A Malawi si anthu owavera chisoni chifukwa ndi omwe Amati tione Zina nde lero bwa chakwera wakoyo akungopwitsa Ku state house Mbali inayi ine ndiku dyelera Kuno Ku Jozi
Choka iwe Amayi analamula bwino dzikoli zaka ziwiri zija. Zoti anaba ndala m'boma ndi nsanje ndi nkhwidzi za DPP no wonder the woman is still a free person till now
Malawi wafika ponukha uyu palibe chomwe chomwe chikuyenda😢
Chakwela ndifiti satana mapwala wake pati
ma president osewa alindmavuto awo JB wen we say cash gate maboma osewa amaba uyuyu bola JB
A Malawi si anthu owavera chisoni chifukwa ndi omwe Amati tione Zina nde lero bwa chakwera wakoyo akungopwitsa Ku state house Mbali inayi ine ndiku dyelera Kuno Ku Jozi
Paja adpp kukonda kutukwana
Ndagwilizana Nanu kwambili
mmm😢😢😢
Mayi Banda pachiongolero
Ndiye misalayo ndiye kulozedwatu mayi cashgate ndi yemweyo akafuna ayime payekha kapena apite ku MCP
Choka iwe
Amayi analamula bwino dzikoli zaka ziwiri zija.
Zoti anaba ndala m'boma ndi nsanje ndi nkhwidzi za DPP no wonder the woman is still a free person till now