Exactly ndpo a opposition komaso a Malawi first amaenera kukhala pa top kutisogolera Ife athu wamba,,,,komano to be honest izizi 🇲🇼 zikundnyasa kowopsa,,,,,😢😢😢amene mulindkuthekera kukumana ND akulu akulu talumikizanani nao tisinthe znthu guys this is too much
Komatu chakwera waposa satana amalawi tiyeni tisiye kumutenga president ngati mulungu ndipo azidziwa kuti no one is above the law nayenso wakhara miyezi yochepa bcz what goes round comes around dziko. Lamalawi chakwera silake ayiGod help us
@@isaacchiwaula731 Ukuyenera upite kusukulu adha, ukaphunzira Topic ya Human Rights, yomwe Muli freedom of expression. Tsegu maso pls inoyo sinthawi ya asamunda
Sorry about Malawi kwa vuta kwambili kom akulukulu anane chomwe wakulu wayangu wolopatalichebe zimachitika cong les ndiyachabe chabe siizi ukuwona uvulu uli pati wa athu
Kod chakwera ameneyo anabadwa ndi munthu kapena galu akanabadwa ku muntu bwenzi siku lina tikananva mawu amai ake akumuresa zomwe akuchitazi but one day is one day.
For the next generation yet unborn , whenever you come across this comment, just know that we were once alive this day to witness this masterpiece... Mtanyiwa the great man
We worn you guys before 2019 election that this Chakwera guy you are about to vote him into power he will make you cry. Amalawi kusamva ndi umbuli komaso kususuka.
Office in charge yo anapanga rate munda wanga wa mizimbe, week ya mawa ndioti akubwera, so long time vampire tikamuthimisila komweko, ngati akufuna moyo andisiyila mzimbe.
Malawi army overthrow chakwera government now if you really love your country.. .....coz your duty is to protect the country and its citizen......dont allow chakwera to bribe you see how many people are suffering.......where is your power MDF
Chakwera afa infa yopwetekeka mumuwuze kuti amalawi enafe sitikugona naye tulo... tell him to begin counting down his days of living. SITILOLA KUTI AWONONGE MALAWI WATHU OKONGOLA Just coz of his greedy and negligence. Kulibwino kadziko kamalawika tingogawanapo basi.
Komatu ku bomaku uzanani chilungamo zinthu zalakwika kale and u continue kuwonongelawonongela why? And why mistreating Mr kalindo like that Ili ndiziko ndipo limazungulila musayiwale zimenezo. Remember that there's tomorrow
Ndipo amene ataziwine 2025 azamuwonese mbonawona ameneyu mukuti president yu azawone zimene akuwawonesa amzakezi God is there watching as long as he didn't create himself
Taswela bwanji amalawi, pepani pepani masiku akudusa ndithu, Kodi ndi m'mene zikunvekelamu tikufuna tizazaze ku maliro malo mokasokha ku polici kiti atimasulire athuwa?
Mulungu wathu wa kumwamba timakudalirani muzonse tichitireni chifundo pa zomwe zikuchitika mu dziko la Malawi chonde. Pulumutsani abon kalindo ndi a kamulepo kaluwa komwe aliko Mulungu wathu chonde usalore kuti satana aambane tithandizeni kumenya nkhonoyi pathoka sitingate
A Malawi tiyeni tichitepo kanthu, apapa ndi nthawi ya zionetsero.......
Let's protect our human rights
Let's stand with our fighters.....
Exactly ndpo a opposition komaso a Malawi first amaenera kukhala pa top kutisogolera Ife athu wamba,,,,komano to be honest izizi 🇲🇼 zikundnyasa kowopsa,,,,,😢😢😢amene mulindkuthekera kukumana ND akulu akulu talumikizanani nao tisinthe znthu guys this is too much
Tidikire Monde ngati satuluka tipanga ximenezo
@@CassimMbalaka kumutulusa za mtendere sizingaatheke . Unless atamupanga something ....bcz anthuwa akuyesesa
Akulu akulu chonde ndikukupemphan chonde mudzina lamulungu chonde tatiyeni tigwilane manja tipange zoti Born kalindo atulutsidwe chonde nd munthu yekhayo yemwe akutionetsela zisinsi za momwe Boma likupangila nkhanza Amalawi
Exactly
And tisachedwepo akhonza kupanga ma plan awo achabe
May the Almighty God be with Mr kalindo and all Malawians
Amalawi titeni tiyeni konko and tikaphwanye police pokhapokha atamututsa Bon Kalindo pls
Lipopo FM number one ❤
Chakwela waonjeza kodi munthu ameneyi bwanji akupanga mkhaza zimenezi very shame to u chakwela mulungu akulange munthu oipa iwe
Bon kalindo ndimunthu wabwino kuyambila momwe anali mphunzisi wanga pa nkolokoti primary School, I stand with him.
