BON KALINDO LERO PA 28 JUNE NDETU KULI NKHANI |

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 28 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 195

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl 3 หลายเดือนก่อน +5

    That's very wonderful massage it's true,tiyeni Malawi tisegule maso

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember 3 หลายเดือนก่อน +14

    Mwana oopsa kwambiri the DC

    • @limbanimtitima9170
      @limbanimtitima9170 3 หลายเดือนก่อน

      Awa ndi big man amayankhura chilungamo ❤

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 หลายเดือนก่อน +4

    Ndalama ndi zimenezo koma mzipatala mulibemo mankhwala shame. Bon kalindo Mulungu anasankha inuyo ngati ngelo wamulungu pakati pa dziko amalawi I silute you

  • @EmmanuelThambo
    @EmmanuelThambo 3 หลายเดือนก่อน +21

    Umboni tauwona kuno ku Zomba ma centre ena anatsegulidwa kwa 5 days ajambula kwa masiku awiri masiku enawo amati mafuta anawathera mu magenarators. Keep it up Kalindo we're proud of you.

    • @AmirGeloo
      @AmirGeloo 3 หลายเดือนก่อน +2

      Why translating it English ?

  • @Jasonnyatwa
    @Jasonnyatwa 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ayi ndithu tikuyenela kukavota opanda ID chifukwa zimenezi zitiphela maufulu athu,

  • @davedavie6211
    @davedavie6211 3 หลายเดือนก่อน +3

    Ukhalise DC Ukutisegula maso

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 3 หลายเดือนก่อน

    Ndiyeno zikusonyeza kuti anthu amene akubwezedwao Sitidzavota? Chonde chinyengo chimenechi tayambatu kale kudandaula.

  • @Mpondapromise9
    @Mpondapromise9 3 หลายเดือนก่อน +2

    Big up DC

  • @LawrenceDickens-jk3zx
    @LawrenceDickens-jk3zx 3 หลายเดือนก่อน +5

    End of MCP ndanena ndanena /wetting zachitika ku Kenya basi!!!!

    • @EliasOdala
      @EliasOdala 3 หลายเดือนก่อน +1

      DCcc ndiwe katundu omanga ndi wire always proud of yu

    • @JackMvura-ik2td
      @JackMvura-ik2td 3 หลายเดือนก่อน

      If only your family will vote you can talk that rubbish MCP it's not the way simple you think most MCP members they don't respond rubbish the don't talk nonsense they make sure keep quiet no fight with empty teen wait and see chakwera is not a small boy of Malawi so he is always showing the nation of Malawi that he is full grown up man always is away from the stupid people 2025 be careful

    • @UTHMAN-WAYA
      @UTHMAN-WAYA 3 หลายเดือนก่อน

      ​@@JackMvura-ik2td🤣🤣🤣Inu MCP ikumanga anthu ndemuzit ili Quit aaa🤣🤣💔

    • @LawrenceDickens-jk3zx
      @LawrenceDickens-jk3zx 3 หลายเดือนก่อน

      @@JackMvura-ik2td uziwo ase kapena umadyanawo za chipanizo? Zako zimene asaah.....

    • @JackMvura-ik2td
      @JackMvura-ik2td 3 หลายเดือนก่อน

      @@UTHMAN-WAYA police kapena MCP tell people the truth don't just talk cause you can talk what I need people must go to court tell them MCP is no longer MCP is a police but talking while you're sleeping by house it won't solve the problem

  • @LeviChakwira
    @LeviChakwira 3 หลายเดือนก่อน

    Campaign will be easier for opposition parties. A mcp apha chilima. 90% ya anthu mu Malawi akuziwa kuti mcp ndi amene apha chilima.

