May God regide you Mtanyiwa I always pray for you all the time. Chenjezo osalora kukumana ndi munthu Don't trust a human being. Ena akumabwebwetawa ngat kt akumenyera ufulu ndi bodza akufuna akukore. Tinaluza chilima tisaluzenso iweyo Mtanyiwa. God protects you all the time during this miserable time. Amen
May God punish poverty ndlama ya fertilizer agula company ya ku Ghana akuti iphe Ntanyiwa ndi Bakili TV km okumbira dzenje Ntanyiwa Muluzi TV agweram yekha Chakwerayo ndi mkazi wakeyo
Chilungamo chiyende ngat maz warrior big up Ntanyiwa
May God regide you Mtanyiwa I always pray for you all the time. Chenjezo osalora kukumana ndi munthu Don't trust a human being. Ena akumabwebwetawa ngat kt akumenyera ufulu ndi bodza akufuna akukore. Tinaluza chilima tisaluzenso iweyo Mtanyiwa. God protects you all the time during this miserable time. Amen
Nanuso mayi chikangawa mukusekelela zamanji amuna anu mudzalila limozi simuzalemezsdwa moyo wanu onse munyoyeletu belatuni ndithu muzalila mulungu sangakonde inu nonkha
Mai osamuuzako zanzeru mamunake mmmmmmm big shame
Wamuiwala chsru chaximai icho kulikonse ky chimaphika kaya
Kupanda inu bambo Mthanyiwa ife sitinakadziwa kathu.Mulungu dalitsani mayi awa a Mthaniwa Amen.
Tanyiwa ❤️❤️❤️
Tanyiwa ndi machine mumantha Big man
Comrade..... Ntanyiwa...,❤❤❤❤
Welcome back Dad ❤❤
Lipopo is the best
Gwenembe family
😊kondwani Nankhumwa asamatipusitse, iiyeyu ndiwa MCP, kachipani kake ndika branch ka MCP
May God punish poverty ndlama ya fertilizer agula company ya ku Ghana akuti iphe Ntanyiwa ndi Bakili TV km okumbira dzenje Ntanyiwa Muluzi TV agweram yekha Chakwerayo ndi mkazi wakeyo
Chakwera muramwake wa chakwera nkanzake wa Chakwera wankanzi wa muramwake wa Chakwera osewo machende awooooooo.athu owononga marawi tikomana tsiku rovotabasi .komatu ndiye kuseroko kudzakhara banj rose.kumenya kugwetsa mcp.
Welcome antanyiwa tinakusowani big man
Ntanyiwa ❤❤.mumatiyimilila😅😅
Ndiwatsoka amene adzavotere mcp mulungu atichitire chifundo kkkkk anankhumwa palibe ndale apa alephera kale anankhumwa awonetsa kt anzake ndi chakwera
Boma loyendesedwa ndi zisilu ili ..
Palibe Boma apa .
...achakwera ndi achisilu bwanji
Big up ntanyiwaa
Machine nde akugulidwa tu sleep but keep one eye open
Chikangawa team
Mkazi wanzeru amamuuza mamuna wake zanzeru km mbuzi iyo chimangoseka zili znse kukamwa ngt wapana mbewa
A NTANYIWA MALATA NDI WODWARA NDANI SAKUDZIWA??
More ❤❤❤
Anankhumwa mwala kwitsatu mawu amenewo chifukwa anthu akutsikani apo mwaonetsa kuti simunga kwanitse kudyetsa malawi yose
Mtanyiwa ndi biggy ulemu wanu nthawi zonse
Big man more fire
Mwause.ntanyiwa.apolisi.oo.koma.akufutika.mkwambili
More fire Ntanyiwa
Machine machine ntanyiwa
Bola kumeneko akhaula chikangawa uyo
Good muyankheni amatumbwa was VN yopepelayo
Zamphavu
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Bile malata ndi galu okuwa kukhomo kwaeni pofun chakudya
Welcome back
Makolo Ake acomryde ntanyiwa landilani ulemu
Game on
Akunama sangampeze Nta nyiwa ndi Bakili Muluzi Tv
😂😂😂 koma nangumwa bolaso ine mamamam 😂😂😂nangumwa ndichani chimene amayankhula uyu ndi mbunzi yeniyeni
Okuba abelana
Kkkkk km ntanyiwa uphetsa athu kuno
Nkhope zangati mizukwa izi nzakuti
❤❤❤❤
Bendulo uti uzabwino zanu chikangawa
❤
Zikumveka Mr wanzeru akunva
Muzaziwona Ana achakwela Inu mukungowayang'. Ana bambo wanu akuononga dzilo usawadzudzula muzalila
Azifufu kkkkkk
Comment on 17 September
One off the best mr ntanyiwa ❤❤❤❤
Ati akupwetekani a kunja akuphani
😂😂😂
😂😂😂Koma anthu awa wonyasa
Kom iwe umatha 💯🌽🌽🌽🌽 basi
Koma yaaaa
Mbava zokhazokha
Kkkkkkk
Kkkkkkkk
😂😂😂😂 km Khan zake
Gwenembe family