Komatu chakwera waposa satana amalawi tiyeni tisiye kumutenga president ngati mulungu ndipo azidziwa kuti no one is above the law nayenso wakhara miyezi yochepa bcz what goes round comes around dziko. Lamalawi chakwera silake ayiGod help us
Amalawi why tikungoyang'ana Bon Kalindo ndi Mr Kaluwa Kuti azidzudzika chonchi kudzudzikira ifeyo????😢😢😢😢😢 Kodi tikufuna tizizalira anthuwa ataphedwa ndi MCP?????😢😢 Why tisakupanga kanthu tikungoyang'ana?????😢😢😢😢😢😢
Tikuchitiranji mantha chonchi abale
@@chifunilojalasi2337 Ndipo big aaaaa chonsecho dziko lathu aaa
Mukufuna dzikoli likhale losatsatira malamulo kod kut aliyense azingochita zomwe akufuna? Ndie likhalaso dziko lotetezeka? Ngat wapanga zosemphana ndi malamulo adziko Basi aziona, ifeso tazunzikaso titalakwira malamulo adziko amphwanga mwanva!!
@@isaacchiwaula731 Ukuyenera upite kusukulu adha, ukaphunzira Topic ya Human Rights, yomwe Muli freedom of expression. Tsegu maso pls inoyo sinthawi ya asamunda
Ambuye inu ndinu mulungu wamoyo woziwa kuyang'ana pena paripose mumenyereni nkhondo bon karinde kuti satana m' dyerekezi amugwire manyazi
Dziko lanthu lomwe kusowa nalo mtendere my Allah protect you bon kalindo 😢😢😢
Zovuta zedi Lu mmmmmm😢😢😢😢😢😢😢😢
Aaa hahaha😅😅😅
Ambuye Mulungu wanga kumwambako titakheni Ife tetedzerani Bon Kalindo kumene Ali tikulira pa maso panu mokupemphani Yehova nchitoreni chifundo
Mbuye timenyereni nkhondo chonde abale athu kumalawi akuxuzika dziko lokhala lawo,ndipemphero ndipembezero Kuti atuluke amoyo ambuye imvani kulila kwathu ananu Ife talema Ife ,km chomwe angaziwe ndichi muyezo omwe umamuyeza nzako naweso uzayezedwa omwe mulungu sangatisiye tokha
Sorry about Malawi kwa vuta kwambili kom akulukulu anane chomwe wakulu wayangu wolopatalichebe zimachitika cong les ndiyachabe chabe siizi ukuwona uvulu uli pati wa athu
Just loving what happened in Niger 🇳🇪 and Burkina Faso 🇧🇫. Army yachabe imene ija. Don't tolerate nonsense from President
Chakwera mulungu akukhululukire ukudzuza mizimu kom chmwe muziwe achakwera zanu zida mulibeso chaka
God protect Malawi
Limpopo ntchito mukugwira yotamandika
Where are you mr Namiwa?
Can't you guide us?
Daniele 6:16 sadileki ndi miseki ndi abitinego anaturuka mudede yagajo Yamato winiko atulukawamoyo
Amen
mcp yatha coz nkhaza akupangazi akudziwa kuti anthu awatuluka
Kkkkk zavuta
Palibe chobisika pamaso pa Mulungu. All the hidden treasures must out in Jesus Mighty Name🙏🙏
Kod chakwera ameneyo anabadwa ndi munthu kapena galu akanabadwa ku muntu bwenzi siku lina tikananva mawu amai ake akumuresa zomwe akuchitazi but one day is one day.
So if akumukaniza to go to toilet ndiye even food angamupatse may good Lord have mercy upon Kalindo's life 😢
Keep on rebuking them please
Your number one and only to be trusted
Guys apa ndiye wafikapo bwanji ameneyu Eeee chakwela umeneu ndiufiti.
Chakwera ndiye gwenembeyo coz anapha Vice wake chifukwa cha dyera
Ambuye chitanipo kathu a Malawi tiyeni titengepo gawo kupempheraela akalindo ndi aka mlepo kalua
May the lord protect mr Bon kalindo in Jesus name
Mr mnthanyiwa tikukutsan ntchito mukuigwir kwmbr proud of u
Kodi chakwela akuganiza bwanji ndizopatsa manyazi zomwe akuchita,koma amalawi tithadi ndikuphedwa komaaaaa???? Musamale kunja kuno kuli mulungu.
Nanga manganya Alibe udindo wowombola nzake winiko?
Chakwale akuzitenga ngati wamuyaya ayi ndithu
Big up bravo
Ndiyekuti iweyo ukunamaka cz sizimatheka munthu kumuletsa kuwonedwa komanso kupita ku chimbudzi.
