Brother saro mukunena zoona mayi Ameneyo ndi oipa satanic walemera lemera and zomwe anenazo ndi kuthedwa mzeru chifukwa amalawi awasiya pa mbala Banda afuna awoneke ngati amzeru ajoice Banda a kondwani nankhumwa mwendo wawo umodzi uli ku MCP
ALUFUNA KUTI MUDZAPESE MCP MAVOTI AKUWONEKA NGATI SALI KU MCP KOMA DZIWANI AFTER KUVOTA MAVOTI JOYISI BANDA ADZAPATSA CHAKWERA SAMALANI NDI JOYISI BANDA
Mai Joyce Banda akulamulira anali woipa kwa a malawi..amazunza ma civil servants ndipo ife ma civil servants tinawapangira m demo kuti achoke ndipo afe !@ ife ma civil servants tinawaika mu coffiñ ndimaluwa .ife nkumaimba nyimbo yolira kutì amai wa akutizunza iÿeyu ndi mfiti kwambiri ndipo mulungu mdzina la Ambuye Yesu Mnkhrustù anaĺephera zisankĥo .!! Aaah akagwère ku gehena
Mai JB ndi akuba adatibera ndalama chakachatha potinamiza kuti atipatsa ngongole dziko lonse lamalawi adazungulira kutolera ndalama mpaka kutitsekulitsa ma account up to now kuli ziiiiiiii tikuchita kusowa kokafunsa voti asaione
Tapezani zina zochita osamangokhalila kunyoza zinthu zopanda pake... Ena akupatsani ndalama kuti mugundike kutukwana that one will not change that Mama JB changed Malawi within 100 days.. Ndimtsogoleri yekhayo anthu ammidzi ali mumtima mwawo
Keep it up brother from Capetown
Amayi awa ayi muli boza ndipo ndi ampeni kumphasa
Brother saro mukunena zoona mayi Ameneyo ndi oipa satanic walemera lemera and zomwe anenazo ndi kuthedwa mzeru chifukwa amalawi awasiya pa mbala Banda afuna awoneke ngati amzeru ajoice Banda a kondwani nankhumwa mwendo wawo umodzi uli ku MCP
Atupele adalephela mp ku balaka
Upresident sangauthe
Welll said brother very true 👏👏🔥🔥💯
Chilima yekhayo musiye CHITSILU iwe
Ma hule ose aku malawi president wao ndi Joyce Banda
Malawi is no longer at comfort.We have many misleaders in religions and politics.May God intervene !
If she had listened to the people Joyce Banda had listened before the elections against mutharika she would be here now
Ben longweyo ndiye ukulakwitsa kumawa nyoza ase amene tikumvera nkhani zambili ndikwa Ben longweyo iweyo sumatha
Zoona brother
Take it or leave it
It's true brother sallo
Nkozi Nanu muzipita direct pa zifundo
Zoona zake mau
Zoona Atupere mulibe utsogoleri,,,Mai Joyce ndi a kuwiri kuwiri
ALUFUNA KUTI MUDZAPESE MCP MAVOTI AKUWONEKA NGATI SALI KU MCP KOMA DZIWANI AFTER KUVOTA MAVOTI JOYISI BANDA ADZAPATSA CHAKWERA SAMALANI NDI JOYISI BANDA
Takuziwani inuo ndi Adppp
Kodi bon kalindo atangoti aimire u pre anthu angamuvotere
It's true story
Kusowa zochita kumangokhala kunamiza anthu
Mai Joyce Banda akulamulira anali woipa kwa a malawi..amazunza ma civil servants ndipo ife ma civil servants tinawapangira m demo kuti achoke ndipo afe !@ ife ma civil servants tinawaika mu coffiñ ndimaluwa .ife nkumaimba nyimbo yolira kutì amai wa akutizunza iÿeyu ndi mfiti kwambiri ndipo mulungu mdzina la Ambuye Yesu Mnkhrustù anaĺephera zisankĥo .!! Aaah akagwère ku gehena
Komatu mukulankhula za bodzatu...Malawi yake yomweyi anazunza ma civil servant???? Ndale zikukupengesanitu.
Munene zina mwina mumawada osati mwanenazo
Mmmm abodza inu mayi Joyce Banda anawonjezela malipilo ma civil servant kawili konse kuzuza kwake kuti kunama basi siinu APA mukhulu inu which Malawi
Ukagwele kugahena ndiwe kuwano akuyamkhulawo nkhope ngati kugehena komweko kkkkkk
Bro mukamba zoona atupele ndi odontha
Wabwino ndiiweyo ndi banja lako
As a country let's do away with family political dynasties .