  • @juntoiman
    @juntoiman 3 หลายเดือนก่อน

    Mr DC timakunyadilani Cox mumatisegula maso and mumaima pachilungamo

  • @JafaBulhm
    @JafaBulhm 3 หลายเดือนก่อน

    Ulemu wanu bon kalindo Mwana oyopsa Kwabsi

  • @ChimwemweWanga
    @ChimwemweWanga 3 หลายเดือนก่อน

    Mumatiimila bro

  • @JoshuaMagodi
    @JoshuaMagodi 3 หลายเดือนก่อน +2

    Umakwana ase

  • @GiftFrancesco
    @GiftFrancesco 3 หลายเดือนก่อน

    The DC ❤❤❤❤

  • @RodgersChikumbutso-jr7fh
    @RodgersChikumbutso-jr7fh 3 หลายเดือนก่อน

    Ichi chimandisangalatsa

  • @mathewsmhone8953
    @mathewsmhone8953 3 หลายเดือนก่อน

    The last man standing umakwana big man

  • @MacKamanga
    @MacKamanga 3 หลายเดือนก่อน

    Wake up call

  • @FanizoKawindula
    @FanizoKawindula 3 หลายเดือนก่อน

    Chitsiru ichi

  • @KeziaAmoss
    @KeziaAmoss 3 หลายเดือนก่อน

    Bon Kalindo ndi katundu

  • @FridayMpanga
    @FridayMpanga 3 หลายเดือนก่อน

  • @tariroJinya
    @tariroJinya 3 หลายเดือนก่อน

    Yes tell him he think he is live president

  • @NASP-g7h
    @NASP-g7h 3 หลายเดือนก่อน

    Kom mcp kuwina tizavotaso cz axakhala kuti abela 99

  • @PeaceMafait
    @PeaceMafait 3 หลายเดือนก่อน

    Koma chi DC

  • @lovemorenaluso8965
    @lovemorenaluso8965 3 หลายเดือนก่อน

    Intel yachabe the DCCCCCCCCCCC mwana woooopsa kwambiri

  • @VictorKachulu-y3n
    @VictorKachulu-y3n 3 หลายเดือนก่อน

    Mbuli izi ndi kalindo wanuyo ine ndatulukamo mu DPP ndimaganiza anthu ake ndi a mzeru koma eeeeeeeee kuyambila atsogoleri ndi owatsatila omwe akuyendera magazi a ndale panopa akufesa ndalezo adzakololanso ndale zomwezo

  • @charlesmuwanya7845
    @charlesmuwanya7845 3 หลายเดือนก่อน +9

    Please a Law Society of Malawi ndi zipani za opposition zonse pitani Ku court mukane mfundo yoti opanda National Id asavote.
    Kuchokera pachiyambi timavota polembetsa mu voter register pogwilitsa ntchito passport, driver's licence,Kalata yochokera kwa mfumu etc .
    Every Malawian above the age of 18 is eligible to vote without National ID restrictions.

  • @AlexPhaloni
    @AlexPhaloni 3 หลายเดือนก่อน +6

    Muthu openga ndiyekhayo angasapote mcp

  • @JosephMichael-x7v
    @JosephMichael-x7v 3 หลายเดือนก่อน +3

    I wish bon kalindo atakhala president ku Malawi

  • @amosphakira7936
    @amosphakira7936 3 หลายเดือนก่อน +2

    Mr kalindo ,mfundo imeneo ndiyoona a kufuna kubela ma vote njira yake imeneo .Ndie ndikofunika kti anthu asavotere through l D chifukwa xisokonexa xithuxi pls.

  • @BhekiMavundla-po2bq
    @BhekiMavundla-po2bq 3 หลายเดือนก่อน +3

    Zonwe akunena Bon Kalindo zokhuza NRB ndivomelezane naye ndithu,kuno Kumangochi zachitika ndipo zikuchitikabe madela ena.Pano anthu ambiri asiyidwa mu masenta olembesela zaunzika kut alephele kukhala ndichipatso chaunzika ndicholinga kut anthu asazavote ambiri kuno kumwela ndipo Ineyo ndimboni ndithu kwa Born Kalindo.Pa anthu okwana 300 pamudzi uliwonse amene alembedwa zaunzika ndi anthu okwana 100 akha basi Kumangochi kuno,ambiri enafe tasiyidwa akuti nthawi yatha sapitiliza koma 2days yokha ndimene akhala akupanga process ya NRB mumasenta onse kumangochi kuno

