M’BUSA EMWE WAZUZULA BOMA LA ACHAKWERA UJA NDI UYU NDIPO ANAYANKHULA MOSAPSYATILA MAU CHONCHI

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 14 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 57

  • @BrightZionga
    @BrightZionga 2 หลายเดือนก่อน +4

    Azibusa opanda mantha keep it up ❤❤❤may the good Lord bless you

  • @ChimsyUlemu
    @ChimsyUlemu 2 หลายเดือนก่อน +3

    Amen abusa much appreciated for ur message osaopaaaaa osafooka

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 2 หลายเดือนก่อน +3

    Kkkkkk mo fire munthu wamulungu auzeni Zowona afitiwo

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 2 หลายเดือนก่อน

    🔥🔥🔥💪💪💪

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน

    Mau ngati amamwa kachaso chisilu ndi chakwera wakoyo

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 2 หลายเดือนก่อน +2

    😂😂😂😂😂😂😂 mcp yabalalikadi eishiiii kupha Chilima imene ija ndi Mistake yaikulu heavy

  • @MasChisi-v4l
    @MasChisi-v4l 2 หลายเดือนก่อน

    Ndiye mwati adzudzula chakwera?

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน

    Chisilu ichi ndipo ndiamene amakonza ziwembu zonse zikuchitika mmalawi muno ku mcp

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 2 หลายเดือนก่อน

    Tamumveni mau ake osasa ngati amamwa kachaso chisilu cha munthu

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws 2 หลายเดือนก่อน

    Ngati boma likulakwitsa kuli bwino kuli zuzula otsaliopa this is democracy,,zachamba aii

  • @brightcharlie2396
    @brightcharlie2396 2 หลายเดือนก่อน +2

    Vuto la Ife a Malawi kukoka nkhani eeshiii mpaka mufuna a phedwe bas

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 2 หลายเดือนก่อน

    Galu ameneyi

  • @RoseMkandawire-e2g
    @RoseMkandawire-e2g 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 ziriko

  • @temwarachaelkhonje3733
    @temwarachaelkhonje3733 2 หลายเดือนก่อน +1

    Boldness at its best

  • @Mazzy-zu5fo
    @Mazzy-zu5fo 2 หลายเดือนก่อน

    Chimwendo Banda anganene chani kudziko lamalawi ndikumva mfiti yachikhalireni abusa munalalika mulungu akudaliseni Chilima anatisiira mau osaopa osafooka tizafera mbendera yamalawi

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 2 หลายเดือนก่อน +1

    Chimwendo banda machende ake inu simwapha anthu pa 10 june dzausilu

  • @hackwellkagolo6614
    @hackwellkagolo6614 2 หลายเดือนก่อน

    Koma iwotu mademo ndi mademo umenewo ndi umodzi akufuna ayakhule kuti chani makamaka kapena zimenezo aziwa liti. Iwo m'mene amanyozela ma speach awo alipotu kodi

  • @malikoezala
    @malikoezala 2 หลายเดือนก่อน

    Upiteso Kwa skc

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 2 หลายเดือนก่อน

    Achimwendo mumayankhula ngt munthu wa mzeru koma zimene mukuyankhula pamenepo zo simumadzikwanilitsa inuyo so ndamene mumatsogolera zosankhana mitindu

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa 2 หลายเดือนก่อน

    Aliyese watopa mu dziko muno ndi ulamuliro wa Chakwela ndi chipani chake chopusa cha mcp

  • @MustafaLikaomba
    @MustafaLikaomba 2 หลายเดือนก่อน

    Koma galu uyu wausilu bwanji

  • @AndrewMagombo
    @AndrewMagombo 2 หลายเดือนก่อน

    Boma lopusa molomoti ankhale buxy ndi mabvuto a mlw km ayi kumanga anthu

  • @hesbaluku7281
    @hesbaluku7281 2 หลายเดือนก่อน

    Aaaa mesa anayambisa ndiyeyo zot achewa alipo 14 mita aaaaaa mboli yake😢

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 2 หลายเดือนก่อน

    MCP ndi chipani cha makape bwanji akuyankhula ngati anthu akuwanyonza pamene anthuwo akuzuzula nkhanza, umbava, kupha anthu,mabodza ndi tsankho lomwe MCP ikupanga.

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica 2 หลายเดือนก่อน

    Kudulira ma speech panjira?

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 2 หลายเดือนก่อน

    Chilungamo chimawawa palibe chomwe walakwitsa m'busayo.