Komatu Antanyiwa mukuyesetsa kwambiri mbari yanu komano vuto A Malawi ife sitimatha kugwilana manja komaso anthu omwe mukuti ndinu azipani bwanji mwangokhala chete osatuluka mesa munthu uyu amakulankhulilani? Tadzukani plz gwilanani manja pangani zothekera zowona zinthu izi zizichitika inu mukuona? Tadzukani apa tamuuzeni chakwelayo kut tili kunyengo ya Democracy timalankhula zakukhosi kwathu
Please koma akoro apolice anakunzani please musayese kuwachura ndipo munziwawunza popa kuti sindizakulurani ndipo munzindi unza zambili ena ofuna kukzani zambili alipo koma amawopa
Pepani bwana chonde tiuzeni choonadi zokhudza Magalimoto asilikali achilendo amene alowa dziko Muno more than 20 adusa pa Luzu Ku Blantyre atanyamula ma contena akudzatani plz #NTANYIWA tiuezeni...????
Komatu anyamata amenewo asamale asangoti tili mwamba ndiye aziona ngati pansi palibe mame aziona akazasikamo mwambamo mpomwe azazione ndithu!!!!
Falawo wawumisa mitima muziko la Malawi koma tisataye mutima Mulungu ali kumwamba akuona zose ikwana nthawi yoti falawo alangidwe
Bon kalindo atetezedwa ndi Mulungu.
Zosakhala bwino... hmmmm
For the next generation yet unborn , whenever you come across this comment, just know that we were once alive this day to witness this masterpiece... Mtanyiwa the great man
Saíd m,bawa pa mkongo wamako, limozi ndi MCP yakoyo, munthu wankhaza ukumusekelera chakwela nonse ndi chakwela wako nyini za amayi anu
We worn you guys before 2019 election that this Chakwera guy you are about to vote him into power he will make you cry.
Amalawi kusamva ndi umbuli komaso kususuka.
Even our parents warn us about the MCP leadership anthu kusanva now ndi izi we are no longer safe at all
Chakwela akatula udindo choyambilila asazakhale kumalawiko chifukwa choti azayasidwa moto zuwa likuswa ntengo azaphedwa
Zosayenda
Zikufunika kupita kunja ndikuyamba mandemo paka watuluke bon kalindo walakwachani
Mavuto abale afuna apange chani
Office in charge yo anapanga rate munda wanga wa mizimbe, week ya mawa ndioti akubwera, so long time vampire tikamuthimisila komweko, ngati akufuna moyo andisiyila mzimbe.
Ambuye alowelerepo anatulusa Petro mundende tulusani boni kalindo
Mudziko.lapansi kuli athu ankhaza koma uyu ndie Ali special without any shame oooooo my God do something
Allah alipaliyatu amuteteza 😢😢😢😢
Allah will protect him
Malawi army overthrow chakwera government now if you really love your country.. .....coz your duty is to protect the country and its citizen......dont allow chakwera to bribe you see how many people are suffering.......where is your power MDF
Thanyiwa tumizilen number yanu please ndimakukondan kwambili❤❤❤❤❤❤
Come on Limpopo 💪💪💪
ZITSIRU CHIFUKWA CHA KUPUTSA KWANU LHOMWE. YOU THOUGHT THIS COUNTRY BELONGS TO YOU
Kodi kalindo akafuna kudzithandidzila adzichita kumuyimbila chakwela ndiye iyeyo chakwelayo amamuudza ndani
Sorry ana amu khonje tinachedwa ku timavanukukoma bother
Mumakwana pakanakuziwa kwamaveya koma ife tilipokupepela kuti akalido atetezeke dipoatulukako muzinalayesu masalimo 119:126
Tiyeni tituluke abale anthu awa atikwana bwanji zoona munthu akuzizika ife tili pheee zoona Malawi tisala ndi anthu olimba tima ngati kalindo mulungu musalole choyipa chilichonse chimupeze bon kalindo
😮God will reveal everything done secretly
Anthu akunkhotakota chonde onesani kukhuzidwa kwanu nanu pazimene boma lachakwelayu likuchita tisalole kuti bomali litizunze ife amalawi
May God protect Bon Kalindo wherever he z....
Chakwera chilipo chikumusata MULUNGU si munthu khalani chete Let's pray for him.