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o 3 หลายเดือนก่อน +4

    Mose atamwalila mulungu anapeleka wina mtsolelli mpaka anakafika ku dziko lamalonjezano ndiye autm msabwelel ayi mulungu atipasa wina tisafooke tisapange mantha tipite chisogolo

  • @LeviChakwira
    @LeviChakwira 3 หลายเดือนก่อน +2

    A utm please stand up and be united. We love this party. We are behind you. We thank you Boni kalindo for saying the truth

  • @MaxwellDzaone-ym1vg
    @MaxwellDzaone-ym1vg 3 หลายเดือนก่อน +6

    Big Freedom fighter of Malawi

  • @DafterKhungwa
    @DafterKhungwa 3 หลายเดือนก่อน +6

    Yes,zoonadi tiyeni a Malawi tisagone tulo

  • @SophieKamanga
    @SophieKamanga 3 หลายเดือนก่อน +1

    Zawapengetsadi ndlam ndichifukwa akugula masuti ovala mwana opanda size ndipo olo chigawo chapakati sitikuwafuna achakwela ndi nduna zawo onse amenewo salowaso boma chaka cha 2025

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 3 หลายเดือนก่อน

    Wanthu azavota ngakhale alibe cha u nzika ngati bungwe lo imirira chisánkho achite zopusa Litha, Chakwera wapha Chilima.aliyense waziwa Ndipo Chakwera pa nyero pa mache

  • @RoseMkandawire-e2g
    @RoseMkandawire-e2g 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂 a president ndeno mukuzikanda pasaya apo pakuyabwa mumanivesa kukoma inu aboni pangani chipani tizakuvotereni ife anthu osauka chonde

  • @YamieManda
    @YamieManda 3 หลายเดือนก่อน

    Muthu uyu wa dpp,osangobwerela ku dpp bwanji mbuzi yamuthu iwe😊

  • @williamdaka79
    @williamdaka79 3 หลายเดือนก่อน

    Anzathu ku Kenya amuonetsa Ruto koma ifeyo a malawi Kaye tinabadwa bwanji?

  • @GustarLafisha
    @GustarLafisha 3 หลายเดือนก่อน

    Nkhani ya azanu nde simukamba ya avice pulesidenti takambani wez

  • @BittonRashid
    @BittonRashid 3 หลายเดือนก่อน

    Pangolini ululani tikavote asinthe zimenezo isagwilentchito.

  • @Centre-m6f
    @Centre-m6f 3 หลายเดือนก่อน

    UTM ingotuluka mwachangu isanafike thawi ya campaign

  • @ZaccheousPetrol
    @ZaccheousPetrol 3 หลายเดือนก่อน

    Iwedi ndikatundu....ine kudabwa kuti opposition mukudikila liti

  • @ELINATengule
    @ELINATengule 3 หลายเดือนก่อน

    Akalindo mulungu azikutsogolerani thawi zose❤

  • @simeonkatema6484
    @simeonkatema6484 3 หลายเดือนก่อน

    Zoona zake DC umakwanira iweyo tikavota bas ooanda cha uzika

  • @JamesTobiasNkhoma
    @JamesTobiasNkhoma 3 หลายเดือนก่อน +1

    Thanks kalindo for the good information.....keep it up am behind u

  • @arthurkayuza
    @arthurkayuza 3 หลายเดือนก่อน

    Neighbour waionera patali game ....this is true !

  • @PeterRabson-z3w
    @PeterRabson-z3w 3 หลายเดือนก่อน +5

    Ndipo ñdinu nokha otimenyera ufulu

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 3 หลายเดือนก่อน

    🔥New clear BOM,Bonn Kalindo!