Usatanic muwauze mai joyce kt amalawi panopa ndiochenjela sakusatila zilizonse km sikulina muzamuthawa malawi amalawi atatopa nanu
Eya zoona
Machine ako aye
Ya achilima uyisiye wamva usatchukire pa iye chifukwa anaphedwa wamva,???
Ndiwe osokoneza poti wati ndi maganizo ako koma palibe chomwe wanena iweso ndiwe wonyasaso kwambiri ulibe khalidwe
Chitsiru iwe wa DPP
Ajoce bada asowe
Galu lwe ndi gogo wa dpp
Ndiye poti amalawi timafuna tione Kaye zoopsyazo
Zoona mayi uyu ndi mbuzi
Musamathe mau pa Joyce Banda muzitha mau kwa chakwera Joyce Banda apepese chifukwa chani osanyoza Joyce wathuyo
Mai JB ndi akuba adatibera ndalama chakachatha potinamiza kuti atipatsa ngongole dziko lonse lamalawi adazungulira kutolera ndalama mpaka kutitsekulitsa ma account up to now kuli ziiiiiiii tikuchita kusowa kokafunsa voti asaione
😂😂😂😂😂 komaditu
Chilimayonso ndi amene anabweretsa mavuto omwe amalawi akulira lero lino koma amalawi sakuona zimenezi ndipo timamulilabe ngati mmalawi zathu koma tikudzi kuti anatisiyila mavuto ndiye plz mulekeni atupele muluzi
Mayi awa Malawi akuthandizila Kuti tizivutika kufika pomwe tilipa kuvutikaku chifukwa chamayi ameneyi ndimuuza JB awathile ma phuzo
Wabwino ndiiweyo
Ukawawuze agogo ako ZOPUSA zako ukamaGalu
Joyce banda upepese ndithu
Apepese kwa iweyo ngati ndani galu iwe
Za ziiii apepese kwa iweyo aaah koma anthu ndinu osekesa
Kaya ndioipa kaya ndiotani akunena zoona, wayenda nawo ndipo waona kuti ndioipa ndiye asanene ,Atupele yenkha ndiye ai ndizoona alibe ulamuliro,
Palibe chanzeru chimene ukukamba apa za nzeru ndizokhazo za ma bridge zo
Wangokhala ndi udani ndi Mama JB...ulibe manyazi kunyoza kumeneko ngati sunabadwe ndi mzimayi.
Munthu womvesa chisoni iwe
Nanu achisilu mukukambait
Kulibeko mp komwe kulibe ma bridge ko
Ndizoonadi atupere muluzi simunaganize bwino,ukaoneka wabwino kudziko Lina osapepesa kumwalira Kwa chilima?
alibe utsogoleli mayi banda
Julie mavuto Ku Malawi mavuto ali mnyumba mwako chifukwa cha ulesi wako kuzolowera kupmpha
Zoonadi
Zaziiiii
Be brief
Zowona
Bambo iyetu amangozuzula ntchitedwe umene ukupitilira kupwanya democracy mu Africa atupele amalankhula ngati mu Africa nzawo kodi umene chilima boni kalindo wakhala akulankhula naye kangati koma mumamumvela boni kalindo chaka chatha analankhula ndi Bryan banda kuti ngati chilima sanganene any statement kufika January chilima is finish ndiye sanathe iye amadziona kuphulazila kwambiri komanso palibe angamuwunze zochita ndiye asalo musiyeni Atupele muluzi ngati mwasowa zochita nanu
Zoonadi
Ndiwe wa DPP iwe.Ukunamiza ñdani?
Ati ndiyizukute za ziiii asiyeni masten ati ndimangomuswa tinakupempha ife
Machende ako kape ndiwe wa dpp
Mapwala ako mr chikangawa
Tapezani zina zochita osamangokhalila kunyoza zinthu zopanda pake...
Ena akupatsani ndalama kuti mugundike kutukwana that one will not change that Mama JB changed Malawi within 100 days.. Ndimtsogoleri yekhayo anthu ammidzi ali mumtima mwawo
Iwe ndiwe chisilu kwabasi
Wopanda nzeru uyu..
Find other things worthy to do other than being busy tarnishing other people's names for the sake of useless views
Kupusa kweni kweni...ndipo muzawonesetse amanyoza ali kunja zopusa akupangazi sangapangile ali mdziko muno..kufuna kutamika ndi zinthu zopusa
iweyo ndi wa DPP galu 😂😂😂😂😂😂😂