Network ya NRB kulilongwe kokha
Network ya ku immigration ku Lilongwe kokha
Ayi zikomo ndithu tionana 2025
Why Malawians are not doing as the Kenyans are doing..... This is not good guys
Apapa ndiye zanyanya koma MOTi koma tiziti ikuchitika apayi ndi democrats olo bwanji kapena Mr chakwela asandukano mulungu mwina
Apa boma latengedwa ngati banja, osati democrany
Yomweyooo Galu iweee, Yudasi Chakwera woyeeeee,wakuphayoooo thawani, thawani,uyooo Goliath,uyooo🎉🎉🎉
Ambuye mulungu kumwambako tioneni ife 😭😭😭mr chilima,mukadadziwa abale simukanakopa amalawife kulowesaso congress mb'oma 🥲
Plz alindi nyimbo yomwe ikuveka pasipai kumapeto kolankhura mr mthanyiwa anaimba ndna yandisangalatsa kwmbr
Anayimba nd a Mec uyiva 2025 osadanda
May almighty Allah protect Bon kalindo 🤲
Tiyeni tipange ziwonetsero tisamangomvetsela Limpopo tiyeni tizuke Malawi
Amalawi, tiyeni tisawasekelele ang'aziwa, tiwachose b4 2025, palibenso reason yoti tifikile 2025 apaa, time to change is now!, achoke wagule ameneyu , mxiem
MULUNGU ndi wa chifundo chosatha amuteteze Bon Kalindo.
Iiiiii koma a MCP kupha kalindo utsayembekedzela zabwino dzikoli mulimva kuwawa chiwanda chakupha chili ndi MCP ukuko kumapeto nsono mwadzi wa chilima wakupengetsani mudzaliwona dziko kuwawa MULUNGU SIMUNTHU AKUWONA ZONSEDZI
Chakwera afa infa yopwetekeka mumuwuze kuti amalawi enafe sitikugona naye tulo... tell him to begin counting down his days of living. SITILOLA KUTI AWONONGE MALAWI WATHU OKONGOLA Just coz of his greedy and negligence.
Kulibwino kadziko kamalawika tingogawanapo basi.
Zimene akupanga apulezidenti zikunyatsa zedi chifukwa palibe chimwene analakwa Koma azafa Ngati galu
asiyeni adzipanga dzimene akupangazo siku lachiweruzo lizabwela olo pachedwa
Ayi zikomo kwambiri chakwera koma chomwe ungaziwe kaya sindikumiziwa koma chomwe mungaziwe Bon kalindo kungofa ndikuti Bon kalindo kungofa tiziona
Kodi a tsogoleri osutsa boma bwanji ochitapo kanthu mophatikizana ndi a Human rights. Malawi is finished.
Pamenepatu pakufunika kukatchola policeyo komko ngat muja amkachitila iwo nthawi yamademo kwamsunde
But why chakwera? Kodi galu ameneyu akufuna chani Ku dziko la malawi?
Kodi wapha aja sanakukwanire ?
Usatilakwitss Ife , realise kalindo
Bola kukaocha moto police ya kumenekoyo ndalama anagwiritsa ntchito pomanga police sindalama ya chakwera
Kmatu kungopha kalindo kuvuta coz zachilima sitidaiwale
Kutukwanidwa kwa chakwera sinkhaza kutengeka pachinthu chakut sukuchidziwa ndibwino kusachitsatira okay
MCP AKUFUNA ASINTHE MALAMULO AZIKO AKUFUNA AWONGWEZELE ZAKA ZA PULEZ ASANAVONTENSO PHEKESELAZIKUNVEKA
Chakwela sinthakoni nkhanza zanu chonde simoyo mukupangawo
Komatu ku bomaku uzanani chilungamo zinthu zalakwika kale and u continue kuwonongelawonongela why? And why mistreating Mr kalindo like that Ili ndiziko ndipo limazungulila musayiwale zimenezo. Remember that there's tomorrow
Amabungwe owona za ufulu waanthu alikuti?, azibusa amipingo yosiyanasiyana alikuti
Kmatu tikadikila kut zifike povuta bwanji ndigoyambisa mademo
Dzikomo kwambiri munthu wa mulungu pitilizani ntchito yotamandika
Bola lasatanikili la chakwela ng'ona ng'azi gule likufuna kuyambisa nkhondo mdziko muno ndizomwe akufuna asatana amenewa 😡👺👹👿😈👹👺
mpando ndiwosiilana umenewo usaiwale kt mwatsala ndi miyezi yochepa chabe
Kalindo anachipeza chomwe ankachifuna paja anali patsogolo kufuna kongelesi lero ndi izi
Keep fire 🔥 Limpopo tilipompo nafeso
Yehova tenganiponi mbali populumusa moyo was akalindo
Ine ndi kuti chakwera kupanga zosedzi chifukwa akuopa kuluza MA vote ndipo akudziwa kt adzafera kundende ndipo adzafera kundende ndithu
Ndipo amene ataziwine 2025 azamuwonese mbonawona ameneyu mukuti president yu azawone zimene akuwawonesa amzakezi God is there watching as long as he didn't create himself
Taswela bwanji amalawi, pepani pepani masiku akudusa ndithu, Kodi ndi m'mene zikunvekelamu tikufuna tizazaze ku maliro malo mokasokha ku polici kiti atimasulire athuwa?