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 3 หลายเดือนก่อน +1

    Tivote ndi ngati kale ma id tilibe

  • @JosephMichael-x7v
    @JosephMichael-x7v 3 หลายเดือนก่อน

    I wish bon kalindo atakhala president ku Malawi

  • @JosephMichael-x7v
    @JosephMichael-x7v 3 หลายเดือนก่อน

    I wish bon kalindo atakhala president ku Malawi

  • @MeniyaMikaya
    @MeniyaMikaya 3 หลายเดือนก่อน

    Openga kwambili ndiyemwe angabweleleso ku DPP mutu wake unayima fwetseke zanu ndi kalindo wanu yemweyo mwalandila ndalama kwa gogo wanu opanda mano mkamwayo ndinu zitsilu shupt

    • @MbaulaJames
      @MbaulaJames 3 หลายเดือนก่อน

      Lemekeza atateako ndi amako kut masiku amoyo wako apitilile

  • @IsakyIsak
    @IsakyIsak 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwela awukhudzidwa za ifa ya saulo chilima

  • @AndrewWyson
    @AndrewWyson 3 หลายเดือนก่อน

    Pompano 😅Kenya Kenya game ndizikwanje

  • @ShiraKasekaNyirenda
    @ShiraKasekaNyirenda 3 หลายเดือนก่อน

    Timadalira inu bwana DC mumatiyimila amphawi

  • @FrankChingudu-pi8kn
    @FrankChingudu-pi8kn 3 หลายเดือนก่อน

    Muleken mwana wa eni alankhule za kumtima kwake.

  • @AdamChirwa-u3d
    @AdamChirwa-u3d 3 หลายเดือนก่อน

    Ulem wanu mnthu wamkulu kwambili

  • @AdamChirwa-u3d
    @AdamChirwa-u3d 3 หลายเดือนก่อน

    Ulem wanu mnthu wamkulu kwambili

  • @EliasPhiri-yv8gv
    @EliasPhiri-yv8gv 3 หลายเดือนก่อน

    Koma uyu Nde amatokotadi eish

  • @MussaHassani-zg1hm
    @MussaHassani-zg1hm 3 หลายเดือนก่อน +2

    Is our president thanks

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 3 หลายเดือนก่อน

    For sure this is State Capture

  • @WilfredYekha
    @WilfredYekha 3 หลายเดือนก่อน

    Mbambande, keep it up

  • @Jasper-xk9iv
    @Jasper-xk9iv 3 หลายเดือนก่อน

    Tili pambuyo pano DC

  • @MacleanKwacha
    @MacleanKwacha 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ulemu wanu big man,mumatiyimilila

  • @JamesPonds-j9v
    @JamesPonds-j9v 3 หลายเดือนก่อน

    Big up our own DC

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt 3 หลายเดือนก่อน

    Zoona big man kalindo

  • @frankjolijo
    @frankjolijo 3 หลายเดือนก่อน +1

    .... Kuswa kuswa....opha mnzake, naye aphedwe

  • @NumeliKambo
    @NumeliKambo 3 หลายเดือนก่อน

    Born kalindo nd Dolo

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwera why are you evil 😈
    Chakwera why are you wicked
    God will punish you soon

  • @MercyChavula-qy1my
    @MercyChavula-qy1my 3 หลายเดือนก่อน

    Mumakwana ulem wanu

  • @Djmsakama-kj3ne
    @Djmsakama-kj3ne 3 หลายเดือนก่อน

    Osamabisila

  • @RhulaniMukasi
    @RhulaniMukasi 3 หลายเดือนก่อน

    Pari galu wina mmenemu waremba masege yonyoza chilungamo cha DC mancgendeake ameneyo mot Malawi mmene akuvutikila ndipo ndikuuzen agalunonse zomwemwaba mukudyazo mukanyera mundende apa sitikusekerelan tatopananu iwenamachende chakwera segula zimakhutuzo uve nthawiyanu yatha

  • @MarkKaliati
    @MarkKaliati 3 หลายเดือนก่อน

    It's fact

  • @MessiahPitros
    @MessiahPitros 3 หลายเดือนก่อน

    It's true

  • @KelvinBAligiza
    @KelvinBAligiza 3 หลายเดือนก่อน

    Bg up Dc

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate 3 หลายเดือนก่อน

    DC 🥰

  • @MauriceTayali
    @MauriceTayali 3 หลายเดือนก่อน

    Ndalama za satanic, samalani. AMALAWI amzanga dziko ili laipa satanic yalowa mudziko lathu ili CHAKWERA atipereka kwa satana

