I love the truth in JB. The passion and determination she has towards MALAWI. She never get tire working up to date despite not being the president, God bless you Mama
Kmatu tamapangani balance mkamaganiza mukunena kt bingu anagulitsa jet mkubwezeretsapo ndege kuposaso pa jet po, nde iyeyo atagulisa ndege nchani cholozeka chomwe anagura poti ndalama zake mzija anthu amakazipeza mnkhalango za cash gate. Tiyen tingomuyamikira pazinthu zomwe akupanga za charity in communities
Almighty God continue to bless her excellence Dr Joyce banda, she developed all what a leader need to have , am learning a lot from his hustling, hard work, patriotic to her country Malawi, and dynamic leadership , umu mli umunthu ndi dzeru❤
Ndipo akukwanilitsadi kuti mmela poyamba ana anthu akupita Ku school chifukwa akupezako chakudya kunjaku kuli njala koma ana ambili akuthandizika through Joyce Banda foundation feeding centers
HE Dr Joyce Banda full of wisdom kuyankhula zowona ndipo ntchito zachifundo mukuzigwila kumangila nyumba anthu with community Development initiative anthu ku kasungu anapeza chakudya mulungu apitilize kukudalitsani
Amayi is an amazing creature. I salute 🎉. Zimandipwetekeka day and night amayi tikanawapatsa mpata Malawi could have been another national. I cry for my Malawi
Mama JB pa 2 years analamula Malawiyu ìmfa za azimayi pobeleka kunalibe chifukwa amalimbikitsa uchembele wabwino..ndipo anamanga ma guardian shelters muzipatala zambiri za Boma mu Malawi muno
She's a hope of Malawians and she deserved to be a leader indeed because she didn't stop doing her leadership work despite of her not being on the throne
I am a living testimony, under dynamic leadership of JB and climate justice needs to be reached out in our curriculum. Long_live_leadership @H.E JB. #necessary_noiz
Aaaah imwe yoywoyani unenesyo wakasanga charu chanangika no magetsi,Forex mafuta wagalimo kwene wakawezyelapo vyose in 100 days nyengo zinyanke tiyowoyenge unenesyo no soni
I love the truth in JB. The passion and determination she has towards MALAWI. She never get tire working up to date despite not being the president, God bless you Mama
Ndenge anagulisa Bingu yoyamba ija ilikuti Jet yakamuzu...ukufunsa iyii chifukwa anagulitsa nzimai...iyi ukufunsa anafotoza kale unali kuti?ndarama zake Dziko linagulira dzithu zadziko...koma tatiuze ya Kamuzu Bingu anagulitsa....Amai Mumagwira ntchito yotamandika...just 100days mavuto onse anatha...Long Live Your Excellency....We are proud of you..❤
Kmatu tamapangani balance mkamaganiza mukunena kt bingu anagulitsa jet mkubwezeretsapo ndege kuposaso pa jet po, nde iyeyo atagulisa ndege nchani cholozeka chomwe anagura poti ndalama zake mzija anthu amakazipeza mnkhalango za cash gate. Tiyen tingomuyamikira pazinthu zomwe akupanga za charity in communities
Almighty God continue to bless her excellence Dr Joyce banda, she developed all what a leader need to have , am learning a lot from his hustling, hard work, patriotic to her country Malawi, and dynamic leadership , umu mli umunthu ndi dzeru❤
Akudyetsa ana ķu Malawi kuno opotsa 15,000 tsiku lilinse phala...palibenso mtsogoleri amene amayika anthu ovutika pa mtima pake kuposa Dr Joyce Banda
Ndipo akukwanilitsadi kuti mmela poyamba ana anthu akupita Ku school chifukwa akupezako chakudya kunjaku kuli njala koma ana ambili akuthandizika through Joyce Banda foundation feeding centers
May Almighty Allah continue to bless her excellence Dr Joyce Banda
Dr Joyce Banda anapanga zinthu zambiri choyamba:adakwedza salary yaziphunzitsi,analora kutumiza achinyamata kukagwira ntchito kunja komaso kumangira anthu ovutika manyumba just to mention afew
HE Dr Joyce Banda full of wisdom kuyankhula zowona ndipo ntchito zachifundo mukuzigwila kumangila nyumba anthu with community Development initiative anthu ku kasungu anapeza chakudya mulungu apitilize kukudalitsani
Amayi is an amazing creature. I salute 🎉. Zimandipwetekeka day and night amayi tikanawapatsa mpata Malawi could have been another national. I cry for my Malawi
Ndipo bwezi tili patali kwambili anali ndimasophenya otukula dziko lino
H.E. JB is full of wisdom and plays smart and sophisticated politics
My role model, continue serving well.
