROAD

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 10 ก.พ. 2025
  • PA DZANA - ZOSAYIWALIKA ZOMWE ANALANKHULA LATE DR SAULOS CHILIMA KU SALIMA, KAMUZU ROAD

ความคิดเห็น • 15

  • @TonyMhone
    @TonyMhone 6 วันที่ผ่านมา +4

    Mhuuuuuu Koma akanadziwa. Mphuno salota. Sankadziwa adzathera mu chikangawa

  • @EdwardShawa-u7l
    @EdwardShawa-u7l 5 วันที่ผ่านมา +1

    Mkulu uyu adaononga malawi koposa 😢

  • @LastonMmanga-r2u
    @LastonMmanga-r2u 6 วันที่ผ่านมา +1

    Eeeee😢😢😢😢 chosadziwa adayimbira mfiti m'manja🤔🤔🤔

  • @FracksonMadani
    @FracksonMadani 6 วันที่ผ่านมา +1

    Ngati anachitadi kupha monga mphekesera zikubvekera, okuphawo ankadziwa kuti mulitsogolo laMalawi....uyu kwaine ndinkawona katundu ofunika kudziko, any way Kabande my vote

  • @StevenPiyo-c7e
    @StevenPiyo-c7e 5 วันที่ผ่านมา

    That's Malawi koma easy bwana ife tinkakundan koma pot sinu dollar simungakomelebe ose

  • @Kenmoney-xp7tz
    @Kenmoney-xp7tz 6 วันที่ผ่านมา +2

    Munthu oyipa iwe ana chita bwino kukunyenya unangophesa anthu osalakwa galu

  • @HestingsZiba-d6k
    @HestingsZiba-d6k 6 วันที่ผ่านมา +1

    Mhuu chakwela uja ndi njoka ndithu kumuphela mu chilangawa mwana osalakwa

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 5 วันที่ผ่านมา

    My vote is for Apm osati zisilu zinazi .....ineyo sindizavotelanso chisilu ayi ndipo ndikanaziwa sindikanavotela chakwera ....mbuzi yeniyeni ya munthu ....galu

  • @Malekano-k3x
    @Malekano-k3x 5 วันที่ผ่านมา

    Phuno salota chilima

  • @Mirriumkamwendo
    @Mirriumkamwendo 5 วันที่ผ่านมา

    Chilima koma mwano unalimo

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 5 วันที่ผ่านมา

    Komansotu chilima amasuta chamba mutha kuona mmene amayankhulila zinali zachamba basi

  • @EdwardShawa-u7l
    @EdwardShawa-u7l 5 วันที่ผ่านมา

    Koma mkulu uyu

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 5 วันที่ผ่านมา

    Mkulu uyu ndichifukwa anaphedwa kuyankhula mwa matama .....achisilu awa ndichifukwa Ali mmanda lelo ndiponso anali munthu wokuba uyu

  • @brianmakina8157
    @brianmakina8157 5 วันที่ผ่านมา

    Ukakanakhala kuti umalota sibwezi ukupanga zinthu ngati zimenezi mphuno salota

  • @spargomw
    @spargomw 5 วันที่ผ่านมา

    Kunena moona mtima Chilima anali munthu wamwano kwambiri ndipo chipongwe chonse amkayankhula apachi amkanena APM, lero ali kunthaka, APM ali ku page House kamphepo kochokera m'mbali mwa Nyanja kakumudutsa😂😂😂😂😂. Anyway RIP bwana 😭😭😭😭