  • @SenzoKatopola
    @SenzoKatopola 3 หลายเดือนก่อน

    Umakwana fadah

  • @YammsyZebron
    @YammsyZebron 3 หลายเดือนก่อน

    DC ❤

  • @EviePhiri
    @EviePhiri 3 หลายเดือนก่อน

    Dc

  • @SelinadeniasDenias
    @SelinadeniasDenias 3 หลายเดือนก่อน

    Ulemu wanu

  • @HarlodLemwe
    @HarlodLemwe 3 หลายเดือนก่อน

    kod bwana DC ukamapanga zimenezi umafuna chani kwenikweni ??? anthu andale awa amafuna kumatisokoneza anthu akumidzife mbolatu iyi

  • @MasterHeadson-ki7ji
    @MasterHeadson-ki7ji 3 หลายเดือนก่อน

    📌

  • @AkibuMdala-sr1dy
    @AkibuMdala-sr1dy 3 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 3 หลายเดือนก่อน

    Izi ndizoonadi ku south kuno nrb palibe chikuchitika ife tikudabwa kuti a oppositions Ali kuti??? Nkhani ya ziphatso ikuyenda bwino only central region wat is this after all?? Nrb ikufunika kuyipangira ma demo akuzolowera tsopano kaya adya ndalama azisanza ndithu.

  • @ThivadoartistDyson
    @ThivadoartistDyson 3 หลายเดือนก่อน

    Chilombo chachilungamo koma bon kalindo mulungu akutetezele until nkhwandwe itachoka 'l think akufuna tipange ngat anthu akukenya.

  • @LeviChakwira
    @LeviChakwira 3 หลายเดือนก่อน

    Palibe munthu amene angavotere nkhope ya chakwera ndi mcp. Never

  • @sukiemapemba4094
    @sukiemapemba4094 3 หลายเดือนก่อน

    Tizavota zopanda ma ID apo ayi miyala izagwila ntchito kuphanakuphana basi

  • @StevenNathaya
    @StevenNathaya 3 หลายเดือนก่อน

    Bwana Dc mumakwanila hvy ndipo musasye kutimenyel ufulu

  • @VioletMovella
    @VioletMovella 3 หลายเดือนก่อน

    Born kalindo umatiyimilila,,,tili kumbali yako
    Malawi cwa mun2 uyu

  • @GanizaniPhiri-f2i
    @GanizaniPhiri-f2i 3 หลายเดือนก่อน

    Umakwana mr DC tingopita pa nseu basi .mbuzi zimene zatitopesa kwambiri.

  • @johnchitenji4
    @johnchitenji4 3 หลายเดือนก่อน

    Big up born kalindo With powerful message 👍

  • @MartinKapanga-q6m
    @MartinKapanga-q6m 3 หลายเดือนก่อน +1

    ndimakukondani a born kalindo ❤❤❤

  • @GetrudeBanda-sd1yf
    @GetrudeBanda-sd1yf 3 หลายเดือนก่อน +1

    Osafooka go on

  • @AbdikaniDasar
    @AbdikaniDasar 3 หลายเดือนก่อน

    That's powerful message continue to show them the right way to catch this big fish mr nyo

  • @MeliaMichael
    @MeliaMichael 3 หลายเดือนก่อน

    I support the motion
    Pamene anthu akuvota NRB izakhare pomwepo

  • @FrancisDinala
    @FrancisDinala 3 หลายเดือนก่อน

    Ndikungopanga scroll koma ndisanapeze pomwe amunenera zoyipa Bon kalindo more fire

  • @ZephMbeleswa-n8m
    @ZephMbeleswa-n8m 3 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkk akuti ndi president osauka ndiye inu ndi osauka moti daily amakupatsani chakudya