Our ambassador to the international community..Mmatiimilira mama
Ndale zake ndiza mtendere, amalimbikitsa kuti ndale sitimadya tiyeni tizikondana tonse ndi a Malawi ndipo palibe dziko lomwe tingalilodze kuti ndi kwathu..
Amalimbikitsa kulemekeza atsogoleri ndikuwopa Chauta.
Ambuye azikupatsani moyo wautali Amayi
Mai wamzeru uyu ndipo i wish chipani chake chikanakhala strong ndithu ndikanamvotera ndimamkonda kuyambila pachiyambi ndipo amandilimbikitsa kukhala mzimai olimbikira.
Mama JB pa 2 years analamula Malawiyu ìmfa za azimayi pobeleka kunalibe chifukwa amalimbikitsa uchembele wabwino..ndipo anamanga ma guardian shelters muzipatala zambiri za Boma mu Malawi muno
She's a hope of Malawians and she deserved to be a leader indeed because she didn't stop doing her leadership work despite of her not being on the throne
H.E JB, a woman of integrity. A true leader. I love H.E JB.
Ambuye adzikudalitsani masten , ntchito zachifundo ndiye mukuzichita
HER EXCELLENCY 🙏🏽🙏🏽🙏🏽
I love this mama.
Sangagone tulo anthu ena akugona nyumba zodontha ndichifukwa pa 2 years anamanga manyumba almost every district of Malawi under Mudzi Transformation
Inunso mayi ndiamene munalipatsa soka dzikoli 😢
Anasintha zinthu in just 30 days mu office
Ndipo mafuta ,Forex magetsi kusiya kuzima masten amagwila ntchito
She was born a leader and full of love and passion
My favorite
She knew what to priotize in her leadership..mankhwala sankasowa mzipatala
Mayi wanzeru anasintha dziko 100days
Munthawi yake anapanga zinthu zimene amuna alephera
Mama J.B. yoù are brilliant, but why can't you tell Chakwera, of which you supported.
Anthu ambiri akapeza mipando amasiya kumva
Masten 🔥
Zowonadi Chilungamo cheni cheni
Joyce Banda alibetu size oho!!
Tyen tziyamikila zomwe wachita munthu amalaw tyen tisinthe
We are not Europeans pliz next time ur interview make with Chichewa
Mai amenewa anayesesa
I am a living testimony, under dynamic leadership of JB and climate justice needs to be reached out in our curriculum.
Long_live_leadership @H.E JB.
#necessary_noiz
Joyce NDI ndani galu aneneyo
Our former president she is not yet know,Where she is going to Alliance or not😂😂
Mfit yayikaz
Mbamva imakhala ndimbaluwe simasewera
Mama you look young 😂
If you want Malawians to trust you bring the money that you sold Jet.
Komatu akuonda mayiwa
Kukula
Komaso it's fine coz kunenepa kumabweretsa mavuto kwa anthu achikulire
Hmmmm🤔🤔🤔🤔
Mai opanda nzeru
Inu muli nazo
Kuwawona akunenawo kkkkk kuvesa chisoni ndipo ngati iwowo alinazo zeruzo
Mulungu sangakhale opusa kuwapatsa udindo wolamula mdziko muno zinthu ndikusintha pa 100 days..
Mwinatu munali ku theba mmene iye amalamula.
Fice iwina uyo
Mbuzi yamunthu iyi
When conscious escapes, you talk like this
Ndale zavutatu
Chi mzimayi choyipa chimenechi.
Onama iwe
Koma nde mkwiyotu za ziiiii
Mh
😱😱😱
Mama wambula mahala uyu walikutisokezela chalu panyengo yake she was acontributor of troubles in this country during her time stupid
Nzeru Mulibe
Aaaah imwe yoywoyani unenesyo wakasanga charu chanangika no magetsi,Forex mafuta wagalimo kwene wakawezyelapo vyose in 100 days nyengo zinyanke tiyowoyenge unenesyo no soni
Stupid ndimwe apo ntheee palije nachimoza mulikuvwilapo olo kukaya kwinu
Mbava yikuyankhula ngati zenizeni, ndege yathu yilikuti? You celebrated the death of Bingu, this was not a Malawian culture.
Munali ndi ndege?😂
@@Pembamuhammad yes, a jet bought by Bingu