Bravo!! Mr. Kamangira Dzuka Malawi Dzuka. Ma youths this is the right way to fight for our country osati kutumidwa kuyambitsa zisokonezo. Nthawi yakwana kuti achinyamata atenge udindo to shape their future. This is very commendable. More fire bwana Kamangira.
Truth is a spirit from God. No one can attack the truth because it's a product of Holly spirit. No matter how much the corrupt judges would try to silence the truth, they cannot win. Kamangila is a God sent lawyer to save justice at it's extreme level
Let all Malawi'an tigwilane manja timusspote mu njira ili yonse chinyengo chikuchuluka kundende angopezeka osauka okha mbava zikuluzikulu zolemela sazimanga Kaya ndalama let's lez fund to support this laywer
Apa Justice wo alowe mu khoti ndi a kamangilawo. Ndipo ikhale pa radio. Mlandu omveledwe ndipo ma CSO ndi ma Judge atatu amvele mlandu wo. Guys dziko limene athu akukayikila ma Court limakhala Lawlessness.
Dziko lidaipa ili it's better maiko anzathu adaonongeka koma ku zachuma adasunthako,koma sikwathu kuno umphawi wa thoo koma kumangopondeleza anthu osuka Iwo nkumalemera modabwitsa why Malawi??? For example njala ili muziko muno sibwino kumafinyana tokhatokha pofuna kusangalatsa anthu oononga dziko ndi odzikonda 😢😢😢
Osawanyengera a justice lenani Manda atumbukawo kuopitsa mtundu wao..ife a malawi tatopa ndi zachinyengo zimene atumbukawa amachita mma office a bomawo..kodi ndi umphawi kodi ? Nkuona Dr H kamuzu Banda anawathamingitsa atumbuka onse azipita kwao in 1987..cos they are all corrupt .them are thieves.. ndiye apa akapitiliza onse atumbuka adzipita kwao not live in the southernbregion or the central region.
DONT LET THEM,BUT WE NEED THE TRUTH TO FOCUS IN OUR NATION .INDEED IT IS HAPPENING IN OUR GORVERMENT OF MALAWI.START WITH CHAKWERA AND ALL MINISTERS,JUDICIAL ,AND ALL DEPARTEMENTS.
Bravo!! Mr. Kamangira
Dzuka Malawi Dzuka.
Ma youths this is the right way to fight for our country osati kutumidwa kuyambitsa zisokonezo. Nthawi yakwana kuti achinyamata atenge udindo to shape their future. This is very commendable. More fire bwana Kamangira.
Me too , I will in front... Amalawi nthawi yakwana kuti Malawi yopulumuke ku muchitidwe wobela amalawi aumphawi
Congratulations brother Kamangira
Mulungu akhale nanu nthawi zonse
angakhale khamu la wanthu limadana ndi chilungamo
pambuyo panu ngangangaaaa timakunyadirani kopotsa zedi
Truth is a spirit from God. No one can attack the truth because it's a product of Holly spirit.
No matter how much the corrupt judges would try to silence the truth, they cannot win.
Kamangila is a God sent lawyer to save justice at it's extreme level
Powerful message
Let all Malawi'an tigwilane manja timusspote mu njira ili yonse chinyengo chikuchuluka kundende angopezeka osauka okha mbava zikuluzikulu zolemela sazimanga Kaya ndalama let's lez fund to support this laywer
Mr kamangila pitilizani kukoza Malawi wathu,,,wakutumani ndi mulungu,,anthu akufa osalakwa,,,kumangidwa,,okuba ali khale chifukwa ali ndi ndalama,,mulungu wakutumani kuti mupulumuse anthu osauka
Well done ✅ guys good job thanks, again well done guys together we can make Malawi better place for all,,
Komaso ukunena zooona kuyamikaso ndikwabwino kwayamika anthu amenewa
Apa Justice wo alowe mu khoti ndi a kamangilawo. Ndipo ikhale pa radio.
Mlandu omveledwe ndipo ma CSO ndi ma Judge atatu amvele mlandu wo.
Guys dziko limene athu akukayikila ma Court limakhala Lawlessness.
More fire 👦 🔥 guys 🇲🇼 Malawi is badly now 😫 😢 😩 be strong 💪 👏 we trust you guys 👦 more fire 👦 🔥 again
Well done brother kamangila.
Powerful massage
Powerful message ❤❤❤
Let's protect this property ❤
😊😊😊😊
I totally support this statement
I can sense seriousness in these guys...
Go,guys go and bite hard.
IT IS TIME TO RESTORE MALAWI BELOVED COUNTRY
I see changes in Malawi 10-15 years come
Well done
Asasowetu ameneyo
Even the devil knows that justice is sold in the country 's courts .
Nkhani ndiyayikulu iyi
Nthawi yakwana
Aaa mamvuto TIKUKOMANA NAWO LELLO AMALAWI NDIWOMWE AMABWALO LAMILANDIKU KUGAMULA MWA DZIPHUPHU LELO MALAW ALI PAMOTO APA AGALU KWABASI
Restoration
Chilungamo chibwere poyera basi
Dziko lidaipa ili it's better maiko anzathu adaonongeka koma ku zachuma adasunthako,koma sikwathu kuno umphawi wa thoo koma kumangopondeleza anthu osuka Iwo nkumalemera modabwitsa why Malawi??? For example njala ili muziko muno sibwino kumafinyana tokhatokha pofuna kusangalatsa anthu oononga dziko ndi odzikonda 😢😢😢
Osawanyengera a justice lenani Manda atumbukawo kuopitsa mtundu wao..ife a malawi tatopa ndi zachinyengo zimene atumbukawa amachita mma office a bomawo..kodi ndi umphawi kodi ? Nkuona Dr H kamuzu Banda anawathamingitsa atumbuka onse azipita kwao in 1987..cos they are all corrupt .them are thieves.. ndiye apa akapitiliza onse atumbuka adzipita kwao not live in the southernbregion or the central region.
Vuto lomwe tili nalo ife aMalawi ndi matha chifukwa zinthu zambiri zikukhala zovuta chonchi tiyeni tione maiko ena akupangira kutuluka sikukutengera kuti atipha ai, ndipo sangaphe tonse ai.lets open our 👂 ndikuonaso
Ndipo Nkhaniyo ndiyoona a Malawi tili ndi matha anyooo
Ma judge akakhala kuti ndi achinyengo dziko so silimalongosoka, komanso ma judge akumalawi panopa ali mbali ndi boma
Ayitu uyu yekha simukhwasula akuimila amphawife ma judge ena ndiomwe agudwa ndi boma cholinga azathandizile kubela chisankho
Kwatentha 😂 palibe kucheza
These people the dont have ashame ,when the west money for poor people.
Zikomo kwambiri pothandiza dziko lino kwa Malawi aliens kuti tiziziwa chilungamo kwa anthu akuba ndalama za misonkho Mexico la Malawi.Wabayo asathawe ndipo tiwadziwe ndithu poyera.
DONT LET THEM,BUT WE NEED THE TRUTH TO FOCUS IN OUR NATION .INDEED IT IS HAPPENING IN OUR GORVERMENT OF MALAWI.START WITH CHAKWERA AND ALL MINISTERS,JUDICIAL ,AND ALL DEPARTEMENTS.
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Corruption Corruption
Judiciary is wrong, you think kamangila is mentally ill... judiciary is rotten
Kamangila anaconda dziko lake wachita bwino kuyalutsa a galu amenewa kamangila suli wekha tili pambuyo pako ndinthawi yoti chilungamo chiyende ngati madzi coz chikangawa akuononga malawi
Following