  • @ModicaiChirwa
    @ModicaiChirwa 2 หลายเดือนก่อน

    Chimwendo Komanso MCP yonse ndiyoipa kwambiri ,chifukwa ndiichi MCP yagula mifuti 400 yophera Malawi chifukwa cholidzudzula bomalawo lomwe laononga Komanso kupha Komanso akulamula dziko kamba Koti anagwiritsa ntchito anyamata omweo kupanga ziwawa ndikunyoza atsolleri azipani Zina lero akuononga ndiwo ndiye zawaophya anthu opanda umunthu awa amcp muchoke basi mukuyambitsa nkhondo mdziko inuyo mukumayankhula Kuti mupha wanthu inuyo pomwe anzanusaanayankhuleko choncho

  • @EdisonNakulenga
    @EdisonNakulenga 2 หลายเดือนก่อน +1

    Auzeni asatanawo

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe Chimwendo Banda pamtumbo pako ndithu zoti munapha Chilima aliyese akudziwa

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ndichitsiru chimwendo..mutu ngat bans

  • @WedsonVinkhumbo-q9l
    @WedsonVinkhumbo-q9l 2 หลายเดือนก่อน

    Mmmmm sititopa

  • @christopherbanda4698
    @christopherbanda4698 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe chimwendo get out

  • @Cathy-oc7vd
    @Cathy-oc7vd 2 หลายเดือนก่อน

    Akufuna kutamidwa

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 2 หลายเดือนก่อน +1

    Chimwendo iwe ndi galu kwabasi ngati mukuchita zoipa athu asazuzule pakanwa ngati pa toilet

    • @MasterMwandira-q8v
      @MasterMwandira-q8v 2 หลายเดือนก่อน

      Chimwendo kazidyelanithu ndalama za mcp, chaka chamawa mkakhale pansi

    • @TrizaGeorge-q8w
      @TrizaGeorge-q8w 2 หลายเดือนก่อน

      @@MasterMwandira-q8v muziti ndi eakundende

  • @SammyKasolota
    @SammyKasolota 2 หลายเดือนก่อน

    Kwachemeratu

  • @inamrigala
    @inamrigala 2 หลายเดือนก่อน +1

    Olo amusake km wa wakamba zowona chimwendo ndi nkumba

  • @CosmasChikwindi
    @CosmasChikwindi 2 หลายเดือนก่อน

    Azibusa ngati atopa asiye ubusa akalowendale, maka azibusa a ccap mumaonjeza dyela.

    • @VenançioZocueza
      @VenançioZocueza 2 หลายเดือนก่อน

      Ngakhale nthawi ya David anadzudzulidwa ndi mneneri atagona ndi mkazi wa uliya muhitu

    • @RonaldGama-gz9ug
      @RonaldGama-gz9ug 2 หลายเดือนก่อน +1

      Uchitsiru si Ndiwe uja dzana umanena ku achewa mulipo ambiri

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 2 หลายเดือนก่อน +1

      Inu ndinu achitsiru palibe chamzeru mmayakhula pamtumbo pako ndi Chanyera wakoyo anthu amagazi inu

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 2 หลายเดือนก่อน

    Kkkk awudze munthu wa.
    mulungu

  • @BillyKalambo-jx3vf
    @BillyKalambo-jx3vf 2 หลายเดือนก่อน

    Chimwendo kungokula kukamwa koma palibe chanzeru chomwe anganene iyeyu akuti umodzi pomwe akupha anzawo

  • @HarriePearson
    @HarriePearson 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe wopusa kwambiri chimwendo

  • @BrightZionga
    @BrightZionga 2 หลายเดือนก่อน

    Chimwendo ndiwe kape

  • @SammyKasolota
    @SammyKasolota 2 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkkkkkkkkk

  • @RomeoLapken
    @RomeoLapken 2 หลายเดือนก่อน

    A malitili amakhala okuba?

  • @ChizymanJason
    @ChizymanJason 2 หลายเดือนก่อน

    Kma ya

  • @YoungMwacho
    @YoungMwacho 2 หลายเดือนก่อน

    The whole synod attending such stupid gatherings which are pure political. A matili anakhala akuba, these people were thieves. Waste of time and resources.

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 2 หลายเดือนก่อน

    Chimwendo banda chisilu cha munthu

  • @YoungMwacho
    @YoungMwacho 2 หลายเดือนก่อน

    Buzi zokhazokha

  • @KulinjiGoodsonnkhoma
    @KulinjiGoodsonnkhoma 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂 zavuta basi

  • @JamesMopiha
    @JamesMopiha 2 หลายเดือนก่อน

    Ey

  • @ChizymanJason
    @ChizymanJason 2 หลายเดือนก่อน +1

    Umodzi ndikupha anthu 9?

  • @ChifundoJohn-w3t
    @ChifundoJohn-w3t 2 หลายเดือนก่อน

    Chimwendo banda zimachende zako