NKHANI_CHIPANI CHANI CHA PP

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 8 ก.พ. 2025

ความคิดเห็น • 10

  • @AustinNangwale
    @AustinNangwale 5 วันที่ผ่านมา +2

    Malawi wafika ponukha uyu palibe chomwe chomwe chikuyenda😢

  • @BrightonMkandawire
    @BrightonMkandawire 5 วันที่ผ่านมา +2

    Chakwela ndifiti satana mapwala wake pati

  • @FrancisKatunga-u5f
    @FrancisKatunga-u5f 4 วันที่ผ่านมา

    ma president osewa alindmavuto awo JB wen we say cash gate maboma osewa amaba uyuyu bola JB

  • @OsmanPatrick
    @OsmanPatrick 5 วันที่ผ่านมา +2

    A Malawi si anthu owavera chisoni chifukwa ndi omwe Amati tione Zina nde lero bwa chakwera wakoyo akungopwitsa Ku state house Mbali inayi ine ndiku dyelera Kuno Ku Jozi

    • @BisiyeleJanuary
      @BisiyeleJanuary 5 วันที่ผ่านมา

      Paja adpp kukonda kutukwana

    • @WhyteSmart
      @WhyteSmart 4 วันที่ผ่านมา

      Ndagwilizana Nanu kwambili

  • @kettiebonjesi-i6c
    @kettiebonjesi-i6c 5 วันที่ผ่านมา

    mmm😢😢😢

  • @Blessings31
    @Blessings31 5 วันที่ผ่านมา

    Mayi Banda pachiongolero

  • @JamesSinyolo
    @JamesSinyolo 5 วันที่ผ่านมา

    Ndiye misalayo ndiye kulozedwatu mayi cashgate ndi yemweyo akafuna ayime payekha kapena apite ku MCP

    • @Blessings31
      @Blessings31 5 วันที่ผ่านมา

      Choka iwe
      Amayi analamula bwino dzikoli zaka ziwiri zija.
      Zoti anaba ndala m'boma ndi nsanje ndi nkhwidzi za DPP no wonder the woman is still a free person till now